kumalawi kuno ndani wandale angamake??

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 6. 07. 2024

Komentáře • 827

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y Před 22 dny +48

    This guy is most Genius. Congratulations Mibawa TV shame to mother Medias they can't cover this.

  • @DemisterKhuzumule
    @DemisterKhuzumule Před 7 dny +2

    Ichichi ndicholombo guys,we need people like this

  • @Syakinongwa
    @Syakinongwa Před 22 dny +41

    Wow. Wisdom of Solomon. God has revealed the leader we have been searching for. How i wish SKC was around to groom this "born leader".

  • @KINGSLEYDINIWA
    @KINGSLEYDINIWA Před 22 dny +35

    This guy wasemphana ndi Chilima anakavana hvy ndipo dziko lino tinakaliva kukoma.....komabe Mulungu salakwitsa APA nduu wabweretsaso Chilima wina,, ndag WA naye mchikondi Munthu amenei

  • @saulosmwaungulu1782
    @saulosmwaungulu1782 Před 21 dnem +23

    I am completely convinced with this leader how I feel the majority should see the same as some of us are seeing in him...May the good Lord direct him more to build this nation

  • @StewartGoma
    @StewartGoma Před 21 dnem +14

    Man u are brilliant than any president of malawi u need to be respected

  • @MisasaRomano
    @MisasaRomano Před 13 dny +3

    As good citizens this is our chance to change our Malawi. Once we support this GUY and his team technically we have joined the GAME CHANGERS TO THE WINNING TEAM. BRAVOOOO!!!

  • @calvinjamal7117
    @calvinjamal7117 Před 23 dny +28

    SKC spirit big up

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya Před 21 dnem +1

      Osamangoti skc chilichonse ngati kuti inuyo you were genuinely loving him.This guy has got good ideas which is needed to be taken seriously koma aMalawi gullibility imatipweteka ,kutengeka ngati kuti brain zanu munagulitsa, stop kumangotengeka ndale will never help single you kutukuka work hard atati alowe m'boma he will be advised and will forget everything he's saying now I tell you, Our late professor ngwazi Bingu Wam'thalika was a man koma lots of you simnamuonetu ,he was man I was telling my fellas akumavomeleza panopa chikufunika NB: n'kuzasintha government system everything will change thus all .. I like this guy but I already lost hope in policians, maybe tingapeze ozamuvotela next yr amenye campaign...tizamuone next yr..✊

    • @amaleeehmuzik-official
      @amaleeehmuzik-official Před 20 dny

      ​@@InnocentMtafya khala serious bro disflareting politic ndi game yoopsa take care

  • @IbrahimKampira-pe2cb
    @IbrahimKampira-pe2cb Před 21 dnem +15

    Kwamunthu yemwe analowako mkalasi kumva mfundo izi mkosavuta,koma munthu wakumudzi yemwe akangopeza tima handouts amangoti MY VOTE😢😮😮.Bwana Dennis muli mmaganizo abwino ndithuu....

    • @user-hs4bm2yj8r
      @user-hs4bm2yj8r Před 14 dny

      Ndipo ndi zoona zake,Koma mkulu wa Ku chikangawa sangamve izi

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 Před 23 dny +28

    Seems to be Malawi's Ibrahim Traore

  • @mishecksipolo7153
    @mishecksipolo7153 Před 23 dny +31

    He sounds genuine, I think God does not run out of ideas,SKC is gone but look at this khang'a now, so powerful

  • @limbanimtitima9170
    @limbanimtitima9170 Před 22 dny +12

    Uyo ndi big man ❤❤ lets hope the born kalindo akuva kuti amumenyere nkhondo uyu akhare president 😂

  • @user-wm2lx6hf2n
    @user-wm2lx6hf2n Před 20 dny +8

    Tamutchulen dzina timupange follow 💥💥💥 the guy is just extraordinary 🎉🎉🎉 The Dawn is just Here 🤟

  • @StevenFombe
    @StevenFombe Před 22 dny +13

    The one who might win presidency should include this guy pliz he has strong upstair

    • @MisasaRomano
      @MisasaRomano Před 13 dny

      Akaonongekako let him be as he is with his team. The most important thing to do is to support him and his team.

