Inutu ngt mumadziziwa kt ndinu a MCP ndibwino musamamvele Za born kalindo,chifukwatu tsiku lina mudzagwa ndi BP,ngt likumulephera boma nde kulibwanji iweyo????
Ngat utm inatuluka mu mcp pali chifukwa chani chovalirira makaka pa musonkhano wa mcp. Zimene zinapita kukalandira president ndi makaka a utm ndi zisiru zipanda zeru sizikuziwa kuti uku ndi kwa mcp uku ndikwa utm sizikusiyanisa. Or usi asavareso makaka a utm
Palibe zogulitsidwa! Zikuchitika ndi Manganya ndi propaganda ya MCP. Koma ma supporter a UTM enieni tili nganganga pambuyo pa UTM ndi Kaliati. Team iri ku MCP yo ikhale komweko
Aise Kalindo umandiwaza ndi nthabwala zako. Please keep up the good work ya nthabwalazo- the DC mwana oopsya kwambiri kkkk. Bwanji osangonena kuti umafuna UTM ipite kwa Adadi? Come on man be honest...kodi zakuwawa eti? Nobody should be mad at Kalindo because he's a funny dude.
Kupita Ku msonkhano wa MCP doesn't mean uzavotera MCP Mr kalindo aaaaaaaaahh,,,aja anapita Ku convention ya DPP ali mu makaka a utm,afford,why smunanene kut ndi a DPP??? Nde palibe chifukwa wa utm kupita kokalandla chakwera coz vote Nd mtima nde musasegule nazo mmimba..
A DPP adadi Anu amene ananena kuti ovotera MCP amwa mutnjani KOdi amawauzao ndi a Malawi?olo ndaku Mozambique?a Kalindo misara yakulisa yendani ku Mental
a DPP UDF UTM AFORD ndi onse enanu tengani zimene akune bon kalido seriously if not then you are finished completely and forget to be in government in 2025
UTM and Kaliati has no money to run the party. If MCP is funding UTM, let them help UTM an alliance partner. Dr. Kabambe has 50 followers in Thyolo, considering his last rally. He doesnt have money either. Its Utsis camp through MCP n Mary that have money.
Kabambe has money...only that is relatively new in politics and giving out money is not his taste. In UTM Kambala is doing everything by himself. Imagine the whole top guys beg fuel money from him. Money as less than 300, 000 kwacha. They want him to pay. They the rest are not contributing to the party. And seems Kambala is tired. He is being told kuti zabwino zikubwera soon😮
Bwanji tinene kuti IWE CHILUNGAMO NCHAKUTI ndiwe munthu WA NSANJE kwa anthu amene si a Ku Mulanje or Thyolo. Correction. Iwe SI PRESIDENT WATHU ayi. I we ndi president was anthu 50 amapanga ma demo timawaona aka. Kkkkk NSANJE. KKKKKK
Mr DC, watching you live from dar es salaam, Tanzania.just wishing you a very great Sunday, keep on doing good job.
Bwanji manganya asiye utm please
Kalindo wabalalika kuno!!!!!!! This is the game of politics
Wabalalikadiiii kkkkkk
Restening from cape Town pa boma❤
Osasunga legacy iweyo bwa
Akufuna aku banja aziwadyera..ndrama
Yudas anali ophunzila wa yesu , komanso yudas anamugulitsa yesu ,
History is the best teacher .
❤❤ zomwe amayankhula uyu ndi zeni zeni and zikuchita kuwonekelatu
Inutu ngt mumadziziwa kt ndinu a MCP ndibwino musamamvele Za born kalindo,chifukwatu tsiku lina mudzagwa ndi BP,ngt likumulephera boma nde kulibwanji iweyo????
