- 59
- 802 485
TIDZIWE TV
Registrace 20. 02. 2023
This channel for TIDZIWE TV
NKHANGA ZAONA _ DPP YAMENYA GALU NDIPO MBUYACHE WAONEKA
NKHANGA ZAONA _ DPP YAMENYA GALU NDIPO MBUYACHE WAONEKA
zhlédnutí: 10 668
Video
BEN LONGWE WAYAMBA KUMANYOZA MITUNDU YA ANTHU 🇲🇼
zhlédnutí 5KPřed 7 měsíci
BEN LONGWE WAYAMBA KUMANYOZA MITUNDU YA ANTHU 🇲🇼
NKHANGA ZAONA- APOLICE AKUSAKASAKASO VICE PRESIDENT WA A BON KALINDO KUTI AMAGWIDWESO
zhlédnutí 14KPřed 7 měsíci
Tidziwe tv
NKHANGA ZAONA - MA PASSPORT ADINDIDWA KUTI AKAKHALE UMBONI PA KHOTI PA MULANDU WA FELEX MAGANGA🇲🇼🇲🇼
zhlédnutí 14KPřed 8 měsíci
Tidziwe tv
NKHANGA ZAONA - ANTHU OMWE APITA NDI PRESIDENT KUNJA NDI 210 OSAMANAMIZA A MALAWI 🇲🇼
zhlédnutí 7KPřed 8 měsíci
Tidziwe tv
ANTHU KU KASUNGU SAKUFUNANSO KUMVA DZINA LOTI CHAKWERA MAKUTU MWAWO🇲🇼
zhlédnutí 19KPřed 8 měsíci
Tidziwe tv
NKHANGA ZAONA-APEZEKA KWA NSINGANGA NDI CHOVALA CHA MKATI CHA MNYAMATA WAWO
zhlédnutí 68KPřed 8 měsíci
Tidziwe tv
KAMULEPO KALUWA KUYAKHULAPO ZA MALAWI FIRST
zhlédnutí 10KPřed 9 měsíci
KAMULEPO KALUWA KUYAKHULAPO ZA MALAWI FIRST
BUNGWE LA MALAWI FIRST 🇲🇼 KULI PUNGWE PUNGWE PAKATI PA BEN LONGWE KOMASO BON KALINDO🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
zhlédnutí 23KPřed 9 měsíci
BUNGWE LA MALAWI FIRST 🇲🇼 KULI PUNGWE PUNGWE PAKATI PA BEN LONGWE KOMASO BON KALINDO🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼🇲🇼
THOMAS CHIBADE WA MWALIRA KUCHIPATALA CHA KAMUZU CENTRAL KU LILONGWE
zhlédnutí 9KPřed 9 měsíci
THOMAS CHIBADE WA MWALIRA KUCHIPATALA CHA KAMUZU CENTRAL KU LILONGWE
KENNETH MSONDA WAPASIDWA NDALAMA KUCHOKERA KU MCP KUTI ADZITENGA INJUNCTION KU DPP
zhlédnutí 15KPřed 9 měsíci
KENNETH MSONDA WAPASIDWA NDALAMA KUCHOKERA KU MCP KUTI ADZITENGA INJUNCTION KU DPP
NKHANGA ZAONA - YASALA MISIKA IWIRI KUTI A OTCHE ANYAMATA AKWA NSUNDWE
zhlédnutí 12KPřed 9 měsíci
NKHANGA ZAONA - YASALA MISIKA IWIRI KUTI A OTCHE ANYAMATA AKWA NSUNDWE
NKHANGA ZAONA -ANTHU AMENE AKAOTCHA MISIKA MADELAMU APASIDWA NDALAMA ZAWO
zhlédnutí 10KPřed 9 měsíci
NKHANGA ZAONA -ANTHU AMENE AKAOTCHA MISIKA MADELAMU APASIDWA NDALAMA ZAWO
NKHANGA ZAONA - AKUFUNA KUTENGA INJECTION KUTI HRA ISACHITITSE MADEMO
zhlédnutí 8KPřed 9 měsíci
NKHANGA ZAONA - AKUFUNA KUTENGA INJECTION KUTI HRA ISACHITITSE MADEMO
MCP YAKOZANSO UPANDU OLEPHERETSA MADEMO OMWE MALAWI FIRST AKONZA
zhlédnutí 9KPřed 9 měsíci
MCP YAKOZANSO UPANDU OLEPHERETSA MADEMO OMWE MALAWI FIRST AKONZA
NKHANGA ZAONA - TANZANIA YATI IKUFUNA NDALAMA ZAWO ZOMWE BOMA LA MALAWI INANGONGOLA ZA MAFUTA
zhlédnutí 7KPřed 9 měsíci
NKHANGA ZAONA - TANZANIA YATI IKUFUNA NDALAMA ZAWO ZOMWE BOMA LA MALAWI INANGONGOLA ZA MAFUTA
SADYEKA WADYEKA LERO, ANTHU ATAFIKA POTOPA OSACHITIRA MWINA KOMA KUDYA FISI
zhlédnutí 2KPřed 9 měsíci
SADYEKA WADYEKA LERO, ANTHU ATAFIKA POTOPA OSACHITIRA MWINA KOMA KUDYA FISI
NKHANGA ZAONA KULINDERA(RSA) KUNALI CHIPWIRIKITI POMWE AMALAWI AMAMENYANA NDI MZIKA ZA KU MOZAMBIQUE
zhlédnutí 14KPřed 9 měsíci
