Video není dostupné.
Omlouváme se.

KUZUKUTA NKHANI ZOMWE ZACHITIKA.UKU KWATENTHA 🔥🔥🔥🙌🙌

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 25. 08. 2024

Komentáře • 100

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Před měsícem +12

    Mukaona munthu akuti MCP my vote ameneyo ndi wa family ya chakwera mwina ndi ankolo ake kapena chakwera anakwatira pakwawo which means phindu la chakwera akuliwona ameneyo wachita zolozeka kwawoko

  • @macdonaldmunthali9895
    @macdonaldmunthali9895 Před měsícem +9

    Very wrong decision,the end of utm.chilima was the only leader with great vision and calmness, you can't make decision out of anger.

  • @user-nc4vi1jt5g
    @user-nc4vi1jt5g Před měsícem +3

    Kabambe afunampando ku utm koma autm samalanaeni mtsogoleli wanu autm sankhani kaliati ndiponso pamasankho adzawina anthu tilinae ndichikhupililo enawa tawaesa akanika

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem +1

    Nkhani ndiyomweyo mwamva bwino zikomo kwambiri pamibawa.. God bless you two guys... Mamakutu wava koma wopanda makutu mawa wazakuwawani

  • @lifayohbenson1994
    @lifayohbenson1994 Před měsícem +3

    Ku utm kulibe mphungwe mpungwe
    Winayo chipani chake ndi odya zake alibe mulandu

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Před měsícem +1

    Anapha dala chilima cholinga anthu abalalike koma mulungu ndiwadongosolo a utm osafooka osatopa osaopa

  • @SharifChibwana
    @SharifChibwana Před měsícem +5

    Bakili Muluzi tv ndi katundu

  • @user-nv3rf7bl7r
    @user-nv3rf7bl7r Před měsícem +2

    Uku nde kuyankhula kopanga umodzi that's y ndimakukondani amibawa chifukwa mumayankhula chilungamo

  • @DavieChiwale
    @DavieChiwale Před měsícem +1

    Apa a UTM Mukapanda kumva zanu izo

  • @PeterTembo-zj5jk
    @PeterTembo-zj5jk Před měsícem

    Dpp moto❤❤❤

  • @ManzyNgoleka
    @ManzyNgoleka Před měsícem

    vuto inu akulu mukukocha ndale mwachidule nanu mulikuseli kwa enaake

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g Před měsícem +2

    MCP my vote ❤❤❤❤❤❤

  • @JazzdMonga-v6e
    @JazzdMonga-v6e Před měsícem +1

    Kumupeza wina akuti mcp my vote
    Amalawi ndichani

  • @BillyMhone-jp3kn
    @BillyMhone-jp3kn Před měsícem +2

    Khondo Yochita kutiponyera Mcp kumupanga usi
    LET HIM BE THERE WILL MAKE CONVENTION SOON

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před měsícem

    Aaa manganya ngati mutu mwake dziyendamo bwino ayi musiyeni ku MCP koko afela nayo limodzi

  • @VincentMbeye
    @VincentMbeye Před měsícem +1

    Yalakwa UTM kuchoka msanga ....awonesa umbuli kwambili

    • @Aqiec09
      @Aqiec09 Před měsícem

      Ndipo usavage wa athu ophunzira umakhumudwisa

  • @daviskamonde4882
    @daviskamonde4882 Před měsícem +2

    Don't lie to us.
    You support MCP.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem +1

    Njawala number one, kaluati number two be careful ndi anthu awiriwa ndi anthu oyipa mutima kwambiri
    We love utm kwambiri koma isakhale ya munthu

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před měsícem

    Zoona zake anganidze mofasa sure ❤❤❤❤❤

  • @JaphetSakala-pq4fl
    @JaphetSakala-pq4fl Před měsícem +2

    UTM motomoto osadandaula

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Před měsícem

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @TonykalicheloKalichelo
    @TonykalicheloKalichelo Před měsícem +1

