Shehe uyuso wagagada ulariki wake mopanda mantha kusiya anthu akungoombera mmanja

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 5. 07. 2024

Komentáře • 156

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b Před 5 dny +16

    Tayesedwa ndi president wakhaza chakwera ndie timupempha Allah kuti atichosele chakwelayo ameen

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Před 5 dny +10

    Sheikhe ulaliki wanu siukugwilizana ndi ma aya omwe mumatulutsa pakamwa panu, uku ndikugulitsa mawu amulungu, ambuye akumvelen chison Ameen

    • @omardyman8083
      @omardyman8083 Před 5 dny

      Analandila ndalama nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto zachamba

    • @rasulmaulidi2224
      @rasulmaulidi2224 Před 3 dny

      zikomo kwambiri m'bale wanga ndimaganiza ngati ndindekha ndimaganiza choncho..ndikufuna number yake ndimuyankhule mwapadela ndi galu wamunthu uyu ali ndidyela simasewera akuyalutsa chisilamu

  • @abdulhameed7808
    @abdulhameed7808 Před 5 dny +5

    Basi sitilankhula zambili tingokusungirani ulemu Sheikh Anthu.

  • @NenehMasanje
    @NenehMasanje Před 5 dny +12

    Sheikh mwadya now ndrama

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 5 dny +3

    7:53 7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizanu
    Mayeselo aifa muyesa ife sitimaziwaaa,
    Nde imfazake zochita kumugwira munthu pakhosi mwadaladala , kumuombela mfuti mkamwa munthu ,kodi yinu mulankhulabwanj muli ndiwumunthuyinu ,aaa muzichotsela ulemu nokhatuyinu mwangotengana nonse odya ndalama zamagazibasi ,
    Afitiwo alimwetuuuu ati zikuyenda malawi wake utiyo amene mungamunamize lelo ,
    Azibusa muzichotsera ulemu nokha mwamva

  • @SulaimanaJames-b9v
    @SulaimanaJames-b9v Před 3 dny

    Maa Shaa Allah
    May Allah bless this message and make it beneficial

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny +3

    Wadya nawo ndalama zamagazi iwee, usatinamize asilamufe pamodzi ndi amalawife, ifenso ndife asilamutu, mayesero ukunena apawa simayesero ochokeraxkwa ALLAH, awa ndimayesero ochokera kwa satana kudzela kwa chizukulu tudzi chake chotchedwa chakwela ndi boma less lake 😂😂😂😂😂

  • @DeliaKaduya
    @DeliaKaduya Před 5 dny +3

    Odya ndalama zamagazi ngati akumasowa zoyankhula zawo? Allah mukunenayo akuyendereni Sheik😢

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam Před 5 dny +2

    Ameen sheikh Allah ahead u. From Cape Town centre

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny +3

    Chemoto alipomwepo anapha ALLAN WITIKA, anapha chilima kuchikangawa 😂😂😂😂

  • @SteveriaZimba-qs1id
    @SteveriaZimba-qs1id Před 5 dny +1

    Amen and amen uthenga wamphavu ambuye alemekezeke ndipo akhululukire zochimwa zathu

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali Před 5 dny +1

    Naam sheikh ma shaa Allah ulaliki wabwino ndithu ❤❤❤❤

  • @BrownMatonyola-xi3lb
    @BrownMatonyola-xi3lb Před 3 dny

    Mwadya zingati
    Aliyese wanyambita ndalama zoti azizilise za imfa yachilima ndikupepha Yehovah Mulungu wathu amuonetse kiyama akumane ndi mavuto

  • @FebbieMaulidi
    @FebbieMaulidi Před 5 dny +1

    God bless you sheik for unity message ❤

  • @SayidiIshmael
    @SayidiIshmael Před 3 dny

    ❤Allah give you more life and imaan to defending this deen

  • @IshaaakKango
    @IshaaakKango Před 2 dny

    Maashallah sheikh

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 15 hodinami

    Aaaa sizomwezija Izi inu asheikh opanda manyazi ,
    Panja peni peni wadya ndalama Za Chikangawa uyu,
    Sali pachilungamo uyu

