Minyama yathu ngati amalawi ikuchokera pati?

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 16. 08. 2023

Komentáře • 191

  • @farookousmane715
    @farookousmane715 Před 10 měsíci +10

    We are all Africans...when I see a burund person I see myself.

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 Před 11 měsíci +10

    Mkhoza kuona nokha kuti zikhaleyo kuyipa nkhope angakhale ndichisoni. Tomorrow never end will see

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Před 11 měsíci +10

    You're the great man in malawi!!

  • @markoviskyhernandez9706
    @markoviskyhernandez9706 Před 11 měsíci +11

    Thank you very much brother!! You are the best even though you tell people who have no ears nor brains!!
    Pepani ndithu!!

    • @greychizaka4088
      @greychizaka4088 Před 10 měsíci +2

      anthu odzikonda chabe

    • @raytavares2256
      @raytavares2256 Před 10 měsíci +1

      It's sad even in Angola Malawians used to sell its former Africans who were fighting the regime and that's how they killed my father and tortured my mother as a Christian missionary helping children who were forced on armed labour. My mum helped and was hiding those children to a place of safety.

    • @markoviskyhernandez9706
      @markoviskyhernandez9706 Před 10 měsíci +1

      @@raytavares2256 Sorry Dear Sister/Brother😔!! It's very sad to hear 🙆🙆!! But most of the time, the governments of Malawi and many Malawians show a surprising behavior!! Imagine that Malawi was the only black country which was supporting discriminating government in South Africa!! Can you imagine that!!??🤔🙆!!
      Go there in Malawi right now and see what they are doing to black african refugees. It's shameful!! Remember that there are more than 6 millions malawians in South Africa, more than 5 millions malawians in Zimbabwe, more than 1.5 millions in Botswana, .... without forgeting in Europe, America and other different regions of this Earth. But the animosity that they are inflicting to the refugees is surprising!! Nothing to say 🤔😔!!

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 Před 10 měsíci +13

    Malawi Congress Party is a party that was not supposed to rule Malawi again

  • @BenissoneErnesto-kn9bd
    @BenissoneErnesto-kn9bd Před 9 měsíci +2

    Komaditu brother Malawi ndikachani panagaga ngati pamenepa anyamatuso ambir Ali maiko ena kuthawa kupandako kanthu kumalawi zinkhale Ng,OMA watani kd komatu zimenezi siku Lina zizamusata

  • @raspeterkasengwa1390
    @raspeterkasengwa1390 Před 10 měsíci +4

    Though you don't show your identity. You remain iconic

  • @AhmaduWilson-jl2br
    @AhmaduWilson-jl2br Před 11 měsíci +4

    Umakwana ulemuwanu big thanks for telling us true

  • @thomassimbaya197
    @thomassimbaya197 Před 10 měsíci +3

    watching from zambia you are great big man ,thy is a gold scalndal that has just happened here in zambia at K K international airport which is very compliceted i wish u could search about it

  • @Wesleywisk-lf5hw
    @Wesleywisk-lf5hw Před 11 měsíci +2

    Achakwelaso uthengau ukupezeni

  • @user-zb1sp7ur6i
    @user-zb1sp7ur6i Před 11 měsíci +3

    Zikomo brother mumatitsangalasa 🙏🙏🙏🙏

  • @idrissaKGO
    @idrissaKGO Před 11 měsíci +2

    Jerous siimapindula gyx amalawi

  • @user-fn7eh4hd7x
    @user-fn7eh4hd7x Před 11 měsíci +1

    Am here waiting you boss from Johannesburg

  • @NgendahayoSosthene-qn7qn
    @NgendahayoSosthene-qn7qn Před 10 měsíci +2

    mukanena dzina ra charichi cyo ndikanafufuza umboni wa nkhani imeneyo rero romwe.

