Mulungu wamwamba mwambayo azikutetezelan nthawi zonse pamene mukuuza choonad a Malawi ndipo tili pambuyo panu Imani pa chilungamo ndipo chidzakumasulan
CHAKWERA, KUNKUYU, KEN ZIKHALE NG'OMA, MKAKA, CHIMWENDO BANDA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching your footsteps. MCP IS ENDED!!! IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!
The best redio Limpopo fm ndakukondani anthu okonda Malawi tisankhale mu ubuli much love the fm Limpopo
Best radio station
Tili pambuyo pano the Best channels of Malawi
The best Radio Limphopo
We love you guys keep on letting us know what is happening in our funken country
Tili pa mbuyo mpanu bro mtanyiwa comrade excellent
💪💪💪mmakwana comrade ntanyiwa
Chakwera amusankhe mkazi wa Sidik Mia kuti akhale VP apo biiii sapezeka wina aliyense.
Ambuye amava a tiyakha ndinthu amen
Great job comrade,❤️
Keep it up limpopo fm,tell the nation the truth without fear
Powerful speech ever
Keep it up comrade mtanyiwa cralify everything we are tired with mcp
Best channel!!!!!!
Our only best radio
❤❤❤❤ mumakwan guys Limpopo FM ntanyiwa
Man zaululika kale,pali audio inayake yomwe ili ndi maumboni onse.
Pangatalike bwanji,, mulungu apereka mayankho ake,,,, panopa ambuye aulura zonse mwez uwuwu usanathe. Limpompo fm wailes koma iyiii. Pitilizani osaopa kupereka chilungamo
We will find and give you a good position in our new Government ❤❤❤
Nanga ndale zomapanga anthu atagona ndiye ndale zanji zimenezo
Nyumba ya magazi
Galimoto ya magazi a chilima
Koma chonde muzika ma date kuti tiziziwa kuti ndiya lero kapena ya kale
Even here your neighbor countries we are not happy
U r the best
Best Limpopo fmmm
Takuyamikani mayi chilima pokana zachibwana zimenezi
This is very painful too sad politics killed 9 people 😭😭😭💔
Kusaganiza akufuna nayeso asowe
Km achakwela km ndiwesilu kwabas
Ma radio akanakhala ngati awa bwenzi kulibe chinyengo
Mr Ntanyuwa you're eyes of malawian haaa tawaululani a fiti amenewa McP ndi anthu inuyo muzafa imfa yanu yosakhulukilidwa
Best fm radio
Ikhalitse limpopo fm with Comrade ntanyiwa
Kutsatila mwachidwi
Achakwera Munthu wakhaza kwambri
This is our 👀 radio ❤❤❤❤
Koma Limpopo ndi number one
Mulungu wamwamba mwambayo azikutetezelan nthawi zonse pamene mukuuza choonad a Malawi ndipo tili pambuyo panu Imani pa chilungamo ndipo chidzakumasulan
CHAKWERA, KUNKUYU, KEN ZIKHALE NG'OMA, MKAKA, CHIMWENDO BANDA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching your footsteps. MCP IS ENDED!!! IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!
Iwe mtanyiwa ndi 1 palibeso
Tiyakhadi tokha amalawi vot yanga nde phavu yanga😢😢😢😢
Big proud💪
Ngati kuli munthu amene anakonda kuyankhula chilungamo anali a Chilima ndipo Mzimu wawo ufukulambe chilichonse chomwe a Malawi akuyenela kudziwa.
Antanyiwa koma mulipo mwangoti ziiii
Paja or fiti yimapemphera yapempheradi
Brother timakunyadira timamva zambiri, kodi iwowa akungosakha akazi kukhala VP chifukwa chani akufuna azigona nawo chifukwa alibe mamuna
Comredy mtanyiwa agogo Anga akufuna akupaseni zukulu wawo akuti muzikhala naye
Apenga misala anthu oipawa
Aiwale ndipo amwene azavotere MCP Mwadzi wa chilima ndi anthu onse uzakukanthani
💪💪💪💪
Very painful 😢😢
Mai Zamba chinyemba Ngati kalongonda😢😢😢😢
Koma a Malawi ndife anthu okanika ma umboni wose akutchura anthu angapo ndipo anthuwo alipo kunkuno Ku Malawi bwanji osawagwira eeee ayi
Palibenso kutiudza lipoti labodza Limpopo ilipo tiziwa zonse mulungu wasikira mwa Limpopo manyadzi bwanji ku state ?
Iweyo jemus chakwera apa ndipo ungadziwe kuti kudziko lapansi kulibe chobisika koma ndiye mwayaluka amphawi kufuna kukakamira kudya ndalama zaamphawi
Dzikomo mayi chilima chifukwa chakuyankha kwanu uvice umenewo akapase akadxi achakwera chifukwa sitikufuna kuliranso
Vuto la chakwera ndi hule ndinanena ine amaona ngati kuti mai chilima ndi ophweka ngati hule la sadik mia tamangomu kwela mkazi wa sadik mia mbuzi iwe
Ndichoseni umbuli guys,kodi radio imeneyi ndi ya mmalawi muno?koz ena akuti ai ndi ya ku Joni?
Odziwa chilungamo satsogoza kugwira ufiti ena
Kom ndiye mcp alibe zelu why
Bola musamatinamize
Ndiposooo iiii,
Chakwera kumuseweresa mulungu koma chikhalirenicho anthu unawawerusa anthu amundege asanapedzeke unkaganiza chani ?
APAPA COMLED FALITSANI UTHENGA OTI 21 DAYS IKANGOTHA MADEMO AYAMBE CHAKWERA NDI NDUNA ZAKE ZONSE ACHOKE
He suppose to resign,ndpo thus the bst angachte asatikwiyisebe
Uyu payekha sangapange resign PAKUFUNIKA kuyenda pa mseu kuti adziwezoti amalawi sitikumufuna
Ndili okonzeka kulimbana ndi MCP ndife ndife
Israel kapena America
Awapatsa ndege achakwera posachedwapa ponamizira kuti ndi ya chipepeso
Koma pali pa chifriend chawo
Limpoo limpo limpopo
😢😢😢 achakwera ayalukatu apa
Don't worry, pompanonso chakwera anfanso!!! Sipapita nthawi
kkkkk
Kkkkkkkk koma guys eish,eee chilima watiphweteka mmmm
Go dipa
❤
💪💪💪
Owo
Osafooka
Tikuvera
😢😢😢
Kod8
Very bad
Tili pa mbuyo mpanu bro mtanyiwa comrade excellent
He suppose to resign,ndpo thus the bst angachte asatikwiyisebe