GWEDEGWEDE LERO NDE KUNALI KUGUDULA NDIWO ZAGULU | ZITHUNZI ZA ANDUNA KUNO |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 10. 07. 2024

Komentáře • 35

  • @kadijachilwan967
    @kadijachilwan967 Před 23 dny +5

    Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 22 dny +1

    Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 Před 22 dny +1

    A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 Před 22 dny

    Live from south Africa cape town

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před 23 dny +2

    Powerful GwedeGwede,,bambo banda

  • @B1Chitatata
    @B1Chitatata Před 23 dny +3

    Salute

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Před 23 dny +1

    Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Před 22 dny

    Munadza makosana ❤❤

  • @MerryWayson
    @MerryWayson Před 22 dny

    Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV

  • @ishmaelchirwa9303
    @ishmaelchirwa9303 Před 21 dnem

    Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂

  • @mathewsmdzanja3276
    @mathewsmdzanja3276 Před 23 dny

    I salute mibawa

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj Před 22 dny +1

    Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg Před 22 dny

    Mumakwana guys 💥

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 22 dny

    😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Před 23 dny +2

    Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 Před 23 dny

    Nkaka akulembaso MSCE

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z Před 21 dnem

    Zoonadi apolice amaonjeza

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 22 dny

    Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂

  • @StevieChikaonda
    @StevieChikaonda Před 23 dny

    Muli ndi mtopola guyz😊

  • @HarryMasamba
    @HarryMasamba Před 22 dny

    Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi

  • @user-gw2zb8pf7n
    @user-gw2zb8pf7n Před 22 dny

    Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 22 dny

    Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa

  • @LucianoKapepuza-sy9wx
    @LucianoKapepuza-sy9wx Před 22 dny

    Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo

  • @wilisonbornface4282
    @wilisonbornface4282 Před 22 dny

    Steve ndi Selina mativesa kukoma

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s Před 22 dny

    Mbambande mibawa

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 Před 22 dny

    Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Před 22 dny

    Ku malawi zimathera tikufufuza.

  • @NaduMbewe-zz6iw
    @NaduMbewe-zz6iw Před 23 dny

    Kkkkkk

  • @user-bc2mu2ns5n
    @user-bc2mu2ns5n Před 22 dny

    Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?

  • @CatherineDesire
    @CatherineDesire Před 23 dny

    Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Před 22 dny

    Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?

  • @OfwaMwambila
    @OfwaMwambila Před 22 dny

    If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u

  • @AlasonPaulo-ht7zb
    @AlasonPaulo-ht7zb Před 22 dny

    Zoonadi Inu muli bwino kwambili

  • @gwatandingo9502
    @gwatandingo9502 Před 22 dny +1

    Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢

  • @WysonYohan
    @WysonYohan Před 22 dny

    Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc