Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.
Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.
Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030
This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like
Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.
A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo
Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢
Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi
How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?
Mr John Kapito has given a true account of the real situation in Malawi. He is a senior soothsayer. He is always for the whole truth. He doesn't mince words & his desire is to set things right.
Jst straight to the point
chakwera ndi chitsiru cha munthu mdziko muno mbava
koma maiko anzathu zimachitika ngati zimachitika kwathu kunozi kapena nkhani ndiyathu kunjaku....malawi wafika penipeni pomvesa chisoni mmmmm Mulungu atithandize
Malawi needs such people to develop!!!
Koma apapa mwayankhula chilungamo ngakhale msogoleli alindimaganizo amenewa likhoza kukhala boma mkhoza kuyendesa boma bwino ❤❤❤❤
Mr Kapito a man himself he doesn't fear nothing .He is so intelligent
Good explanation without taking politics but only justice ⚖ landilani ulemu Mr John Kapito😊😊😊
Big up Bwana Kapito, you are indeed a great man, I have really enjoyed your explanations 🔥🔥🔥🔥
Very clear message Mr Kapito may God bless you and your family and God bless Malawi country
Well spoken Mr Kapito..Indeed Malawi tikufuna anthu wolankhula dzokupsa ngati momwe alankhulira Mr KAPITO apamu
Kapito umakwana... If possible mungoyima pa u president.. we will vote for you
Ur a man full of wisdom.
Good explanation sounds like izeck somewhere (kukagwirana ndi azungu 😅😅😅 nice one Mr kapito
thank you sir kapito for your explanation
Respect Mr kapito otsaopa ,otsapweketsa we're all malawian don't fear lf there's justice
Mr kapita you're true leader
Brilliant ❤ Mr John kapito
Kapito your e a big man ayi pano ndiye ku Malawi sikulibwno ayi.
Thank you Mr kapito mwanena zothandiza ziko la malawi Kodi achakwera mkuva please pasto mrungu akuyang,oneni
Mr kapito ukunena zoona koma nkhani yimozi yonkha ndiyankhepo.
Chilima sangayendese boma ndimunthu wonama kwambiri. Ndiye ngati mutsogoleri ali ndiboza sangatumikire anthu.
Chilima ndi chakwera ndichimozimozi.
Chilima ngati akanankhala kuti akufunila zabwino amalawi bwezi atatuluka mu MCP chifukwa akanamuwuza chakwera kuti zimene tinauza anthu kuti tiwachitira sizikuchitika naye ali mphee
Choyamba kuyendesa ziko ukhale wa zeru and kuzichepesa kwa amene anakukweza. Kuopa Mulungu.
mfundo ndipo ndizoona
Zimangovuta koma chaka China tizapeza wabwinoyo❤ msogoleli wabwinoyo is our hope tizabowoleza tili ndi anthu azelu kumalawi ambiri
Yes
Anangokhala ndi nsanje kumuchosa peter pampando
Good explanation posatengela ndale ❤ koma chilungamo chokhachokha
Good explanation uncle. The Country need people like you not Chakwera,He must go back to his church not rule the country. The citizens are suffering alot because of him.
I like this Man, Mr Kapito keep on😊
God bless you and keep it up and this is well said
Mr kapito please 2025 please stand for people
Kma mr kapita you are the great man ❤😂
100% Mr man matiimilila ifeyo anthu amene tilibe kuthekela kofikitsa nkhawa zathu koyenela kupititsa nkhawa coz anthu tilinazo zolankhula zodzadza mitima komaso chilungamo dziko lamalawi lofunika fix kugwedeza kukhutchumula nyansi tikhale ndiatsogoleli osadzikonda moonjeza amene amalimbikitsa timbamva ma offence ndicholinga chofuna kukhututsa mimbazawo kumamupsinja munthu angakhale olimbikila paiye yekha km Mmmm oky god bless you Mr kapito please musakakhale pansi mubweleso kumalankhula osaopa please thanks
Bravo kapito!...respect
You deserve to be a leader...
Well explanation, Malawi needs such people
Big up boss man... you're a great man
Bravo kapito 100% agree 👍
Uwuwu ndi kantho kapena chilango cha mulungu pochosa msogoleli wabwino peter ndijuika mbava ngothi ndizisilu zones zili mu tonse palibe chomwe chisinthe mpaka 2030
Respect kapito osaopa achakwera ndi nyani
Mr Kapita Bravo.... awa ndi mau
Bwana kapito kuzang"alula khokhooo
True Malawian, Mr Kapito. Okumbira mnzake dzenje, adzagweramo yekha. Lero anadzikumbira okha dzenje ku IMF.
Great ones Mr kapito
This Mr Kapito why he's true and direct like this.......shaaaa ndipo ndamkonda bwanj.....in Malawi we also have brilliant and straight people this like
Brian ndi bambo kapito, boma ili ndi masanje eni eni, ndipo ukunena zoona bambo kapito, Chakwera sankhadziwa kuti angalamule dziko, mu mutu muli gwa! Sadziwa chilichose.
The real situation. Mr kapito is a soothsayer. He doesn't mince words. He calls a spade by its name.
