Abale zikuoneka kuti atsirikali athu sidzikudziwika mbali yeni yeni komanso ntchito yawo akuyenera kugwira chifukwa kale a Malawi timadalira atsirikali kuposa police popedza zonyansa zonsezi akuchitazi anayamba kale mogwiridzana ndi mbiri ikufotokodzera
Koma nde kuyalukatu boma la chisembwere ngati ili sinaliwonepo yohh
Keep it up Mr ntanyiwa more fire
More fare🔥🔥🔥🔥 tili pambuyopanu
Continue telling the truth
LIMPOPO FM moto kuti buuuuuuuu with Comrade MTANYIWA
Awululeni ayaluke anthu oyipa a Mcp
I like the song
Nice one song
From nsanje boma Limpopo fm ❤❤❤❤🔥
Watching form South Africa
Ndiyakhepo pa mayi akunedwayo malemba akunena kut . Wawuze athu zomwe wawona ndimaso wosati zakuva ndiyena ayi kid chikakhala chabodza wukwanitsa kwawuza athu ones amen wawuzawo pepani baba yakhulani zowomwe mwawona ndimaso
Limpopo FM keep it up
I like Bakili muluz, amapeleka ma umboni, pankhani zake
Zoona zake man
A NEW THINKER WISE WILL GOVERN OUR LAND SO HELP ME GOD
Mark pastor 9:14
Ai A Cormled Kunotu tadzuka bwino ndithu , Aaaa A MCP mama Mr Chakwera akusaka pofera awapeza amene wawasogozao Chakwera pompano
Usapelekele umboni wabonza Mulungu akuwona zonse
Takunvani a Limpopo FM nkhanga zaona poti mayi Wina wadyesa nyemba Kwa dotolo was apresident kkkk
Continue is a good story
Mmmmm nanga mpachisanu, kwa a banje, cha MMA 4,😮
Kkkkkkkkk km kwathu nkokoma umangovuta ndi umphawi basi
Ameneyu kennako agona ndi a president 😅😂😂
Ayaluse moto kuti boooo😊
😢😢😢
Nde pali vuto lanji?mwaiwala kuti mkazi wa bakili muluzi anagonana ndi bodygurd inunso ukape bwanji
Mmmmmm zamabodza izi ndinu macadet inu 16:40
Usatanic wawowo 😂😂
Kodi mayi ameneyo wabuyi buyi ndindani abale
You Malawias you need president like Kamuzu Banda .you dnt have respeck
Thaulandndila moni
10:09 10:10 10:11
Osawopa inu nde mumanena zoona
Ndi aBakili mulizi TV
Bakiri muruzi tv
takudyadirani tizikupemperelani kut asakupezeni
Awadiaziwada ofunikila motobasi ahebili 12:29
Limpopo FM zikomo moni talandira koma mabvuto onsewa anthu ena oipa anachita kuwasankha
Nkhanga zaona!!!!!
Chiwandadi chimenecho
Mumativesa kukoma amkanga zaona mupitilize kutelo ine Balakasi
Nkhanga zawona kkkkkk
Kustate kwasunduka ku ndagala chifukwa chotenga mahule osalimba nsalu nkumamagwira ntchito lero ndiidzi nyumba yolemekedzeka ikungomveka zausiru zokha zokha kodi nthawi zija simungamakambirane zosisa mitengo ya zinthu zomwe munkalonjedza zija kapena mwalephera kusisa ? 😂😂😂😂😂😂
Koma yah
Komano man ngati umanena zoona iweyo ndi katundu umakwanila
Achitsilu mulibe zochita mukufuna kumanamiza Malawi basi
Chitsiru ndiwe pamtumbo pako galu
Koma kuli zinthu 😮😮😮😮
Chakwera ananyenga kale mkazi ameneyu chitsilu choke alone ena dzamuchima
Innnuu mwatani kodi pezani nthawi nanu mukaloweko kenako tidzamve za inuyooo mmmm
Koma azibale ndichani kwenikweni agalu amenewa?
Nkhanga zoona mumatiimilira
Za bodza
Munthu wamkulu ngati iweyo pali nkhani yoseketsa
Mau onyasawo
La 40 limakwana
Akatero ndinkazi wamweni wake uhule basi zisilu ziyanthu zaku paliyameti ko
Kwachema
🤓🤓🤓🤓 Kwamvuta akutinyasa ife achakwela
Nthawi yake iiiiiiiiiiiiiii
Koma man mukunenadi zoona kuti anthu agonanadi aaaaa
Ufitiwawo waonekera
Koma ngt irinyere😂😂😂😂
Kkkkkkkk ayaluka nayo
Chonde muzifika pa point msanga pankhani osamachulutsa zolubwalubwa
Abale zikuoneka kuti atsirikali athu sidzikudziwika mbali yeni yeni komanso ntchito yawo akuyenera kugwira chifukwa kale a Malawi timadalira atsirikali kuposa police popedza zonyansa zonsezi akuchitazi anayamba kale mogwiridzana ndi mbiri ikufotokodzera
Anawagura akulu akulu a boma nde ntchito zawo sizingaoneke komanso ovutika ndi apansiwa
Nkhanga zaona
Mulungu aliko atimenyere nkhondo 😜😜
Koma.abale misonkho yaamalawi ikungowonongeka
😅😅😅😅
Alomwe namwe tikati panji mazelu muli vizeleza kuyowoya unenesko cha muli vindele
Imwenso namwe ulichindere chakufikapo
Komatu zomatchulana mitunduzi sizabwinotu ayi. Chondechonde
Chakwela anamunyenga kale mai ameneyu
😂😂😂😂😂
Kkkkkkkk kuyaluka
Koma boma la MCP imeneyi, laposa la Kamuzu.
Ma cadet a lomwe a khutukumve inu usatibowe mulibe zochita koma kupeka nkhani zabodza
Mumativetsa kukoma ankhanga zaona
Chofunika.mulungu.amukkhudze
Izi SI zoona chifukwa simuonetsa zithuzi kuti ngati ndizoona muzionetsa zithuzi zao mkumalankhula nao
Washing for south Africa 😂😂😂yomweyo galuwee
Tiuze cadat
Fake channel i like Bakili Muluzi Tv he provides evidence
Hi
Bodza kufuna kutchuka awa
😂😂😂😂😂 koma nde zovuta bwanji
Koma nkhani Zina muzitipatsako ma umboni osamayankhula ndiye pot a Malawi tazolowera kunamizidwa
Zikuchitika kuti zimenezi,propangand yake ndie yopanda umboni.
Mmmm this is political propaganda, you are not a true journalist my friend but a politician
😅😅😅😅