Some few people are saying kuti maburundi azipita kwawo chifukwa ku Rwanda ndi ku Burundi kulibe nkhondo. Mukudziwa kuti ku South Afrika kuli amalawi 6 miliyoni? Ndee kuno ku Malawi kuli nkhondo? Ku Zimbabwe, malawians are 5 millions. Kuno kuli nkhondo? Ku Botswana, kuli 1.5 millions of malawians who are working mostly in construction sector. Is there war in Malawi? Europe ndi USA, Canada, ....muli amalawi ambili, sakubwelera chifukwa cha nkhondo ili kuno!??? Mukudana ndi anthu omwe ali mu midzi ndi ma towns who are less than 10 thausands whereas Malawi has 6 millions citizens in South Africa?? Xenophobia is not good and kumbukilani kuti onse awa ndi ma black ngati ife. We are brothers. And you don't flee your country because of war only. Human Right violations and poverty make also people to flee their countries. Do you think munthu amathawa kwawo pa kufuna kwake without reasons? Jealousy!!
Money killed Jesus,,,,aah malawi,,,,thanks brother ,,continue bible Suzanne was saved ,,lies lies Killes, and then ,,,! ,!?may God protect you wise speaker.. continue the wisdom to open malawi ,,,,if Only he could resign!, is respectful than to destroy poor innocent creatures and create disorders of no peace ,,Lord keep malawi land of peace, malawi pray pray,,God loves you,,
Thank you very much you the owner of this channel. You are widely opening my eyes. I was ignorant about the issues of Rwanda, Burundi and great lakes region in general. I had information that the current president of Rwanda is a good president, but on another hand, I had information that he is a monster, savage. Simply, the ones who make the publicities and whitewashing his image are westerners who put him on power and he is working for them by stealing in the Democratic Republic of Congo. But for an awake african, this is a bad leader, a traitor of Africa. The western media presents him as savior of Africa, but you know that if an African leader is loved by the ones who always steal from Africa, it means that this leader is working for them!! He is selling Africa to them. He is a traitor for africans!!
Eish Mulungu atithandize Chakwera Ndi unduna wake wonse Mulungu awakanthe sure Ndipo zikhale ng'oma usamale ndalama imeneyo ndi makape anzakowo ndithu God will punish you Paul Kagame ndi mfiti wachabe chabe
Koma pls Malawi wanga ndalama izi tikunzisa nawo anthu osalakwa mmhh Ambuye atichotsere mtima wamwala omwe wangobwera from no where mwa ife bro Ambuye Ali mbali akhala mboni yako osadanda ay pitiliza kulilira kwa Mulungu wako amamva ndpo akumenyera nkhondo Amen
Indeed you are a great man may God bless your days I hope you search the story of Adamson mushala in Zambia and The story of the mailing brothers in Zambia watching from Zambia muchinga province
I told you my fellow malawans ,. that USA and British Army can destroy entire world world if they want, so who's kagame? panyopake asabwere KU Malawi na KU Zambia cause we have beautiful girl s in Zambia and Malawi they can't manage to run, MR H h and Chakwera Mwaona? Careful plz,Stick to USA and British
A Malawi tisayawile nkulu uyu pamene anali chief of stuff wa malemu Bingu wa mutharika kuti nduna zimavutika kuti zikomane ndi President masiku apitawo. Hello Mr. Chakwera beware the Ades of march!
Paul Kagame anabwera kuno ku Malawi nthawi Bingu Wa Muthalika mpaka nseu wa Chilambula anautchula dzina lake,sanayambe lero kugwirizana ndi boma la Malawi,ngati Zikhale walandila ndalama kamusumire
Some few people are saying kuti maburundi azipita kwawo chifukwa ku Rwanda ndi ku Burundi kulibe nkhondo. Mukudziwa kuti ku South Afrika kuli amalawi 6 miliyoni? Ndee kuno ku Malawi kuli nkhondo? Ku Zimbabwe, malawians are 5 millions. Kuno kuli nkhondo? Ku Botswana, kuli 1.5 millions of malawians who are working mostly in construction sector. Is there war in Malawi? Europe ndi USA, Canada, ....muli amalawi ambili, sakubwelera chifukwa cha nkhondo ili kuno!??? Mukudana ndi anthu omwe ali mu midzi ndi ma towns who are less than 10 thausands whereas Malawi has 6 millions citizens in South Africa?? Xenophobia is not good and kumbukilani kuti onse awa ndi ma black ngati ife. We are brothers. And you don't flee your country because of war only. Human Right violations and poverty make also people to flee their countries. Do you think munthu amathawa kwawo pa kufuna kwake without reasons? Jealousy!!