  • @rickiez
    @rickiez Před 11 měsíci +1

    And I quoted "za mawa sizidziwika" ndili wokudzika kwambiri. Thanks for the information may God bless you

  • @chrisboyce229
    @chrisboyce229 Před 10 měsíci +2

    Zoonadi brother Jealous simasunga mudzi tikuyenera kusintha A Malawi chifukwa Cha mawa sichidziwika

  • @johnman4619
    @johnman4619 Před 10 měsíci +1

    Ndizomvetsa chisoni mbiri yadziko lathu mutati muoni the holl Africa ndife thokha amalawi tilindi mbiri yoyipa mu independence koma zonzezi ndi Cecelia and John tembo

  • @frankfriday3141
    @frankfriday3141 Před 11 měsíci +1

    From Johannesburg near alberton ulemu wanu Big nde chifukwe chake aku Mozambique samatipasa magesi khamusu anatenga gawo ifa ya Zamora

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 Před 10 měsíci +1

    Ndizoona, tilikonkuno ndipo akutisunga ndiomwewa

  • @BlessingsBanda-qn7xr
    @BlessingsBanda-qn7xr Před 10 měsíci +2

    Mngopusa zikhale mbale zake mapoto ake komaso paniyo pake 😂😂😂😂😂😂

  • @anafieintuka8090
    @anafieintuka8090 Před 10 měsíci +1

    Good history sir
    Inu mumatiuza zoona zokazoka, thanks sir

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 11 měsíci +1

    Amalawi ambiri ndi ma illegal immigrants ku America, koma ali ndi ma business, amaloledwa kutenga loan ku bank even kugula nyumba kapena galimoto pa ngongole,, ndipo akuchita bwino kuposa ma americans. Boma la America limatolera misonkho kwa onse koma mabulutu amene akuyendetsa dziko la malawi sakuona patali.

  • @OmarAskimu-cn4ti
    @OmarAskimu-cn4ti Před 10 měsíci +1

    Even makolo athu anatiuza zakuipa kwa MCP

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 10 měsíci

    Thank you for revealing the TRUTH. You must write a book about this history. It's true Malawi never ever bothered to help South Africans and yet today they still go to South Africa to work. Even now they follow the same patterns. Look at how they prefer keeping criminals and yet on Sadec. Do you recall how Kwacha Ng"ambi committed crimes more than Bushiri in South Africa? And South Africa will always be loyal to Malawi. Look at the Wenela period?

  • @user-bt3qi1gt8b
    @user-bt3qi1gt8b Před 10 měsíci +2

    Pilizani bro kutsegula maso a Malawi

  • @anifoiuene6301
    @anifoiuene6301 Před 10 měsíci

    Andrew chimwendo sanayendepo kupita ku dziko laeni asiye kuyankhula za utsilu.Anifo from Moçambique

  • @markoviskyhernandez9706
    @markoviskyhernandez9706 Před 11 měsíci +2

    Munthu wakuda kugwilizana ndi anthu omwe amapanga za Apartheid !??🤔🤔!! Za wutsilu ziminezo ndithu !! And they had no shame!!???🤔🤔
    There is nothing worst than to be on the wrong side 🤮🤮🤧🤧!!

  • @abudardachilangwe6791
    @abudardachilangwe6791 Před 10 měsíci

    It's true...ndinakumana ndi muthu mu Bank kuno ku South Africa ndipo anati Dr banda munthu akathawa ku South Africa mkubwela ku malawi kamuzu amamugwila ndikumtumiza ku South Africa ndipo akafika ku South Africa amaphedwa ndikumangidwa.....I was ashamed kumva zimenezi

  • @aubreykanyenda8008
    @aubreykanyenda8008 Před 10 měsíci +2

    Please TEACH US and don't stop teaching this Government too

  • @christophermomba7127
    @christophermomba7127 Před 11 měsíci +1

    Thanks for information keep it up Bakili

  • @ThokiseWiriyam-ws1ec
    @ThokiseWiriyam-ws1ec Před 11 měsíci +2

    Chakwera ndimbuzi

  • @Gibbs-yp6um
    @Gibbs-yp6um Před 10 měsíci +1

    Mumakwana munthu wa'kulu kip on giving us nothing but the best history.

