Video není dostupné.
Omlouváme se.
Nkhanga zaona Chakwera watumiza Asilikali kuti Akamuphe Peter Muthalika lero.
Komentáře • 436
Další v pořadí
Automatické přehrávání
MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSILIKI-LIKI TELEVISION
zhlédnutí 9K
ANTHU SANAGONE NDIPO TIKUNENA PANO CONVENTION YA MCP ILI MKATI ACHEZELA KUVOTAMakosana
zhlédnutí 3,2K
Ochutnáváme Nejsmradlavější Vajíčka na světě - Stoleté Vejce @Duklock @VidrailEvilBender47
zhlédnutí 237K
Barbie Style Gear Knob Makeover: Glamour for Your Drive! 💅🏻🚗Crafty Champions
zhlédnutí 16M
Cane salvato grazie alla prontezza di riflessi dei bambini e all'abilità del veterinario #shortsI migliori trucchetti di Fabiosa
zhlédnutí 2,9M
UDĚLAL Z 20KČ 1200KČ!Štěps
zhlédnutí 135K
FULL INTERVIEW: Donald Trump takes questions from NABJ panelABC News
zhlédnutí 1,2M
FULL SPEECH: Donald Trump speaks before the NABJ in ChicagoFOX 32 Chicago
zhlédnutí 402K
ZIKUULULIKA KU CONVENTION YA MCP KU LILONGWE - BRIAN BANDA NDI CATHY MAULIDI🙌🙌🔥🔥HOT 265
zhlédnutí 21K
FULL EVENT: Trump Gives Fiery Interview At National Association Of Black Journalists Convention Q&AForbes Breaking News
zhlédnutí 3M
MALAWI COURT.... TAMVANI IZI ABALE 🤔Jimmy
zhlédnutí 63K
Amalawi ndi mbuli, asiye kudzudzula Chakwera;Bakili Muluzi TV
zhlédnutí 64K
Hamas Chief Ismail Haniyeh's Funeral in Qatar LIVE: Hamas Chief Haniyeh Buried in QatarFirstpost
zhlédnutí 122K
Proč si Fotbalisti STŘÍHAJÍ Díry do Kopaček?Horis PLUS
zhlédnutí 138K
English or SpanishGL Show
zhlédnutí 896K
iShowSpeeda Takhke OkradliTaky Bige
zhlédnutí 401K
Jumping off balcony pulls her tooth! 🫣🦷Justin Flom
zhlédnutí 30M
Amazing weight loss transformation !! 😱😱Tibo InShape
zhlédnutí 68M
VAŠE DÁVKA USPOKOJENÍ #74 😍HouseBox
zhlédnutí 196K
I CAN'T BELIEVE THIS HAPPEND!Zhong
zhlédnutí 35M
Pineapple Pizza (ft. Lionfield)Nick DiGiovanni
zhlédnutí 8M
This is the beginning of the end of Chakwera government.
AMbuye mutisogolere Peter ndi salimo 91 ambuye mupase I mzimu wachiziwitso
Ndiye MCP tikuidziwa ife ndimeneyo ndale zake ndi zakupha
Achisale pls motsongozedwa ndambuye protect our APM
Kwa APM yekhayo ndiye sangamukwanise dinner and dance ndi imeneyo koma Peter Muthalika yekhayo ku dinnerko Peter Muthalika akudziwa zokachita ifa ya Bingu Muthalika ndi ifa za anthu padege ukumupasa phunziro Peter amandisangalasa ndi omvera malangizo awanthu ngati Inu Amtanyiwa ndi Bakili Muluzi TV 🔥
Asamale kwambiribe koma
Eti
@@augustMag ndipo kwambiri tu mmm
Shame on MCP
Ngati iyeyo akuphanso Pieter nayenso ayenera kusogozana naye.
Ndipo kwambiri tu mmm
I love the way momwe mumachenjeza Malawi kwa zigawenga . Ndiye nimamutsatilani kwambiri pa CZcams Kono ku Zambia
Eeeee mayo ndalama yanga ine Peter munthalika iwe ndi Wilson msemanjira iwe anthu okuba inu
L
I'm here following you step by step each and everyday.
