Chifukwa Chenicheni Chomwe Shepherd Bushiri Akumangira Mzinda Wa GOSHEN CITY

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 23. 06. 2022
  • if you like my content and would like to support me further, please
    PayPal
    ➡️To Donate please use PayPal www.paypal.me/hanifamalawi
    Business/Sponsor Inquiries //hanifamw.suggestions@gmail.com
    Mu November mchaka cha 2021, pamene mlaliki Shepherd Bushiri pamodzi ndi mkazi wake Mary anathawa belo mdziko la South Africa mkubwera kuno ku Malawi, anthu ambiri anayesa kuti basi watha ndipo sangapangenso chilichonse cholozeka. Hotel yake yotchedwa Sparkling and Spa yomwe ili mu dera wa Rustenburg mdzikolo inayamba kupita pansi popeza malonda sankayenda. Ndalama zomwe amkazipeza kuchoka mu chopereka chaku tchalichi kamba kakuthawaku izi zinayima. Kenako ali ku Malawi analengeza za scholarship yomwe iye akufuna kuthandiza ana osowa fees mma sukulu osiyanasiyana. Apa anthu sanamukhulupilire popeza amkati alibe ndalama ndipo amapanga izi pongofuna kutchuka.
    Komatu Bushiri wadabwitsa ndikututumutsa anthu ambiri posachedwapa atalengeza kuti akumanga mzinda m’boma wa Mangochi womwe akuwutcha kuti Goshen City.

Komentáře • 120

  • @LovenessLester
    @LovenessLester Před 3 dny

    That's a great city for many Malawians let's learn how to appreciate this our man of God 🙏

  • @alfednjolobvi1591
    @alfednjolobvi1591 Před 2 lety +5

    Bushiri ur a great man that's why ur very blessed I wish if Malawi having too many people like u Bushiri who thinking about there homeland ur great indeed keep it up God bless you more

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe7231 Před 2 lety +5

    I salute Bushiri, he is one of a kind
    Creating jobs for the young people

  • @josephkaputa8502
    @josephkaputa8502 Před 2 lety +3

    He is agood man coz he is dealing with poverty,big up B

  • @teddybanda8989
    @teddybanda8989 Před 2 lety +12

    That guy has got gold mines here in zambia 🇿🇲 and different countries

  • @stevechizaka9908
    @stevechizaka9908 Před 2 lety +3

    Dziko la malawi silimatukuka ndi nkhani ngati zimenezi. Munthu ngati akumanga town yamakono ngati imeneyi mudziko lathu.ife bwezi tikuonesa chikondi kwaiye ndikumulimbikisa osati kumufookesa pazinkhani zopanda Pache. Anthu akatangale akuwaziwa kale bwanji osamakawafufuza amenewo

  • @mussawilliam5684
    @mussawilliam5684 Před 2 lety +2

    Vuto ndilokuti ife a malawi makamaka kumipandoko kwachuluka achule kwambili mwachisanzo ine ndili kuno ku south Africa ndapedza ndalama ndithawile dziko lakwathu adzafuna kundifufudza ndiye uchulewo ugalu a aphaka Bushili akufuna kutukula dziko lakumalawi ndiye pakupedzeka agalu ena monga amulaka malilo ndijelasi yao kudzolowela kuvutika ugalu basi Bushiri akufuna kutukula dziko lamalawi

  • @michealmwimba6084
    @michealmwimba6084 Před rokem +2

    I just like the way you express yourself in chichewa its so amazing and keep up the good work

  • @lucksonlongwe1658
    @lucksonlongwe1658 Před rokem +4

    Best wishes to man of God. Continue your work. God is with you.

  • @madakasosoch4322
    @madakasosoch4322 Před rokem +3

    He is going great work to develop Malawi

  • @maxwellmustaffaalickalick1745

    Ife anthu akuda ndichoncho sanje kwambiri i respect him a lot

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Před rokem +2

    Goshen City is a product of powerful vision

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 Před rokem +2

    Hard workers always think about changing things .All the best man

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 Před 2 lety +17

    He is doing great work to develop Malawi

  • @isaacschamatwa3596
    @isaacschamatwa3596 Před rokem +1

    such a very good tone,Bushiri is doing such a good job

  • @mollymadzibane
    @mollymadzibane Před rokem

    My Father My Prophet you are doing great job . You are creating work also for Malawians generation . I tap into your Annointing my Prophet . May God bless you all your Enemies will Scarter one by one Molly limpopo

  • @biggyk7740
    @biggyk7740 Před rokem

    I will always support bushiri he is a true citizen of Malawi

  • @williamlahman2787
    @williamlahman2787 Před rokem +1

    Let him to fulfill his duties,. He's so young, hope will do mo than that. All those jealous people must fall. Almighty bless him

  • @joebanda3732
    @joebanda3732 Před rokem +3

    You are doing extremely well Sir I like your tone. U got a very bright future. God will exalt you this year. Stay focused and pray more

  • @hoekboy1102
    @hoekboy1102 Před 2 lety +3

    I salute you Bushiri I will be Uber driver there

  • @harrietmwika8695
    @harrietmwika8695 Před rokem +1

    Love the Bushiris keep it up and God bless.