  • @muhmmadsarwer9527
    @muhmmadsarwer9527 Před 4 dny

    Ameen thuma ameen Allah tichotseleni President ameneyu..ndipo tipatseni mtsogoleri wabwino mdziko mwathu muno

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Před 5 dny +1

    Mukufuna mutamike. M'nungu tam'nyekule ngulumbira une

  • @mosewallace9717
    @mosewallace9717 Před 3 dny

    mweye che kuntamba 🔥🔥

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi9834 Před 5 dny +2

    *WA ALYKUM SSALAAM WARAHAMATULLAHI WABARAKATUHU,,,,Inna lillah wa Inna ilayh rajoon*

  • @TWAIBAKBANIES
    @TWAIBAKBANIES Před 4 dny

    Ma vesi ali apa zili kutali tali . Aaaaaaa koma akulu akulu sheikh mudziima pachilungamo komanso ma ves osamawakhitetsa ai

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson Před 5 dny

    Kkkkkkkkkkk wabodza ndiwe ma inovolopu yakutseka pakamwa ya chakwela, zikhale ndi kunkuyu 😂😂😂 waukape ndani sakudziwa.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 5 dny +1

    Sheikh awa salibwino akugulitsa mawu aMulungu ndi ntengo wotsika mukankhanthidwa mutsiku lomaliza

  • @AndersonTsoyo
    @AndersonTsoyo Před 22 hodinami

    100% shehe uthenga omanganga dziko

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 2 dny

    Ili ndiye gulu loyitana chakwela ku Eid atawapasa mbia makwacha mashehe adyera ichoooo!

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny +1

    Usatiipisile Islam yathu iwe wamva , bwanji sukuwalesa makafiir omwe ulinawo pomwepowo kuti azikha okonda anzawo?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 5 dny +2

    Mwapatsidwa ndalama

  • @Macsaidi
    @Macsaidi Před 5 dny

    Komabe sitinganame pa chilungamo.
    Saulos Chilima anaphedwa ndi ndege ya boma la mcp

  • @omardyman8083
    @omardyman8083 Před 5 dny

    Ndine msilamunso koma sheikh uyu wapochelaapo nkhani anaiyamba bwino kukasokoneza kumapeto akatero anali ku state house

  • @MollenMponya
    @MollenMponya Před 2 dny

    Awa ndye mau ochokwera kwa Mulungu osati Za Anja amaziyesa Okha opambana

  • @PeterThomas-lw3io
    @PeterThomas-lw3io Před 5 dny

    Alhamudulillla sheih my Allah bless you all the time what's a sweet Message like 💋💗 this Marshall ( port Erizabeth SA missionvale

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese108 Před 5 dny +1

    Ana usawi chemwalimu apochele silingwa

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před 5 dny

    God bless you Sheik all the time ❤❤❤❤❤

  • @juntoiman
    @juntoiman Před 4 dny

    Mmmmm sheikh zoona malo molankhula chilungamo pamaso pa anthu muli busy kubisa choona.Pamenepotu padali anzanu koma lero alikyt

  • @JeanKambala-gm1zr
    @JeanKambala-gm1zr Před 5 dny

    Nyasi zenizeni pamaso pamulungu chilungamo mukuchidziwa Shehe iwe. Wadya ndalama

  • @MafumuBanda
    @MafumuBanda Před 5 dny

    Sheikh ilim yanu ndiyochepa mupite mukaphunzirenso, ngati mukuzitenga zinthu za Allah maso mmwamba eeeeee chilango chaukali chkupezani pompo mulipo asakutameni awowo andalewo ndizotsala , ifenso tinaphunzira kwambiri kuposa iweyo xxx

