Mu history yathu tili ndi nthawi yokumbukira achina John chilembwe Ndi gulu lake Achina Sangala Gadama Ndi ena Otero Osati anthu amene sanapindulire amalawiwa Tilibe ubwino wawo ndithu Kwa munthu amene anasatapo kapena kumva za mcp bwino lomwe Palibe angaifunire Rest in peace gulu limeneli Asogoleri ambiri ankalimbana ndi Asamunda nkumaika anthu awo pasogolo koma anthu awa amazuza anthu awo osusna nawo nkumaphedwa Zooona mmalawi weni weni Rest in peace Kwa zigawengazi Osaisunga bwanji misoziyo tizalire pa chilembwe day either kumukumbukira Bingu better than this crimals
You are a powerful researcher. I like how you put pieces together. I have learnt a lot of historical facts for malawi. My father is zambian but mother is malawi. Great documentary.
It's very complicated to remember this man his death when we remember our parents who died through him and Kamuzu Banda Cecilia Kazamila eish munthu amakoma akamwalira only God knows rest in peace
We can't remember him without remembering the death of Aaron Sangala, Gadama, Dick Matenje and some other people who were sent to their early graves because of politics.
Kodi iweyo ukakhala nawo pa chiweluzo kuti udziti John Tembo sakalowa kumwamba? Do u know the the relationship he had with God at the time of his passing? Sitiyankhula chonchi pa nthawi ya maliro galu iwe opanda khalidwe ndi mwambo
Muluzi TV ndi number One tchanelo of Malawi utube I like you man
Akumudikila achina mr Dundudzu chisiza Mr chipembele ndi amalawi ochuluka omwe anawampa 😭😭😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔
Km brother inuyo mumayimad pachlungamo, ndpo simumawopa, mulungu apitilize kukutetezan🙏
John tembo no rest in peace wakumoto basi
Kkkkkkkkk
Kkkkkkkkkkk
Nobody knows it's only God who can judge...
Timakonda kumvela khani zanu big course mumaikamo chilungamo chokha chokha. Big up broh
We will remember him like Malawian Yudas
He always stood for evil. He supported one-party system during Kamuzu. During Bakili he supported 3rd term just to fight Gwanda Chakwamba.
😂😂😂u are right 👍
Mu history yathu tili ndi nthawi yokumbukira achina John chilembwe
Ndi gulu lake
Achina Sangala Gadama
Ndi ena Otero
Osati anthu amene sanapindulire amalawiwa
Tilibe ubwino wawo ndithu
Kwa munthu amene anasatapo kapena kumva za mcp bwino lomwe
Palibe angaifunire Rest in peace gulu limeneli
Asogoleri ambiri ankalimbana ndi Asamunda nkumaika anthu awo pasogolo koma anthu awa amazuza anthu awo osusna nawo nkumaphedwa
Zooona mmalawi weni weni Rest in peace
Kwa zigawengazi
Osaisunga bwanji misoziyo tizalire pa chilembwe day either kumukumbukira Bingu better than this crimals
😂😂😂😂😂😂
@@CHINDEBVU You're very wise
Please give us history of Gwanda Chakwamba and why kamuzu choose him over John Tembo to be success of MCP
All in all we shallow remember Tembo but in a wrong way
Mzimu wa Gadama on repeat
The great historian. Man u r a good narrator ever, sending some from Lusaka Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Kip doin de good work bro God is and will protect u.
Munthu ochita zabwno amalandila madaliso. Upitilize kusegula anthu maso.
Our own interpreter ❤️🔥🔥
Rest in peace Mr Tembo🙏🙏
You are a powerful researcher. I like how you put pieces together. I have learnt a lot of historical facts for malawi. My father is zambian but mother is malawi. Great documentary.
Chipepeso kwa mabanja omwe sawona chilungamo pamilanduyi. Apume mumtendere. Thank you for documenting our history.
