Chifukwa Chenicheni Chomwe Shepherd Bushiri Akumangira Mzinda Wa GOSHEN CITY
Vložit
- čas přidán 23. 06. 2022
- if you like my content and would like to support me further, please
PayPal
➡️To Donate please use PayPal www.paypal.me/hanifamalawi
Business/Sponsor Inquiries //hanifamw.suggestions@gmail.com
Mu November mchaka cha 2021, pamene mlaliki Shepherd Bushiri pamodzi ndi mkazi wake Mary anathawa belo mdziko la South Africa mkubwera kuno ku Malawi, anthu ambiri anayesa kuti basi watha ndipo sangapangenso chilichonse cholozeka. Hotel yake yotchedwa Sparkling and Spa yomwe ili mu dera wa Rustenburg mdzikolo inayamba kupita pansi popeza malonda sankayenda. Ndalama zomwe amkazipeza kuchoka mu chopereka chaku tchalichi kamba kakuthawaku izi zinayima. Kenako ali ku Malawi analengeza za scholarship yomwe iye akufuna kuthandiza ana osowa fees mma sukulu osiyanasiyana. Apa anthu sanamukhulupilire popeza amkati alibe ndalama ndipo amapanga izi pongofuna kutchuka.
Komatu Bushiri wadabwitsa ndikututumutsa anthu ambiri posachedwapa atalengeza kuti akumanga mzinda m’boma wa Mangochi womwe akuwutcha kuti Goshen City.
That's a great city for many Malawians let's learn how to appreciate this our man of God 🙏
Bushiri ur a great man that's why ur very blessed I wish if Malawi having too many people like u Bushiri who thinking about there homeland ur great indeed keep it up God bless you more
I salute Bushiri, he is one of a kind
Creating jobs for the young people
He is agood man coz he is dealing with poverty,big up B
That guy has got gold mines here in zambia 🇿🇲 and different countries
Where in Zambia?
Dziko la malawi silimatukuka ndi nkhani ngati zimenezi. Munthu ngati akumanga town yamakono ngati imeneyi mudziko lathu.ife bwezi tikuonesa chikondi kwaiye ndikumulimbikisa osati kumufookesa pazinkhani zopanda Pache. Anthu akatangale akuwaziwa kale bwanji osamakawafufuza amenewo
Vuto ndilokuti ife a malawi makamaka kumipandoko kwachuluka achule kwambili mwachisanzo ine ndili kuno ku south Africa ndapedza ndalama ndithawile dziko lakwathu adzafuna kundifufudza ndiye uchulewo ugalu a aphaka Bushili akufuna kutukula dziko lakumalawi ndiye pakupedzeka agalu ena monga amulaka malilo ndijelasi yao kudzolowela kuvutika ugalu basi Bushiri akufuna kutukula dziko lamalawi
I just like the way you express yourself in chichewa its so amazing and keep up the good work
Best wishes to man of God. Continue your work. God is with you.
He is going great work to develop Malawi
Ife anthu akuda ndichoncho sanje kwambiri i respect him a lot
Goshen City is a product of powerful vision
Hard workers always think about changing things .All the best man
He is doing great work to develop Malawi
t
such a very good tone,Bushiri is doing such a good job
My Father My Prophet you are doing great job . You are creating work also for Malawians generation . I tap into your Annointing my Prophet . May God bless you all your Enemies will Scarter one by one Molly limpopo
I will always support bushiri he is a true citizen of Malawi
Let him to fulfill his duties,. He's so young, hope will do mo than that. All those jealous people must fall. Almighty bless him
You are doing extremely well Sir I like your tone. U got a very bright future. God will exalt you this year. Stay focused and pray more
I salute you Bushiri I will be Uber driver there
Love the Bushiris keep it up and God bless.
Good work Prophet Bushiri
Bushili ndi one akupotsa president ulemu wanu a bushili za ndare simupanga nawo koma kukwedza malawi pa sogolo ..koma muzandilembeko tchito
Akurephera chakwera kutukura ziko.rino angoononga ndarama chakwera chito zamanja ako zikuchitire umboni bushiri
Hanifa you are the best ♥️♥️🙏🙏
Komatu anthu mupole moto... Mmalo mopanga njira zothana ndi umphawi omwe satana anakutembererani nawowo.. Mukulimbana ndiwo mulungu adawadalitsa, kutaya nthawi ndi za zii limbikirani kupemphera siyani msanje, mulungu adzaona mokudalitsira musiyeni Shepherd Bushiri apange zothandiza human kind
Don't be jealous with someone who is doing great work,because that city will change many Malawians
The annointing of Papa Bushiri breaks the yokes of poverty. Try it. You don't know the businesses Bushiri has. Why being so rough without the knowledge of his wealth and Riches. He is the third richest person in Malawi nde mumati ndalama azitani nazo?
