Awawa amalalika okunva wanva osanvaso akhale mosanva momwemo. Powerful preaching
Very good preacher.very good preaching for everyone
Wow great preaching man of God ❤❤
Zikomo Abusa Mau Achilimbikitso. To God be all the glory.
Uyu ukuyenera kukhala mlangizi wa a president on religious affairs l ❤ you Rev Yasin Gama
Powerful preaching
2:08 Ambuye alemekezeke chifukwa cha uthenga umenewu. Ndikungoganizira kuti abusawa akanakhala ndi nthawi yokwanira, chachitatu chomwe Yobu anachichitabe modabwitsa tonse ndi chakuti, ngakhale anzake a mkulu ameneyi anamunyozanso kufikira kunena kuti analuza zonse chifukwa choti anachimwira Mulungu, koma iyeyu sanawamvere, koma analankhulabe zomutama Mulungu pa moyo wake. Yobu 13vs13-15
Amen powerful message 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🔥🔥🔥
May God bless you&protect you in all aspects. Chakwera must listen &change
Amen and amen Ambuye azikudaritsani abusa🙏💕🔥
Inu nda busa weniweni osati akupha wanthu ambuye akuze malile amoyo wanu ndi masithika ndi ulaliki wanu amen and amen
Amen. Very powerful message!!
A gama lalikirani amve a chakwera mau amvetsetse kuti mulungu ndiyankho nthawi zomse
Ndiye mumuone kunkuyu ndizikhaleyo kkkkkk ngat akudabwatu afiti kkkkk mukanthidwa kuli Mwari kudenga just wait chakwela ngat akumva nkhutukumve yeniyeni Mulungu akupeleka uthenga tiyenazoni
You are blessed sir. God continue to bless you
Very powerful preaching 👏 🙌 🙏
Mashallah 🙏 abusa,mau anu,nkhope yanu,thupi lanu likutipasa ma answers abwino,mulungu azikudalisani😢
God bless pastor yasin
Amen and amen Abusa uthenga wachilimbikitso Amen
Mawu ogwila ntima ambuye adalitse mawu amenewa Amen 🙏
This is powerfully teaching that is affecting full life
Ufulu wanokha a mcp umenewu mwatiphera Chilima ndiye nkumati tilimu ufulu?
Amene koma asogoleli osaopa mulungu akumangobela a Malawi osauka kumangolemela amodzi modzi mulungu awayankhule mwapadela
Ameni ameni ameeen . MULUNGU akudalitsen Abusa Amen
Ambuye alemekezeke ,ndipo Mulungu apitilize kudalitsa ndikuchjitira chifundo Malawi AMEN.
Powerful message
You're our own Prof Lumumba In Malawi
Love you
Amen. Powerful massage
To I very sorry to those who didn't listen properly the preaching, it's not Chakwera, it was a general powerful preaching even to those in a opposition who chose not to attend the function. Those are real witches and thieves
God bless you pastor Gamba
Amen and Amen powerful 🙏 🙌 👏
Glory be to God. My faith is lifted up.
Amen more wisdom
Tikamati uyuyu anabwera kuzatumikira anthu ku umzimu ❤❤❤ amen
Powerful man of God 🙏🙏 Amen
Amen powerful message ❤
So powerful 👏
Amen abusa God bless you ❤❤❤❤.
Yobu had one wife and David had many wives but the commonly recognized wives were 8 Bible limodzi lomwelo lomwe timati buku lopatulika la mawu a Mulungu.
I wonder why many people run away from that uncircumcised truth.
Indirectly a Yasini Gama akuti kukhala nd akazi oposela mmodzi ndi ntchimo zomwe zili zosemphana ndi zomwe limafotokoza buku lopatulika.
Powerful massage 💪💪💪
Amen abusa mau amphamvu.
Amen Abusa wakumva wamva
Amen ndizowonadi
Emeni auzeni mopanda matha mulungu awa Kathe zed
Always God news is powerful big up of God!!!
Great preaching
Amen Pastor!
amen papa
Wow powerful
Amen 🔥🔥🔥mwawuka amveka
AMBUYE alemekezeke cifukwa cauthenga wabwino
A yasin Gama kulalika mopanda mantha ngati akhalira mfuti
0:42 Powerful massage Amen and Amen
Amene abusa mumtidaritsa
ulendo uno i give salute ...amen osati kumalalika za ma buckets
Amen pastor
Amen abusa ulaliki wamphamvu ❤❤
amen mawu achilimbikitso may God be with you
powerful preaching
Amen amen and amen
Powerful man of God
Mbusa uyo aaaaa Ali ndi ndi mulungu wapepheratu mwa maso a tsogoleri
Alalikira bwino abusawa🙏
Good
Powerful words
Mulungu akudalinseni chifukwa chachinthunji kulinga ndi dziko lamalawi komanso ndimiyoyo yamansiku ano yomwe tilikudunsamo 🙏🙏🙏
amen postar
nice paster
Muwuzeni chakwela aside khupa anthu wosalakwa
Mau amphavu wakuva wamva osamvaso sanave koma ambuye adalitse mau amene
Amen and amen 🙏
Amen Abusa
Mwalalika wakumva wamva
Mau ndamenewo mwanva
Zikomo mulungu akuze moyo wanu
Amén!!!
Azikazi aYobu onsewo analikumenekowo in men's suits wo
Abusa mulungu akudalitseni osati Ena woyipawo
Chirungam mwayankhura abusa amen
Amen and Amen
this was powerful
Mawu achilimbikitso. Ambuye adalitse mawu ake
Kodi inuso abusa mwaganidza kudya nao ndalama dzamagazi 😢😢
Powerful!!!
Munthu ngati pakamwa pali Chibazi sasowa mubusa Yasin chabazi chamupweteka
Maganizo inu. Inunso penanso akukudandaulani you're not 100% . God is the only judhe
Amen amen Mtumiki 🙏🙏🙏🙏🙏
Chakwera wazimvera yekha
Zikomo kwambiri abusa anthu Mulungu azikudalisani ku nthawi zonse.
Koma achakwera ndi nduna zawo sakuva mawu a Mulungu ali pompo koma mawu a Mulungu akupita ku nkhongo. Malawi siziko laumphawi bwanji azitsogoleri akulemera ndi mabanja awo. Malawi wakusowekera atsogoleri ngati inu abusa athu.
Amen powerful
Ambuye azipitiliza kukudalitsani abusa, mawu amphamvu kwambiri awa
Masha Allah
Amen
Mamvuto athu siwochokeka Kwa Mulungu ayi Koma ndiochita kupanga afisi ena Ake ,
Ati kuzilemeletsa okha nde must mpaka liti pepeza simufika angakhale 150 years muli Moyo ,
mukafika 100 years mwakhala Kona kuyika shugar mkamwa mwanumo osamumvayi kumangotuluka thofu ,mukankhanthidwayinu musiku lomaliza nde popeza simuopa hayi chabwino
Awa nde odziwa kulalikira
Ulaliki ogwila mtima 9:54
Chakwera ukunvakoma
Uthenga wa mvemvemve tisiye kutembelera dziko lathu .timuone ,Malawi pamalo takhalapo osaloza kwina abale.Mulungu atidalitse tonse.
Mau amphambvu ndithu Mulungu apitilirebe kukhala nanu kukutetezerani komanso akulitse malire amoyo wanu abusa Amen