Problem with democracy is everyone wants to be leader.Everyone has solutions to the problems but you vote them in they are clueless. They start doing they own ways
Great wisdom and speech, but trust ya aMalawi inathawa on politicians, becoz you change within seconds. Kukuvoteran basi ma adviser mbwee opanda nzeru, without economic backbone and expected services to poor Malawians. But anyway, may God intervene pa zochitika pa mpando umeneu.
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND DON'T TELL ME WHAT TO DO I KNOW MYSELF HOW TO GOVERN A MY PEOPLE I KNOW HOW A SUCCESSFUL NATION SHOULD BE AND I WILL BE SUCCESSFUL SO HELP ME GOD
Akulu akulu musamvutike zomalira kuti ndalama zikuchotsedwa ku bank ,komanso ndalama yagwa,nkhani yake ndi yakuti pali chinsinsi ndi ichi, akufuna ibwere ndalama yomwe imanenedwa ija ,kuti we are going to use one money,ziyambira ku Malawiko, ndalama zomwe zikubwera ku chokera kuja zikupita kuti ? 1, 2 achotsa ndalama ku bank ,cholinga chawo ndi chiyani? Pali chinsinsi chowopsya pamenepo chomwe chikuchitika
Useless voice you were there kmano nothing you did ndie apa mukuoneka ngati wanzeru poti uli kunja kwa office, mnthawi ya Peter muthalika kwacha inagwa kangati? Kod chi nyengo chimene zonnet sattar amapanga ndi boma anayamba liti?
Moto kubuuuu Dr kabambe muliphule dziko lili pa moto god bls u
Dr Kabambe, is the great man..may God bless him
Thanks
I like the way he analysis the issue
Nice explanation koma unali konko you did not think this wise..... killing Malawi for your fame, shame to our educated machines.
Dr D, freedom fighter, we need best Malawi
This guy is intelligent...DPP got brilliant economist ❤
Nonsenu mbava zokha zokha palibe wabwino. Musaononge mawu Chauta akuonongani nonse. Inu ngati mumayendetsa bwino Malawiyu bwenzi titaona zabwino zambiri. Enawa ndiye a alowa ndi njala kudzakokotamo zonse. Malawi akufunika mamasulidwe a uzimu wadzadza ndi ziwanda
Sikut sangabe ai koma kabedwe kake mpaka anthu kuyenda maliseche panthunda esh mcp ndi mbatata zeni zeni
Chakwela anazolowela kuvina nyau kwao kwa malembo pamene chilima Wakulila tchile kusaka nyama ku tcheu sangakwanitse kuyendetsa Boma
We need a town monger to run a state
Dr Kabambe, come and teach me economics plzzzzz
I would vote this person into govt but not with DPP!
This man has a vision 'cos of his education
U deserve my vote wakumulanjeyu akumachezaso ndi makapewa ndiye ndamutaya
Kubambe politician and economic moto kuti buuu chakwera kuti fwaaa
Reminds me of Bingu. This guy knows his story.
Problem with democracy is everyone wants to be leader.Everyone has solutions to the problems but you vote them in they are clueless. They start doing they own ways
😊😊😊😊❤😊😊😊😊😊
The wise man!!!respect...
A chakwela walephela kuyendetsa bom. Steven from mozambique
Thats true mr Kabambe zinazi ndi mbudzi zawononga dziko lokoma lija
No fear tell them truth how the dragon 🐲 swallow all the money
Just like Monday coaches
What did you do when you were in govt
Wise and great munthu oganiza boh amanenedwa uyuyu osati apuludzuwa
Am waiting your book about your experience and economics please
👏🏽👏🏽👏🏽👏🏽
🎉🎉🎉🎉🎉🎉✊✊✊
Great wisdom and speech, but trust ya aMalawi inathawa on politicians, becoz you change within seconds. Kukuvoteran basi ma adviser mbwee opanda nzeru, without economic backbone and expected services to poor Malawians. But anyway, may God intervene pa zochitika pa mpando umeneu.
This guy is brilliant " l wish kuti anthu amupase mpata wolamula zikoli🙏
Zapakamwa.Kungo peza mpando zimayiwarika.Amangofuna podyerera
This is best
Making sense
Chakwera ndi Chilima please stop playing games please
That's voice of the failures just accept
kuti mavuto athe amafunika yemwe akudziwa vutolo this man may be capable sure
A NEW VERSION WILL GOVERN OUR LAND DON'T TELL ME WHAT TO DO I KNOW MYSELF HOW TO GOVERN A MY PEOPLE I KNOW HOW A SUCCESSFUL NATION SHOULD BE AND I WILL BE SUCCESSFUL SO HELP ME GOD
Akulu akulu musamvutike zomalira kuti ndalama zikuchotsedwa ku bank ,komanso ndalama yagwa,nkhani yake ndi yakuti pali chinsinsi ndi ichi, akufuna ibwere ndalama yomwe imanenedwa ija ,kuti we are going to use one money,ziyambira ku Malawiko, ndalama zomwe zikubwera ku chokera kuja zikupita kuti ? 1, 2 achotsa ndalama ku bank ,cholinga chawo ndi chiyani? Pali chinsinsi chowopsya pamenepo chomwe chikuchitika
Mwalakhula zovekatu
True economy can't develop
I like u Mrs man
Malawi 🇲🇼,,,,,,,,.....,,,,,,,,,
President wakhala wovina nyau angakhale ndi nzeru that's why boma likumuvuta
👏👏👏👍
Kodi momwe munali pa mpando ku Bank kuja zonse zimayenda bwino?
