Welcome Dr George Thupuwela Chaponda as leader of opposition. Your opposition leadership reminds me of the old good days of Mbuya Gwanda Chakuamba as leader of opposition in Malawi. Kudos and bravo to your team Dr George Thupuwela Chaponda otherwise we have wasted good 4 yrs of opposition duties under Kondwani Nakhumwa (from 2020-2024). The past 4 yrs was just useless and waste of time. God bless malawi and God bless the leadership of opposition in malawi.
Mwachepa , MCP is a very big party. Munachipeza chipani cha MCP ndipo muzachisiya chili even stronger. Inu muzingokhalira kulongolola ngati ntchentche zikusangalalira manyi.
We can confirm Kuti Kondwani uja watitayisa thawi Kwambiri. Kususa kwake kukanakhala ngati Kumeneku zinthu i hope zinthu zikuyenda bwino kwambiri and Malawi sakanaonongeka ngati m'mene waonongekelamu. Komano MCP they make mistake kumuhonga Kondwani kuti asamawasuse koma azingopanga zinthu m'mene angathele and the end zawagwesa m'mavuto and the result no more kulamulila they are finish!!!!!!
Alone gadama...dicki matenje...twaibu sangala ...achiwanga... Sadiki Miya... Albert muwalo.. Alani witika .. saulos chilima.. and 8 others...my question is..how many people did MCP killed all together?? chakwela what is your problem??😭😭😭😭😭
Andale nonse zanu ndizimodzi. Panopa kwakucherani mdziputsitsa amalawi. Nonsenu simukonda dziko lino. You are just power hungrily. Mkavoteredwa basi anthufe mwatisiya. Nonsenu ndinu akapsyala. Panopa ndipo mwaona ubwino wa Chilima ndi UTM?
Anthu angapo takhala tikudandaula nkhani ya ka sound kamamveka pansipo koma simumatimvera bwanji??munanena kut mwamva koma mpamene mwaonjezera volume,,,why?!
Exactly this is their own problem ukukudi kuyake Moto, they are taking us for granted, ku trip kopita president koma akumachita kutenga gulu for what and which Money are you using kukusa anthu onsewo wokakwela ndege, for what, and what will some of the people going to do there,,this is unacceptable they can't embazzle our Money Infront of our nose, Enough is Enough
I would like anthu monga hon :suleman,jean ansah,Mr kaluwa kuti akhale ndi ma udindo akalu akulu ku DPP party I hope anthu ngati awa they can change life of malawians including Mr president author Peter wamutharika and hon :namomba ndi anthu olimba mtima kuteteza life and situations of poor malawians anthu monga ine omwe tili kumudzi
Chakwera kuyendayenda ndi m'mene ziriri kumlw sikoyenera But I don't blame him coz he do knw what he's doing and he is the state president without knowing the meaning 😢😢😢
I agree with mmwenyeyo wa BT ku 2025 kwatalika kwambiri anthuwa achoke basi atikwana chisankhoso chisakhaleko ayi chifkwa aluza kale
Yomweyo a DPP apa mukubwera boo
2025 kwatalika adzipita dzikoli litha ngati ma curtains
Ambuye alemekezeke kuti sopano tili ndi opposition ku parliament, hopefully zinthu zisintha sopano,,wow!!!am very happy for that
Llg meet😮 hi bed x BBC l
😅
Jinx😅v😊
V😮😢 job
L
🎉
😅
Lv😮bh.ln.😅
Am happy for u all guys this is what we call patriotic leadership 💪💪💪
Amene amapangisa kuti opposition ikhale yofooka anali nankhumwa uja chifukwa anali mnthira kuwiri
Fire fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mademo achitidwe ndipo chikangawa aona polekela
Zikatele mademo ali pafupi ❤❤❤
Sammeeir sagawa masiwiti
Uyu ndamuziwa mochedwa 😂😂😂 alibwino kwabasi nasaaa
Ndipo mr samy ndi one ndipo amaimilira amalawi
Ndipo Man osatekeseka
Anthu akufunika ku Malawi kuno nd amenewa
Very powerful man
❤❤ God is good bolako tili ndi anthu akutiyimilira a DPP musatope and musasiyile pa njila god bless you all
Nanu pangani mademo mesa nawo analowela mademo omweo aaaaaa
Nkhani yabwino ma MPS athu, tonse tikhala pansewu mademo basi.
