Uyuyu si brave ndichitsilu akuonesa kuti anali ndi information yokwanila koma sanayigwikise ntchito ndikumadikila pa khoti Iyeyu ngati amawava anthu akulila and kudziwa mbali imene anali osanena or palediyo kuti ngati aboma akubisa koma team ina yofuna kufufuza mwachilungamo ipite ikapulumuse anthuwa😢 Anthu ambiri akuonesa kuti amadziwa komwe kunagwera ndege koma osalankhula mpaka tsiku kutha kudzayambilaso mawa lake
Mulungu akuteteze fearless soldier for the first time to reveal the truth about chilima's and eight others death once again may Allah protect you all the time 🙏🙏 amen
Timafuna asilikali ngat awa...zkuvuta pati kodi kungodzuka kumpanga zomwe znachitika ndi nthawi ya pioneers....mukuchedwetsa zinthu bwanji kodi General 😢
soldier I salute you for the bravery. Loyalty is always to the nation and its citizens and those in that plane were the citizens of this nation who died without being given a chance to live again
Osawopo bro god will protect your Malawi akufuna chilungamo mau a dr chilima azitilipikiska ngatikulikufa tizafele 🇲🇼 koma ifa chalima ndi zawo wose ife Malawi sitizayiwala moyo wa2wose never 😭😭
Koma mabodza a Malawi tisiye, dzikoli ndi losauka, ma Vn enawa atha kuyambisa nkhondo, bwanji zonse timusiire Mulungu basi, ili ndi boza akunena mkuluyi.
That soldier needs our support Let's not hear and keep quiet action is what needed most Fellow Malawians let's woke up from our sleeping together we can
That's true bro what is needed to be done is we all Malawians kuti tonse kugwilana manja basi izizi osaziziyilira ndithu let's woke up our force is what can make him resign soon 🤞💔
Pa kolona pokha paja, chilima knew kuti politics is dirty game and anapeleka moyo wake kwa mulungu. Mizimu ya anthu amfa ija those souls will never crossover into the light before chilungamo chidziwike
My heavenly Father, perform wonders in Malawi especially in the minds of our callous political and religious leaders so that they know You in Truth and in Spirit as opposed to hypocrisy(Matthew 23:1-)
Ine ndinabadwa m'ma 70s Koma maonedwe athu ndi osiyana. Democracy inaononga,economically komanso chikhalidwe cha a Malawi chinaora.Malawi anapenga mwachidule. Ma politician ndimbava zokha-zokha,Ali busy kusintha-sintha zipani chifukwa aliyense target ndi ndalama osati kutukula miyoyo ya a Malawi ayi.Komanso ndi ma puppets,amauzidwa zochita ndi azungu osati Ife amene tinawayika ma udindo.
The problem we have Malawians we always say we need people like you but we don't support tilibe kugwilizana that's y things zikumkeramkera koonongeka ..........dziko la Democracy limeneri? ....ufulu wanthu ukuonongedwa ife tili chete ........DZUKA MALAWI PLEASE!!!!!!!!!!!!!!!!!!
If he knew about this he’d have done something right way before the plane took off because he knew the damage and danger ⛔️ that would happen why he didn’t stop it 😢he’s guilt too? He could have gone on and reported this before the flight ✈️ took off if he knew all this information. He played part too mxiii
I choose to mourn our VP and those other innocent lives without pointing fingures . If he has evidence let him bring it , but we cannot just believe speculation.
We need such brave soldiers in Malawi
He is a liar
Uyuyu si brave ndichitsilu akuonesa kuti anali ndi information yokwanila koma sanayigwikise ntchito ndikumadikila pa khoti
Iyeyu ngati amawava anthu akulila and kudziwa mbali imene anali osanena or palediyo kuti ngati aboma akubisa koma team ina yofuna kufufuza mwachilungamo ipite ikapulumuse anthuwa😢
Anthu ambiri akuonesa kuti amadziwa komwe kunagwera ndege koma osalankhula mpaka tsiku kutha kudzayambilaso mawa lake
Amalawi anzanga tiyen tisaloleso kulamulidwa ndi mfiti chakwelayu
Are you sure ndi soldier di
Mulungu akuteteze fearless soldier for the first time to reveal the truth about chilima's and eight others death once again may Allah protect you all the time 🙏🙏 amen
Yesu adafela kuyankhula chilungamo My God protect you Sargent
Mzimu wa munthu osalakwa ngovutaaaaa Ichi nchiyambiii ziululika ndithuuu ñdipo nonse mwapanga izi mubweza one by one.......God he is watching
Sitikuopa sitifooka dziko ndi latose ili ndipo tidzafera mbendera yake imenei 🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼 very powerful word😢😢😢
Zomwe zayakhulidwa apazi chimodzi modzi zomwe wayakhula wa bakili muluzi,nkhani iyi musayitenge ngati yabodza
Msilikari wabwino olimba mtima uyu tiyeni tigwire naye ntchito yothana ndi Chakwera
Tinthana nae chakwela ameneyu
Dat's true bro
@@harrisbanda5891 Brother tigwirane Manja tonse ndimunthu m'modzi asatikwaneyi kumangoswa mitima yathu tiyeni timukodze
@@user-uc1pd1tc2x I agree with you bro, zikufunika mademo adziko lonse kuti ng'onazi zituluke m'bomamu, tikupempha amabungwe kuti ayitanitse mademo ochosela asatana amenewa👉 👹👉👹👺👉👹👉👿👉☻👉👽👉👹
Wonderful wankhondo
Good Messnge Chakwela achoke ndi galu
A real soldier is like this man now deal with chakwera a Malawi don't leave him live.