  • @ScrarNation
    @ScrarNation Před 22 dny +21

    Guys this is our guy let's support him

  • @giftkantayeni2042
    @giftkantayeni2042 Před 22 dny +11

    This is powerful lecturing and mind blowing

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y Před 22 dny +18

    Zinakati maphunzilo athu amakhala mchilankhulo chathu bwenzi dzikoli liri la chuma ndi kulemera koopsa. Phunzilo ili ndilovuta kwambiri mchingelezi koma apa olo nkhalamba ya zaka 80 itha kunvetsetsa.😢😢

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk Před 21 dnem +23

    This is the leader we expected to have in this country

    • @Gilbert-bk9ml
      @Gilbert-bk9ml Před 5 dny

      What about aisenhowa mkaka and his friend bwanji are not good

  • @thomasyohane987
    @thomasyohane987 Před 22 dny +11

    Anthu ngati awawa ndi chiombolo cha dziko, (akundikumbusa ndi Bingu nkuluyu) chifukwa amayendesa dziko ndi mutu wawo monga akuonera pa ground osati kumangosatila ndondomeko zoti zinapangidwa kale ndi azungu.
    Koma kuti ayamba zandalezi payekha sizingatheke ndipo sangazakhale president mpaka kalekale.koma angochita kutengedwa ndi chipani chomwe chili chothekera kuwina mosavuta ngati DPP ija monga anachitila Bakili 2004 kungomutenga Bingu ku convention kuti ndi amene azaime ngati president wa chipanicho basi.

    • @alexdombe4991
      @alexdombe4991 Před 21 dnem

      Vuto ndi lakuti anthu Ngati awa satengedwa serious,, anthu amakonda ndalama, ma t shirt ndi munthu wamolaro not nzeru,, Koma if party's like DPP, or UTM atamutenga zingathandize Kuti akalowe mu parliament

    • @sokojane4015
      @sokojane4015 Před 21 dnem

      Bingu Wamthalika anayesesadi chilungamo zinthu zimayenda bwino njala inatha ndithu Malawi nthawi ija

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před 23 dny +10

    Munthu ameneyu akhale otetezedwa chifukwa dziko limadana ndi month wanzeru ngati ameneyu amaziwa kuti atisegula maso timuteteze

  • @mikebernabechimundi3472
    @mikebernabechimundi3472 Před 23 dny +21

    Honestly the guy is genius,all the way from Mozambique adawa ndi dolo

  • @user-vx5kv8dz3d
    @user-vx5kv8dz3d Před 23 dny +16

    Uyuyu nde president

  • @GeomarkBanda
    @GeomarkBanda Před 17 dny +3

    Aaaah guys this is extraordinary , join forces,you and kabambe ,I love this ideology,we can move forward with him

  • @user-nz5jg5hv1m
    @user-nz5jg5hv1m Před 23 dny +48

    Adah awawa akuganiza ngat Ibrahim Traore the captain

    • @user-re7fo3be2z
      @user-re7fo3be2z Před 23 dny +1

      Ndipo heavy

    • @ScrarNation
      @ScrarNation Před 22 dny +1

      Kwambili he needs our support

    • @user-rv8gi4ro6r
      @user-rv8gi4ro6r Před 22 dny +2

      Tiyeni tiyetseko achinyamatawa

    • @fleshar-j6i
      @fleshar-j6i Před 22 dny +2

      Uja nd messiah

    • @SolokingChimzy-yt7dj
      @SolokingChimzy-yt7dj Před 21 dnem +1

      Derete ua comment..mesiah ndi Mulungu in humana flesh don't compare Him with anybody else..mind you tinabadwa through brood shareling while the Messiah was born through the Word power of God​@@fleshar-j6i

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 Před 23 dny +14

    Kupasidwa ngongole koma anthu kudukula kutsala pang'ono kudula chiwuno kusangalala 😂😂

