Malemu John Tembo; Tidzamukumbukira bwanji ngati amalawi

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 30. 09. 2023

Komentáře • 240

  • @husseinmoffatt
    @husseinmoffatt Před 9 měsíci +11

    Muluzi TV ndi number One tchanelo of Malawi utube I like you man

  • @user-vu8si9eb6k
    @user-vu8si9eb6k Před 9 měsíci +7

    Akumudikila achina mr Dundudzu chisiza Mr chipembele ndi amalawi ochuluka omwe anawampa 😭😭😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔

  • @elizamaster2168
    @elizamaster2168 Před 9 měsíci +6

    Km brother inuyo mumayimad pachlungamo, ndpo simumawopa, mulungu apitilize kukutetezan🙏

  • @rosseshaibu1576
    @rosseshaibu1576 Před 9 měsíci +16

    John tembo no rest in peace wakumoto basi

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h Před 9 měsíci +5

    Timakonda kumvela khani zanu big course mumaikamo chilungamo chokha chokha. Big up broh

  • @CHINDEBVU
    @CHINDEBVU Před 9 měsíci +24

    We will remember him like Malawian Yudas

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Před 9 měsíci

      He always stood for evil. He supported one-party system during Kamuzu. During Bakili he supported 3rd term just to fight Gwanda Chakwamba.

    • @GwazaGomuzy
      @GwazaGomuzy Před 9 měsíci

      😂😂😂u are right 👍

    • @CHINDEBVU
      @CHINDEBVU Před 9 měsíci +2

      Mu history yathu tili ndi nthawi yokumbukira achina John chilembwe
      Ndi gulu lake
      Achina Sangala Gadama
      Ndi ena Otero
      Osati anthu amene sanapindulire amalawiwa
      Tilibe ubwino wawo ndithu
      Kwa munthu amene anasatapo kapena kumva za mcp bwino lomwe
      Palibe angaifunire Rest in peace gulu limeneli
      Asogoleri ambiri ankalimbana ndi Asamunda nkumaika anthu awo pasogolo koma anthu awa amazuza anthu awo osusna nawo nkumaphedwa
      Zooona mmalawi weni weni Rest in peace
      Kwa zigawengazi
      Osaisunga bwanji misoziyo tizalire pa chilembwe day either kumukumbukira Bingu better than this crimals

    • @patriciacraiton-sf5vu
      @patriciacraiton-sf5vu Před 9 měsíci

      😂😂😂😂😂😂

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Před 9 měsíci

      @@CHINDEBVU You're very wise

  • @prayphiri3184
    @prayphiri3184 Před 9 měsíci +8

    Please give us history of Gwanda Chakwamba and why kamuzu choose him over John Tembo to be success of MCP

  • @WashingtonMalunga-cw2pe
    @WashingtonMalunga-cw2pe Před 9 měsíci +7

    All in all we shallow remember Tembo but in a wrong way
    Mzimu wa Gadama on repeat

  • @josephphiri4185
    @josephphiri4185 Před 9 měsíci +2

    The great historian. Man u r a good narrator ever, sending some from Lusaka Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 Před 9 měsíci +2

    Kip doin de good work bro God is and will protect u.
    Munthu ochita zabwno amalandila madaliso. Upitilize kusegula anthu maso.

  • @JacksonDamiano-ko8ui
    @JacksonDamiano-ko8ui Před 9 měsíci +7

    Our own interpreter ❤️🔥🔥
    Rest in peace Mr Tembo🙏🙏

  • @cheruartsofficial
    @cheruartsofficial Před 9 měsíci +9

    You are a powerful researcher. I like how you put pieces together. I have learnt a lot of historical facts for malawi. My father is zambian but mother is malawi. Great documentary.

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p Před 9 měsíci +1

    Chipepeso kwa mabanja omwe sawona chilungamo pamilanduyi. Apume mumtendere. Thank you for documenting our history.

