JOYCE BANDA WAING’ALURA POYELA LERO KU ZOMBA PA NSOKHANO KUTI IWO NGATI PP ARE NO LONGER IN ALLIANCE

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 09. 2024

Komentáře • 141

  • @BawulenLuka
    @BawulenLuka Před 29 dny +12

    Joyce Banda, saulos chilima, timothy mtambo ndi ma judge komanso ampingo mulungu akakukanthani agalu inu

    • @user-jn9tz3li3v
      @user-jn9tz3li3v Před 29 dny +2

      I like your comment kkkk agalu amenewa ariwika mmavuto kwambiri.

    • @vitujames53
      @vitujames53 Před 29 dny +2

      Anthu ndinuyo..kusowa umunthu ukutu

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Před 29 dny +1

      Iyi ndi comment yabwino yopotsa ma comment onse lero muone zinthu mmene zakwelera + njala ndi Kuba ndalama

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Před 29 dny +2

      ​@@vitujames53zomwe ankapanga zija zopusitsa anthu zija ndie zinali umunthu? Aaaaaa

    • @MaggieCement
      @MaggieCement Před 29 dny +1

      Pomsooooooo ndiye poti Amalawi ngopusa kumagosatila komwe mbuzi zulowera poti kuli nsipu ubwino wake ayamba kuphana okhaokha mene amanenera chakwera kuti akhesa mwazi pozakhesa wa mphawife atathana kale okhaokha

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo Před 29 dny +5

    Bring back the jet first....otherwise forget.

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x Před 29 dny +7

    Kupeperesa anthu munawapeperesaku mupepesenso coz dziko lero tikulira coz chainu. Lero njala ilipaliponse, Chilima anaphedwa, zinthu zinakwera kwacha ingogwesedwa mmene banja lawo lafunira, misonkho yathu ikubedwa koopsa + nepotism. Malawi waonongeka coz chainuyo, Timothy Mtambo ndi chilima. Mukuyenera mupepese kuntundu wa anthu.

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 Před 29 dny +7

    KUTI MVETSELE BWINO ZOMWE ALANKHULA KU MSONKHANO A PP ANENA KUTI ATULUKA KOMA KWA IFE OZIWA NDALE SANATULUKE AYI AKUFUNA AWONE MPHAMVU ZA CHIPANI CHAWO AFTER ABWERERASO KU MCP .

    • @user-uc1pd1tc2x
      @user-uc1pd1tc2x Před 29 dny +1

      😂😂😂😂😂Koma nanunso mnzeru zinakuperewerani bwanji 😂😂

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn Před 29 dny +2

    Akufuna ma vote then azaphakize ku mcp segulan maso amalawi ,sanatuluke awakugwilizano awa

  • @HappyAutumnTrees-cd9ye
    @HappyAutumnTrees-cd9ye Před 29 dny +2

    Anthuwa akuona ngt kusauka ndikupepera et asamatiseweretse ,,

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 29 dny +4

    Amalawi Mai uyu ndi clook ndi wa MCP musamuvotele

    • @MatthewKanyenda
      @MatthewKanyenda Před 29 dny

      Akufuna kusokoneza anthu awa, adalikuti pamene dziko lalowa chi vuto chimene talowachi.?

  • @JaffaliShaibu
    @JaffaliShaibu Před 28 dny

    Alipo ku PP konko ena tinasankha koma samatiyankha mafoni chinzake chinatha. Ndikanamutchula dzina koma basi.

  • @FredLeman-v5j
    @FredLeman-v5j Před 17 dny

    Munthu watuluka ku Mcp Kom ulibusy kulemekesa M'busa opusayu unyatu Palibe azakuvotere Mai wa cashgate

  • @FredLeman-v5j
    @FredLeman-v5j Před 17 dny

    Munthu watuluka ku Mcp Kom ulibusy kulemekesa M'busa opusayu unyatu Palibe azakuvotere Mai wa cashgate😂

  • @sanudiphimba8619
    @sanudiphimba8619 Před 29 dny +2

    Kupanda nzeru kwa mai uyu ndikomwe kwaika dziko pamoto, dyera linakula zedi.