Timafuna asilikali ngat awa...zkuvuta pati kodi kungodzuka kumpanga zomwe znachitika ndi nthawi ya pioneers....mukuchedwetsa zinthu bwanji kodi General 😢
Yehova akhale mbali yako
Impeachment ichike achoke chakwerayo ndi munthu oyipa kwambili MCP ichikoke mboma ndipo anthu onse anduna zaboma amenewa aoñe nyekhwe Chaka Chino osawasekerera ayi apa zafika athipja tionse chakwera Mai amphamvu ulemu wanu msilikali wa bwino ameneyu
Komatu ati amutsekera
Brother, you are our hero,keep it up and may almighty God protect you,chakwera ndi galu kwabasi,watipweka,😢😢
soldier I salute you for the bravery. Loyalty is always to the nation and its citizens and those in that plane were the citizens of this nation who died without being given a chance to live again
Excellent work soldier. That's what Malawians want light know. Keep us updated
Apapa tidikiranso umboni wina wotani, chakwera akusowekera kudulidwa pa khosi ndi mpeni
Sindinamuonepo mtsilikali olimba mtima ngati uyu ndipo pamene ulipo landilan ulemu wanu. Ndipo tigwirane manja tipange zothekera kut chilungamo chonse chidziwike
Komaso msilikali uyu chonde tisamusiye yekha pliz a Malawi timupange sapoti pa chilichose kaye apita ku court tisonkhe chilungamo chioneke and wose amene sikuwakhudza agwidweso osawaiya ndi moyo
No peace for wicked pipo😭😭😭😭😭😭😭
Osawopo bro god will protect your Malawi akufuna chilungamo mau a dr chilima azitilipikiska ngatikulikufa tizafele 🇲🇼 koma ifa chalima ndi zawo wose ife Malawi sitizayiwala moyo wa2wose never 😭😭
Zoonadi
Koma mabodza a Malawi tisiye, dzikoli ndi losauka, ma Vn enawa atha kuyambisa nkhondo, bwanji zonse timusiire Mulungu basi, ili ndi boza akunena mkuluyi.
Silikaliyi akunena zoona m'bale wanga ndi silikali ku moyale balacks wayakhulaso kuti ndegeyo inafika bwino bwino koma pilot anaopsedwa ndipamene imatembenuka muona nkhondo mene imakhalila ku malawi
Ndpo nkhan zabodza kuyenda changu.macadet😊
Malawi is not poor country but these greed politics
Ndipo amene angakhulupilire VN iyiyi ndi osaganiza bwino
Ndipo anthu angopekera nkhani zabodza chakwera
Chakwera ndi mfiti guys tibweze tisaloreyi
Ooh my beloved Malawi 😢. We've been robbed 😢
😢😢😢robbed a good promising leader.. ambuye atichitile chifundo❤
Go ahead a real soldier 💪💪
That soldier needs our support
Let's not hear and keep quiet action is what needed most
Fellow Malawians let's woke up from our sleeping together we can
The president must resign
Exactly
That's true bro what is needed to be done is we all Malawians kuti tonse kugwilana manja basi izizi osaziziyilira ndithu let's woke up our force is what can make him resign soon 🤞💔
That's for sure he must go the useless President ever in Malawi is Chakwera
Not even to resign komano angotichokera pakati pa amoyo
Kuyipa moyo
That's my Nation kumangodziwa zophana kukakamira maudindo koma zinthu osayenda ayii eeh enafe nde tizangofera moyenda basi
May the good Lord bless and be with you comrade, for sure God I'll protect you and cilungamo cioneka
True brother chilima sanalakwedi
Thanks so much God bless you silikali adzilimba mtima chilungamo chimamansula chakwela wawonje watibweletsela chitibwe wachilendo padzaka dzino koma pakale nthawi ya kamudzi tidziwona kunena chilungamo ayi mulungu alowelelepo ife tachepa nadzo 🙏🙏
What a soldier!, continue braving up, tingoyika kaye malirowa ava kuyabwa Sangaphe tonse ,ukatambatamba look east😮
Ndipo zoonadi