Zowona m bomamu muli nyasi
ACHAKWERA AKUFUNA KULEMERA SINANGA AKUDZIWA SAKHALANSO PA MPANDO. PALOWANSO ENA .NDIYE OSAMADABWA RATE YAKUNJAILI KUTI .UTSOGOLERI SASITHA NGATI MALAYA .MAPETO AKE ALIYENSE AZINGOLOWA CHOLINGA CHOTI NDILEMELELETU SINANGA CHAKA CHAMMAWA AKULOWA ENA. AWA NDI MAVUTO AWAYAMBA DALA. VUTO NDI IEFE OKHALA KUMUDZI.
More fire mr Kapito🔥 🔥 🔥
Sir Kapiti ndinu munthu wanseru. Genius man
We're together mr Kapito
Kodi akapito amagwira ntchito yanji kodi abale
A brian banda mulibenso nzeru ndiyesa ndi mankhwala oyeretsa thupiwo mwina ,kodi ndege ku malawi zinasowa liti?
😂😂kugwilana zanja ndi mzungu mkumatinamiza ife kuti zinthu ziyenda 😂😂😂
Our own KAPITO mumatiyimilira koma kunsanva a President,ndakusokosela mkulinga utava!
Zayekha adaviyika nsima madzi musiyeni timuona 2025 Chakwera
Good Mr kapito
I like Mr kapito's explanation
Well said kapito🔥🔥🔥🔥🔥
Mr Kapito muyakhura chilungamo
This man is speaks the truth
Ndilibe mau mbili bwana kapito you're good man you're a m'dala 😂😂😂😂😂😂😂😂
Paja nyau yonunkha manyi ija amati zinalake chani?la chakwera tachosa koma la nyau yonkha ija😂😂😂
Mr kapito God bless you sir
Big up mr kapita malawi need people like you.
Good speech kapito
A chakwera Ali ngati chipilala 2angokhala mu office ndiye zinduna zano zimangobwela zainani apa chakwera ku zaina palibe chomwe akuziwa dzikoli akuyendeza ndi zinduna pamodzi ndi banja lawo
I am sorry for my self I missed this program, but I koma Mr kapito Mulungu azikudalisani ngati chakwer a sakumva ixi afe ndithu
Pempho Mr Brian Banda. Would you please visit anthu anchimidzi kuti muone how pple are suffering and see how they are surviving with every days life. Anthu amene adavota akufatu😢
Take this comment very seriously. Take a chance and visit voters in the the remote areas. For example, come and visit Dedza South Constituency the most Least Developed Constituency in Malawi
Eish ndipo very pain full vote lako lomwe kumagona osadya😢
@@user-zz3lf9qd5mkoma Mesa amati tizidya katatuh everydey
Appreciate bwana kapito
Boma lavuta ili pangolini amanena zoona respect the DC
Mr kapito please imilani u president pano mboma mwazaza a yes bwana okhaokha anthu a mamina mmutu
Mr kapito i respect you 🙏
Zovetsa chisoni mmene yatulukila maina oti apindule ndi zipangizo zotsika mtengo pa fumu dzina limodzi
Yea man of confidence
Chakwera Ndi Galu Kwambili We Are Tired Of Him
Bambo Kapito now you are Talking. Keep it up
Bravo Mr kapito
God bless you sir Mr kapito
Good one
Respect Mr kapito
Us Malawians we need to have readers from over seaze
50 years plus depend on foreign aid....i wish bingu was alive
Mr John kapito keep on trying to assist the blind
Mr Kapito katswiri
M'manja mwa akapito pwa pwa pwa
Thanks alote
Big up
Ndizoonadi alowa m,boma alibe Maso mphenye then nsamadziwa kuti kuyendetsa dziko ndichinthu chomvuta
True about fac leadership
Akulu awa ndagwilizan nawo kwambir
Bele munayamba inu a Kapito tilodala.
Mr kapito inutu inutu mukukamba dzeni dzeni
Bravo kapito chakwera and his government they have failed to read 🇲🇼
Nde wina adzikati Chakwera yemweyoooo akhomedwa
Izizo ndi zoona,Koma ku malawi sikudzatheka muika bwanji munthu osaphuzila Kukhala president,inu mmaona ngati m'busa ndiwomukhulupilira kwambili,munatilakwila kwambili ndipo mulungu azikukhulukilani anthu inu
Kkkk kugwilana chanza ndi mzungu ,koma a Kapito
Nice Kapito
Exactly 💯
True talk
Mr kapito mumakwana mukunena zoona
That's true mr kapito
That's true chakwera has failed eeeich Malawi 😢 need good leaders
How can you say Chilima has not been tested and yet he was arrested for thieving yet still working getting payed on Malawian tax payers? Was he not suspended?
Truth only, kapito wabwera
Palibe angamutsutse mkuluyu
Cakwera ndi wasatanic sAngamve china chiri conse sangaone Kuti anthu akuvutika akufuna anthu afe ndi njala kumidimakupite magazi ambiri
Time to say truth has come
iwe chakwera ndi chilima mboleizamanu anthu anga akubvutika kwambiri mwanva...
He is agreat man
Kapito machine