  • @charlesRajabu-cc4bx
    @charlesRajabu-cc4bx Před 10 měsíci +2

    Always you mumanena chulungamo mumayipasa fire

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 Před 10 měsíci +1

    Reference ya andrew chimwendo yandikhudza dont burn bridges you crossed.

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 8 měsíci +1

    This is very powerful massage ❤❤

  • @johnsong7236
    @johnsong7236 Před 10 měsíci +2

    i always smile and learn something at the same time

  • @bjmtalimanja5073
    @bjmtalimanja5073 Před 11 měsíci +1

    Andrew chimwendo kumwamba siwukalowa ndithu

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 Před 11 měsíci +1

    Thanks very much continue doing that

  • @hopembendela
    @hopembendela Před 10 měsíci

    Nkhuyu dzodwa mwana zipota mkulu thanks bro

  • @titomethiwa4213
    @titomethiwa4213 Před 10 měsíci +1

    Zikhale ndichisilu ndimuthu oipa kwambiri

  • @JohnChibalo-wf8gr
    @JohnChibalo-wf8gr Před 10 měsíci

    Boma la m c p langodzaza ndi mbuli zosazindikira chilichonse kuyambira business mpaka zolima Lima. Chomwe akuchidziwa ndi kuba ndiye poona kuti upresidernt uli mbali yawo ndiye angopedzerapo mwayi okuwabera ndi kuzunza mabulundi. Iweyo zikhale ng'oma ukati Sisi lomosoka m'mbali nkhati kumaliseche kwakoko.😅😅😅😅😅

  • @gladysbonongwe1038
    @gladysbonongwe1038 Před 10 měsíci +1

    Auzeni asiye majelous

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před dnem

    We still learned a lot from you ❤❤

  • @parker2104
    @parker2104 Před 11 měsíci +1

    You know man I hate being a friend with this refugees, samanvetsetsa tikafuna tipakambilane zithu, ndamakani especially Ma Rwanda iiiiiii

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 Před 10 měsíci

    Tamugwileni mum'menye nachimutuyo, ana omwe anabadwila ku Malawi ko, ndi Malawian, chotelo akuzunzisa anawo

  • @sammyree8843
    @sammyree8843 Před 10 měsíci +1

    I have been following for while brother very educative as we grew up in a country that real history was hidden to us.
    Please can I donate to you?

    • @henrysoko3283
      @henrysoko3283 Před 10 měsíci

      I wish to donate too, this man has brain washed me

  • @user-uw8gu4tc1y
    @user-uw8gu4tc1y Před 10 měsíci +1

    From Pretoria, love ur stories

  • @RaheemNgoma-pk1ev
    @RaheemNgoma-pk1ev Před 11 měsíci +1

    Apa ndizothekano kumagona thx bradah man

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 Před 10 měsíci

    That the fact ndithu thank you so much bg mn

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Před 2 měsíci

    This shows exactly that we are acursed nation

  • @user-bp2ty8ll3k
    @user-bp2ty8ll3k Před 11 měsíci +2

    Chanel yomwe ndimaikonda palibeso kuposer iyi ulemuwanu big

  • @jameschipula4475
    @jameschipula4475 Před 10 měsíci +1

    Mumatha ndinu madala-madala

  • @jonathankwangulero4450
    @jonathankwangulero4450 Před 10 měsíci

    Chakwera and his MCP has failed Malawians... But, politicizing the issue of Refugees is wrong. Ma refugee kulikonse amayenera kukhala in designated places. It's no rocket science.... Mpaka Refugee azipanga business aaah sizowonaa

  • @maxwellchibwe5956
    @maxwellchibwe5956 Před 5 měsíci

    Ngakhale ena atsutse or ayi koma nkhaniyi ndiyoona kamuzu doesn't been regarded as pan africanist or one of greatest African leaders we had in Africa. Muone mu history ya Africa ikuonetsani zimenezi

  • @EphraimNaveya-fc4iu
    @EphraimNaveya-fc4iu Před 10 měsíci

    Nice 👍 talking sir,mcp it's one party that makes Malawi to be poor/minyama country

  • @wysonnamaona6497
    @wysonnamaona6497 Před 10 měsíci

    With you all times... Thank you for opening up our eyes.

