Limpopo FM Ntanyiwa wayiphedula nzammene black box inachotsedwela mu ndege madzulo zonse zili umu

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 17. 06. 2024

Komentáře • 84

  • @ShakilahMbwanaa
    @ShakilahMbwanaa Před měsícem +9

    The best redio Limpopo fm ndakukondani anthu okonda Malawi tisankhale mu ubuli much love the fm Limpopo

  • @JamesKhudze
    @JamesKhudze Před měsícem +6

    Best radio station

  • @JaiMkupa
    @JaiMkupa Před měsícem +2

    Tili pambuyo pano the Best channels of Malawi

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Před 11 dny

    The best Radio Limphopo

  • @user-oh9bh1cl3b
    @user-oh9bh1cl3b Před měsícem

    We love you guys keep on letting us know what is happening in our funken country

  • @DavieMathyola
    @DavieMathyola Před měsícem

    Tili pa mbuyo mpanu bro mtanyiwa comrade excellent

  • @CarenNamwera
    @CarenNamwera Před 13 dny

    💪💪💪mmakwana comrade ntanyiwa

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Před měsícem +2

    Chakwera amusankhe mkazi wa Sidik Mia kuti akhale VP apo biiii sapezeka wina aliyense.

  • @SalaJawali
    @SalaJawali Před 8 dny

    Ambuye amava a tiyakha ndinthu amen

  • @TapiwaMwanjah
    @TapiwaMwanjah Před měsícem

    Great job comrade,❤️

  • @user-mk9ro8fd4u
    @user-mk9ro8fd4u Před měsícem

    Keep it up limpopo fm,tell the nation the truth without fear

  • @LysonMtalika-tb6fk
    @LysonMtalika-tb6fk Před měsícem +1

    Powerful speech ever

  • @HiryChimalizeni
    @HiryChimalizeni Před měsícem

    Keep it up comrade mtanyiwa cralify everything we are tired with mcp

  • @SteveChirwa-ne9nt
    @SteveChirwa-ne9nt Před měsícem

    Best channel!!!!!!

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi Před měsícem +1

    Our only best radio

  • @CharleGollie
    @CharleGollie Před 22 dny

    ❤❤❤❤ mumakwan guys Limpopo FM ntanyiwa

  • @fidelixdezembro4599
    @fidelixdezembro4599 Před měsícem +2

    Man zaululika kale,pali audio inayake yomwe ili ndi maumboni onse.

  • @InnocentNgeya
    @InnocentNgeya Před měsícem

    Pangatalike bwanji,, mulungu apereka mayankho ake,,,, panopa ambuye aulura zonse mwez uwuwu usanathe. Limpompo fm wailes koma iyiii. Pitilizani osaopa kupereka chilungamo

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Před měsícem

    We will find and give you a good position in our new Government ❤❤❤

  • @ChristopherUmari
    @ChristopherUmari Před měsícem

    Nanga ndale zomapanga anthu atagona ndiye ndale zanji zimenezo

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi Před měsícem +1

    Nyumba ya magazi
    Galimoto ya magazi a chilima

  • @user-ug6ox9rf7c
    @user-ug6ox9rf7c Před 13 dny

    Koma chonde muzika ma date kuti tiziziwa kuti ndiya lero kapena ya kale

  • @FREEJOEKASONGO
    @FREEJOEKASONGO Před měsícem +1

    Even here your neighbor countries we are not happy

  • @MoseChikopa-qy3og
    @MoseChikopa-qy3og Před měsícem

    U r the best

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Před měsícem

    Best Limpopo fmmm

  • @ChristopherUmari
    @ChristopherUmari Před měsícem

    Takuyamikani mayi chilima pokana zachibwana zimenezi

  • @StewartGoma
    @StewartGoma Před 23 dny

    This is very painful too sad politics killed 9 people 😭😭😭💔

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 Před měsícem +1

    Kusaganiza akufuna nayeso asowe

  • @KasimIbbu
    @KasimIbbu Před měsícem +2

    Km achakwela km ndiwesilu kwabas

  • @user-oe6hy4fy5v
    @user-oe6hy4fy5v Před měsícem

    Ma radio akanakhala ngati awa bwenzi kulibe chinyengo

  • @ChettoSongeah
    @ChettoSongeah Před měsícem

    Mr Ntanyuwa you're eyes of malawian haaa tawaululani a fiti amenewa McP ndi anthu inuyo muzafa imfa yanu yosakhulukilidwa