Kom guyz chakwera khani ndiyotu wina kungofanso kukhala ma demo anyooo!! Mwatitola mcp kwambiri
Ndipo apitilira Aku Kenya kuvutatu owo
Mission impossible God is watching 😢
Thanks for your information Mr Limpopo FM 🙏 we always with you
May Allah protect APM
Achisale motsogozedwa nd mulungu please protect apm
That's end of mcp in this country again.....God ll protect Amp
May God protect APM
Nyimbo imeneyo ntanyiwa ukamabwera pa Limpopo FM usayisiye chonde Limpopo FM moto kuti buuu 🔥🔥 🔥🔥🔥
Apa ndiye alimbana ndi achina chisale 🔥🔥 Malawi wafika posauzana
Chakwela and Rwanda foreigner based in Malawi you will get what you want warning to Rwanda you will see
APM SANGAPITE NGATI CHIWETO .YEMWE UJA MUNAPANGA UJA BANSI .. APM ATUPELE CHIHANA ANTHU AWAWA SANGAPANFIDWE NTINTINI NEVER
Eti
Mwachita bwino
Comrade mtanyiwa
Tili nawenawe sitingakutaye
Ambuye apitilize kukudalitsani 🙏🙏🙏🙏musafooke chonde chonde mulungu ali mbali yanu ndi ife ofuna mtendere ndiochitila chifundo malawi aliyese amen!🙏🙏🙏🙏
NDIPO SIZITHEKA AYI MULUNGU ALI KOMWEKO AMENEUJA SANGAKWANISE CHAKWERA KWAKE KWATHA NDIPO ALI NDI THAWI YOCHEPA MULUNGU AMULANGA ANANGOKHALA BUSA KOMA NDICHIGAWENGA CHACHABECHABE BUT I BELIEVE GOD IS THERE TO PROTECT PETER WA MUTHALIKA
Or nkhope ya Chakwerayo ikuchitakuonetsa kut ndinkhandwe yoopsa....asapotilidze.konse aidya malawi yonse
Zoonad
Koma ngati mgwirizano watha ndiye tikhale chisankho tu coz utsogoleri wu unasankhidwa pansi pa mgwirizano wa Tonse. Lets vote guys
Kumeneko ndiye ku mafelano kuja sopano koma anthu awa akuti bwanji ndi dziko lathu cholinga chawo ndi chani? Komaso asilikali athu angoti ziiiii kumangowonelela dziko likuwinengeka koma zoti abale awo ndi makolo awo ku mamamidziku akuvutika iwowo sakuziwa kodi? Nanga chomwe akumakhalila chete ndi chani ? Chakwela kwake kwatha ife tikufuna mtendele mu dziko musakomedwe ndi ndalama komaso omwe akudya ndalama za magazizi si asikali onse pali omwe akumadya enanu dzukani kutha ndi boma lopusali lakupha la mabodza komaso pa katangale azathu aku mangochi tetedzani PM kumeneko akaziwika anthuwo apondeni or kuwapha kumene np afela zintchito zawo
Asilikali a Malawi amawoneka kuti ndi opepera safuna kuthandiza Zika za Malawi akowopa kuyimbira anthu akulemekeza zigawenga zi Achina Chakwera
We don't have any police in our country
Plz plz achisale amunkhitho plz maso ndinu kt amene mumapeleka chitetezo Kwa Pam
Dr Bakili Muluzi amkatuza koma ife aMalawi kusamva
May Allah almighty protect Apm 🤲 amiina
Yes
In Jesus name, God protect APM
Mulungu amene anapulumutsa shadrec ,Mishec ndi abitinego kuphatikiza Daniel mudzenje lamikango apulumutsenso azitsogoleri amene atsalawa. kuti kudziwike kuti kumwamba kuli mulungu wamoyo amene sagona komaso saphethira amawona chilichose cha pasi pa thambo. mulungu apitilize kuulula zisisi pa ana ake amen.