  • @fostersimbi8820
    @fostersimbi8820 Před 20 dny +3

    I'm totally impressed with this guy... We need such leaders in our country

  • @claramenyani8606
    @claramenyani8606 Před 16 dny +5

    Guys let's support this man ... He is a genius

  • @thomasmwitiya1447
    @thomasmwitiya1447 Před 23 dny +8

    Here is another Bingu,,,welcome bro,,,mdziko muno tikufuna anthu ngati inu🔥🔥🔥🔥

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p Před 23 dny +9

    Big man Muthu ameneyu akuyankhula zanzerukwabansi

  • @stanleystagar8433
    @stanleystagar8433 Před 15 dny +1

    I will vote for him

  • @FumbwaLyson-3710
    @FumbwaLyson-3710 Před 21 dnem +5

    Uyuu katundu tiyeni timulange sponsor muwone agwetse yekha chakwera😂😂😂😂😂😂
    I will I will be minister of finance in his government kungotero ma youth ntchito 5 million azipeza 😂😂😂😂 tiyeni timisapote nfanayu❤❤❤❤

  • @PhiriChiyambi
    @PhiriChiyambi Před 22 dny +5

    She deserves to be a leader

  • @BlackdeeJamooh-gd7wq
    @BlackdeeJamooh-gd7wq Před 22 dny +6

    skc is back akuluakulu they cant stop us the reader is here

    • @user-og4dg6kz5s
      @user-og4dg6kz5s Před 17 dny

      If ur leader was dinning with puppets then also he was ...May his soul rest in peace.....

  • @chimajrbhahat2334
    @chimajrbhahat2334 Před 19 dny +1

    Even though he is young and inexperienced. He carries my vote, experience aipezera pawu presidency pomwepo

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 Před 16 dny +1

    Graat man we need people like you lets work together to change our country

  • @DennmichSimb
    @DennmichSimb Před 21 dnem +4

    That's great news, God should guide you and protect you from all evils.

  • @danielmuriya8675
    @danielmuriya8675 Před 23 dny +4

    I this this guy is good at economics

  • @ChivumbulutsoMbewe
    @ChivumbulutsoMbewe Před 20 dny +2

    This is wat Malawi needs in a leader...

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Před 23 dny +8

    Ngati Martha Chizuma ananena live pa maso pa president kuti ndikugwilizana ndi maganizo a DENNIS MAHATA ineso I will support you brother..

    • @fivemoobateam6521
      @fivemoobateam6521 Před 18 dny +2

      I love this guy kanduthu pachuma❤this as solution 😂

  • @JoyKagwada-kx3oo
    @JoyKagwada-kx3oo Před 23 dny +3

    The guys has good basis more especially on economics which is every key to development, however am still following him

  • @hopesato
    @hopesato Před 13 dny +1

    He deserves my vote

  • @victorchidothi-gd8bu
    @victorchidothi-gd8bu Před 8 dny

    He has inspired me, very genuine person. My vote

  • @peterbakuwo1249
    @peterbakuwo1249 Před 21 dnem +2

    Akuluwa alibwino kwambiri,...Nzeru zomveka bwino ngakhale ma system azungu ndi amphamvu,....Pamodzi ndi achina Julius Malema,Bobi Wine,Ibrahim Traore nzotheka.
    Nkhani ndi zakazo chisankho chikubwelachi sangakwanitse kuima..
    Ndulingalira ataenda ndi Martha Chidzuma ngati president,..zitithandiza.
    Bravo DMNk,...
    Mitu

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m Před 23 dny +12

    Now I think we hv our own traore in Malawi

  • @EbenTechnologies-xq5op
    @EbenTechnologies-xq5op Před 21 dnem +3

    Chilima's resurrection, i am ur prospect #my vote

  • @nsamampundu4278
    @nsamampundu4278 Před 23 dny +3

    Powerful my brother 👏🏿👏🏿👏🏿

  • @jamejoeljere0149
    @jamejoeljere0149 Před 8 dny +1

    Actually one of the source of finance is Seigniorage finance and the government we can use it because we in trouble now

  • @lacfunnytv1251
    @lacfunnytv1251 Před 12 dny +1

    Lets make this person known

  • @InnocentMtafya
    @InnocentMtafya Před 21 dnem +1

    He's good with his brains 2030 constitution ikadzalola we will vote for his fundo...

