KAMLEPO KALUWA BOMA ZOMWE MUKUFUNA KUPANGA NDIKUDZIWA

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 10. 07. 2024

Komentáře • 49

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe Před 20 dny +5

    Uku mkuchikweza amputa olakwika, voice imeneyo ikumveka mwa simple koma ili fire😊

  • @user-ux8bc6wy1i
    @user-ux8bc6wy1i Před 20 dny +6

    Even neba ku Zambia they know that we don't have president in Malawi

  • @wittinessnkhokwe
    @wittinessnkhokwe Před 20 dny +6

    Inu a mcp nenani kuti tonse amalawi tichokemo tifune kolowela muone kuti mudzilanulira ndani?

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki Před 20 dny +1

    Mr Kaluwa i appreciate you,,,you a true gentleman a hero,, if it takes you to go back to your past to resolve this chakwera issue so it be,,

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před 20 dny +3

    You have to take this Government to court for this damage.

  • @HenryLaidon-pl9ly
    @HenryLaidon-pl9ly Před 20 dny +3

    Guys Kamlepo ndi One of True democrat ku Malawi kuno tsopano kodi kuzunza mukumuzuza munthu wobweretsa democracy koma kokoliko ndalama zamisonkho yamphawi zakomadi

  • @luuu22mwanjabala79
    @luuu22mwanjabala79 Před 20 dny +3

    Wise man from the North side

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Před 20 dny +1

    Bora ilili tikachotsa chakwera a police ambili akuyenera kuchotsedwa tchito

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 Před 20 dny +2

    Well said, loud and clear

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 20 dny +2

    Wise man mr kamulepo ❤❤❤❤❤

  • @user-zy2nh4lj4h
    @user-zy2nh4lj4h Před 20 dny

    Zinazo muzipanga koma za artist fredokiss mukangoesera 😮 malawi tiyatsa mukangopha fredo achinyamata tifafaniza state house

  • @JamayakoJamayako-rv2he
    @JamayakoJamayako-rv2he Před 20 dny +1

    Am agreed with you
    Pipo shud open their eyes
    Wise man

  • @brendamakokola7498
    @brendamakokola7498 Před 20 dny +1

    Politics is dirty game

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr Před 19 dny

    Chomwe wachiona wankulu atakhala pansi, mwana olo atakwera mumtengo sangachione. Welcome Big

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w Před 20 dny +1

    Ndikatundu ameneyu aboma musamutengele masewelo zomwewakambazo ndizoona ndithu

  • @chipilirokalison1334
    @chipilirokalison1334 Před 19 dny

    Sizitheka mulungu alipo kumwamba osamara

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b Před 19 dny

    Amenewo ndie mawu amphamvu mbuzi za police zogwilisidwa ntchito ndi chikangawazo makape amenewo akuti agulidwa ndi mcp gvrt Makamaka mai yolamu nayeso chipawa chosamukhala mutu chija mbuzi ya munthu aziwona makape amenewo mu 2025 wonsewo akathela ku mawulapalibeso kuwakhululukila inshaAllah

  • @JameChome
    @JameChome Před 20 dny

    Ask Bakii Muluzi anamtangwanitsa kooopya 😂😂😂😂😂

  • @NescotNyamwela
    @NescotNyamwela Před 20 dny

    Ine president wanga ndi Dad Bingu wa mutharika kwa ine sanafe i can see kuti anapanga chani. Kma mbuz zinaz zimangozuza amalawi osalakwa anyway sindili ku malawi kma home is best mbuziyi izaziwa kazachopa pamwambapo

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr Před 20 dny +1

    Boma iliri azitsogoleri mitu sikuyenda bwino why still keeping cellphones of Born kalindo and kamlepo why why Malawi President and the Police why can you please change your decisions why.

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 Před 20 dny +1

    Aputa olakwika tu....

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf Před 20 dny

    Oh no osat Fredo ayi.Komano kukhetsa Mwazi chifukwa Cha mpamdo Kaya Mulungu amaona amakantha

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b Před 19 dny

    Apolice yakhani kuti umuyaya uja udakalipobe kapena ai?

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 20 dny

    Collect your phone via the attorneys and high court on releasing it without prejudice and bias. We are praying for you. Ndine kuno ku Great Britain. Yes the late dad Green Ng'oma used to w for Southern Bottles even when they lived in Mzimba before moving to Zingwangwa Blantyre and after ZINGWANGWA THEY MOVED TO ALIMAUNDE AREA 25 LILONGWE. We must all pray for each other and the countries experiencing the political tarmoils.

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Před 20 dny

    Mcp ikuyenera kuchoka basi ikuzuza athu osarakwa chakwera wakupha ayende basi

  • @MaxWell-d7o
    @MaxWell-d7o Před 20 dny +1

    Pambuyo panu bwana..iponden

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn Před 19 dny

    Yooo zilichonchoso 😢

  • @mbewemisoyaanenenji1908

    You fought ngwazi , who are these dogs to fear .

  • @IdahNyasulu
    @IdahNyasulu Před 20 dny +1

    Deal with them bwana kalua

  • @zelliachamboto5744
    @zelliachamboto5744 Před 18 dny

    Kulibedi wamuyaya

  • @peterchikwakwa8476
    @peterchikwakwa8476 Před 20 dny

    Pena pache MCP tu , mukuonjeza eti!!?? Is this what we wanted? Why why why??

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw Před 20 dny +1

    Zosaesanda

  • @babranzima8120
    @babranzima8120 Před 20 dny

    Athu akupha abusa wokopha kodi eeeeee athu akumpoto mwasiye mutha ndinu achakwera ndi azanu wood

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri Před 20 dny

    Amen Amen...

  • @CharlesKachipanda-jz9jv

    Awuzeni makapewa adziwe kuti inu madala madala

  • @user-ss9bj5eh6b
    @user-ss9bj5eh6b Před 20 dny

    chonde bwelerani muzakale bwana tithane nawo anthu oipawa

  • @ShorayChimera
    @ShorayChimera Před 20 dny

    I feel ur pain father 💔

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 Před 20 dny

    Good 👍

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před 20 dny +2

    😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @AgnessMzengo
    @AgnessMzengo Před 19 dny

    Iponden fadah,,,,,

  • @user-kp7le2pu7h
    @user-kp7le2pu7h Před 20 dny

    Wise man❤❤❤

  • @user-fq4kv8dj4t
    @user-fq4kv8dj4t Před 20 dny +3

    Mwaonjeza English enafe sitimva nde izizo muzilankhulako chichewa chifukwa nzatonse amalawi kuti timve

  • @Standwell78
    @Standwell78 Před 20 dny

    Chana?? Ayesele

  • @MagaLassi-tg7lj
    @MagaLassi-tg7lj Před 20 dny

    🆓✊

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před 20 dny

    Akupa mcp

  • @MilacleSankhani
    @MilacleSankhani Před 20 dny

    Ask late kamazu about u

  • @HamzaMkwanda-bh8dc
    @HamzaMkwanda-bh8dc Před 20 dny +1

    Wise man