DPP congratulations apa ndiye mukuonetsa kuimila a malawi
Ndipo apitilize a DPP adziwe kuti dzikoli ndi la a Malawi si la achewa okha ayi
Palibe Za kuyimila amalawi DPP chipani choipa kwambiri
Zako zmenezo 🥱🥱@@LukaThawe
Tiyeni kumademo. Chakwera asatuluke kupita ku China.
Welcome Dr George Thupuwela Chaponda as leader of opposition. Your opposition leadership reminds me of the old good days of Mbuya Gwanda Chakuamba as leader of opposition in Malawi. Kudos and bravo to your team Dr George Thupuwela Chaponda otherwise we have wasted good 4 yrs of opposition duties under Kondwani Nakhumwa (from 2020-2024). The past 4 yrs was just useless and waste of time. God bless malawi and God bless the leadership of opposition in malawi.
I agree with Sameer Suleman this Manyaka Government ( Mcp) must go we are tired of this nonsense 4sec Chikangawa
Mwachepa , MCP is a very big party. Munachipeza chipani cha MCP ndipo muzachisiya chili even stronger. Inu muzingokhalira kulongolola ngati ntchentche zikusangalalira manyi.
@@tasmania527chikangawa oyeeeee😂
Sulemani ndi zungu musaiwale zungu amanena chilungamo koma bodza amadananalo. Ndibwino kuvomeleza kulakwa kenako anthu amakukhululukila. Well done Mr Sulemani, DPP my Vote ❤
Chikangawa he must go
Good message guys Chakwela you mast go watikwana
Kodi zikuvuta pati kunena chilungamo,kaya ndizaboza anthu adziwe choona
Simunamve kuti report atulutsa ndi aku germany?
Athu akuziwa kale chilungamo kodi muthu akakhala mfiti amavomera?kuma voti basi next year
@@dilmayankam4052 Kwatalika amwene tiyeni tivote next month
Much appreciate to the leader of opposition
Akuziwa kuti chilungamo chinaziweka kare kuti anachita kupha anthuwo nanga akurephera kubwere poyera bwanji anthu amatopa ndiye ndatopa
Game changer,ndipamene pati paonekele khoswe pa sindwi.Opposition timayembekezela koma imeneyi.
Ku dpp kuli ma shashanso kani,,keep it up zawavuta a MCP
😂😂😂😂❤
AmasingorA joker kkkkkk🔥
Pamademopo pali bwino 😊😊izi zikuchitikazi zopusa srs
We can confirm Kuti Kondwani uja watitayisa thawi Kwambiri. Kususa kwake kukanakhala ngati Kumeneku zinthu i hope zinthu zikuyenda bwino kwambiri and Malawi sakanaonongeka ngati m'mene waonongekelamu. Komano MCP they make mistake kumuhonga Kondwani kuti asamawasuse koma azingopanga zinthu m'mene angathele and the end zawagwesa m'mavuto and the result no more kulamulila they are finish!!!!!!
100%❤❤
We need report out,,,,
Refreshing to see the opposition at play follow through on issues to logical conclusions. Checks and balances is your duty. #Malawi 🇲🇼
Kukanika kutulusa LIPOTI LA NDEGE 😂😂😂... Afiti 😅
Mr chaponda job well done, siza Nankhumwa zija ayii
2025 is far guys duleni ma battery mr chikangawa yooo 😂😂😂😂
Keep it up ma honorable ❤❤❤❤ this is what we called opposition
Anaba boma ndi ma demo achokanso ndi ma demo omwewo ndipo masatana amenewo akazangochoka mmboma azafinyidwe mpaka azabweze ndalama za misonkho yathu ndipo azafe imfa zowawa kwambiri naonse anthu oyipa amenewa
Nice one thanks so much keep it up please
Let the government know that as citizens we will not sit while they are abusing our patience. we will go in the streets till the recind
Achakwera ndi munthu ouma mtima alibe chifundo ndi umphawi womwe amalawi akukumana nawo
Nchifukwa chake Tembo adamusankha.adamuona kuti ndi oipa mtima.alibe chifundo ndi munthu.akungoyenda opanda chomwe akubwera nacho.