Pa kolona pokha paja, chilima knew kuti politics is dirty game and anapeleka moyo wake kwa mulungu. Mizimu ya anthu amfa ija those souls will never crossover into the light before chilungamo chidziwike
Sounds good bro
Thanks very much Sargent James much appreciate for that God be with you at all times
Expose them mfiti za MCP
U r v chosen one by God to tell us v truth,bigup
Fact Mr,Just KP your self safe apalibe chisisi pazikolapasi Mulungu alindinjila zake
Go Go Soldier
U can't even die,God is with you. And he will protect you, Go ahead and we will going to support you
Awa ndi asilikali omwe dziko limafuna tiyeni tipange support chilungamo chifalikire paliponse aliyense achiwone
🙌🏼🙌🏼🙌🏼 our mighty father protect you really soldier chilungamo chiyende ngt madzi mlungu atimenyela nkhondo zonse ziwoneka poyela I salute you chief ✊💪
Tiphana asapite kumalilo
Osadanda we will ll fight together 😢
Ndipo uyu ayenela kuduwa bas
Good move chakwera akuyenera kubwera 0yera apo bii akuyenera kuphedwaso sangaphe osalakwa
Ndipo usaope aliyese azamfa yakhula basi chilungamo chiyende ngati madZi anyapala achabe chabe awa akupha azawo ngati khuku
May God protect you General Wasili
Mtsilikali Okonda,dziko lake chilungamo Chiyende
ngati madzi Malawi wake up
Mulungu akutetezereni inuyo biggy zombvesa chisoni kwabasi yohhh
Bola asakuphe ase uyu ndi Satan weniweni chakwera wapha chilima 😭😭😭😭😭😭 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭 Why Why. Chakwera Why 😢😢😢
God bless and protect you dear brother a true son of the land Malawi,
Ayaluka amenewa
Chakwela you mast go
Pangani zomwezo bwana chilungamo chidziwike basi thank you mr
My heavenly Father, perform wonders in Malawi especially in the minds of our callous political and religious leaders so that they know You in Truth and in Spirit as opposed to hypocrisy(Matthew 23:1-)
We need people like you bru keep going we are not afraid
We need soldier like you in this country
We need people like you, boss
Ana a muma 2000,simumadziwa za mcp singasinthe ndichipani chankhaza si iziiii
Ine ndinabadwa m'ma 70s Koma maonedwe athu ndi osiyana.
Democracy inaononga,economically komanso chikhalidwe cha a Malawi chinaora.Malawi anapenga mwachidule.
Ma politician ndimbava zokha-zokha,Ali busy kusintha-sintha zipani chifukwa aliyense target ndi ndalama osati kutukula miyoyo ya a Malawi ayi.Komanso ndi ma puppets,amauzidwa zochita ndi azungu osati Ife amene tinawayika ma udindo.
Kkkkk ndipo zoona taziwano
We are with you we need justice
Brave soldier ku malawi mulungu akhale nanu bro
There is GOD in the world tell us truth ❤❤❤❤
Brave man. We pray 4you
Mulungu siwosewelesa zibwanakumapanga koma pazikhala malile apapa ngat nzoona tithana osat masewero
I respect u mr sir may God will stand for u for ever
It's time for Dr Manga 🎉... bachedwani mmabodzawa apa
May God bless and protect you
Tisathe mawu wamoyo kulibe wabwino amakhala wabwino akamwalila amene tikuwanyoza lerowa mudikile akatichokela ubwino wawo mudzuona
Komano tilhale ndi mzeru mdithu osangotsegula kukamwa ngati anthu amisala
Ine sinaoneko mtsogoleri wabwino munthawi imene akulamulila maka kumalawi kuno koma timazindikila ubwino wake mbari ina akamwalila
Ooh my allah guide and protect you mr watsili your really good ma of allah 🤲🤲🤲
Mmmm chakwera afunika umumangilira pa mtengo angathawe buzi ya munthu
Ma God protect u until you accomplish your mission. Dziko sili bwino.