    Inu ngat mwin wake amafuna kusazika ndiye mukufuna omusatila atan

  • @lyiemax
    @lyiemax Před měsícem

    Proper narration, big up guys ❤❤❤

  • @RegistermoseskashonKashon
    @RegistermoseskashonKashon Před měsícem +1

    Inu nde munabwela kudzauza amalawi tchutchutchu osat akapilikon enawa ongokamba zinthu zopanda kumutu

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z Před měsícem +2

    Mwawathandiza ulemu

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl Před měsícem

    Skc ankafuna kutchoka after kusalemekdza mgwirizano omwe unalipo ndiyeno kutchoka it's a good move komano to agree with ndikutenga mnthu kunja that's wrong indeed

  • @EdsonNjonjo
    @EdsonNjonjo Před měsícem +1

    Munthu uyu akunena zoona

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Před měsícem +5

    Athu akuda ndife opanda nzeru

  • @OsmanMasamba-ck4mo
    @OsmanMasamba-ck4mo Před měsícem +1

    Manganya iwetu wagulidwa ndichisilu chinzako

  • @FloraBanda-w7t
    @FloraBanda-w7t Před měsícem

    Koma selina 😂😂😂akut kod akabambe akulowela kut 😂😂😂😂

  • @user-ux9ik4zr5x
    @user-ux9ik4zr5x Před měsícem

    Probably the best program

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Před měsícem +1

    Ndibwino kt atengane okhaokah

  • @StevieTaiza-r9j
    @StevieTaiza-r9j Před měsícem

    Mulungu azikutete bro

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Před měsícem +1

    Akumatibera zathu zomwezi zamisokho

  • @EstherManda-ex3bc
    @EstherManda-ex3bc Před měsícem +1

    🤣🤣🤣🤣 nkhani zake

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 Před měsícem

    Yea that's very true and I see it ku utm utsogoleri unali wa chilima ena onsewa mavuto bola ku MCP komweko mudziwa bwanji mwina the death of chilima was planned with those who are on top blaming MCP for the death yets amafuna mpando wachilimawo why so early kutuluka mugwilizana without solid proof that is MCP guilty , ine unless pa social media muzabwerese real proof how you saw the killing happen that's when I will find them guilty

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nw Před měsícem

    Njawala ndi kaliati mutiwonongera chipani chathu ndakwiya Nanu heavy kuno kuntheu mutisamale awirinu

  • @Ishriss1999
    @Ishriss1999 Před měsícem

    Ma prophet watu koma atilankhilitsa pambali mxiiiiew

  • @mzeewandembonyirongo2972
    @mzeewandembonyirongo2972 Před měsícem

    Gwende u have fairly advised

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Před měsícem

    Kkk😂😂😂😂😂😂😂😂 anzanga afumu owuka

  • @SabinaNkhoma-sf7kz
    @SabinaNkhoma-sf7kz Před měsícem

    Mmmmm km mcp yaonjeza,zot amalawi akuvutika sakuganizako

  • @user-rx7cc7tc6b
    @user-rx7cc7tc6b Před měsícem +1

    MCP 💥💥💥❣

  • @GiftKaunda-f8j
    @GiftKaunda-f8j Před měsícem

    Analysis yanzeru zozama koma imeneyo?

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Před měsícem

    anthu atamalankhura ngati mmene ukuyankhulira lweyo anthu akhoza kumachitazinthu mwanzelu

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha Před měsícem +2

    Mcp ya wina kale

  • @user-he5ol5or7f
    @user-he5ol5or7f Před měsícem

    Gwede is the best

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 Před měsícem

    Nduna zomwe zikugawa ndalamazo akumatibera misonkho yathu yomweyi...ifetu maso athu tikuona ndipo tilankhula chaka cha m'ma chino....40million plus just for one meeting business yanji imene akupanga? Apapa zaonekeratu kuti andale amatibera pomwe anthu akufa ndi njala. Ambuye akukuonani ndithu