  • @AshrafuBwanali-qi3my
    @AshrafuBwanali-qi3my Před 9 měsíci +8

    Ànzanu atulusatso mbili yake koma sitinamvele kudikla inu inu Mulungu anakupasan nyota yakayankhulidwe mukamayankula munthu amamva sekeseke

  • @martinkalaka2667
    @martinkalaka2667 Před 9 měsíci +3

    Resting In Piece Mr Tembo we don't want unnesessary history please only God judges the problem

    • @eunicemoyo6024
      @eunicemoyo6024 Před 9 měsíci +3

      Nanga osasiya kumveselako bwanji hiyaaa

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 Před 9 měsíci +5

    It's very complicated to remember this man his death when we remember our parents who died through him and Kamuzu Banda Cecilia Kazamila eish munthu amakoma akamwalira only God knows rest in peace

  • @dingiswayokatundu2696
    @dingiswayokatundu2696 Před 9 měsíci +5

    May the blessings of anger fall upon him

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev Před 9 měsíci +3

    Zainu aliyese akudziwa Big up Mr kma za RIP kwa chigawengachi ndepalibe

  • @ibrahimmeemzy9754
    @ibrahimmeemzy9754 Před 9 měsíci +4

    Original bakili muluzi tv ❤❤❤

  • @mbaliehaward947
    @mbaliehaward947 Před 9 měsíci +1

    Big up bro you need to be our president future

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 Před 9 měsíci +2

    Thanks for the nice video continue providing wonderful data

  • @mataxsimon1737
    @mataxsimon1737 Před 9 měsíci +2

    penatu I just like your voice, koma kanyimboko mopempha ndimayesera kukasewera pa keyboard, I wish simudzandipanga sue?

  • @abisalomchunga6695
    @abisalomchunga6695 Před 9 měsíci +2

    Thanks brother 🙏

  • @christophermkhize1991
    @christophermkhize1991 Před 9 měsíci +6

    Ndimakhala ndikudikilila kuti no matter what muyiponya imeneyo big up bro mulungu adzikhala nanu nthawi zonse my brother

  • @gracetjomane-jj3ib
    @gracetjomane-jj3ib Před 9 měsíci +3

    Mbamba bigger wanga❤❤❤❤❤🎉

  • @JacksonDamiano-ko8ui
    @JacksonDamiano-ko8ui Před 9 měsíci +3

    Big up bro out own interpreter ❤️🔥🔥🔥🔥

  • @ChomeNgondolo-uh5mu
    @ChomeNgondolo-uh5mu Před 9 měsíci +3

    Mwanena mwanena basi chilungamo chimawawa but anyway ndimamukonda John tembo moti nkhata yanga ndiyo ili patsogoloyo ndukapeleka 🔥

    • @Sandi-xr6ug
      @Sandi-xr6ug Před 9 měsíci +1

      Akanyimbi ozola manyi ku maso

  • @user-hs5xv6bk2f
    @user-hs5xv6bk2f Před 9 měsíci +2

    AAAA munthu woyipa uyu Joni unawona ngati uzakhala wamuyaya unapha azibale anthu iwe

  • @Cr7bianca
    @Cr7bianca Před 9 měsíci +3

    I love you bro

  • @YusufRahimu-be9hu
    @YusufRahimu-be9hu Před 9 měsíci +2

    Big man❤❤❤❤

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Před 9 měsíci +1

    Imfayi osatengakoso amene akutizunza lerowa bwanji apite onsewa basi

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w Před 9 měsíci +3

    My king ❤

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 9 měsíci

    God will continue to panish you where ever you are, Enjoy it John Tembo 👉🔥🔥 Kadzamila will join you very soon

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Před 9 měsíci +2

    BIG 👍

  • @edsonndalama2334
    @edsonndalama2334 Před 9 měsíci +2

    We can't remember him without remembering the death of Aaron Sangala, Gadama, Dick Matenje and some other people who were sent to their early graves because of politics.