@@user-wx1jt5fd2j U President wu anawutengera mphuzo. Sanatengere kuti a thandize Amayi ayi. Mbuzi ya ku Kasiya
Now we know that there is an opposition....thanks to all opposition parties present here❤❤
Alone gadama...dicki matenje...twaibu sangala ...achiwanga... Sadiki Miya... Albert muwalo.. Alani witika .. saulos chilima.. and 8 others...my question is..how many people did MCP killed all together?? chakwela what is your problem??😭😭😭😭😭
Dpp my vote ❤
Waiting allowance for UTM And Dpp 🥳🥳🥳🥳
Chichewa chikifunika, ife sitikumva
Zoona
Ndipo ku china akukapangako chani chitsiru ameneyu mutu wopanda zeruwo
Thanks our readers these are the checks and balances we craved for... keep up the pressure
Powerful Powerful Powerful mgwilizano❤❤❤❤
More 🔥🔥 DPP kumeneko ndiye kuzuka your only hope for Malawian 💃💃💃
Am in support of Suleiman the guy is saying the truth enough is enough
Chakwela wapha chilima ujha chifukwa Cha udindo 😢
Madem akhalepo akuzolowela asatanic amenewa
Chakwela... silent killer... manipulator... A man with flowery speech without action is called... chakwela...Mr chikangawa
Andale nonse zanu ndizimodzi. Panopa kwakucherani mdziputsitsa amalawi. Nonsenu simukonda dziko lino. You are just power hungrily. Mkavoteredwa basi anthufe mwatisiya. Nonsenu ndinu akapsyala. Panopa ndipo mwaona ubwino wa Chilima ndi UTM?
Kodi akuyendetsa dziko ngati farm yake bwanji hahahahaha you beta resign Mr Pule
Anthu angapo takhala tikudandaula nkhani ya ka sound kamamveka pansipo koma simumatimvera bwanji??munanena kut mwamva koma mpamene mwaonjezera volume,,,why?!
😅😅ndpo inuuu
Akuna mxiwe kt payima ophunzira😂
Kakutopetsa hvy
Ndiye tamuoneni chilima pa mbalipo😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 handsome guy
Anaphela njilu
Ndipo kuvetsa chisoni
Ankayesa zida waonekera poyera Mr Chikangawa ayalulepo watitopetsa atitha mfiti m'busa wakupha chisatana chanyanga
We really needed this kind of opposition earlier on
kondwani Nakhumwa watichedwesa 😢
Kodwani Nankhumwa uja Mulungu amukhululukire chifukwa amanga chija sichilungamo 😢😢😢
I love you mama grace kwelepeta am your child from jokala tc Zomba
Mafuta asakwele plz ndipo anthu otsutsa m'boma musalole makina oyesela mavoti chifukwa mukangolola ndiye kut iyo akhala kut avotelatu ndiye kut mavuto amenewa atikakamila ife tatopa nawo mavuto achekwela
Carry on guys
Kodi maulendo chakwera opita kunja amalawi tikupindulapo chani?
Congratulations DPP, UTM and AFORD now we can confirm that us Malawians we have strong Opposition in Parliament.