Amen ❤❤
Amen
Amen
Uthenga upite kwa Norman chisale .onesetsani kuti chitetedzo chakhwimisidwa pa gate
God have mercy on our country
Mission impossible
Zamaboza basi mulungu akuwoneni
Prayer Malawi
End of chakwera and MCP, achepa, wapha uja Chilima wakwana basi. Thanks to Limpopo FM.
Awili aziwika kale tikuimbolani kuti muziwe zosatila anafika pa asoko ndiye atawapo koma tikuwalondolola anyani amenewa komanso mangochi boys ili paliponse 💯
Lord have mercy on us
Amen
Koma apa pali anthu odwala amene amakhulilupilila social media dziko lathadi basi munthu kungodzuka kupanga plan yoyipitsa munthu basi the opposite is true inu ndi amene mukufuna chakwera ataphedwa mu nthawi ya DPP anthu amaphedwa ambili apa lero iliso layipa bndiyetu sankhani yesu osati satana mudzakondwa
I love u mr khanga osawopa ngwilanani manja pls
Inu antanyiwa mwina inuyo ndinu mmapha anthu ndiye mzinamizila ena ndinu zizsilu ndi maboza anuwo
Ntanyiwa ndiwe one, continue ,tilibe asilikali angakhale police, kulibe ndattttiii aaaaaaa !!!!!!
Agalu alipowo ntchito ndi zigololo bas😰😭😭
Osazamuphwekesa comrade
Antanyiwa pitilizani kuchenjeza amalawi zazigawenga za mcp
Limpopo FM and BAKILI MULUZI TV mukuyesetsa ndithu kutitsegula mmaso koma amene alikutsogolo kwathu n'gokhumudwitsa. A Opposition aliko????
Continue with good news we always listen u ukutimvetsa kukoma ntanyiwa
Nyimboyi ndaikonda Antanyiwa cain ndi abelo
God will protect Peter ❤❤❤😢😢
Akangopha peter l tell you chakwela we come by the trip cross the country kukathana ndi iweyo alu continue.
Ndipo kwambiri tu mmm
Can I come to Malawi and show my position to chakwera government?
God protect APM
Yoo alipachintchito eti
Thanks
Mwasowa nkhani, akaphe nkhalamba ngati imeneyi
Mmmm
Ndipo inu!mabodza basi
Nipamene wina akt chakwera 😢😢koma zowawa izi menyeren nkhondo Ambuye titan padziko pano
Mulungu ndiwamphavu yonse Nothing can happen to them in the name of Jesus
Limpopo FM ndi bakili muluzi tv, mulungu akupaseni moyo wautali
Munthalika wakuti sangalanulire Dziko la Malawi ali ndi ntchito yanji?
Za fodya basi Kodi mwasiya za Tea mwayamba za chamba eti
Ku kholo kwa amako wamva
Pantumbo pa mayi wako galu iwe
Koma mtanyiwa ndi masewero ako ukuzuza anthu kwabasi ona ena ayamba kale kupempherera APM kkkkk
I think this is a sign that we have so many satanists in Malawi, we need God, anthu afika pongoyankhula zimene akugani as long as it will black mail Chakwera, how can you feel if that happens to your father. Too bad
Anthu amenewo asamale mangochi sigawa ma sweet
MCp ndichigawenga kuchokela ma 90s nde wina iziti chakwera Alobwino walowa nzwiwanda wangofika pa misara
Eeeee koma ma cadet muli pa ntchito. Kkkkkk
Chigawengacho Chichewa Chakwera chikutseweretsa miyoyo ya wanthu.
Keep it up
Anthu ndiye kuwadodatu ndi mabodza
Yanjiru simatani..?