Chilungamo chi mamasula ukuteteza ndi mulungu
Amutsekeratu ati
Zikomo msirikali kulimba kwako mtima Ambuye akudalisen mochuluka usazione kuchepa wanyamula amalawi ambiri ndakudalira msirikali dziko ndirathu palibe zoopyesana
Keep it up
ndiye wati abwanawa amakunyasa 🥲🥲🥲
Apato apresedent atiuze choonadi chifukwa dzikoli lamunthu Wina aliyese silanu nonkha ayi no kuopse zana
Vuto asilikali akumalawi tulo limakuzazani mmakhalangat simuziwa chomwe silikali amayenela kupanga enafe mwai unangotiphanya bwez tikuthana konko mafelano
The problem we have Malawians we always say we need people like you but we don't support tilibe kugwilizana that's y things zikumkeramkera koonongeka ..........dziko la Democracy limeneri? ....ufulu wanthu ukuonongedwa ife tili chete ........DZUKA MALAWI PLEASE!!!!!!!!!!!!!!!!!!
Kodi akuluakulu chakwelayu... Akuonangati ife ndizitsilu... Ife timaganizatu
Ntchito ya mulungu nde imeneyo . Mulungu sakusiya wekha gwira ntchito molimbika strong soldier ✊
Ameneyi aulule basi munthu wabwino iweyo tanena tiwone ponamila achakwela ku anena chiyan
Chilungamo chibwera poyera God is watching
Ndilitu mbali yanu ineyo ndipo 100% akufuna kuoneka ochenjela amalawi ake siapanowatu ayi muziwe kuti sife ogona ndipo muziwe kuti zomwe mwapangazi mulungu aliko muzafa imfa yowawa ndiyochitisa manyazi kwambili afisi azang'ambilana thupi lanu ndikulidya mosakupasaniso ulemu kuti munali ndani zowona chifukwa chani koma kumumpha zanu ngat chinyama 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
Ameneyo ndiye Msilikali okonda dziko lake
Mmmmmm awatu apupuluma ndipo awapha mpaka sitipeza uboni 😢 mukanadekha Kaye ndikuona ngati mwafulumura
Ndiwabodza uyu sisilikari uyu ali ku South Africa uyu
If he knew about this he’d have done something right way before the plane took off because he knew the damage and danger ⛔️ that would happen why he didn’t stop it 😢he’s guilt too? He could have gone on and reported this before the flight ✈️ took off if he knew all this information. He played part too mxiii
Oooh God, awonetseni kuti mumatha
Asilikali wose akanakhala ngat uyu bwez zinthu zikusintha but we are sheem na president
God bless you ,watching from Durban❤
Akulu ndikupempheni kuti information yonse muli nayo mugawire wina wachinsinsi kuti nayenso asunge chifukwa anthuwa akhoza kukukwenjani kuti muwapatse zonsezo kufafaniza umboni so please take my advice
Thank you sir. I’m with you.
Wonderful wa nkhondo
Bravo, the true, courageous soldier
magazi amunthu osarakwa chilichonse chiziwika la 40 likakwana
But why?! Why?! Why? Mr President Chakwera u are so wicked, Evil man kupha Anthu osakulakwira why?😭😭😭😭😭😭😭
I choose to mourn our VP and those other innocent lives without pointing fingures . If he has evidence let him bring it , but we cannot just believe speculation.
Thank you
Mulungu mutetezere ,msilikaliyo asamuphe chakwerayo NDI we otani kuyipa tima chomcho iweso chakwera sukhala NDI Moyo Ufa ndithu mulungu akutenga
God protect you boss
We need people like this Man is telling people the truth keep it up Chakwera is a killer
Akanakhala hero akanapanga chothekela kuti ndege ya Chilima isanyamuke, apapa we can't yield anything zachitika munthu wapita basi
Ana ma 2000 akuvuta
AMALAWI IF YOU REALLY love chilima and your country you must rise up
Amen brother
Kupanga campaign paground pakuvutani aphumbwa ndiye mwalowela paimfa ya chilima, Blackbox itiuza zonse. Munatha ma albino inu. Ndipo mnalonjeza kuti muzathana naye chilima,
Ambuye akudalitseni bother ndipo akutetezeni koditu muthu umatha kunena kuti ndi kumupha uyu kuti ineyo mawa ndidzale papando sudziwa kuti mawa lako ndulotani ndipo uve kuwawa chakwela mulungu akupatse chilango uli moyo ukuzuza a Malawi munjila zambili chifukwa uli papando koma mulungu akuone iweyo