  • @AbouzaidahSayeed
    @AbouzaidahSayeed Před 5 dny

    Kkkkkk sheikh wasanjatu uyu 😅

  • @NuradinaAbrahima-rt9ip

    No i was interested ndi ulaliki wanu Sheikh koma kumapetoko mwandionongela data yanga😭😭😭😭

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny +1

    Ine ndine Msilamu, uyu ndi sheikh wa chishiya uyu kafiir weniweni uyu,

    • @HusseinAdamLidezo
      @HusseinAdamLidezo Před 5 dny +1

      Sheikhe wamanyi uyu mbuz

    • @harrisbanda5891
      @harrisbanda5891 Před 5 dny

      @@HusseinAdamLidezo zoona angamasinthanise chisilamu ndi ndalama?, bwanji sakulesa asatana anzakewa kuzunza ndikupha anthu mdziko muno ?

  • @trickermussa472
    @trickermussa472 Před 4 dny

    Kukangotinyasisila deen yathu mbuzi ya shaikh

  • @marvelousmadzimure1811

    Masha Allah ❤❤❤

  • @Sasha-g3z
    @Sasha-g3z Před 4 dny

    Bas allah awadalotse ndi ulaliki wawow

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Před 3 dny

    Msilamu wolakira zau Mulungu osati enewa .Akuti ngati munthu wa mulungu walalika osanyoza president akuti ndiye sadziwa kulalikira. Shame

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember Před 5 dny +1

    Soka kwaiye akupindisa chilungamo popeza akuziyandikisa matako ake kumoto

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny

    Zikhale ng'oma akuwombelanso mmanja pamfundoless zomwe wanena, kodi unamulesa kuti asamaphe ma ruandaniz and Burundians komanso amalawi?.

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
    @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 15 hodinami

    Inu nde muletsa zoipazooo suyu muyamikira mfiti ,wakuba, musatinyase

  • @Musa-cz1nm
    @Musa-cz1nm Před 5 dny

    Ma shaallah ma shaallah ma shaallah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny

    Izo mzoona zoti tiziphunzisana zabwino ndikulesana zoyipa, funso kwa iweyo shehe ndiloti;
    Kodi zoipa zomwe akuchita chakwelayo wamulesa?
    Kupha kumene akupha aboma anthu kumalawi kuno wawalesa aboma ako awusiluwo ?,

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo Před dnem

    Thanks shelk potipatsa ulaliki wabwnowu

  • @KasundaAbbasi
    @KasundaAbbasi Před 5 dny

    Ngakhale mawu akewo akupepuka zoyakhula zakeso kumalemelera abusa aja

  • @abwinoamatani4921
    @abwinoamatani4921 Před 5 dny

    Mzimu wa Chilima ukunyetseni nonse amene mukugawa ma yellow band ndi inu amene mukudya ma bans

  • @AminahMussah
    @AminahMussah Před 5 dny +3

    sheikh zamanyazitu iziii kufuna kuoneka wabwino pamanso pa pule mwadya zingat

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před 5 dny

    Chemoto akhale Kunkuyu😅😅😅😅

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv

    Munthu angopha anthu inu mukamuyimile , munthu onyoza chisilamuyo inu mukamuyimile angapilile zimenezo ndani
    Kodi yinu mufuna azakupheleni agogo anu mpamene muzaone? Kuti izi ndizilombo!!!? Aaaaa mwatipsesa mitimatu nsilamu wantundu wanji osadzudzula munthu akupanga zoipa , bwanji simukuyima pa deen ndikulalika chilungamo aaaaa yinu nde mwalalika mophusa bolani abusa aja nawonso yinde anyika koma yinu mwanyanya ,
    Ndipo palibe akutameni kupatula okhawo akulipilani ndalamawo ife ndife asilamu eni eni choipa timadzudzula basi angakhale Allah anamudzudzula ntumiki wake Muhammad ( saw ) sametime atabwera munthu kuzamfutsa koma ntumiki anayang'ana kumbali
    Alkah pompo pompo anamudzudzura awa ndayani aaaaa musatinyase mwamva