Siiswa
Ndi Ana awa zomwe akufuna sizitheka komwe in the name of Jesus
Tiyamike kut okonda dziko ngati achina Mtanyiwa alipo ambiri....chifukwa chaichi choipa sichibweredzedwa....a Gadama, Matenje ndiena monga a Chilima ndiena aja akwana, pa Muthalika pokha usayerekedze ndithu iwe Chakwera (kungokhala anthu amagazi basi)
Bakili Muluzi amkanenatu kut MCP siyoyanjana nayo lero ndiiyo itangolawa mpandowo basi kupha kwadzuka ASAAAAA
Zinazi zalowa fodya zinthu.. apa nde trust pa nkhani zanu ndachosa.... Maboza
Mudzina la yesu christu mnazaleti mutetezelnini Peter mutalika kulikonse komwe kuli iye
Inu munthu watha kale uyu mufuna mudanitse basi
Nkhope za Rwandans zimadziwika asalowe dara kumeneko
A Ntanyiwa tengani ndi inuyo dzikoli,musawauze azanu kuti atenge koma inuyo, a Bon Kalindo, wa Bakili Muluzi TV,atenge dzikoli,kuti kunyoza,ndikutukwana kusiye, kumangonyoza basi, zambiri zimene mumanena ndizabodza kwambiri, zonse akunena za Peter Muntharika ndi zabodza zimenezo, kungofuna kudzionetsa kuti achina Peter Muntharika awaone kuti akupanga za iwowo,kuti DPP ikadzawina adzawatole,adzadyetse mimba zawo
CHAKWERA tamachita manyazi zinazi popanga, nawenso Manganya ndiwe katukule, Mulungu wakumwamba, achite nanu mwapadera ndipo asakusiyani chonchi
Longlive APM ..God is in control !!
We're here my brother ❤
🤣🤣🤣🤣 this is Comred ntanyiwa on Lipompo FM
Timakunyadilani big
🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏yomweyo chikangawa
Mulungu mumutetezere peter muthalika kulikose komwe apita 🙏🙏🙏
Akuluwa misala chani kapena mwaz wachilima nd anthu ena aja zikuwazunguza😂😂😂
Mabozatu amenewo
mumakwana bwana wanthuu🎉🎉🎉
Shame you chakwera fiti Yopanda manyazi wunapha chilima Pano wayamba kusaka Peter wupha anthu angati iwe
Ambuye akutetezeleni APM
Asiyeni akafa ndiiwowo ili ndi dziko
Inu anthu akungofuna kutchuka ndiye inu muli busy 😂😂😂😂😂
Umakwana ntanyiwa koma akangopha muntalika nafe tipha ndimiyala chakwerayo
We pray for God's intervention. Mission iyi Ambuye alowererepo.
koma mmm ntanyiwa boza ngati mnthu wa nkazi aaaa mnthu oti si wa dpp akagula ticket mnthu wachilendo aaa
Kodi amalawi bingu anakulakwirani chani?? Munamuchotsa mwachipongwe, peter uyu mukuti peter ndimunthu amene munamuchotsa mwa chipongwe again kungoni peter ndi chitsiru akuloranso kuti azapangidwenso chipongwe, saulos chilima zana zanali mumamutukwana limodzi ndi chakwera nde poti lero wamwalira wasanduka wabwino amalawi mulibe nzeru you deserve what is happening and there is no way out until you change, you will reap what you sowing
May Lord for everything please protect our beloved president
Asilikali nanuso bwanji otsangomupha iyeyo wakutumani Kodi anzako sakufuna moyo
Mmmm koma akachoka kwa Peter abwera kwa inu a UDF inunso mukuyenera kukhala osamala
Kodi asirikali athu bwanji ku Malawi uko mwangokhala pheeee 😂😂😂
Kulandira ndalama
Adadya chimbanzi
Asiya chilungamo asogoza ndalama.
Koma aPrasident opuma ananenatu kuti Doom sumafayira mkamwatu ndizitu pano tubwelera ku ulamuliro wa chipani chimodzi
Anthu akamatenthedwa zolankhula zake zimakhala ngati zingatheke 😂😂😂😂 mulira simunati
Moti chikangawa yalusa sikugawanso masweet 🤣🤣🤣🤣 atimaliza
My bsst ladio station limpopo
Iyiyi ndiye akufuna Kenya Kenya tsopano 🏹🏹🏹