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 Před rokem +2

    Good work Prophet Bushiri

  • @mederinausain6913
    @mederinausain6913 Před rokem +1

    Bushili ndi one akupotsa president ulemu wanu a bushili za ndare simupanga nawo koma kukwedza malawi pa sogolo ..koma muzandilembeko tchito

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Před 9 dny

    Akurephera chakwera kutukura ziko.rino angoononga ndarama chakwera chito zamanja ako zikuchitire umboni bushiri

  • @machonabanda5752
    @machonabanda5752 Před 2 lety +5

    Hanifa you are the best ♥️♥️🙏🙏

  • @chifundonkhoma3642
    @chifundonkhoma3642 Před 2 lety +1

    Komatu anthu mupole moto... Mmalo mopanga njira zothana ndi umphawi omwe satana anakutembererani nawowo.. Mukulimbana ndiwo mulungu adawadalitsa, kutaya nthawi ndi za zii limbikirani kupemphera siyani msanje, mulungu adzaona mokudalitsira musiyeni Shepherd Bushiri apange zothandiza human kind

  • @benitozack6523
    @benitozack6523 Před rokem

    Don't be jealous with someone who is doing great work,because that city will change many Malawians

  • @jestinanamkonda1495
    @jestinanamkonda1495 Před 2 lety +4

    The annointing of Papa Bushiri breaks the yokes of poverty. Try it. You don't know the businesses Bushiri has. Why being so rough without the knowledge of his wealth and Riches. He is the third richest person in Malawi nde mumati ndalama azitani nazo?
    They devil will never be happy with a progressive person

  • @willardakidy6916
    @willardakidy6916 Před 2 lety +1

    Akulephera mapulesident kutukura dziko lanthu ineyo ndingoti Malawi mwana tingathe kumaloza chala kwaathu kuti town yakwathu iyo mulungu pasongolo basi

  • @agnessmpungalume1446
    @agnessmpungalume1446 Před rokem

    Just wow
    Beautiful masophenya

  • @bashiriyusufu1224
    @bashiriyusufu1224 Před 2 lety

    🔥🔥🔥Wabwela ngat coming
    💪💪💪

  • @mbumbajilowele6511
    @mbumbajilowele6511 Před 2 lety

    Greatest man

  • @gloriabanda6552
    @gloriabanda6552 Před rokem +1

    this is great💯

  • @anthuochukapazambiaelishas4978

    Perfect

  • @wisdomktitus660
    @wisdomktitus660 Před rokem

    Aaa pajatu Malawi is full of kaduka,,enawa angofuna amudyere

  • @williamjusten6646
    @williamjusten6646 Před 2 lety +1

    Great job

  • @user-gs7wc3nx3q
    @user-gs7wc3nx3q Před 9 dny

    Bushiri uzangokhara president

  • @bobkenneth2947
    @bobkenneth2947 Před 2 lety +3

    A Malawi Munatani kodi kumangovuta pa zinthu zopanda pake MAJOR 1 akufuna kutimagira Town mukufuna kumufufuza chiyani at least he's creating jobs zomwe Atsogoleri athu saangakwanitse koma kuba basi ndi ma slangs and fluent English opanda pake hands of BUSHIRI Manga Town SHEPHERD...👏👏💪 Let Them Talk, Idiot's come on Homies If you want someone to investigate I'm gonna show you where to go Pitani ku TONSE ALLIANCE that's where you'll find thieves,mbava,akamatule,matsotsi,wawii,🤞😊

  • @innocentkandulu2825
    @innocentkandulu2825 Před rokem

    That's great

  • @praisemkutumula3348
    @praisemkutumula3348 Před rokem

    Great ideas

  • @johnboscozgambo71
    @johnboscozgambo71 Před rokem

    Thanks for budget

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 Před rokem

    I like profet he only does God mind not his

  • @promise3693
    @promise3693 Před 2 lety +1

    Nsanje aMalawi iiiii munthu akapanga chinthu basi zokamba mbweeee

  • @richardchaupe7231
    @richardchaupe7231 Před 2 lety +6

    Please do the same content in English to enable none Malawians understand
    Unless you are from Zambia and some Zimbabwians can understand

    • @brucewarchild2156
      @brucewarchild2156 Před 2 lety

      It's none of foreigners business

    • @chifundonkhoma3642
      @chifundonkhoma3642 Před 2 lety

      Kkkkkkk OK fine.... Please people stop being jealous,instead of focusing on your demonic poverty , you waste time with whom YAHWE blessed... Learn to love one another.. Learn to thank God......