  • @frankchavula3594
    @frankchavula3594 Před 9 měsíci +1

    Next mai kazamila dai please

  • @christopherbottoman9131
    @christopherbottoman9131 Před 9 měsíci +1

    Congratulations bro everything else is good

  • @user-tg8ye9yp8p
    @user-tg8ye9yp8p Před 9 měsíci +1

    Ndimupemphe mulungu kuti amukaniretu ameneyi pansi pompano asanamukwilire. Galu wa sankho ameneyi, anabalitsa umasiye ku mtundu wa amalawi, Nsaname ankhanza asamamveredwe chisoni. 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥Apserere ku gehena akupitako

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před 9 měsíci +2

    Tidzamukumbukira ngati mfiti. Kupha ndi chikhalidwe cha MCP. Pano ikupha a Malawi ndi njala.

  • @LUCIUSCHARLES-ei5vu
    @LUCIUSCHARLES-ei5vu Před 9 měsíci +1

    Yeah salute big

  • @francispanyenyeramithi764
    @francispanyenyeramithi764 Před 5 měsíci +1

    This man has a stinking legacy.

  • @ashikalam8616
    @ashikalam8616 Před 9 měsíci +3

    We will remember John Tembo as a thug .

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 Před 9 měsíci

    Thank you bg mn respectful

  • @robertchikaonda-mu1bg
    @robertchikaonda-mu1bg Před 9 měsíci +2

    I hope he is enjoying the 🔥

  • @edwinrobert5346
    @edwinrobert5346 Před 9 měsíci +3

    Rest in peace Mr Tembo

  • @user-tp7ze7qy3s
    @user-tp7ze7qy3s Před 9 měsíci +3

    Ayende bwino ku gahenako ameneyo

  • @sharifujoe7633
    @sharifujoe7633 Před 9 měsíci

    Exactly madder case Brah

  • @BenissoneErnesto-kn9bd
    @BenissoneErnesto-kn9bd Před 8 měsíci

    Mai mulungu wanga ine Joni tembo nde panopo Ali kuti siwafaso mulungutu simunthu

  • @rosseshaibu1576
    @rosseshaibu1576 Před 9 měsíci +2

    John tembo ndimunthu wakumoto

  • @shaik4123
    @shaik4123 Před 9 měsíci +1

    Akuti Nyimbo ikhale Nzimu wa Agadama

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před 8 měsíci

    Rest in the 🔥🔥🔥 John Tembo , Kadzamila will join you later 👉🔥🔥🔥

  • @TakosaGideon-ho6ng
    @TakosaGideon-ho6ng Před 9 měsíci

    Nobody knows it's only God who can judge.

  • @ishmaelmkuluma2013
    @ishmaelmkuluma2013 Před 9 měsíci +1

    Azikhale ngoma ndale ndizosala tembo ndameneo wafayo uziyakhula bwino ngt uzafa wamva umuuzeso cakwelayo kut amwene tifa tiyen tizikhala bwino ndi anthu

  • @joegibsonzulu2599
    @joegibsonzulu2599 Před 9 měsíci +3

    Munthu wankhanza, wakupha, opanda chisoni

  • @juniortsegula3847
    @juniortsegula3847 Před 9 měsíci +2

    Udasi😢

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Před 12 dny

    It good to remind people

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete Před 9 měsíci +1

    Go's round comes round palibe wamuyaya anayiwalazimenezo

  • @JohnesDishan
    @JohnesDishan Před 9 měsíci +1

    Ndizamkumbuka ngat chimuthu choipisisa pokupha a Malawi azake Rest in fire

  • @ririvilla1423
    @ririvilla1423 Před 9 měsíci +1

    😂 You are funny ya interpreter yokhayo wakhwana

  • @user-px9jd9co3v
    @user-px9jd9co3v Před 9 měsíci +1

    Akawapeza komweko onse omwe anaphawa ..