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m Před 28 dny

    Kunama maiwa kufuna mavote aanthu basi ndi wa MCP Joice banda tikukuziwani ife munatipusisa kale

  • @user-xo8ms5wh2s
    @user-xo8ms5wh2s Před 29 dny +3

    Mwakalamba tazisiyana izi zikuchedwetsani zikufunika anthu amuna tipitani mukalape ku Church amai inu 😢

  • @user-zk7jw9up6m
    @user-zk7jw9up6m Před 28 dny

    Mulungu azikukanthani modzi modzi mpaka mutha phiti ndi ndalama za misonkho yathu ife amalawi

  • @user-mj4lp9fj4c
    @user-mj4lp9fj4c Před 29 dny +2

    Iwe ukuti unamaga sewu wathekerani wake wakuti wasowa zonama kumeneko munthu oipa iwe

  • @ChristopherNamatika
    @ChristopherNamatika Před 27 dny

    Ndinamanga manyumba ee misewu mamatiresi kkk sabola wakale sawawa masiten ndi mcp yanuyo

  • @EnerstBanda-m4s
    @EnerstBanda-m4s Před 29 dny +1

    Unamangaso Bingu Stadium osaiwala kuyatsaso magazi komaso kubweletsa mafuta omwe kunalibiletu munthawi ya Bingu komaso ndalama za kunja koma sutikukufunani pokhapokha mutaphatikuzana ndi utm

  • @IqrahSikweya-wm5mn
    @IqrahSikweya-wm5mn Před 28 dny

    Ndi ndale izitu koma iyeyo akunama sanatuluke angofuna kwapusitsa Amalawi

  • @kekeaufi9834
    @kekeaufi9834 Před 29 dny +9

    *Kumvesa chisoni ndi manyazi kwake ,,ambili akusokosa lerowa ndi amene amati mcp ilowe boma,,,lero ali pokopoko 😂😂😂😂tikusowa zotola,,,Atupeletu akhanena zonsezi amatiuza 😢😢*

    • @JohnJohn-og8rt
      @JohnJohn-og8rt Před 29 dny

      Patupere ndi maso mbenya atu amene asala mulungu akudalisene moyo wako tupere alamulire mzikolo rathu la Malawi inshall allah

  • @ObediMkwala
    @ObediMkwala Před 28 dny

    A JB,mudaitanitsa amayi akunyumba ya malemu Diet Mkwala kuti apite ku state House nthawi imene muli apresident koma palibe thandizo limene mudawapatsa amayi onfedwa,mudawonetsa kulephera kwanu

  • @ObediMkwala
    @ObediMkwala Před 28 dny

    Amayi aja mudawatsiya ali ndimisonzi m'manso awo muwalondole kunyumba kwawo ,muwafufuze kunthalireko mukawapepese chifukwa amuna awo adafera akutumikira inu,pangani zomwezo

  • @Blessings31
    @Blessings31 Před 29 dny +2

    Amayi ndi deal
    Yemwe zikumunyansa asanze

  • @BrownNamondwe
    @BrownNamondwe Před 27 dny

    Mfumu chopi yo ngati wakomedwa ndinsaluzo zake sitifuna nsaru ife

  • @GoldenIneyo
    @GoldenIneyo Před 21 dnem

    Ndine Golden k phiri kukasungu pepani Amayi musawavele Anthu achipongwe ife tilipambuyo panu

  • @user-qe6wr6wr8p
    @user-qe6wr6wr8p Před 27 dny

    I we about mayi wabodza,Loma dziko limenelo silako,silamakolo ako,koma ndilamulungu ,simunaphunzile koma kuyankhula

