MOSES KUNKUYU MUTU SUKUKOKA UKU KWANUNKHA UTSI

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 09. 2024

Komentáře • 96

  • @user-iv6iw1ck8s
    @user-iv6iw1ck8s Před měsícem +2

    Times 360 it's my best, Brian Banda and your Team pitilizani kutidziwitsa ndi kutivetsa kukoma, Brian Stanley Nowa, Capetown # from Monkey Bay chantulo

  • @gradsonmayira9336
    @gradsonmayira9336 Před měsícem +13

    Brian ntchito muyigwira🔥🔥

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga Před měsícem +1

    Mai chindevu mumakwana mwati Olira alile mwandisangalatsa

  • @LenoMvula
    @LenoMvula Před měsícem +7

    Times mmatha mmatiimilira kuno ku malawi nice job

  • @user-um2es1yp5y
    @user-um2es1yp5y Před měsícem +2

    Wonder chipongwe mzako akwatire 😅😅😅😅

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před měsícem +1

    Watching live fro RSA😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @PortiaMhlambi-y4g
    @PortiaMhlambi-y4g Před měsícem +4

    Brian Banda and ur team mumakwana

  • @annembepula
    @annembepula Před měsícem +6

    Omse okupha sadutsa munali buzy kupha,kumanga amzanu kuophyeza anthu muziwona zangoyambapo 2025 mulila munanyanyanya mmayesa mzamuyaya

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Před měsícem +2

    KUCHOKERS KUMOZAMBIKI A FELIX CATONHEZA TEMBO NSANJE SOUTH CONSITUENCY NSAMBA POLING CENTER PAMWAMBA A CHAKWERA 365TIMES

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf Před měsícem +8

    zigawenga za mcp pamenepo manyazi bwaa BICC chitukuko chandan inu 5yrs chitukuko chanu kupha mr chikangawa ndi umbava

  • @Martha-m6e
    @Martha-m6e Před měsícem +2

    Times mumandipangitsa ngati ndili komweko ❤❤❤

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 Před měsícem +5

    Wamenya campaign yomwaza chuma chochuluka ndiye aluzeso eeeehhh timva ena atamwalira ndima BP sure

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Před měsícem +1

    Wishing mcp.all.the best.choose patriotic leaders please!!!

  • @user-ij1yz4ex2v
    @user-ij1yz4ex2v Před měsícem +1

    Eeee koma Brian ndi wonder ayi ndithu nkhawa zomaopa chikangawa munapachika

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r Před 24 dny +1

    Zisilu mcp kupha anthu apule chikangawa party

  • @TimothyKabumbuKendrix
    @TimothyKabumbuKendrix Před měsícem +1

    Mr Brian Banda zabwino zonse ndi timu yanu kumeneko, ndine Hendrix Timothy kuno ku Botswana

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Před měsícem +1

    Well organised,convention kuyipasa moto viva mcp😮😮😅

  • @munashemoyo4190
    @munashemoyo4190 Před měsícem +1

    😂😂😂😂😂 kumkuyu wandiwaza zed ndinapemphera kut usawine ai 😂😂😂😂😂

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před měsícem +2

    Onse okupha sakudusa kkkkkk

  • @MadalitsoGama
    @MadalitsoGama Před měsícem +1

    Zoledzera izi

  • @RichmanIssah
    @RichmanIssah Před měsícem +1

    😂ine Koma mayi chindevu😂

  • @BrianMaganga
    @BrianMaganga Před měsícem +1

    Wina athawà

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Před měsícem +4

    Agaluwo asakozele makoma kumeneko paja ndi khalidwe lawo lowononga

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Před měsícem +1

    ABALE ANGA PANGANI CHILONGAMO POPANDA CHIWAWA DZIKO LOWOPA MLUNGU YEKHA NDIWAMKULU MLUNGU ALANGE OPANGA ZOIPA NAWONSO APANGE

  • @CassimCawanga
    @CassimCawanga Před měsícem +1

    Best television n plograms in malawi

  • @MichaelMbona-ch2kc
    @MichaelMbona-ch2kc Před 29 dny +1

    Chikangawa aut

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Před měsícem +1

    Time group machine machine ❤

  • @ConeriasPhiri
    @ConeriasPhiri Před měsícem +1

    Times 360 mumatiimilira mumativesa kukoma zukachitika tivera kwa inu

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona Před měsícem +1

    " Pakuti Malamulo a Dziko lino amalora, choncho dzina langa likakatulukanso Ku Ballot, ine mkayimanso"
    Mr Lazarus Macathy Chikangawa ndinu munayankhula mawu amenewa pamaso pa yemwe munasayinira naye mgwirizano . Tulusani za kafukufuku wa ngozi ku Chikangawa simukutulusa.
    Pali ???????
    Munthu woyipa iwe,
    M'busa okuba ndi okupha. God Will judge you evil man 👹🔨⛏️⚒️🔨👹.
    Lero zisangalala koma Amalawi sangayiwale Kuti unapha kufuna zonse zikhale zako.