Ànzanu atulusatso mbili yake koma sitinamvele kudikla inu inu Mulungu anakupasan nyota yakayankhulidwe mukamayankula munthu amamva sekeseke
Resting In Piece Mr Tembo we don't want unnesessary history please only God judges the problem
Nanga osasiya kumveselako bwanji hiyaaa
It's very complicated to remember this man his death when we remember our parents who died through him and Kamuzu Banda Cecilia Kazamila eish munthu amakoma akamwalira only God knows rest in peace
Akazipedza ntchito zake zoipazo
May the blessings of anger fall upon him
Zainu aliyese akudziwa Big up Mr kma za RIP kwa chigawengachi ndepalibe
😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Original bakili muluzi tv ❤❤❤
Big up bro you need to be our president future
Thanks for the nice video continue providing wonderful data
penatu I just like your voice, koma kanyimboko mopempha ndimayesera kukasewera pa keyboard, I wish simudzandipanga sue?
Thanks brother 🙏
Ndimakhala ndikudikilila kuti no matter what muyiponya imeneyo big up bro mulungu adzikhala nanu nthawi zonse my brother
Kkkkkkkk this guy yooo
Mbamba bigger wanga❤❤❤❤❤🎉
Big up bro out own interpreter ❤️🔥🔥🔥🔥
Mwanena mwanena basi chilungamo chimawawa but anyway ndimamukonda John tembo moti nkhata yanga ndiyo ili patsogoloyo ndukapeleka 🔥
Akanyimbi ozola manyi ku maso
AAAA munthu woyipa uyu Joni unawona ngati uzakhala wamuyaya unapha azibale anthu iwe
I love you bro
Big man❤❤❤❤
Imfayi osatengakoso amene akutizunza lerowa bwanji apite onsewa basi
My king ❤
God will continue to panish you where ever you are, Enjoy it John Tembo 👉🔥🔥 Kadzamila will join you very soon
BIG 👍
We can't remember him without remembering the death of Aaron Sangala, Gadama, Dick Matenje and some other people who were sent to their early graves because of politics.
Next mai kazamila dai please
Congratulations bro everything else is good
Ndimupemphe mulungu kuti amukaniretu ameneyi pansi pompano asanamukwilire. Galu wa sankho ameneyi, anabalitsa umasiye ku mtundu wa amalawi, Nsaname ankhanza asamamveredwe chisoni. 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥Apserere ku gehena akupitako
Tidzamukumbukira ngati mfiti. Kupha ndi chikhalidwe cha MCP. Pano ikupha a Malawi ndi njala.
Yeah salute big
This man has a stinking legacy.
We will remember John Tembo as a thug .
Thank you bg mn respectful
I hope he is enjoying the 🔥
Rest in peace Mr Tembo
Ayende bwino ku gahenako ameneyo
Exactly madder case Brah
Mai mulungu wanga ine Joni tembo nde panopo Ali kuti siwafaso mulungutu simunthu
John tembo ndimunthu wakumoto
Akuti Nyimbo ikhale Nzimu wa Agadama
Rest in the 🔥🔥🔥 John Tembo , Kadzamila will join you later 👉🔥🔥🔥
Nobody knows it's only God who can judge.
Azikhale ngoma ndale ndizosala tembo ndameneo wafayo uziyakhula bwino ngt uzafa wamva umuuzeso cakwelayo kut amwene tifa tiyen tizikhala bwino ndi anthu
Munthu wankhanza, wakupha, opanda chisoni
Udasi😢
It good to remind people
Go's round comes round palibe wamuyaya anayiwalazimenezo
Ndizamkumbuka ngat chimuthu choipisisa pokupha a Malawi azake Rest in fire
Nobody knows it's only God who can judge..
😂 You are funny ya interpreter yokhayo wakhwana
Akawapeza komweko onse omwe anaphawa ..
Rest well Mr murderer
Following 😊
❤❤❤
Let Malawians mourn Tembo peacefully than br br br
Good
Nah I can't say rest in peace coz I know that he is not going to rest this guy did alot there rest for people who did murder
Nobody knows it's only God who can judge.