  • @TatendaMakuyana-su7fe
    @TatendaMakuyana-su7fe Před měsícem +1

    Best fm radio

  • @WillyAndaki
    @WillyAndaki Před měsícem

    Ikhalitse limpopo fm with Comrade ntanyiwa

  • @user-et1tl1qs2j
    @user-et1tl1qs2j Před 20 dny

    Kutsatila mwachidwi

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Před měsícem

    Achakwera Munthu wakhaza kwambri

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w Před měsícem

    This is our 👀 radio ❤❤❤❤

  • @user-mi3ot6ms8x
    @user-mi3ot6ms8x Před měsícem

    Koma Limpopo ndi number one

  • @MirriamRaja
    @MirriamRaja Před měsícem

    Mulungu wamwamba mwambayo azikutetezelan nthawi zonse pamene mukuuza choonad a Malawi ndipo tili pambuyo panu Imani pa chilungamo ndipo chidzakumasulan

  • @NEBERTMVULA
    @NEBERTMVULA Před měsícem +1

    CHAKWERA, KUNKUYU, KEN ZIKHALE NG'OMA, MKAKA, CHIMWENDO BANDA, CATHERINE HARA be careful Malawians are watching your footsteps. MCP IS ENDED!!! IT WILL NEVER EVER BE AGAIN!!!

  • @JuliusLuwanda
    @JuliusLuwanda Před měsícem

    Iwe mtanyiwa ndi 1 palibeso

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Před měsícem

    Tiyakhadi tokha amalawi vot yanga nde phavu yanga😢😢😢😢

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm Před měsícem

    Big proud💪

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 Před měsícem

    Ngati kuli munthu amene anakonda kuyankhula chilungamo anali a Chilima ndipo Mzimu wawo ufukulambe chilichonse chomwe a Malawi akuyenela kudziwa.

  • @KingsiryMchona
    @KingsiryMchona Před měsícem

    Antanyiwa koma mulipo mwangoti ziiii

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne Před 25 dny

    Paja or fiti yimapemphera yapempheradi

  • @user-cl5qw1kp1h
    @user-cl5qw1kp1h Před měsícem

    Brother timakunyadira timamva zambiri, kodi iwowa akungosakha akazi kukhala VP chifukwa chani akufuna azigona nawo chifukwa alibe mamuna

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 Před měsícem

    Comredy mtanyiwa agogo Anga akufuna akupaseni zukulu wawo akuti muzikhala naye

  • @user-zp3fb7el4z
    @user-zp3fb7el4z Před měsícem

    Apenga misala anthu oipawa

  • @maskinmsungeni8763
    @maskinmsungeni8763 Před měsícem

    Aiwale ndipo amwene azavotere MCP Mwadzi wa chilima ndi anthu onse uzakukanthani

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga Před měsícem +2

    💪💪💪💪

  • @AroushMussah
    @AroushMussah Před 12 dny

    Very painful 😢😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem

    Mai Zamba chinyemba Ngati kalongonda😢😢😢😢

  • @user-es4jt6ds8m
    @user-es4jt6ds8m Před měsícem

    Koma a Malawi ndife anthu okanika ma umboni wose akutchura anthu angapo ndipo anthuwo alipo kunkuno Ku Malawi bwanji osawagwira eeee ayi

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před měsícem

    Palibenso kutiudza lipoti labodza Limpopo ilipo tiziwa zonse mulungu wasikira mwa Limpopo manyadzi bwanji ku state ?