  • @geoffreychimutu6654
    @geoffreychimutu6654 Před rokem

    More fire

  • @duduzilesimelane9208
    @duduzilesimelane9208 Před rokem

    Man of God who only does God mind not him

  • @englishboy6570
    @englishboy6570 Před 2 lety +4

    Vuto la amalawi ndinsanje basi

    • @jestinanamkonda1495
      @jestinanamkonda1495 Před 2 lety +2

      That is the problem of Malawians

    • @jtpi8362
      @jtpi8362 Před 2 lety +1

      Ndi izi mukuziona ku ma comments kuno, anthu a nsanje akumunyozabe m'malo moyamikila kuti a Malawi ambiri apeza ntchito kumeneko, komanso dziko lathu litchuka ntchito imeneyi ikatha.

  • @nelsonkausiwa4754
    @nelsonkausiwa4754 Před rokem

    Major one

  • @phikamomo9755
    @phikamomo9755 Před rokem

    Nice job

  • @mikegoodblessyoumenofgoodm3482

    Moti musangalale akubwelesa
    Chitukuko ku malawi sanjebasi

  • @limpopolimpopo2623
    @limpopolimpopo2623 Před 2 lety +2

    A Malawi sanje mlekeni atukule dziko lathu la Malawi

  • @simonndou5236
    @simonndou5236 Před rokem

    We need ro underatand in english too. Inam in South Africa.

  • @trymoo8479
    @trymoo8479 Před 2 lety +2

    Ohhh? At least

  • @webbyasterchengo4006
    @webbyasterchengo4006 Před 2 lety +1

    That's why ziko lamalawi lizakalabe losauka mphaka kale kale amufufuza bwanji ngati ziko lamalawi labeledwapo nsaja basi ziko losafuninara anthu zabwino

  • @beautyandnatureofafrica5334

    Nsanje amalawi.. Musiyen bushiri atukule dzulo lathu

  • @kondwanileonard9868
    @kondwanileonard9868 Před rokem

    Is right

  • @bonimpoya1439
    @bonimpoya1439 Před rokem

    Malawi goas on

  • @mabvutochimkondenji910

    uyu akhale vice

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw Před 5 měsíci

    Zoona zake afufuzidwee munali asadiki miya muzikomo olemera oti amatha kukuthandiza boma lo koma sanafikepo apo fufuzani ndithu

  • @newdavidomw
    @newdavidomw Před rokem

    bushiri ndi munthu modzi wachuma yemwe akuyika pa map malawi

  • @snetawailiyasa3215
    @snetawailiyasa3215 Před 2 lety

    Ok

  • @VincentChikopa-mm6ig
    @VincentChikopa-mm6ig Před 18 dny

    Muuze bushili mon

  • @thekuhespodcast
    @thekuhespodcast Před 2 lety +1

    The first to comment and hopefully will be the first resident of Goshen 😂

  • @giftphiri595
    @giftphiri595 Před 2 lety

    A Malawi ambiri amadana ndi chitukuko amafuna kuba chabe, Bushiri asaope munthu.

  • @manuelsamuel293
    @manuelsamuel293 Před rokem +1

    Let him to do what he want to do and moreover he is doing that in his country, so let those dogs who has jealous with him to smile urine

  • @hendmorsoni32
    @hendmorsoni32 Před rokem

    Malawi akukanika kutukuka chifukwa chansanje

  • @olipamaseko2693
    @olipamaseko2693 Před 8 měsíci

    Aaaa ndalamazi aaaa

  • @collinsassenga3711
    @collinsassenga3711 Před rokem

    Maiko azathu anthu ngati amene ndi amene amatukura dziko,

  • @innocentchirwa3677
    @innocentchirwa3677 Před 2 lety

    Wabwera mwa coming

  • @tuntufyesichinga1071
    @tuntufyesichinga1071 Před rokem

    Okay?

  • @frankkamunde4575
    @frankkamunde4575 Před 2 lety

    nsanje ndimene yakula nsinkhu

  • @vitumbikochirwa2830
    @vitumbikochirwa2830 Před rokem

    Enemies of progress.Bushiri is doing this for the betterment of the country. This is malawi property,bushiri is just engineering.its the government which is going to benefit

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos1484 Před 2 lety

    Humm

  • @squatmansaidi561
    @squatmansaidi561 Před rokem

    Kkkk kma guys mawu awa akuyenera munthu wa ndemvu ku face

  • @ayamijackson1443
    @ayamijackson1443 Před 2 lety +1

    Gays tangoyamikilani muthuyu popangachiganizo chotukula zikolovesa chisonili ngati palizolakwika aakoze ndimulungu

    • @olipamaseko2693
      @olipamaseko2693 Před 8 měsíci

      Zokaikitsa ndalama zake aaa

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 Před 7 měsíci

      @@olipamaseko2693and so???? Nde mukufuna kuti munthu atani kodi. Olo Chakwera atasiya kupusa kwakeku this country can’t still go further because of people like you. Bitter and pathetic person

  • @mustafailanga5010
    @mustafailanga5010 Před 2 lety

    Sanje amalawi

  • @johnbihali9883
    @johnbihali9883 Před rokem

    But your report doesn't relate with the title of your presentation. Improve pliz

  • @lonmediatech5864
    @lonmediatech5864 Před 2 lety

    Iwe anthu azakumangisa.

