Palibe Chamuyaya Pa Dziko La Pansi - Hon Kamlepo Kalua
Vložit
- čas přidán 10. 07. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Hon Kamlepo Kalua says nothing is forever. Especially Political Power and Politicians.
Pa Nyasa VoiceBox, Olemekezeka a Kamlepo Kalua akuti pa Dziko La Pansi Palibe Chamuyaya. Makamaka Mphamvu za Ndale Komanso anthu andale.
#malawi
Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go
Amene kamulepo kalua ndimamziwa ndi ameneyo nthawi yamakezanayo ankayimba nyimbo zamatikitikii tiki tiki zamatikitiki so samalani amcp ndi chakwera wanuyo
A great speech sir ...so wise and mature
We are wit you sir, all the way.... God be wit u n the whole family
Ulemu wanu Mr kamulepo ambuye akutetezeni Ku khwandwe za MCP we love you ❤
Ndipo ndizoonadi apolice akumalawi ziwani kuti mawa limafika ine ndikupepha kuti ualamulilo wakuphau ukazangochoka apolice ose azawachotse tchito mmm ayi
Viva KK, great message 👍
Wise man 😊
Listen is better than beautiful sacrifice, palibe chamuyaya
Yex thus fact becareful ma fon amene anaranda apolice akufune ayikemo ma poison at the end aperekeno what kind of this government am be shame😢😢😢
I salute you Mr K K
Mwaputa olakwika....
Respect to you Mr kamulepo
Bravo Mr kamlepi kaluwa
Great voice sir
Patiently waiting for the day to see cctv footage of the fools mumu police
This Chakwera must go they take people like fools
Ku Malawi si kulilongwe kapena kukasungu hiyaaaa!!!!
Kamulepo Kaluwa🙏🔥👊🔥
Tell them the liyaliya😅😅😅
Mawu amphavu Mr Kalua
Tell dem sir agalu amenewa hiyaaa
Hiyaa! Mwanyanya a MCP kwatola amalawi lero mwakumana nazo,muyesa Malawi yu ndi wamanu agalu okupha
Respect
Mwalasa honourable Kaluwa you should stand for presidency you will get support from Malawians
Aaaa MCP anadzolowela kupha ndi kudzuza anthu mistake tinapanga poyibwedzelatso boma iiii
😂😂😂😂 kwachema
We worn you guys about Chakwera and MCP you didn't listen. Chakwera ndi munthu oipa mtima and he has never been a pastor.
You always chase money... thumba mukauma (dry) you make noise.. it has been ur tricks.. you have been always following the party that is ruling kusaka ndalama... ine simungandipusise nawo Mr Kalua...
Kukula kumeneko kkkkkk
Bwanawa alindi umboni kapena akungolumbwalubwa
🤣🤣🤣🤣🤣
Zoona munthu uyu anathana kale ndi kamuzu ku one party system panonso aszuzinke mmmmmm koma chakwera bwenzi utakhala ndi umuthu pena
Ambuye mutetedzereni penjani kalua mmanja mwa satanic awa chakwera ndi mcp akufuna aononge moyo wace but ladzalo cakwera why moyo wako umakondwa ukamapha anthu popanda kukhetsa mwazi thupi lako kukapwanya tulo silibwera mmaso mwako bwanji osamupha nick chakwera bwanji
❤awudzeni chilungamo 🔥
Awuzeni dppppppppppp
Please do not abandon the Lord Jesus Christ for the sake of politics. Please be a true Christian. It's surprising that the former man of God has gone satanic.