  • @FarhaazbashaMdoka
    @FarhaazbashaMdoka Před 3 dny

    Koma ma ayah wa tikugwilitsa ntchito molakwika 😆😆😆😆😆😆👏👏👏👏👏👏

  • @udkconsultancy5567
    @udkconsultancy5567 Před 5 dny

    POWERFUL

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Před 5 dny

    SHEIH MWAPALA ULALIKIWANU MUMAFUNA AKUTAMENI A PRESIDENT PALIBE CHANZERU MWAYANKHULAPO APA ALLA WAKE UTIYO ANGAKONDEE NDI ZOMWE AKUCHITA CHAKWERAYO AYI INUSO ALLA AKUONENI

  • @Ishmael376
    @Ishmael376 Před 5 dny

    Komati choti muziwe kulankhula boA pamaso pamulungu pomwe chilungamo mukuziwa muziwe kuti akakuwochani

  • @user-ti8ds7iq8z
    @user-ti8ds7iq8z Před 5 dny +1

    Chakwela akusapoter Israel shehe wa mabi

  • @AugustineIshmael
    @AugustineIshmael Před 4 dny

    Naam ena akwiya chifukwa mwayakhula zosephana ndizomwe Iwo akufuna

  • @princedetbozsmallboy1749

    Awaso nawo aaaaaa zaziiii mazidyani wosatipusitsa

  • @emilynthite6545
    @emilynthite6545 Před 5 dny +1

    Apasidwa ndarama alaliki adyela

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja Před 4 dny

    Akutuma Kodi sheikh wachinyengo iwe nde akupasa zingati ?

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv

    7:53 Chikangawa akupatsani million yinu zaziiiiii nkhanizaunu

  • @Hassankazembe-d3o
    @Hassankazembe-d3o Před 5 dny

    Sheikh apatu nanu mwanama kwambiri 😂😂😂😂😂😂

  • @medicoastkzn
    @medicoastkzn Před 5 dny

    Mashala

  • @ChristianMtambalika
    @ChristianMtambalika Před 5 dny

    Anthu muzinena chirungamo osamabisala mukaona omunenayo kuti alipopo mamizimu anthu akuvutika pqmene iweyo ukufunq kukomesera president umenewo moyo oyipa ngati uli sogoleri wapingo ndiwe waboza liuze chirungamo dziko

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi Před 5 dny

    Walykum ssalam wakahmatul llah wabaraktu

  • @KassimIssa-bn3od
    @KassimIssa-bn3od Před 5 dny

    Kmatu musamapange zindu kut akutamen shehe Allah wanji angasangalale ulaliki zimayi sisi kunja osamvala pango 😢😢😢 dini ulindo bas inarilah

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny

    Moses kumkuyu akukuwombela mmanja pamfundoless zakozo, kodi unamulesa kuti asamaphe anthu ngati mmene anaphela ALLAN WITIKA uja?

  • @user-zf7xk8fk5s
    @user-zf7xk8fk5s Před 5 dny +1

    Km Inu sheikh ndinu opanda nzeru apurezident akunyoza chisilam kms amakokomezera nkhondo ku Palestine kut adziwapha asilam zoon Inu kumaim pagulu kwacemera

    • @user-zf7xk8fk5s
      @user-zf7xk8fk5s Před 5 dny

      Ndipo panop asilam akumalaw akuchititsa manyaz chisilam chifukwa chokonda ndalam mmmm zomvetsa chison

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon Před 5 dny

      Ndipo sheih uyu watinamizapo wadya nao ndalama za pule malawi sadzathekayi

    • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv
      @AbdulmajeedJbanda-oz3jv Před 5 dny