  • @SimonLikwangulo-xq9oz
    @SimonLikwangulo-xq9oz Před 23 dny +6

    Mcp ilipamoto kuchotsa chilima kubwelanso wina ntchito ilipo

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 Před 22 dny +4

    My bro keep it up we need to change Malawi atikwana anthu Okubawa

  • @AlexMwambera
    @AlexMwambera Před 15 dny +2

    Replacement for chilima, Mai kaliat wapedzeka munthu uja chitanipo kanthu

  • @francisvisage2705
    @francisvisage2705 Před 22 dny +2

    You have my vote sir🎉... May God prosper you..
    Koma chonde add GYM in your daily routine..

  • @PreciousPhiri-f2h
    @PreciousPhiri-f2h Před 21 dnem +1

    You deserve to be a president, go ahead God almighty is with you my dear

  • @danielringo3769
    @danielringo3769 Před 7 dny

    Andale pakamwa nde amayankhula za nzeru ndithu. Koma akangokhalapo pampandopo hip hop yokhayokha
    Alipo wina anachita kulonjeza kudzapanga retire ngati sizisintha ife nkumveradi 🙌🙌

  • @VincentChirwa-bf8zr
    @VincentChirwa-bf8zr Před 20 dny +1

    Nthandwe your advice is effective to transform Malawi , your are like Ibrahim troei of Burkina Faso Kee it up brother

  • @rashedzain6507
    @rashedzain6507 Před 13 dny +1

    Mudima umadana ndi kuunika
    May Allah grant much protection to my brother let's support him guys we need talented youth like this one

  • @Yusufu-Daudi
    @Yusufu-Daudi Před 23 dny +7

    Uyuyu next year akuyenera kukhala pa ballot paper 👍

  • @kazembejuma8277
    @kazembejuma8277 Před 21 dnem +2

    This is powerful indeed , he deserves to lead Africa .....

  • @rayro2694
    @rayro2694 Před 23 dny +2

    I'll vote this year only for you mr President

  • @KevinKathumba
    @KevinKathumba Před 20 dny +1

    You are so genius you deserve to be a reader of our country malawi

  • @lameckwillie3407
    @lameckwillie3407 Před 22 dny +2

    Am not an economics but this is 100% true

  • @sheilachimkomola2281
    @sheilachimkomola2281 Před 19 dny +1

    This guy has that thing 🔥🔥...my vote

  • @kachipapaennockie2677

    this guy anasowa pakatipa I used to follow him ngati nsakulakwisa Ali ku bunda... he I genius...this 2024 let's listen to him

  • @DemisterKhuzumule
    @DemisterKhuzumule Před 7 dny +1

    Chilima wadzuka Amwene ehhh mulungu 🙌

  • @SandikondaChalera-l8q
    @SandikondaChalera-l8q Před 21 dnem +3

    You will be my president

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 Před 23 dny +6

    Kuli mfiti 400 Malawi chikangawa party izakuphani baba.
    Be careful

  • @MathildaZalimba
    @MathildaZalimba Před 21 dnem +4

    Uyuyu ndi mphwake wa chilima....you touched

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před 23 dny +3

    You suppose to be a president I think you can change Malawi

  • @shariefsaiti7417
    @shariefsaiti7417 Před 13 dny +1

    Please someone like my comment, tomorrow must watch this again

  • @enockfrank940
    @enockfrank940 Před 20 dny

    I was skipping this post but I took a few moment to listen to this video,there is wisdom in the guy,i thought tinathera pa Chilima but the guy is a genius.

  • @user-nq9bg8zo4v
    @user-nq9bg8zo4v Před 21 dnem +1

    Ayime uyu we can support him i love this guy

  • @presciouscarlos916
    @presciouscarlos916 Před 12 dny

    I like this way of thinking. Keep up man u have the vision

  • @dyba-x9w
    @dyba-x9w Před 20 dny +3

    UTM leaders this is your vessel

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Před 18 dny +1

    Uyuyu ndi traore wakumalawi may God protect him and make his dream come true for the better Malawi in future

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 Před 22 dny +3

    Information iyitu anyamata tidzuke tiyeni.... powerful eye opener

  • @chrissyamanda5510
    @chrissyamanda5510 Před 22 dny +4

    The Rising of second
    Skc

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 Před 22 dny +2

    He must talk and enlight the youth about pacts and treaties also signed by our government officials behind doors without consult the pple...
    IMF AND WORLD BANK