Mumakwa adala
My president
First to watch
Kukunyadilani
Thanks 🙏
Kalindo drama amatha go ahead we will keep roughing kkkkkk
Usi ndimuthu oyipa kwambili mm ndiapo anamupereka chilima
DC
Mwati M C P ndi yazibekete 😂😂😂😂😂😂
Iwe Kalindo zangokuvuta kkkk you’ve met your match in Jesse Kabwira…..munatumbwa kwambiri pakatipa nde pano mutsegula mmimba simunati 😂😂😂
Kodi Jessie Kabwira ndendani?
dzeru palibe
Dziko la Malawi Lili pa mavuto eeti eeeish 💔😭 which means will be in trouble forever
Ukufuna tiziyendela.maganizo ako ulapa
Inenso munthu uyu ndimamudabwa akayankhula zambiri zomunena chilima pano wafa ..akuonetsa ngati iye amamkonda mmm Ada Inu mdziwen Yesu kusanade...vuto anakumanan udindo..mwamutukwana peter eeeee pano ukutinso peter ndiwabwino😮😮😮😮
Kalondo ife MCP timayikonda enafe zokamba zako sizimatisangalatsa ai
Nkalindo bwanji mullipo mulinkut bwanj malipot andege ankushedwaso after too months guys shonde bk TV mtanyiwwa
Let's admit that politics has become a global problem
We salute you our president
Ngat utm inatuluka mu mcp pali chifukwa chani chovalirira makaka pa musonkhano wa mcp. Zimene zinapita kukalandira president ndi makaka a utm ndi zisiru zipanda zeru sizikuziwa kuti uku ndi kwa mcp uku ndikwa utm sizikusiyanisa. Or usi asavareso makaka a utm
Ndiwe wachipani chanji iweyooo
Palibe zogulitsidwa! Zikuchitika ndi Manganya ndi propaganda ya MCP. Koma ma supporter a UTM enieni tili nganganga pambuyo pa UTM ndi Kaliati. Team iri ku MCP yo ikhale komweko
Dc
Kalulu mwale from jonz D C tiyenaoni ambalame amenewa
The DC great
Aise Kalindo umandiwaza ndi nthabwala zako. Please keep up the good work ya nthabwalazo- the DC mwana oopsya kwambiri kkkk. Bwanji osangonena kuti umafuna UTM ipite kwa Adadi? Come on man be honest...kodi zakuwawa eti? Nobody should be mad at Kalindo because he's a funny dude.
osati nthabwala koma zoona
First comment ❤
Mumakwana
Thanks
l like u born
Zomvetsa chisoni kwambiri, may the spirit of SKC do something on this bad move
Zoona
Kupita Ku msonkhano wa MCP doesn't mean uzavotera MCP Mr kalindo aaaaaaaaahh,,,aja anapita Ku convention ya DPP ali mu makaka a utm,afford,why smunanene kut ndi a DPP??? Nde palibe chifukwa wa utm kupita kokalandla chakwera coz vote Nd mtima nde musasegule nazo mmimba..
Maganya ayakhule za 5 years tione pomwe uziwe kut siwa utm
Inu mwaoneka kale vote yanu munama kuti ndi mtima bwanji
Wamisara wamisara wamisara zindikiran nose mumatsata citsiru ici kt ndiwamisala watsara pang'ono kuyamba kutora zinyatsi uyu kkkkk
Iweso ndekuti ndiwamisala bwanji ukumutsata?
No logic why kuveka anthu ma t-shirt yet you know kuti ndi anu kale kkkkk . Aaaaa kulowerera za catholic Kkkk fotseki
Chapompano uyuyu uyu tipita naye ku mental
Ndale ndi choncho
Mbava zaba Chipani cha SKC
M matiimiliradi man
True
Akalindo agwira pambali
Warira mokweza kunooooo 😂😂😂😂
😂😂😂😂 mukharise a president anthu anthu aanthu osauka mumatipasa chirimbikitso ndipo timakhurupirila kuti tsiku rina tidzadyera nyama ndipo dima ungakute bwanji kunja kudzawara dzuwa ridzaomba Bon karindo woyeeeeee, timakutsatani ngankhare tiri kutari ndi dziko ra malawi🇲🇼💗
Amene mekuyankhulanu mukungofuna ndalama ife anatinyasa kale mtambo
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxiwa pa ifa ya chilima
A DPP adadi Anu amene ananena kuti ovotera MCP amwa mutnjani KOdi amawauzao ndi a Malawi?olo ndaku Mozambique?a Kalindo misara yakulisa yendani ku Mental
a DPP UDF UTM AFORD ndi onse enanu tengani zimene akune bon kalido seriously if not then you are finished completely and forget to be in government in 2025
Ulemu wanu bwana Kalindo
Tge DC booooon kalindooooooo mwana owopsyaaa kwambiri
Choti muziwe adale simuzatheka mpakana kalekale ifetinakuziwani
Mr DC sizokanika kung'alula apa ai popeza ndimzanu manganya nenani kuti manganya wagulitsa chipanichi ku MCP ndipo akunama kumwamba Mulungu aliko angoutsa mkwiyio wa Yehova chabe mapangano akeo ndiopusa akuganiza MCP ingakamupatseso u vice president 2025 ndi munthu omvetsa chisoni betrayer
Kalindo wayamba kulila kuno imeneyo ndiye politics kkkkk
Iweyo mesa chili a umamunyozaso lero ukhale ngati umamukonda chili a wosokoneza iwe
Mmmm zabodza izoo
Aliyese akunena zakuti awina wabalalika kalindo😅😅😅
Dziko kuwonongeka chifukwa cha dyera, ndalama.