  • @fedson2050
    @fedson2050 Před 10 měsíci +1

    Chakwera suzamva Munthu opanda Nzeru iwe ndi Mnzako Zikhale N'goma

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Před 10 měsíci

    Shaaaaa kom malawi nsanje ndi ulesi wake ufiti bas kom mukuti ndi mbusaso 😏😏😏

  • @johndaka6368
    @johndaka6368 Před 10 měsíci +1

    We are proud with u in Africa

  • @daudimatolano1715
    @daudimatolano1715 Před 10 měsíci

    Teach us, we are ready to support your work

  • @user-mu4nl9ng6v
    @user-mu4nl9ng6v Před 10 měsíci +1

    Rinse alayasi yatikwana

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Před 10 měsíci +1

    BIG 👍

  • @user-ji3in4cp3m
    @user-ji3in4cp3m Před 4 měsíci

    Ur de best tv

  • @user-xj9sr2vx4q
    @user-xj9sr2vx4q Před 10 měsíci

    Best historian your nomber one

  • @AfiyakazembeKazembe
    @AfiyakazembeKazembe Před 11 měsíci +1

    Zoona big ine Kuno Western Cape Harare

  • @user-ke3jj1yp4z
    @user-ke3jj1yp4z Před 10 měsíci

    zikhale ng'oma mulungu amulanga pompano ndi juma yemweyo mulungu akuwuona akuzunza anthu

  • @josephchitsulo5882
    @josephchitsulo5882 Před 10 měsíci

    Tamuuzeni kumeneko chitsiluyo, ifenso tilikuno kudziko la eni

  • @ModaAckson-sd2yq
    @ModaAckson-sd2yq Před 11 měsíci +1

    Koma 🇲🇼 anatengadi minyama

  • @jameskachulu8141
    @jameskachulu8141 Před 10 měsíci

    Ife kuno ndiye tilipo samativutisaso achewa ngovuta ndaonela pa chakwela

  • @raytavares2256
    @raytavares2256 Před 10 měsíci

    The question is this if there's no foreign currency in Malawi where is the president getting this foreign currency to get to Angola?

  • @christophermkhize1991
    @christophermkhize1991 Před 10 měsíci

    Koma big inuyo mumakwana "nyelele mukuziponda lero mawa zidzadya ntembo wanu" ndimawutu akulu kwambili ngati amvela zimenezi ayenela kusintha zamawa sizidziwika

  • @user-qf9ii2wn4b
    @user-qf9ii2wn4b Před 10 měsíci

    Andrew chimwendoyo pa mtumbo pake, galu ya chabe chabe

  • @ALuz980
    @ALuz980 Před 10 měsíci +1

    Ndizoona Khalidwe la nyau siligatithandize

  • @user-hz5lp6br1e
    @user-hz5lp6br1e Před 10 měsíci +1

    Than you for explaining all history

  • @mondaywoods2975
    @mondaywoods2975 Před 10 měsíci +1

    zoona zokha zokha

  • @giftdulamkalenga7344
    @giftdulamkalenga7344 Před 11 měsíci +1

    Chakwera ndi opanda mutuu

  • @user-nx7yz4qo8f
    @user-nx7yz4qo8f Před 10 měsíci +1

    Kumakhaladi ndi umunthu,ndizoyilanad zithuzi

  • @matembanevermind-po3me
    @matembanevermind-po3me Před 6 měsíci

    Tchutchutchu mofatsiliranso ndpo,mumakwana bigy

  • @davenchimadzi6529
    @davenchimadzi6529 Před 11 měsíci +1

    Power bro.