  • @ChikumbutsoPumani
    @ChikumbutsoPumani Před 9 měsíci +1

    Rest well Mr murderer

  • @user-qv6ey9ul9w
    @user-qv6ey9ul9w Před 9 měsíci

    Following 😊

  • @WysonChinyangalala-qj6oo
    @WysonChinyangalala-qj6oo Před 9 měsíci +2

    ❤❤❤

  • @BrightonPhiri-ug3gk
    @BrightonPhiri-ug3gk Před 9 měsíci +1

    Let Malawians mourn Tembo peacefully than br br br

  • @user-ge8lf8ii6g
    @user-ge8lf8ii6g Před 9 měsíci +1

    Good

  • @KanguwoGift
    @KanguwoGift Před 9 měsíci +3

    Nah I can't say rest in peace coz I know that he is not going to rest this guy did alot there rest for people who did murder

  • @JumaMboneka
    @JumaMboneka Před 9 měsíci +2

    Mumakwana big ulemu wanu

  • @staceycossam5933
    @staceycossam5933 Před 9 měsíci +2

    Yooo kkkkkkkkk great guy

  • @inkprokasungu9287
    @inkprokasungu9287 Před 9 měsíci +1

    There's no need to remember him is only cruel people who support mcp like chilima joice banda lucius banda

  • @DitebogoMarutle-wy8qo
    @DitebogoMarutle-wy8qo Před 9 měsíci +1

    Tidzamukumbukila ngati munthu oyipa amene adapha wanthu osalakwa satana

  • @giftevans2957
    @giftevans2957 Před 9 měsíci

    Yes

  • @fedson2050
    @fedson2050 Před 9 měsíci +1

    Mbuzi iz zonama aaaa a Galu awa

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 Před 9 měsíci +1

    Kodi iweyo ukakhala nawo pa chiweluzo kuti udziti John Tembo sakalowa kumwamba? Do u know the the relationship he had with God at the time of his passing?
    Sitiyankhula chonchi pa nthawi ya maliro galu iwe opanda khalidwe ndi mwambo

    • @rickiez
      @rickiez Před 9 měsíci +1

      In time like this, sikwabwinodi. Any way pakuti ndi nthawi ya demon class

  • @humairamalombe295
    @humairamalombe295 Před 9 měsíci +1

    Tembo kungoka pulumuka ku ufumu wakumwamba dziwani kut anthu onse okupha alubino akapulumuka pamodzi ndi aliyense amene anaphako munthu, mwachudule dziko lonse lapansi likapulumuka

  • @VioletChikopa-mx1ye
    @VioletChikopa-mx1ye Před 8 měsíci +1

    Jon tembe anayili munthu oyipisisa ngati chakwera nd zikhale Ng'oma

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Před 9 měsíci +2

    Rest in peaces son of jazbel pano akukondwa ku helo ndi kamuzu wake rubbish

  • @ishmaelmkuluma2013
    @ishmaelmkuluma2013 Před 9 měsíci +1

    Ndipo ngt galu ameneo sanalape ndithu mulungu amulange komwe aliko mfit yamunthu nde iweo zikhale ngoma uziwe kut chuma sutenga kumanda

  • @user-qi8xe7qh1e
    @user-qi8xe7qh1e Před 9 měsíci +1

    Ndiyenso choti aziwe zikhale ng'oma pano sikuseli kwa 2000 kuti anthu abadwa nthawi ya bakili muluzi kuti zithu zonse zinali chonchi kuseli kwa 2000 kunalibe tv kunalibe ma Radios komanso ukangoyelekeza ku chula zina la kamuzu amakuuzakuti ankhwazi akukumvani ku sanjika kukhala ngati malawi yonse anayi microphone everywhere anthu amaletsedwa kupanga mabissines bottom line John tembo tizamukumbukila ngati munthu mmodzi oipa kwambiri kuno ku malawi John tembo kamuzu banda anali anthu oipa kwambiri Ndiye pano mmalo mwa john tembo akufuna akhale mulowammalo wake zikhale ng'oma munthu oipanso kwambiri