  • @honourablebanda1961
    @honourablebanda1961 Před měsícem +2

    Times 360 is the best.
    Allan Banda pritoria(RSA) #ing'aluleni azibambo

  • @johnkatumbu6846
    @johnkatumbu6846 Před měsícem +1

    Waitchela kale mwati kuluyo?🤣

  • @simonejose8925
    @simonejose8925 Před měsícem +1

    GWIRANI NTCHITO A TMS

  • @BlessingsSeleman
    @BlessingsSeleman Před měsícem +1

    Kod brian unayamba mwazifusa chifukwa chomwe asilikali Ena mwati safuna kuti camera yaonese

  • @DanielKatengeza
    @DanielKatengeza Před měsícem +1

    Times ilengezenso kuti Brian Banda president wa Malawi nzakoyo akhale Vice President I think dzikoli liyenda bwino popanda corruption

  • @SelinaGamaliyere-q8v
    @SelinaGamaliyere-q8v Před měsícem +1

    Onse omwe anapha chilima asawine anthu oyipa

  • @user-hl3st3cc4v
    @user-hl3st3cc4v Před měsícem +1

    Ubwino wake zomvota wochewa wokha wokha ndemukaluza muphanaso nokha nokha ma pb muzikomoka nawo zindalama mumamwaza zija

  • @pauljosephmakaula6835
    @pauljosephmakaula6835 Před měsícem +1

    Katundu Vitumbiko Mumba all the best...new political dimensions

  • @SelemanSimoni
    @SelemanSimoni Před měsícem +1

    Thomas chibade

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Před měsícem +1

    Eeeee km times mukuigwila tchito yopambana

  • @user-ul1fb4yn5o
    @user-ul1fb4yn5o Před měsícem +1

    Times team mumakwanisa

  • @isaacgmc
    @isaacgmc Před měsícem +1

    Koma amalawi mukadali kuivotela MCP mmmmmm😂😂😂😂

  • @user-kh4qp1ji1i
    @user-kh4qp1ji1i Před měsícem +1

    Tea sitidya Brian 😂 timamwa!

  • @TriceGulani
    @TriceGulani Před měsícem +1

    Kkkkkkkkkkkk zavuta achimwene amosesi

  • @CatherineKamsare-cy3yo
    @CatherineKamsare-cy3yo Před měsícem +1

    Kwachema🤣🤣🤣🤣

  • @user-ww9rj2wx8d
    @user-ww9rj2wx8d Před měsícem +1

    Bolani asamupheso Brian Banda mtola nkhani mbambande

  • @KingsleySymon
    @KingsleySymon Před měsícem +1

    Nanga Nanu mtentha ndevuyo bwanj???? kkkkkkk am Kingsley Symon kusalima

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s Před měsícem +1

    President sanalakhule bwino sungadzudzule opeleka ndalama tsiku lovota ai pomwe Anthu ataononga kale ndalama zawo akanawauza nthawi yomwe amapanga kampeni kuti asagwiritse ntchito ndalama komaso akanauza omwe amaletsa enakuti asaime nawo chifukwa sanakhale mu chipani zaka ziwiri izi zapangitsa atidye nawo mong Dausi, Brown Mpinganjira,Uladi Mussa ndi Ken nsonda kuti asapeze nawo mwai opikisana nawo zomwe President akanatha kuzikhoza before not tsiku la master mansakho kumenekuku wapangira kampeni ena wichs not good

  • @zacchaeusbvumbwe391
    @zacchaeusbvumbwe391 Před měsícem +1

    Ntchito mwayigwira

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Před měsícem +2

    Mkasa paja ankati sazatamandanso wa ndale waywala cruise 5 pa zodiac ndi joab, yedye

  • @NewtonSikwese
    @NewtonSikwese Před měsícem +1

    Koma kuyakhura chilungamo ndongotsolo lake likuyenda bwino koma mapeto ake Akala bwino

  • @MaggieKaufa
    @MaggieKaufa Před měsícem +2

    Koma kwachematu😅

  • @andiwochishadreck3753
    @andiwochishadreck3753 Před měsícem +1

    Ndalama zakuba zabwerera kwawo

  • @CatherineMakina-d5o
    @CatherineMakina-d5o Před měsícem +1

    Uncle b

  • @LikangaManuel-sk8yp
    @LikangaManuel-sk8yp Před měsícem +1

    Achewa okha okha kunva kamwamo ochewa weni weni 😂😂😂

  • @SolomonBewula
    @SolomonBewula Před měsícem +1

    Kunkuyu asowe

  • @annembepula
    @annembepula Před měsícem +1

    Komatu mkasa dyela uyu kwa Dad uli nkomko ukunsi eeeee

  • @HenryGoba-m7q
    @HenryGoba-m7q Před měsícem +1

    Anthu akuvotela zigawenga zachilendo ziphe manganyaa

  • @whatsonbanda4277
    @whatsonbanda4277 Před měsícem +1

    Mcp chipani Cha mtendele.