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Před 10 měsíci

    Chakwera, zikhale ng'oma MCP yonse panyini pa mawo,ifeyo panopa tiri kunja poyamba timalandira ulemu koma panopa tiku funa kumama ngiridwa ma camp amalawi akuvutika akuthawira maiko akunja komanso inuyo mukakhala kumeneko ku malawiko muna voteranji MCP kamuzu anawa siyira mizimu ya Ziwanda panyero pa amawo

  • @markoviskyhernandez9706
    @markoviskyhernandez9706 Před 11 měsíci +2

    Anthu akuda amene amadana ndi akuda ena anzao, ndi zitsilu kwabas!!
    Nkhani ya Chimwendo ameneyo ndi onvesa chisoni 🤔🤔!!

  • @MichaelWilliamsNyirenda

    Malawi amangoziwa kutamba usku

  • @julietmwanza
    @julietmwanza Před 10 měsíci

    Malawi back to mcp great mistake full of brood of Gadama matenje and so on

  • @user-hz1ei8jq6m
    @user-hz1ei8jq6m Před 10 měsíci

    Ngati a MALAWI sitinathandize pomenyera ufulu chifukwa tilibe zothandiziraa

  • @user-xc1xt2qd7t
    @user-xc1xt2qd7t Před 10 měsíci

    Ndwe dolo ase keep up

  • @user-mz4tk1pw3f
    @user-mz4tk1pw3f Před 10 měsíci

    Koma chakwera ndi zikhare ng'oma aziganiza kuti kunja kuno kuli ife azasitenge ngati ndiwamuyaya sanje silabwino

  • @lesterkenkandoje5375
    @lesterkenkandoje5375 Před 13 dny

    It's never too late 😞

  • @YAKOBEJUMAH
    @YAKOBEJUMAH Před 11 měsíci +2

  • @wysonnamaona6497
    @wysonnamaona6497 Před 10 měsíci

    Zikhale ng'oma amadziwa iye ndi kuvala Zima trauza zikuluzikulu basi

  • @pastorbinuelf.lamusse6203
    @pastorbinuelf.lamusse6203 Před 10 měsíci

    Timakunyandirani big kuchokera Kuno ku Moçambique Maputo.

  • @manphiri2778
    @manphiri2778 Před 10 měsíci

    Koma nchewa mwamunyoza kkkkkkkkk amangodziwa kudambwe eti

  • @SharifahWillardChampionn-rn8cm

    Machende kamudzu sanali Malawi galu wachabe chabe anangowononga zinthu

  • @user-zk5nu5fh6l
    @user-zk5nu5fh6l Před 10 měsíci

    Zowona ndikumudziwa chimwendo simukunama

  • @PromiseBarton-em1ll
    @PromiseBarton-em1ll Před 10 měsíci +1

    Chakwera zikhale ng'oma anthu awa ndimbuzi za anthu😭😭😭

  • @alickchiumia2616
    @alickchiumia2616 Před 10 měsíci

    KUKANGOCHA KUMANGOGANIZA ZOTI MUNENA CHIYANI CHOKHUZANA NDI MCP .

  • @francokaunga2707
    @francokaunga2707 Před 10 měsíci

    Wachewa xenophobic too much since the time of kamuzu Banda. They always think that Malawi is for them.

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 Před 10 měsíci

    you deserve to be an advicer to this so called

  • @TonyBanda-ch6vo
    @TonyBanda-ch6vo Před 10 měsíci

    Koma inuyo bigy munabwera respect to you .

  • @alickchiumia2616
    @alickchiumia2616 Před 10 měsíci

    KODI BASI NKHANI IZINGOKHALA MCP MCP . MUNALUZA INUYO A DPP . TIMAKUZIWANI KUTI NDINU MA CADATE A DPP PANO ZIKUKUWAWANI

  • @ChisomoNthukwa
    @ChisomoNthukwa Před 15 dny

    Ndipo MCP sizachokaso m'boma