  • @user-hm7wh6ol3m
    @user-hm7wh6ol3m Před 9 měsíci

    Alright

  • @BrownKCMarcDormand-rs3es
    @BrownKCMarcDormand-rs3es Před 9 měsíci

    Anali Muthu woyipa kwambili Tembo anazuza azake mu ndale

  • @BenissoneErnesto-kn9bd
    @BenissoneErnesto-kn9bd Před 9 měsíci +4

    Rest in peace Mr Jon tembo

  • @MUSSAHMBILINGANO
    @MUSSAHMBILINGANO Před 9 měsíci +1

    Oweludza ndi mwini chilengedwe not us

  • @JoyManda-qj6wl
    @JoyManda-qj6wl Před 15 dny

    Remember him as wopereka chakudya ku ng'ona kwa wina aliyense amene amadana ndi kamuzu the real devil

  • @ShadrackMsitweni-sr2uo
    @ShadrackMsitweni-sr2uo Před 9 měsíci

    Ulemu upite kwainu big ulibwino big serious

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Před 9 měsíci +1

    MCP kupha ndikoyamwira, they're being led by Demons 😢😢😢

  • @user-iy8vi7nn8r
    @user-iy8vi7nn8r Před 9 měsíci

    Rest to he'll jonh

  • @DevidoJone
    @DevidoJone Před 2 měsíci +1

    Machende ske

  • @user-nx7yz4qo8f
    @user-nx7yz4qo8f Před 9 měsíci +1

    Zoopsatu zithu zake

  • @williamsmanda8592
    @williamsmanda8592 Před 9 měsíci +2

    Ichi ndi chigawenga chomaliza Cha MCP kukaliwa ku gahena. Chakwera adzakhala chimtseka khomo ku gehenako

  • @jamesmfune8448
    @jamesmfune8448 Před 9 měsíci

    John Tembo chinali Chigewega

  • @sihalimwasama7530
    @sihalimwasama7530 Před 9 měsíci

    Gahena is waiting for him

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 Před 9 měsíci +1

    Eeeeee koma john tembo wagwira ntchito yopha anthu iiiii

  • @ramseycrown483
    @ramseycrown483 Před 8 měsíci

    Akalowa kuthako kwa make mbuzi imeneyi. Ndisaname I don't even want to hear the name of joni tembo. Munthu oyiiipa zedi.

  • @johnchavula3282
    @johnchavula3282 Před 9 měsíci +1

    Ndimadabwatu😂 kuti zikuphonyani bwanj

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Před 9 měsíci

    Nthaw zina kukhala wabwino mu ziko lino lapasi zimakuchitila ubwino shaa

  • @user-nz8mq4ff3e
    @user-nz8mq4ff3e Před 9 měsíci +2

    Wini adziti tikufuna timange wa Bakili muluzi TV koma padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta yes zomwe tikufuna ife ndizimezi wina adziti tikufuna timange wa Bakili muluzi tv zosatheka wina asayelekeze kumanga pa Bakili TVmuluzi asafe chifukwa akafa pavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta chifukwa timakonda kwambil chifukwa chilichose chomwe amanena zoonandi ife timafufuza zonse zomwe mukunena ndizoona ndithu ndiye wina aziti tikufuna timange wa Bakili muluzi TV Malawi mono padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta padzavuta

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Před 9 měsíci

    Ndiwe chitsiru wabodza iwe Tembo anabadwira kukhola ntcheu osati Dedza

  • @OwenNyangu-nv1yt
    @OwenNyangu-nv1yt Před 9 měsíci +2

    Munthu wamwalira mulimbananYe bwanji?

  • @user-nr2bi5zm9f
    @user-nr2bi5zm9f Před měsícem

    Tzamukimbukira chifkwa cha kupha ma minister 4 cha mma 80's

  • @AhmaduAdini-js7ok
    @AhmaduAdini-js7ok Před 9 měsíci

    Ulemuwanu big gayena Malo ake a John temporarily