nde nose nfinu akatangsle or ndalama za misonkho ya amalawi m malo mogula mankhwala chakudya feterizer otchipa koma zaka 4 palibe chomwe mwapanga president ndi nduna zake zonse mbava zokha zokha , minister of finance kupezeka ndimatumba andalama ku airport kumusiya or kulengeza pawailes ayi achoke omenewa
Muchoseni chakwera sakuyenelaso kusogolela ziko lino musakhe ena basi km chikangawa muchoseni akuonengelani mcp ofcz chikangawa ndi mbamva kmaso ndi okupha ndie muonengesa chipani chanucho cha mcp azikusogolela ubusa uja basi ziko walilephela iyeyo 😂😂😂😂
@@ChikupizgaKajawaMkandawire Tandiuza ndani alubino adafaela ku chikangawa, apa aise ndipa social media ndiye zoti uzindifunsa mafunso opoila wamva, panga zako
Sitilukamba za DPP koma tilunena za inu Muli pampandonu . Mukutitsogoleranu. Mwatisaukitsa a Malawi fe. Zaka four kulamilira koma ataaa mavuto okha okha😂😂😂😂 Mayo Malawi uja kumvetsa chisoni. Zinthu kumangokwera chisawawa A Pule Ali chetee.... Olo kulowererapo kuti munthu wakumudzi mwina nkuthandizika ayi tere kungoti duu Busy kumangopakula nkumawomola basi nde ndi ma cabinet onsetu kungoti cheete kumangomva kunong'a. Apa zasendera nde mwayambapo kuyimba nyimbo Malawi athandizikee mmm too late. Nkhanga zaona....
Koma anthu wa apwetekanatu uku😂😂
Anyani awa kapena Kuti bwaa
Ndipo apwetekane ndipo aphane okha okha athu oipa awa asatana
Mk14 billion ku mwaza mwazitenga kuti kuba basi ndi chifukwa chake anthu mmalawi muno sakukufunani mukhulupirira 2025
😂😂tikufuna aphane kumene anthu woyipa kwambili
Lazalo mumuchotsepo sakuyendetsa bwino dziko sankhani wina uyuyu akuonongera
Umva kupweeka ku opposition
"Dzina langa lasowa mayoooo" San B
Amati UTM yagawanika APA MCP ndeyatani yankhani
Akuyankhuala mwamzerutu,,
Mbuzi izi zizigundana kumene
Kupusa eti mukukanga chifkwa chaife ndife ana anu
nde nose nfinu akatangsle or ndalama za misonkho ya amalawi m malo mogula mankhwala chakudya feterizer otchipa koma zaka 4 palibe chomwe mwapanga president ndi nduna zake zonse mbava zokha zokha , minister of finance kupezeka ndimatumba andalama ku airport kumusiya or kulengeza pawailes ayi achoke omenewa
Inu pa nthawi yanu ndarama za amalawi munamanga page house
Chikangawa inazorowera kumpha mapwara anu agaru
Chikangawa party km wangondisangallatsa mkuluyu kuyankhula modekha mwanzeru kuposa chakwera.
Muchoseni chakwera sakuyenelaso kusogolela ziko lino musakhe ena basi km chikangawa muchoseni akuonengelani mcp ofcz chikangawa ndi mbamva kmaso ndi okupha ndie muonengesa chipani chanucho cha mcp azikusogolela ubusa uja basi ziko walilephela iyeyo 😂😂😂😂
Kuyankhul mwachilungamo zokhudza migwirizano eeeeee sizinaende bwinodi mayo ine ABIYENI aja
Bola pamenepo 😊
Koma ndiye simunati mukuona ngati magazi achina chilima ndi ena 8 aja, musowa mtendere muona 😢
Sizikugwilizana ndipo ndiwe waboza asee
Inu ma albino munadya aja mumasowa ntendele?
@@ChikupizgaKajawaMkandawire Tandiuza ndani alubino adafaela ku chikangawa, apa aise ndipa social media ndiye zoti uzindifunsa mafunso opoila wamva, panga zako
@@ChikupizgaKajawaMkandawire🤭🤭🤭🤭🤭
@@ChikupizgaKajawaMkandawire ngati kwanu mumadya anthu ndikwanuko, ine sindidya anthu wamva kunakukanika kungodusa comment yangai ndiwe upusa zedi
Bon kalindo
Agala chauya inu a mcp tinatop nanu ife mutuluk mu boma palibe tikuchiona chazelu ife iyaah shem on you 😒😒😒😒
Agalu anthu inu
Agaluinu mfiti anthu oipa demokarase mmaidziwa kumupha chilima ulendouno unali wachilima apamwasankha chakwera ndichipangano chimenecho mfiti inu amcp pitilizani
Ku dpp kuli democracy ?
Sitilukamba za DPP koma tilunena za inu Muli pampandonu .
Mukutitsogoleranu.
Mwatisaukitsa a Malawi fe.
Zaka four kulamilira koma ataaa mavuto okha okha😂😂😂😂 Mayo Malawi uja kumvetsa chisoni.
Zinthu kumangokwera chisawawa A Pule Ali chetee....
Olo kulowererapo kuti munthu wakumudzi mwina nkuthandizika ayi tere kungoti duu
Busy kumangopakula nkumawomola basi nde ndi ma cabinet onsetu kungoti cheete kumangomva kunong'a.
Apa zasendera nde mwayambapo kuyimba nyimbo Malawi athandizikee mmm too late.
Nkhanga zaona....
Ndizimenezotu
Ife tinanena kale kuti mcp ndi ufiti
Banja la a Tambala munawotcha aja ufiti upose panep?
Buleya Lure MacDonald Masambuka uja bwaaa
@@ChikupizgaKajawaMkandawire Chilima; Raph Kasambala; Lucius Banda; Sidik Mia; Shanil Dzimbiri
Dzitsiru idzi dzabetsa boma anthu opusa kwambri kupha Chilima kuja anapanga mistek yaikulu kwambri nyini zamanu
😂😂😂😂 mwakwiilatu sir
@@LongiMtimabii dzitsiru amwene idzi and kupha chilima ndi mistek yaikulu heavy, ndipo ku Malawi sikuzakhalaso chipani chotchedwa Mcp ikutha basi
Kkkkkkkk chilima anaphedwa munjila yanji a mcp ankayendesa ndege ija
@@Musa1828-l5dMCP siingathe aise, ndipo dziwa kut onsewa ndianthu oti anachokera ku MCP komweko
@@ChikupizgaKajawaMkandawiremzadya kholowa chaka chamawa Inu. Bwanji mitima yanu ndiyokwera? ngt sindinu akupha bwanji zimakuwawani. Iiiiii kma ana achikangawa , mwatumidwa ndi bambo Anu chikangawa? Kut mziziyanganira ma comment ya anthu?
Agaru inu mumpha mufe ndithu