This. was already planned before. chilima was killed
Awuzeni anthu azipita kumunda si nthawi yochemelela zipani iyi. Inu ndi amene mumabweletsa njala every year
Kalindo, you don't have evidence you are just making pipo to fight
Wamisala anaona nkhondo
No ways....anthu ogulidwa ndi Manganya amenewo not real SKC followers
Koma akalindo pumani kaye pathe mwezi umozi nkhani yikuwoneka kuti yatha mumutumo ndiye mukhale kaye cheti muzitipasa nkhani zanzeru ndiye kuti aroma alowelerepo kodi UTM ndiya roma koma munthu uyu
A Mr kalindo ingojoinani ndale chifukwatu mmm zomenyera ufulu zakukanilani ndithu sizikuendapo
No utm singathe utm yeni yeni tikuyidziwa
The DC😂😂😂
Munthu amene angavala zovala za utm koma ali wa chipani china magulu ake ali ngati iweyo the DC
Or atagula sitingavotele awa akanganya awa
Ndare ndi Mabozatu
Pitilizani bwana
Inu munapenga palibe zazelu mungakambe
😢
Eee
apita okha ku chikangawa ife tidangoyikonda utm but the moment they join mcp ife tonse ku dpp basi or atangura anthu 200 ife tikukawinisa dpp
UTM and Kaliati has no money to run the party.
If MCP is funding UTM, let them help UTM an alliance partner.
Dr. Kabambe has 50 followers in Thyolo, considering his last rally. He doesnt have money either.
Its Utsis camp through MCP n Mary that have money.
Kabambe has money...only that is relatively new in politics and giving out money is not his taste. In UTM Kambala is doing everything by himself. Imagine the whole top guys beg fuel money from him. Money as less than 300, 000 kwacha. They want him to pay. They the rest are not contributing to the party. And seems Kambala is tired. He is being told kuti zabwino zikubwera soon😮
Bwanji tinene kuti IWE CHILUNGAMO NCHAKUTI ndiwe munthu WA NSANJE kwa anthu amene si a Ku Mulanje or Thyolo.
Correction.
Iwe SI PRESIDENT WATHU ayi.
I we ndi president was anthu 50 amapanga ma demo timawaona aka. Kkkkk
NSANJE.
KKKKKK
Live show
Akalindo zipitani chabe ku DPP uko
Manganya wagulisa chipani cha UTM kung'ona
Maganya munthu oipa
Mukuva kuwawa man
❤❤❤❤
Zakeyo
Awanso mutu wamaminawo
ⁱᶠ ⁱᵗ ˢᵒ ᵗʰᵉⁿ ᵗⁱᵏᵃᵛᵒᵗᵉʳᵃ ᵉⁿᵃ
A MCP ndi mbulidi zoona, sasiyatsa za boma ndi chipani, mai awa azitengela pa mgong'o.
@@user-pv9uk6sc3w Inuyo mukamayankhula ntudzu mumasiyanitsa ?
Ndipo mbuli ndiyeyo
Mumatha inuyo bwana
Za chamba zokhazokha.
First to watch