  • @EmmaMbewe-vg4td
    @EmmaMbewe-vg4td Před měsícem +1

    Onetsetsani kuti Mkaka asalowenso

  • @courageouslondo1986
    @courageouslondo1986 Před měsícem +1

    Mumatha mabwana

  • @NedsonJosaya-pn1te
    @NedsonJosaya-pn1te Před měsícem +1

    Mwayedzeka kale?

  • @RichardChirwa-em6qj
    @RichardChirwa-em6qj Před měsícem +1

    Mizimu anaononga ku chikangawa iwakanthe ndithu anthu akuphawo

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Před měsícem +1

    Kukuyu 😂😂😂😂

  • @GiftPaulBrownBrown
    @GiftPaulBrownBrown Před měsícem +1

    Kwachema ku LL ine Gift Paul Brown from Mozambique

  • @user-zq3uf5bc8v
    @user-zq3uf5bc8v Před měsícem +3

    Issa manyaka ife tikulira biyeni wathu chauta Ave mapemphero amalawi kuti tidzadziwe chilungamo pokhapokha mcp itagwa muboma kuno ku katonga

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe Před měsícem

    Kkkk Amwe tea wa poison ndi zakudya za poison wa Achakwera..anthuwo asadye chakwera wakupha samalani naye angakudyeni

  • @user-lk8kj9zv6x
    @user-lk8kj9zv6x Před měsícem +1

    Inuyo guys ndi chuma cha boma ma pongolin athu

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w Před měsícem

    Chitukuko chao, ndikupha, kuba ndikuononga

  • @user-zw8ns7bk7s
    @user-zw8ns7bk7s Před měsícem +1

    Aichinja mozey

  • @Maliet-nh6kf
    @Maliet-nh6kf Před měsícem +1

    Panyo pachakwera kuno kuli holiday

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Před měsícem +1

    Sopano zokudyaxo zokanganilana

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Před měsícem +1

    Achikhala a DPP akanakuswa brain muja umawanyozeramu a mcp wo aise Koma poti awa ndi anthu amtendere ukuyenda momasuka

    • @user-ww9rj2wx8d
      @user-ww9rj2wx8d Před měsícem

      Mwayiwala za kuchikangawa eti

    • @MzadziWanga
      @MzadziWanga Před měsícem

      Ku state house munamuthamangisiranji ngt muli a mtendere, osati ma vote akuzunguzan mkanamupheraso konko paja zaugawenga ndinu # 1

    • @uzaleuzale8603
      @uzaleuzale8603 Před měsícem +1

      Mwaiwara kt mwamuika mu list ya anthu ophedwa anthu akupha inu

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Před měsícem

    Kwachema wina alira kuwononga ndrama zaziiiiii

  • @KingsleySymon
    @KingsleySymon Před měsícem +1

    Brain amatha kkkkkkk

  • @DesmondChavula
    @DesmondChavula Před měsícem +1

    Brain ntchito umatha

  • @KHWENGWEYAMAPEMBA-l4w
    @KHWENGWEYAMAPEMBA-l4w Před měsícem +1

    Kwayaka moto kumeneko

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Před měsícem

    Wochakwera amafuna choncho basi kusogoza chilima...mwataya chipangano agalatiya.

  • @CynthiaLusubiroMwalwanda
    @CynthiaLusubiroMwalwanda Před měsícem +1

    2:16 am

  • @ChrispinJohnson-py5ie
    @ChrispinJohnson-py5ie Před měsícem +1

    kunkuyu dyela

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem +1

    Kwachema

  • @hezekiayelemia
    @hezekiayelemia Před měsícem +1

    Brian Banda eiiish experience ikumuthawa

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera Před měsícem +1

    Kodi mec ndiyoyang'ana za chisankho cha chipani chimodzi ? Ndikudabwa

  • @user-gy8yn6qw2k
    @user-gy8yn6qw2k Před měsícem

    😂😂😂😂😂

  • @SebastiaoErnesto-mh6ec
    @SebastiaoErnesto-mh6ec Před měsícem +1

    🎉🎉🎉🎉😢😢

  • @peterkinsLekera
    @peterkinsLekera Před měsícem +1

    Kodi ndizololedwa kuti asirikali atenge nawo gawo ku conversation yachiani? Awapanga hire ngati chipani kapena angwiritsa ntchito misokho yathu

  • @user-ko6kp7jl4d
    @user-ko6kp7jl4d Před měsícem +1

    Palibenso chipani chingakututumuseni pitirizani.mfimdo.zanu.zotukula.dzikoli,linali mkamwa.mwa mimbulu more.fite

  • @BiliatMzungudala
    @BiliatMzungudala Před měsícem +1

    17:15 17:18 Ife sitigona a times tili nanu

  • @StevieChauluka-r4v
    @StevieChauluka-r4v Před měsícem +2

    Chithyola Banda adutsa pa SG basi, am Stevie Chauluka from area 25.

  • @thomasmilanzi6442
    @thomasmilanzi6442 Před měsícem +1

    Kunkuyu moto