  • @deusChikhweru-yd7tb
    @deusChikhweru-yd7tb Před 21 dnem +4

    I know this guy anali president, pa NRC ndikatundu

  • @ChamanChataika-jt4ik
    @ChamanChataika-jt4ik Před 21 dnem +1

    I just like the guy's MFUNDO. Ndiwachichepere, koma wamva maitanidwe muutsogoleri wa dziko lino.
    Sikukulamulani aMalawi amnzanga makamaka inu achinyamata, let's give a guy much support.
    Timupatse sapoti yambiri, kuti Mulungu apitirize kumutsegula maso, komanso akhale nawo omuthandiza kukwaniritsa komanso kufikira masomphenya, for the betterment of ifeyo aeni ake aMalawi....

  • @BlessingsEphraimn
    @BlessingsEphraimn Před 21 dnem

    This guy is brave man ,genius ,I second this brilliant idea, I even read a quote from the bible ,"come let us reason together and make one thing" indeed just like Ibrahim Traore 35yrs he is leading BUKINA FASO ,young man 33yrs leading SENEGAL , why not Malawi ? Lets change our Nation with Servant leadership

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz Před 14 dny

    We need this kind of people in to rule our country ❤

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 23 dny +5

    Bwino abusa angakuphe anapha chilima samala m'bale

  • @raphaeljeremiah2692
    @raphaeljeremiah2692 Před 8 dny

    Well articulated, zamveka zonseee izo mwanena bwana. inuyo mwadzina lanu ndinu Khang'adi. Osafooka,,kankhani ndithu,,pang'onopang'ono kwawani mpakana mudzafikapo..Amalawi takumvani

  • @MaryMlongoti
    @MaryMlongoti Před 23 dny +5

    Muli ndi zelu akulu

  • @AncentMtambo
    @AncentMtambo Před 9 dny

    We need his friends too coz he seems to have good friends who can also assist ...

  • @user-nq9bg8zo4v
    @user-nq9bg8zo4v Před 21 dnem +3

    My vote i see someone ukumva kutentha muno

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m Před 23 dny +2

    Munthuyu ndiwa nzeru ndthu ❤even syllabus yathu I wonder generation after generation with the same syllabus ayi szoona izi

  • @FelixMcDonard
    @FelixMcDonard Před 23 dny +4

    Uyoyu ndikatundu woposa wakatunduyo aaaaa ndagoma naye

  • @HEROTHATNOBODYCANCELEBRATE
    @HEROTHATNOBODYCANCELEBRATE Před 3 hodinami

    This man is upful and creative!!.

  • @yollamoscarmw7173
    @yollamoscarmw7173 Před 22 dny +9

    Koma Denis iweyo Mulungu azikudalitsa. That's an eye opener

  • @AustinCMphango
    @AustinCMphango Před 21 dnem +1

    Uyu nde my Vote.Akukamba zondigwira mtima ❤

  • @salafinamhone-rd1ku
    @salafinamhone-rd1ku Před 23 dny +4

    It’s good Juthoka mu chichewa

  • @dominicmphepo-jk8lk
    @dominicmphepo-jk8lk Před 20 dny

    Our own genius
    Well said boss...

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo3525 Před 21 dnem

    This guy realy he knows Economics wow big brains working ahead.

  • @user-ov4cs3lg4g
    @user-ov4cs3lg4g Před 16 dny

    I swear this is the type of people Malawi needs....:: You have worn my heart my guy, vote ndakusungira!!

  • @Benty_Pro
    @Benty_Pro Před 6 dny

    Dolo Kwambiri... I like his way of thinking

  • @omarkatona3389
    @omarkatona3389 Před 20 dny

    Very constructive ideals of the national transformation for the betterment of all.Much interested in educational part.Indeed education can be another form of slavery.The only mindset to embrance as a nation.Much thanks to u brother for ur courage.

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q Před 8 dny +3

    This young man I respect him
    Let's Support him please 🎉

  • @GodfreyMajomeka
    @GodfreyMajomeka Před 17 dny

    So much wisdom in his sayings and needs much support for this thinking to be fruitful ..azungu anatipweteka 😢