King you can be a good adviser even to a president. I respect you humble beast. Imagine your underground but doing a great job
Thanks very much bg mn respect ndawi zonse matisegura matso ndi ubongo nditu ndikutipatsa mphavu dziko lathu lamalawi srs
Kagame was rebell in Uganda. My fellow Zambians am a historian ,
Munya manyi mulungu akukantheni pa zomwe mukuchita nonse even chakwelayo mulungu akutumizileni matenda ma banja mwanu mu dzina la yesu
😢😢malawi ndalama anaimva kukoma heavy
Komatu a'malawi ngati ndidyela tiphetsa anthu osalakwa please 😭😭
Good job brother continue we really appreciate your information 👍 👏
Big man!! Mumayitha ndinu number one mumakwana!!
Thanks bosses for the extensive variety of information daily themed
Provide other needed data
Thanks your Excellency Dr Bakili muluzi
Money killed Jesus,,,,aah malawi,,,,thanks brother ,,continue bible Suzanne was saved ,,lies lies Killes, and then ,,,! ,!?may God protect you wise speaker.. continue the wisdom to open malawi ,,,,if Only he could resign!, is respectful than to destroy poor innocent creatures and create disorders of no peace ,,Lord keep malawi land of peace, malawi pray pray,,God loves you,,
M'busa wanji wotengeka ndi zinthu za kumidima zokha zokha mkumanamiza anthu kut anali m'busa ...mbuzi za anthu
Only 4 years MALAWI yavunda kale nde kuli-bwanji akaWinaso CHAKWERA yiiih?
Ati yavunda 😂😂😂😂
our government is full of rubbish,,,,bigman you are doing very good job bakili muluzi tv salute
Thank you very much you the owner of this channel. You are widely opening my eyes. I was ignorant about the issues of Rwanda, Burundi and great lakes region in general.
I had information that the current president of Rwanda is a good president, but on another hand, I had information that he is a monster, savage.
Simply, the ones who make the publicities and whitewashing his image are westerners who put him on power and he is working for them by stealing in the Democratic Republic of Congo. But for an awake african, this is a bad leader, a traitor of Africa. The western media presents him as savior of Africa, but you know that if an African leader is loved by the ones who always steal from Africa, it means that this leader is working for them!! He is selling Africa to them. He is a traitor for africans!!
You're the best bro,,,keep it up
Mmmmmm....koma akuenela Ndalamayo ibwezedwe...komanso aNdunawo akuenela apite ku Rwanda akamutuluse Munthu osalakwa please!!!please!!!Very sad 😭😭😭😭😭
Thanks for updating us
Watching from Mozambique kuvesera mwachidwi
Asogoleli alelo ndi mbuzi zaanthu kukonda ndalama munya muona
He is a puppet of NATO and Son of devil I like that one...keep the fire burning Boss much respect and salute
A bakiri chonde mudzawauzekonso anthu za ma prison a ku rwanda.sadziwa kalikonse anthuwa.
Where we're going malawi??
Amalawi tiri kumalawi amoto 😢😢😢😢😢
We need that man to come back to Malawi because have no problem to Rwanda that is business Man to Malawi gagame you can send back that man
I like your page very much broh....
Do a favor by explaining the story of museveni and America on anti gay law😌
Thanx for updates
Koma iweyo ase ur the best
Keep it up big man
Vuto lovotela nyawu
MALAWI LOVE OF MORNEY.CORRAPTION
i like you my brother man. am liseng you from Zambia
Eish Mulungu atithandize
Chakwera Ndi unduna wake wonse Mulungu awakanthe sure
Ndipo zikhale ng'oma usamale ndalama imeneyo ndi makape anzakowo ndithu God will punish you
Paul Kagame ndi mfiti wachabe chabe
A malawi nose amene munavotera chakwera pankholo panu, ngati kuponda bwelani tipondane pompano pantumbopo agalu chifukwa zosezi ndinuyo amene munavotera chakwera
Koma pls Malawi wanga ndalama izi tikunzisa nawo anthu osalakwa mmhh Ambuye atichotsere mtima wamwala omwe wangobwera from no where mwa ife bro Ambuye Ali mbali akhala mboni yako osadanda ay pitiliza kulilira kwa Mulungu wako amamva ndpo akumenyera nkhondo Amen
Thanks boss inu mumanenena chilungamo osaopa munthu
Dziko lathu lalowa chibwana kwambiri, how dare iwowo kumalola kulamulidwa ndi Paul kagame 😢
Zonadi
Best channel ever
❤❤❤ you my man mumatipasa ma update ya boh
Chonde MULUNGU mulangeni zikhala Ng OMA NDA chakwera taonani munthu uja mumati ndi busayu wayamba kuphetsa anthu kodi munthu wamulungu angapange zoipa chonchi
Keep up bro
Anthu akuyenela kuchitapo kanthu, ndipo nduna imeneyi ikuyenela kutula pansi udindo
Ambuye alowelelepo ndalama ziwapweteka anthu awa walakwa chiyani
Ambuye awakhululukire achakwera akufuna kuononga miyoyo ya anthu chifukwa cha ndalama
Tell us more about the health life of yoweli kaguta museveni
Indeed you are a great man may God bless your days I hope you search the story of Adamson mushala in Zambia and The story of the mailing brothers in Zambia watching from Zambia muchinga province
You don't know kagame, kagame is a silent killer it's only Mr Joe Biden and British Army can deal with him,
I told you my fellow malawans ,. that USA and British Army can destroy entire world world if they want, so who's kagame? panyopake asabwere KU Malawi na KU Zambia cause we have beautiful girl s in Zambia and Malawi they can't manage to run, MR H h and Chakwera Mwaona? Careful plz,Stick to USA and British
Nimavera che ma comment anowo ATI uli boo brother Komatsu anthu Akufa but muli nuu pa radio malawi chonde chonde chitaniponi kanthu from zambia 🇿🇲
BIG 👍
Chakwera Why 😭😭😭😭😭😭
Ndakupendasana
May almighty God protecte the man who never deposite gvment
Tinakuzan MCP iribe umunthu lero ndi izi...