NKHANGA ZAONA KULINDERA(RSA) KUNALI CHIPWIRIKITI POMWE AMALAWI AMAMENYANA NDI MZIKA ZA KU MOZAMBIQUE
MA ACTIVIST ANU ALIPO ONSE TISADERE NKHAWA BY RC MPHEPO
zhlédnutí 6KPřed 9 měsíci
MA ACTIVIST ANU ALIPO ONSE TISADERE NKHAWA BY RC MPHEPO
MALO ABOMA AYAMBA KUTENGEDWA KUMAGWIRITSIDWA NTCHITO NDI CHIPANI
zhlédnutí 9KPřed 9 měsíci
MALO ABOMA AYAMBA KUTENGEDWA KUMAGWIRITSIDWA NTCHITO NDI CHIPANI
Mmakhwana adah
Ine ndili pheeeee vela limpopo fm
😂😂
From kasiya Lilongwe Limpopo Fm
Aji moyo Mozambique
Tikumvela ife
Koma awaso zaziiii ndiye iweyo zikukhuza pati kodi iweyo siwugona ndi nkazi wako nanga zimenezo amalawi zapindulira chani zaziiii
More 🔥🔥🔥🔥🔥
Zovuta
Koma mukudabwitsa amalawi kugulitsa mademo chifukwa chiyani?ndinu va mcp nonse?koma anthu mukutinama bodza
Mtaniwa uma kwana
Kkkkkkk
Nokhanokha oipa mwaonana akuonenso iwenso amen
Ku opposition ndie ndi kowawatsa mutu mpakana maina opanda tanthauzo
Ok.amalawi
Kuseka mopwambwana, zoyankhurazo zopanda nzeru , Za ziiiii Koma Ngati anthanyuwa zili ziwanda ambuye akuoneni kunena zoona mukutinyasa kwambiri kamba Koti zokamba Zanu zilibe umboni.
Fullish reporter
Olandana mkazi sanenera zabwino
Also were waiting for bakili tv thanks you guys
Ine niliwokodwa. Kwambiri pazimene mumalengeza leloamalawi tapenya chifukwa cha thanyiwa
Kkkk.kodi ndi ciizimba ca a pulezidentwa kuti doctor wao azigona / azichindana ndi animal ogwila ntchito ku state houseku.? Izitu zikhoza kukhala kuti dokotalayo sakhala wina kuposa mwini wake lazarus Chakwera yekha cizimba ca upulezident
Even in the USA they do same rituals
Mulungu azizikuteteza nthawi zonse.
😭😭😭😭 ooooh Malawi 😭
Tilinanu limozi Mr Tanyiwa kkkkkkkkkkkkkkkkkkk
You are the best
Nde pali vuto lanji?mwaiwala kuti mkazi wa bakili muluzi anagonana ndi bodygurd inunso ukape bwanji
❤❤❤mumakwana ❤❤❤❤❤❤❤kkkkkkkkkkk
Km mumandivesa kukoma timakunyadilani
Koma yah
Usapelekele umboni wabonza Mulungu akuwona zonse
Limpopo anapanga
Mark pastor 9:14
More fare🔥🔥🔥🔥 tili pambuyopanu
takudyadirani tizikupemperelani kut asakupezeni
Only God knows my future
Kodi iwowo sadzafa
Iipopo fm mukutiimilira keep it up to
Continue telling the truth
Mwanena mau bambo kusankhana mitundu sibwino ayi tonse ndife amalawi.
Nice song
Umatha mamwene
MCP inu mwalephera kodizotichipanicha MCP mchakupha anthu anyakunenaliti komansokuopseza Amalawi
Amen mulungu simunthu ndithu mau achirimbikitso
akufuna azabele chisakho km
Koma nyimbo zachuluka
Ndipo musasiye mukutisegula maso❤
Kodi mayi ameneyo wabuyi buyi ndindani abale
Ndiyakhepo pa mayi akunedwayo malemba akunena kut . Wawuze athu zomwe wawona ndimaso wosati zakuva ndiyena ayi kid chikakhala chabodza wukwanitsa kwawuza athu ones amen wawuzawo pepani baba yakhulani zowomwe mwawona ndimaso
Umbon otan nanyero iwe mot wekasukuona muyaluka ambilitu ndikuuzen
Olomwam,bera ndalama kalindo musaganize kut akusiyan choncho kuyaluka muyaruka ndithu apolice otan inu minyeromwanu nonse