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před měsícem

    Iweyo jemus chakwera apa ndipo ungadziwe kuti kudziko lapansi kulibe chobisika koma ndiye mwayaluka amphawi kufuna kukakamira kudya ndalama zaamphawi

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před měsícem

    Dzikomo mayi chilima chifukwa chakuyankha kwanu uvice umenewo akapase akadxi achakwera chifukwa sitikufuna kuliranso

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem

    Vuto la chakwera ndi hule ndinanena ine amaona ngati kuti mai chilima ndi ophweka ngati hule la sadik mia tamangomu kwela mkazi wa sadik mia mbuzi iwe

  • @DoreenKaunda
    @DoreenKaunda Před měsícem

    Ndichoseni umbuli guys,kodi radio imeneyi ndi ya mmalawi muno?koz ena akuti ai ndi ya ku Joni?

  • @martinBPhiri
    @martinBPhiri Před měsícem

    Odziwa chilungamo satsogoza kugwira ufiti ena

  • @moyo77777
    @moyo77777 Před měsícem

    Kom ndiye mcp alibe zelu why

  • @user-nx6dk4bj8v
    @user-nx6dk4bj8v Před měsícem +1

    Bola musamatinamize

  • @user-vl5on2lj8b
    @user-vl5on2lj8b Před měsícem

    Chakwera kumuseweresa mulungu koma chikhalirenicho anthu unawawerusa anthu amundege asanapedzeke unkaganiza chani ?

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Před měsícem

    APAPA COMLED FALITSANI UTHENGA OTI 21 DAYS IKANGOTHA MADEMO AYAMBE CHAKWERA NDI NDUNA ZAKE ZONSE ACHOKE

  • @JacquelineNgondoma
    @JacquelineNgondoma Před měsícem +1

    He suppose to resign,ndpo thus the bst angachte asatikwiyisebe

    • @HalisonSolomon
      @HalisonSolomon Před měsícem

      Uyu payekha sangapange resign PAKUFUNIKA kuyenda pa mseu kuti adziwezoti amalawi sitikumufuna

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki Před měsícem

    Ndili okonzeka kulimbana ndi MCP ndife ndife

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi Před měsícem

    Israel kapena America
    Awapatsa ndege achakwera posachedwapa ponamizira kuti ndi ya chipepeso
    Koma pali pa chifriend chawo

  • @GilbertKuchipinda
    @GilbertKuchipinda Před měsícem

    Limpoo limpo limpopo

  • @user-zi2mj1bn5v
    @user-zi2mj1bn5v Před měsícem

    😢😢😢 achakwera ayalukatu apa

  • @fidelixdezembro4599
    @fidelixdezembro4599 Před měsícem +1

    Don't worry, pompanonso chakwera anfanso!!! Sipapita nthawi

  • @chaleraeaster-ce2kc
    @chaleraeaster-ce2kc Před měsícem

    Go dipa

  • @Telezatembo-de4ng
    @Telezatembo-de4ng Před 22 dny

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Před měsícem

    💪💪💪

  • @user-nx6dk4bj8v
    @user-nx6dk4bj8v Před měsícem

    Owo

  • @PeterSadulo
    @PeterSadulo Před měsícem

    Osafooka

  • @gearardphiri6904
    @gearardphiri6904 Před měsícem

    Tikuvera

  • @El_lam825
    @El_lam825 Před měsícem

    😢😢😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem

    Kod8

  • @TryceMagombo-sh7kb
    @TryceMagombo-sh7kb Před 9 dny

    Very bad

  • @DavieMathyola
    @DavieMathyola Před měsícem

    Tili pa mbuyo mpanu bro mtanyiwa comrade excellent

  • @JacquelineNgondoma
    @JacquelineNgondoma Před měsícem

    He suppose to resign,ndpo thus the bst angachte asatikwiyisebe