Yonse big man umatha
I follow you bro very well
Komatu kamudzu Banda anasiyina kuti munthu yemwe walowa kumalawi sayenera kungwidwa ndikutumizidwa kwawo Malawi ndichani
Timakunyadirani Big man
Koma m tima wanga wandigunda movetsa chisoni kwambili. Huuuuuuuu kulakwatu KUMENEKO.
Komanso Mr chakwela akumaganiza bwanji kwenikweni?
My broda😂😂😂😂boma ili ndilibe nalo mawu
Awasumile basi no two ways about it 😢😢akonda ndalama ngati hule
Malawi ndi Dziko lomvetsa cisoni ndithu😢
My big bro
May almighty God continue protecting u brother
Chagwera ngt uli mdiumunthu siyani zimenezo kagame simunthu wapa enthu ambiri ndiponso amene amagwira chito yake,chake ndikupa nikuononga iweyo ndani thi ndalama timene agupatsani uziwona anzanu sanali wopusa ngt ukuo a ndunama kafuseni peter wa muthalika
mmbusa kumapanga izi zoona ayi mulungu amukanthe
Eysh mchifukwa anamodwee akubwela ku Malawi chifukwa atsogokeleli akee ndi a dyela😂
Wonderful narration
Kodi amatipasa uthengau ndi ndani?amakwanira ndipo ndinaseguka mutu just because of this brother"
Boma likupanga zithu m'chimbulimbuli.
Is corrupt God bless you my brother
Osamvotelas agalu amenewe
Kom Malawi 🇲🇼 mmmm kulibe chabwino
Anduna atichitasa manyazi ndi dyela😂😂
Akatero akamupha Bambo ameneyo eee koma dziko lapasi laora
Osayiwala malawi imasunga zigawenga
Andunawa Mmene wakulira mutuwo koma opanda nzeru
Bolani agwe prezdent ameneyu mu 25 mu sitikufuna chabwerayu
Komano MCP mchani azawo a mu Tonse alliance kuwakhomelera dollar akudya okha plus za fertilizer
Chagwera ambuye akuyendere mwapadera wadxuza mizimu ya anthu ndipo ndalama zimene warandira kwa poul kagame sumuziwa zimene amapanga wapa anthu watsala ndiweyo
One Africa
👍
Malawi dziko losava olopangitsa manyazi
Malawi government must support this man ...mumatha kwambiri man ndipo mumamveka chilungamo kwambiri
A Malawi tisayawile nkulu uyu pamene anali chief of stuff wa malemu Bingu wa mutharika kuti nduna zimavutika kuti zikomane ndi President masiku apitawo.
Hello Mr. Chakwera beware the Ades of march!
Problem is that chakwera ndi Muthu agona kwambili.
Please guy's Malawi stop this nonsense money is nothing than life and freedom
Boma la a chakwera ndiye bola ma boma inatu
Commander woyamba wapita asala foty chakuti
Zomwe mwarankura zonse ndi Zona zokazoka
Eshiiiiiiiii
Facts
Zosakara bwino
Malawi eish
Nthawi zonse ndinu olandilidwa kucheza nanu
❤❤❤❤
Iweyo palbenso ku malawi kuno iwe nd mfumu ya history ku Africa 🌍even ku Europe 🇪🇺
Muthu woipa kwambiri
This is insern government
Koma ngati ali wa ku Ruwanda achita bwino kuntumiza kwawo
Paul Kagame anabwera kuno ku Malawi nthawi Bingu Wa Muthalika mpaka nseu wa Chilambula anautchula dzina lake,sanayambe lero kugwirizana ndi boma la Malawi,ngati Zikhale walandila ndalama kamusumire
Ine ndipanga fasting kuti anthu amenewa angokhala masiku ochepa MULUNGU awachotsere masiku okhalira padzikopano
ndimbudzi sawanthu mulungu asilange