  • @naongarluhanga3218
    @naongarluhanga3218 Před rokem

    No need of AcB because he z not apolitician

  • @fedinadisakala2380
    @fedinadisakala2380 Před 2 lety

    Sanje amalawi musiyeni munthu atukulemalawi

  • @masiyekalisitusidayton9210

    Apanga bwino nd2

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 Před 2 lety +2

    Ppl are serious wth him ......for show bushiri is doing good jobs for better malawians

  • @user-vo4yj7vz2r
    @user-vo4yj7vz2r Před 5 měsíci

    Wabodza iwe

  • @phirisandfore643
    @phirisandfore643 Před rokem

    Papa help me to change my life

  • @user-ng2nu6xn9x
    @user-ng2nu6xn9x Před rokem

    AKADAKHALA KUTI ANTHU ENANSO AMAKHOBILI AKU MALAWI ALI NDI MOYO AKUONETSA A SHEPHERD BUSHIRI PANOPA MALAWI AKADAKHALA ATATUKUKA KOOPSYA

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 Před 7 měsíci

      Ndipo nzoona kunoku anthu ake ngansanje yauchitsilu nayo

  • @cadohjabu5565
    @cadohjabu5565 Před rokem +1

    Mlandu Ukudikila ku South Africa Aonetse chitsanzo chabwino

  • @FacekidofficialmozMoz

    🇲🇿Hi

  • @patchipanga8445
    @patchipanga8445 Před 2 lety

    Amange Malawi basi

  • @sidickbadat1086
    @sidickbadat1086 Před rokem

    You have to screen this man the so called Prophet, whenever he got his money and how he made it, because this doesn’t look normal at all.

  • @jonathandube9422
    @jonathandube9422 Před rokem

    Bushili is a hill

  • @amosnyirenda5712
    @amosnyirenda5712 Před 2 lety +1

    Zot zikuyenda chifukwa cha a Bushiri nde bodza the guy is bad luck kungobwera zinthu kuzsiiratu kuyenda kumalawi kuno. I dont like this guy

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 Před 7 měsíci

      Nchifukwa chake this country can’t go further because of sick and twisted people like you. If you don’t like him very good but don’t shit on whatever good thing he’s doing. And he didn’t ask you to like him or not. Tabakhalabe pa umphawi wakowo mfiti iwe

  • @fridayngungadaud731
    @fridayngungadaud731 Před 2 lety

    Channel ichi sindichikhulupirila anta

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 Před 9 měsíci

      Amaphatikiza choonadi ndi bodza vuto lake ndilimenelo

  • @rasheedbanert7086
    @rasheedbanert7086 Před rokem

    Zasatanic basi mboli yako iwe

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw Před 5 měsíci

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @bryanfuimaono709
    @bryanfuimaono709 Před rokem

    you need to speak in English

  • @KAIPAAA3211
    @KAIPAAA3211 Před 2 lety +1

    Wakuba wabela anthu ambiri ku south aafrica, amawanamiza anthu ambiri aike ndalama ku acount yake miez itatu apeza ndalama zambili ku ma count ao, ambiri akulila

    • @jomonor4915
      @jomonor4915 Před 2 lety +2

      Dziko likufunika kukhala ndi munthu ngati uyu,uyutu amadzigwilila ntchito pa yekha wosati zomaba misonkho ya anthu.papa yr great wishing yu best mwatimasula amalawife

    • @saudamwanyali8700
      @saudamwanyali8700 Před 2 lety

      Do you hv a proof for wat u a sayin

    • @ronaldchirwa253
      @ronaldchirwa253 Před rokem

      Tazingogwirani ntchito apa... wakuberanipo chan chanu kapena cha makolo anu?

    • @yamikanijames6915
      @yamikanijames6915 Před 9 měsíci

      Then akuba bwinotu coz he is stealing to help others

  • @KAIPAAA3211
    @KAIPAAA3211 Před 2 lety +1

    Mbava yoo pya

  • @akiramlw
    @akiramlw Před 2 lety

    Hanifa give me your number ndufuna interview ya late Grace chinga ija

  • @louisbanda643
    @louisbanda643 Před rokem

    Great job