Mumakwana big ulemu wanu
Yooo kkkkkkkkk great guy
There's no need to remember him is only cruel people who support mcp like chilima joice banda lucius banda
Tidzamukumbukila ngati munthu oyipa amene adapha wanthu osalakwa satana
Yes
Mbuzi iz zonama aaaa a Galu awa
Kodi iweyo ukakhala nawo pa chiweluzo kuti udziti John Tembo sakalowa kumwamba? Do u know the the relationship he had with God at the time of his passing?
Sitiyankhula chonchi pa nthawi ya maliro galu iwe opanda khalidwe ndi mwambo
In time like this, sikwabwinodi. Any way pakuti ndi nthawi ya demon class
Tembo kungoka pulumuka ku ufumu wakumwamba dziwani kut anthu onse okupha alubino akapulumuka pamodzi ndi aliyense amene anaphako munthu, mwachudule dziko lonse lapansi likapulumuka
Jon tembe anayili munthu oyipisisa ngati chakwera nd zikhale Ng'oma
Rest in peaces son of jazbel pano akukondwa ku helo ndi kamuzu wake rubbish
Ndipo ngt galu ameneo sanalape ndithu mulungu amulange komwe aliko mfit yamunthu nde iweo zikhale ngoma uziwe kut chuma sutenga kumanda
Ndiyenso choti aziwe zikhale ng'oma pano sikuseli kwa 2000 kuti anthu abadwa nthawi ya bakili muluzi kuti zithu zonse zinali chonchi kuseli kwa 2000 kunalibe tv kunalibe ma Radios komanso ukangoyelekeza ku chula zina la kamuzu amakuuzakuti ankhwazi akukumvani ku sanjika kukhala ngati malawi yonse anayi microphone everywhere anthu amaletsedwa kupanga mabissines bottom line John tembo tizamukumbukila ngati munthu mmodzi oipa kwambiri kuno ku malawi John tembo kamuzu banda anali anthu oipa kwambiri Ndiye pano mmalo mwa john tembo akufuna akhale mulowammalo wake zikhale ng'oma munthu oipanso kwambiri
Alright
Anali Muthu woyipa kwambili Tembo anazuza azake mu ndale
Rest in peace Mr Jon tembo
Oweludza ndi mwini chilengedwe not us
Remember him as wopereka chakudya ku ng'ona kwa wina aliyense amene amadana ndi kamuzu the real devil
Ulemu upite kwainu big ulibwino big serious
MCP kupha ndikoyamwira, they're being led by Demons 😢😢😢
Rest to he'll jonh
Machende ske
Zoopsatu zithu zake
Ichi ndi chigawenga chomaliza Cha MCP kukaliwa ku gahena. Chakwera adzakhala chimtseka khomo ku gehenako
😂😂😂😂
John Tembo chinali Chigewega
Gahena is waiting for him
Eeeeee koma john tembo wagwira ntchito yopha anthu iiiii
Akalowa kuthako kwa make mbuzi imeneyi. Ndisaname I don't even want to hear the name of joni tembo. Munthu oyiiipa zedi.
Ndimadabwatu😂 kuti zikuphonyani bwanj
Nthaw zina kukhala wabwino mu ziko lino lapasi zimakuchitila ubwino shaa
Wini adziti tikufuna timange wa Bakili muluzi TV koma padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta yes zomwe tikufuna ife ndizimezi wina adziti tikufuna timange wa Bakili muluzi tv zosatheka wina asayelekeze kumanga pa Bakili TVmuluzi asafe chifukwa akafa pavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta chifukwa timakonda kwambil chifukwa chilichose chomwe amanena zoonandi ife timafufuza zonse zomwe mukunena ndizoona ndithu ndiye wina aziti tikufuna timange wa Bakili muluzi TV Malawi mono padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta
Ndiwe chitsiru wabodza iwe Tembo anabadwira kukhola ntcheu osati Dedza
Munthu wamwalira mulimbananYe bwanji?
Choka iwe mbuzi
Tzamukimbukira chifkwa cha kupha ma minister 4 cha mma 80's
Ulemuwanu big gayena Malo ake a John temporarily
Nobody knows it's only God who can judge