They devil will never be happy with a progressive person
Akulephera mapulesident kutukura dziko lanthu ineyo ndingoti Malawi mwana tingathe kumaloza chala kwaathu kuti town yakwathu iyo mulungu pasongolo basi
Just wow
Beautiful masophenya
🔥🔥🔥Wabwela ngat coming
💪💪💪
Greatest man
this is great💯
Perfect
Aaa pajatu Malawi is full of kaduka,,enawa angofuna amudyere
Great job
Bushiri uzangokhara president
A Malawi Munatani kodi kumangovuta pa zinthu zopanda pake MAJOR 1 akufuna kutimagira Town mukufuna kumufufuza chiyani at least he's creating jobs zomwe Atsogoleri athu saangakwanitse koma kuba basi ndi ma slangs and fluent English opanda pake hands of BUSHIRI Manga Town SHEPHERD...👏👏💪 Let Them Talk, Idiot's come on Homies If you want someone to investigate I'm gonna show you where to go Pitani ku TONSE ALLIANCE that's where you'll find thieves,mbava,akamatule,matsotsi,wawii,🤞😊
That's great
Great ideas
Thanks for budget
I like profet he only does God mind not his
Nsanje aMalawi iiiii munthu akapanga chinthu basi zokamba mbweeee
Please do the same content in English to enable none Malawians understand
Unless you are from Zambia and some Zimbabwians can understand
It's none of foreigners business
Kkkkkkk OK fine.... Please people stop being jealous,instead of focusing on your demonic poverty , you waste time with whom YAHWE blessed... Learn to love one another.. Learn to thank God......
More fire
Man of God who only does God mind not him
Vuto la amalawi ndinsanje basi
That is the problem of Malawians
Ndi izi mukuziona ku ma comments kuno, anthu a nsanje akumunyozabe m'malo moyamikila kuti a Malawi ambiri apeza ntchito kumeneko, komanso dziko lathu litchuka ntchito imeneyi ikatha.
Major one
Nice job
Moti musangalale akubwelesa
Chitukuko ku malawi sanjebasi
A Malawi sanje mlekeni atukule dziko lathu la Malawi
We need ro underatand in english too. Inam in South Africa.
Ohhh? At least
That's why ziko lamalawi lizakalabe losauka mphaka kale kale amufufuza bwanji ngati ziko lamalawi labeledwapo nsaja basi ziko losafuninara anthu zabwino
Ndipo iyi nde ndi mfundo ndithu
Nsanje amalawi.. Musiyen bushiri atukule dzulo lathu
Is right
Malawi goas on
uyu akhale vice
Zoona zake afufuzidwee munali asadiki miya muzikomo olemera oti amatha kukuthandiza boma lo koma sanafikepo apo fufuzani ndithu
bushiri ndi munthu modzi wachuma yemwe akuyika pa map malawi
Ok
Muuze bushili mon
The first to comment and hopefully will be the first resident of Goshen 😂
L
A Malawi ambiri amadana ndi chitukuko amafuna kuba chabe, Bushiri asaope munthu.
Nzoona ndithu
Let him to do what he want to do and moreover he is doing that in his country, so let those dogs who has jealous with him to smile urine
Malawi akukanika kutukuka chifukwa chansanje
Aaaa ndalamazi aaaa
Maiko azathu anthu ngati amene ndi amene amatukura dziko,
Wabwera mwa coming
Okay?
nsanje ndimene yakula nsinkhu
Enemies of progress.Bushiri is doing this for the betterment of the country. This is malawi property,bushiri is just engineering.its the government which is going to benefit
Humm
Kkkk kma guys mawu awa akuyenera munthu wa ndemvu ku face
Gays tangoyamikilani muthuyu popangachiganizo chotukula zikolovesa chisonili ngati palizolakwika aakoze ndimulungu
Zokaikitsa ndalama zake aaa
@@olipamaseko2693and so???? Nde mukufuna kuti munthu atani kodi. Olo Chakwera atasiya kupusa kwakeku this country can’t still go further because of people like you. Bitter and pathetic person
Sanje amalawi
But your report doesn't relate with the title of your presentation. Improve pliz
Iwe anthu azakumangisa.
No need of AcB because he z not apolitician
Sanje amalawi musiyeni munthu atukulemalawi
Apanga bwino nd2
Ppl are serious wth him ......for show bushiri is doing good jobs for better malawians
Wabodza iwe
Papa help me to change my life
AKADAKHALA KUTI ANTHU ENANSO AMAKHOBILI AKU MALAWI ALI NDI MOYO AKUONETSA A SHEPHERD BUSHIRI PANOPA MALAWI AKADAKHALA ATATUKUKA KOOPSYA
Ndipo nzoona kunoku anthu ake ngansanje yauchitsilu nayo
Mlandu Ukudikila ku South Africa Aonetse chitsanzo chabwino
🇲🇿Hi
Amange Malawi basi
You have to screen this man the so called Prophet, whenever he got his money and how he made it, because this doesn’t look normal at all.
Bushili is a hill
Zot zikuyenda chifukwa cha a Bushiri nde bodza the guy is bad luck kungobwera zinthu kuzsiiratu kuyenda kumalawi kuno. I dont like this guy
Nchifukwa chake this country can’t go further because of sick and twisted people like you. If you don’t like him very good but don’t shit on whatever good thing he’s doing. And he didn’t ask you to like him or not. Tabakhalabe pa umphawi wakowo mfiti iwe
Channel ichi sindichikhulupirila anta
Amaphatikiza choonadi ndi bodza vuto lake ndilimenelo
Zasatanic basi mboli yako iwe
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
you need to speak in English
Wakuba wabela anthu ambiri ku south aafrica, amawanamiza anthu ambiri aike ndalama ku acount yake miez itatu apeza ndalama zambili ku ma count ao, ambiri akulila
Dziko likufunika kukhala ndi munthu ngati uyu,uyutu amadzigwilila ntchito pa yekha wosati zomaba misonkho ya anthu.papa yr great wishing yu best mwatimasula amalawife
Do you hv a proof for wat u a sayin
Tazingogwirani ntchito apa... wakuberanipo chan chanu kapena cha makolo anu?
Then akuba bwinotu coz he is stealing to help others
Mbava yoo pya
Anakubela chiyani????????????
Hanifa give me your number ndufuna interview ya late Grace chinga ija
Great job