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Před měsícem

    Pamaliro wandale athamangitsidwe

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Před měsícem

    😢😢😢😂 ozuka kumandao
    Eeeeee kusokonezatu kkkkkkk

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Před měsícem

    First to comment

  • @MasaukoNyirongo
    @MasaukoNyirongo Před měsícem +1

    😂😂😂😂😂😂😂 koma zinaz abale kkkkkkk kuthamangitsa masiket mudzi kkkk

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Před měsícem

      😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂Koma abale

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Před měsícem

    Kuwechetamwangajimbilambali

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Před měsícem

    Aaaaa
    Malawi

  • @ZioneMkangadzula
    @ZioneMkangadzula Před měsícem

    utm igawana zida zafikapa angonamizana

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Před měsícem +5

    MCP 🔥🔥🔥🔥

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Před měsícem

    Umakwana

  • @PociahMack
    @PociahMack Před měsícem

    Kma nkhani ya a pro andiseketsa bwanj😂😂

  • @PhiriChitani
    @PhiriChitani Před měsícem

    Ndinu a Mcp chokani apa mukuyiwala kuti UTM idayamba yokha without mcp

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Usi ndi munthu yimodzi yomwe mwini wa UTM

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Před měsícem

    Kugawa ndalama Koma ma servants ndee ka salary ka mmanja

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke Před měsícem

    As government I think abalalika ndithu

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Před měsícem

    vuto amalawi timasapota vitsilu kali ndi ........

  • @user-gk4nu4xr8r
    @user-gk4nu4xr8r Před měsícem

    Of course

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Před měsícem +2

    akuononga chipani cha utm ndi mai kaliati ndi azao filex njawala anthu awawa ndithu amaliza chipani cha utm samalani

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda Před měsícem

    Ntchindi mulije mu utm

  • @user-kj7hr2jf1l
    @user-kj7hr2jf1l Před měsícem +1

    Zowona utm yisatenge munthu wakunja

  • @atupelemposa4786
    @atupelemposa4786 Před měsícem

    😂😂😂

  • @MayesoKulea-sh8xd
    @MayesoKulea-sh8xd Před měsícem +2

    MCP ☑️

  • @YohaneMotison
    @YohaneMotison Před měsícem

    😂😂😂😂😂😂

  • @PulayaKalaka
    @PulayaKalaka Před měsícem +1

    Mcp mooootooooooooo

  • @user-cb5gh9md4i
    @user-cb5gh9md4i Před měsícem

    Kodi ntchentche zikutanipo pamibawapo

  • @YamikanAbubakary-my4ie
    @YamikanAbubakary-my4ie Před měsícem +1

    Ambuye mulungu daritsani chipani cha mcp 🇲🇼❤️
    🙏🙏

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Před měsícem +1

      Ndiwe opembedza mafano
      Mulungu wa Abraham sangadalitse MCP...siwachisokonezo ngat Chakwera wakoyo...usamutchule Mulungu pachabe...ungaone tsoka

    • @user-px6kt8rx2p
      @user-px6kt8rx2p Před měsícem

      Ukunama ukadakhumudwa mcp chiyembekezo cha Malawi ambiri

    • @robertkalima874
      @robertkalima874 Před měsícem

      @@user-px6kt8rx2p MCP chipani chafuko

    • @SamKaposa-i5c
      @SamKaposa-i5c Před měsícem

      Usatchule dzina lamulungu wako pachabe chome iwe

  • @MosesNanchinga
    @MosesNanchinga Před měsícem

    Ma comment onsewa bwanji simukukamba za ndalama ai kma UTM sinalakwitse kuchoka ku alliance coz sanalandire ulemu uku ku MCP atizuza ndlmazo mukukanika kugulira mankhwala zipatala bwnj

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus Před měsícem

    Abwenza ndalamazi...eni ake akutuwa kusowa sopo...akuoneka a fumbi lokha lokha km ena akuononga mosaopa Mulungu...ayi tiona posachedwapa....nafe tikudikira

  • @AdenaGuest-g4b
    @AdenaGuest-g4b Před měsícem

    Aaaaa
    Malawi