      Alibenzeru uyu

  • @user-fm7yg5yc2c
    @user-fm7yg5yc2c Před 5 dny

    Walaikum salaam warahmatullah wabarakatuh... Innalillah wainna illaih rajiun

  • @AliSinoya
    @AliSinoya Před 4 dny

    Sheikh uyu manyakwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 5 dny

    Shehee wadya chamba chanji chakwera Mutu Ngati gwafa😂

  • @CHIFUNDOCHINA-lp9lg
    @CHIFUNDOCHINA-lp9lg Před 3 dny

    Mashallah

  • @user-qs7xw4ph7z
    @user-qs7xw4ph7z Před 4 dny

    Amen

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi Před 5 dny

    Chakwera anapha chilima😊

  • @SolomonShaibuh
    @SolomonShaibuh Před 5 dny

    Live from Gaza city

  • @AbdulmajeedJbanda-oz3jv

    Palibe amene angakutameni yinu bodza zidyani ndalamazo msilamu weni weni akuonani Kuti mwanama akulu ndinu adyela

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 5 dny

    Achina chimoto ndi a MCP ndiwe shehe😂

  • @moosakananji1879
    @moosakananji1879 Před 4 dny

    Sheikh awa Malo ngt awa kumafunika Sheikh ayyub azipita kumeneku not awa

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Před 5 dny

    Ndiye ulaliki otaninso uwu, mukulalikila ngati simukumva kuwawa bwanji, odya banzi sasowa.

  • @user-jb5yb9wq3y
    @user-jb5yb9wq3y Před 5 dny +1

    Ndalama Za mcp zikuyakhula

  • @bisweckchimphamba8497

    Iwe undithera nthawi ukuwoneka kuti walandila brown envelope

  • @abbasdamsonamini4888
    @abbasdamsonamini4888 Před 4 dny

    Naam Ameen thumma Ameen

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p Před 5 dny

    Bodza pakadalipano akuliyamba ndi Chakwelayo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 5 dny

    Ameen

  • @shadrackdrums3536
    @shadrackdrums3536 Před 5 dny

    Ulaliki oti sungatingele kumoyo wosatha komaso sungasithe kalikose. Koma anthu akuwombela mmanja. Ulaliki oti mukupanga taget Boni kalindo, Bakili muluzi tv komaso limpopo FM. Ife we are not going to support any usiles speach or teaching like this wadya bamzi shehe.

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t Před 4 dny

    Chemoto ndinu mwandila ma unforp

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja Před 5 dny

    Kodi munthu ameyu ndani alinaye number yake sheikh ameneyo ndimuuze kuipa koononga chipembezo chifukwa chandalama

  • @HallimaMakwinja
    @HallimaMakwinja Před 5 dny

    Inu sheikh watu ndithudi si mslamu weniweni awa akuononga chipembezo cha chislamu ndi mbunzi yamunthu

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 5 dny

    Iwenso waikila kumbuyo asatana mmalo mowalesa zoipa which means ndiwe kafiir

  • @JumaMboneka
    @JumaMboneka Před 4 dny

    Aise kaya ukumati mwiniwakowe Malawi chani kuyambila lelo ndakutuluka ndakuona kut ndiwe wamanyi ukuchwmelela zimenezi kut sheh walalikila mwamphavu mphavuzake zilikut machende ako aise pamoz ndisheh akowo iwe wamanyi kwabas

  • @MussaAndreQuenessi
    @MussaAndreQuenessi Před 5 dny

    Awapasa ndalama 😮 awa

  • @NchocitoTuaibo
    @NchocitoTuaibo Před 5 dny

    Naam sheh

  • @JamesRoben-dy7bx
    @JamesRoben-dy7bx Před 5 dny

    Uyu anadya kale ndalama uyu komaso ndi wa mcp uyu

  • @abdulllahanubieimran06comanubi

    Jazackah alla

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 2 dny

    Shehe my foot 😅😅😅

  • @EmanuelPaul-io2hk
    @EmanuelPaul-io2hk Před 3 dny

    Shehe akufuna chuma chamagazichi eti?