Understand akuti anali just gorvener of reserv bank.nayenso amayendela malamulo a presdent
Naked truth
Àw😢
Mukango khuta madeya mukuganiiza kuyamba za ndale cholinga mukakhala pampando muziba mulemere Mapwara ambwiyanu agalu osauka inu,mitu ngati zitanga sala zosungiramo anamapingo ndikazango bwerera ku malawiko tisaza kumane pazalewa iyai wina ndiza Mu ponda
Awa ndi amunawa kwambili
Dolo Kwambiri
Inde limbikirani blaming the president for everything so you can win in 2025.
Mumatha abwana
Then why u didn't put this energy when u were within the system
Boma lidali bwinotu mu nthawi yawo ija. Sizalerozi
nzeru izi mukalowa mboma zimapita kuti? politicians please please mumalamulira anthu osati nyama consider the welfare of poor malawians, muzikhalako ndi umuthu.
Anthu anzeru alipo
Mmakwana boss posaeopa kutulutsa mau owonawa
for this reason my interest is to know you Dr kabambe
AKabambe mudalikuti apamukunamiza anthu lero? Osangonena kt mwayamba kubwebweta popeza pam'phika adakusamutsaponi? Ife ndi Chakwera 2030 wooolh
Yah ichi nde chilungamo
Mwazidziwa liti izi a Kabambe
Akuba awa
Ratios nazo
Gbu
Zinthu zinali bwino bwino koma tinagomera ndale, umbuli plus kupupuluma lero ndizi
Umatha ntchito yako ayise udangobadwira banja lolakwika 😀😀😀😀😀😀
Dolo kwambiri uyu
Just keep quiet my friend,,,
Jhhjjnkmm. Nkhani ⁹
Machende
Munthu ofunika koma ku DPP ndiye mbola bola angoyambisa chake chifukwa ngati ali wa DPP angofana ndi chilima kapena Peter ku dpp
Uyuso a Malawi tinakuziwa kale mbiri yako...iyaaaah
Double speak....
Tausani
Zofunika okumwa ink izi osati chifukwa amalima bwino fodya kumunda kwanga
Dr ndi ma equasation awo
Chiuta akutumbike nasetamanya apo pafuma suzyo
Mukunena zoona bwana
Iweyo unali koko thawi ya peter koma umalandila 20 billion ndiye apa ufuna unene chiyani
Oyamba kuononga dziko ndi ddp ndiye musatisokosele tionana 2025 takudziwa
Wakuba iwe galu kwanasi
Agalu amkaona ngati kuyendesa boma kobwheka
Tidaonga vote ndithu
Tidaononga vote
MUMANAMIZA AZUNGU INU KUTI MULI NDI MAKOBIDI AMBIRI
Chitsilu cha munthu
Mukanika kupanga produce ma companies ndalama mugula ma expensive houses and cars for your own. Ndalama mukuba Malawi is wise now, useless
mbava zikuluzikulu kunamizano mtundu wamalawi kufuna mavoti 2025 anthuwa zawo ndizimodzi tinatopa ndimodza ife
Kodi satta alikuti
Boma.ili ndi laziiiiii
Fuso labwino kwambili kuti kodi ma doller wose anawapeza mu boma alikuti?
Sono akafusidwa akuyankha
Akut ayi umboni ndi uyu
Khala chete iwe Dalitso suja unatibela ndalama nthawi yako ija ku Reserve Bank pamene unkadzilandiritsa K30 000 000 pamwezi. Sitinaiwale. Komaso unachita manufacture accounting yako kuti upeze ngongole kuIMF kuchitira kuti iwe ndizitsiru zinzako zakuDPP mupezeko kangachepe. Iweyo uli part of Malawi's problems sungatipatse ansala
Ohoo Kod ndaa meneyu wakuba uja eti,??? Aaaaa Anthu Wa mzigawenga ndthu
Useless voice you were there kmano nothing you did ndie apa mukuoneka ngati wanzeru poti uli kunja kwa office, mnthawi ya Peter muthalika kwacha inagwa kangati? Kod chi nyengo chimene zonnet sattar amapanga ndi boma anayamba liti?