If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u
Apolice amaonjeza nkhanza pansewu😢
Zikhale ng'oma ma bombasa wagulakoso 😂😂😂 wausilu iwe
A Traffic police ambiri za miyoyo ya anthu alibe nazo ntchito nde ndizimenezo
Live from south Africa cape town
Powerful GwedeGwede,,bambo banda
Salute
Chipewa cha khwangwala kuteloko amafuna anyemere kaye kuti adutse ndi mwana wodwala ,utsilu dyera
Munadza makosana ❤❤
Sitidya ndale kkkk ndimakunyadilani kwambiri Mibawa TV
Anduna akutsotsola ulusi pano akuti kuionesa 😂
I salute mibawa
Za police mbuzi zaanthu izi kma kuba ndikupempha
Mumakwana guys 💥
😢😢😢😢 apolice apamalawi vuto ndi umphawi anthuni
Kkkk chipanda kuyankhula bwezi ali mumaguza omwewo kkkk
Nkaka akulembaso MSCE
Zoonadi apolice amaonjeza
Chakwera mumuudzeso kuti opha nzake afeso chifukwa chakwera anapha chilima my boss he call chakwera bull dog😂😂
Muli ndi mtopola guyz😊
Kkkkkkkkkkkkkkkkkkk Komatsu dzina izi
Mwanayo anali ndi 1 month and 3 weeks mgalimoto ndinali MO ine😢
Ndipo apolice akumalawi ndinu otembelekdwa ndipo mukulephela kugwila mbava koma kulimbana ndi athu osalakwa
Nawo a MCP asatile malamulo a gwirizano wawo kuti apite s Utm asogoleke nawo
Steve ndi Selina mativesa kukoma
Mbambande mibawa
Tisakubisileni apolice alowa chiwewe kusaka ndalama
Ku malawi zimathera tikufufuza.
Kkkkkk
Futso nkhumati kodi sopano kubako mwathana Nako?
Va police palibe vomwe vikuchita vimangodziwa kupempha ndrama pamseu ndikumanga mbava yoti anthu aigwira kare anthu eniake,ndipo vitengelepo phunziro mwina vingayambe kugwira ntchito bwino vipewa va mbalevo
Madokotalanso ali ndivutolawo munthu akumuwona ali pamzele komakungobwelawinawake wawudindo amakudusila chifukwachani winayusi munthu kodi?
If u stopped by the police officers on the road in ur 🚗 .who is supposed to follow the other? 4me i don't go out to a police office who stopped me coz i had no intention of stopping.u stop me,u come to me &tell me why you stopped me not me coming to ask u
Zoonadi Inu muli bwino kwambili
Wanga kufa mwana chifukwa cha wa police wandigwira nayeso adzafera pompo ineyoso natopa nawo mbuzi zimenezo pofunika osamawanyengelera😢😢
Malawi tingogulisa tigawane ndlama bc