Akwedza bwanji mafuta maulendo ali mkati mpaka ku China and America mmmm
Exactly this is their own problem ukukudi kuyake Moto, they are taking us for granted, ku trip kopita president koma akumachita kutenga gulu for what and which Money are you using kukusa anthu onsewo wokakwela ndege, for what, and what will some of the people going to do there,,this is unacceptable they can't embazzle our Money Infront of our nose, Enough is Enough
Good move let's fight together
Kho anatichedwetsa awa nde anthu viva opposition leader
DPP ndi chiyembekezo cha ife a Malawi
In politics nothing happen by accident... when is happening... just know that it is well planned by the way..
Fire up my mpe
This is a good opposition not that time mumangomenyana nokha nokha muja.... Apa nde mwayamba zantchito keep it up
Apm my vote
💪💪💪
Palibe president amene sanayendel
Ko kwambiri I wish Chaponda atiuseso ,mimene adafera Buleya Lure
Mr Chikangawa Bola akanapanda kubadwa
I would like anthu monga hon :suleman,jean ansah,Mr kaluwa kuti akhale ndi ma udindo akalu akulu ku DPP party I hope anthu ngati awa they can change life of malawians including Mr president author Peter wamutharika and hon :namomba ndi anthu olimba mtima kuteteza life and situations of poor malawians anthu monga ine omwe tili kumudzi
Mesa mumazichemelela kuti mafuta ayamba kubwela pa sitima yapatunda ndiyotchipa chakwela wagwila ntchito lelo mukuti mukweze chani kkkkkk munya osalola zoputsa plz akufuna apane amphawi
Simunali mafuta menemuja chimangoyesedwa koma amafuna kunama
Ndipo asatuluse zosephana ndizomwe a malawi akudziwa, coz a natiphera anthu.
DPP yayamba kuonetsa kwaimilira amalawi dzikomo dad❤❤❤
Sitikusewela kumene 💪💪💪
Chi Nankhumwa uja ndamene amawononga dziko,lero mcp yakumana ndi opposition leader yeni yeni
This one is really an opposition leader
Please mukalowa boma groom Denis Mahata aswell he is king game changer
Amwene please tiyen tipange mademo.koma apapa ndiye chaponda ayi takunyadiran zedi osusa, pitilizan kuimira amalawi osauka.
Tazimitsani motowo tikupysa Kono Inu wolemekezeka athu. Tikukutsatirani mwachidwi❤❤❤❤❤❤🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Tikumva kuwawa
I'm here for suleman
Sure Sulyman
Yes please zigawenga izi za mcp zisowe basi
Bon kalindo Ali it agwirane nawo mania anthuwa😢😢😢
Ya asilikaliyo to DRC......ndi fuel from DRC yabaya koopsa
Yes 2025 kwatalikadi, kodi inu osusa munali kuti inu tavutika nthawi yaitari opanda kutiyankhulira ku parliament.
Oposition ija kuno yayamba kuwanvetsa nyunyunyu😂😂😂
Keep the fire burning Suleyman, 2025 kwatalikadi, tiyeni tiwachotse m'boma asatanawa before 2025,
Akanakhala nankhumwa bwezi akungosekelela izizizi
Panopa yayamba kuiwona opposition osati za Nankhumwa zija
Chakwera kuyendayenda ndi m'mene ziriri kumlw sikoyenera
But I don't blame him coz he do knw what he's doing and he is the state president without knowing the meaning 😢😢😢
we had a dead opposition..for 4yrs....thumbs up akamuna inu
Nkhani ndi mademo adatenga ndi mademo,achokenso ndi mademo.achoke administration ya boma alinayo kutali.
Koma ndiye achoke pa 2530.00 kwacha ........ndiye tilire bwanji abale
Mudziyankhula chichewa kuti anthu ena adzimbva mawo
Salaimana is the best fighter
I like mkaladi uyu chilungamo chimamupweteketsa mutu kuchisunga
Machine opangira machine amnzake
Appaa ndiye opposition yabwera
Yabweradi mesa
Ooh allah protect and guide all leaders how stand with Malawian peoples 🇲🇼🤲
Chakwela apha anthu ndithu
l can't wait chakwera you can go
Apapa ndipamene mwayamba kuwa imilila a Malawi Dpp🤞