  • @MariaDavison-i6y
    @MariaDavison-i6y Před 29 dny

    Mseu wa Thekerani anamanga ndi peter osanamiza anthu

  • @mcsellahntv6896
    @mcsellahntv6896 Před 29 dny

    Kuteroko a MCP akuthamangitsani eti??,

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h Před 29 dny

    Mcp siyomapanga nayo alliance akuphani ohoo

  • @BrownNamondwe
    @BrownNamondwe Před 27 dny

    Zonena pa tv malamba umanga wekha

  • @Okalekale
    @Okalekale Před 29 dny

    Amayi awa ndiopanda manyazi,dyera ndilalikulu mwa amayi amenewa,m'mene anaonongela dziko? Malawi ali chonchi chifukwa cha UDF,DPP ndi PP ndiye akufunanso kulowa m'boma akatani?,akapitilize kuononga?.Anthu andalewa amatitenga aMalawi ngati opusa kwambiri,akuganiza kuti aMalawi anayiwala za ndalama zimakapezeka ku manda zija?.

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Před 29 dny +1

    Ambuye yesu

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x Před 29 dny +1

    Chakwera wakupha garu nyani mbuzi mfiti tombolombolo okumwa madzi ndikuthako

  • @ClementsKamanga
    @ClementsKamanga Před 29 dny +2

    Inuyo fundo zanu zilibwino koma anthu opanganawo mgwilizanowo mbola amai anthu akuopan chifukwa cha awowo

  • @JhdaLifi-vu9sd
    @JhdaLifi-vu9sd Před 29 dny

    Hule lamunthu ili zopepelesana tinasiya kugwadila mafano ife tinatopatu

  • @JevinTeller-en9rh
    @JevinTeller-en9rh Před 29 dny

    Bola JB yu osati Lazaro wa umphawiyu

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 29 dny +1

    Amai kuganidza watsanje lelo malawi ali pamoto pomwe munat anyamata alipula.pamoto dziko lelo nthawi MUTHALIKA ndi CHAKWELA mamvuto ali pati inu mwawononga nawo malawi kumatso mwaphetsa chilima chifukwa chodana ndi MUTHALIKA nde mwatidzudzitsa amai ndi MCP yanuyi yankhaza yakupha

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Před 29 dny +2

    Anapepelesa Amalawi kuti avotere chakwera,mavuto omwe ali lerowanso ali pat of it sangazembe,amati chakwera ndi m'busa sanganame.

  • @FredLeman-v5j
    @FredLeman-v5j Před 17 dny

    Mmai wabodza iwe shut up..... Sunatulukeso ku mcp

  • @FortuneAndrew-nb2im
    @FortuneAndrew-nb2im Před 29 dny

    Anthu opepera ngat inu ndiomwe mwapangisa malawi kukhala ovuta kwambiri mabvuto azaonen

  • @VincentMtambo
    @VincentMtambo Před 29 dny

    Chilungamo akuchidziwa

  • @BoscoWilliams-zl5sl
    @BoscoWilliams-zl5sl Před 29 dny

    Ayi zikomo mayi joyce banda pozindikira lero kuti tonse alliance kulibe. Mangani malamba and i quote

  • @VirginiaMafenda
    @VirginiaMafenda Před 29 dny +1

    Ngati atuluka bwanji akulimbana ndi peter munthalika pa mfundo yoti sanatuluke munyengo ya cyclone moti alunjike za sogolo lawo landale pamene atulukamu

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před 29 dny

    Division of southern votes that is great strategy

  • @user-ov7yw4bq7y
    @user-ov7yw4bq7y Před 29 dny +2

    Nsalu zithandiza chani koma kumalawi tili mubotolo ndithu

    • @MatthewKanyenda
      @MatthewKanyenda Před 29 dny

      Eish akulu inu Mmmm anthu timaganiza mofoila kwambiri et nsalu zoona anthu mkumaombera mmanja?

    • @user-uk3bz1hr5t
      @user-uk3bz1hr5t Před 29 dny

      Enawa nde akugawa chani?

  • @ObediMkwala
    @ObediMkwala Před 28 dny

    A JB adalojeza kuti amangira amayi omwe amuna awo adamwalira pangozi yagalimoto museu wachitipa jembia,koma ny'umbayo sadamange m'paka pano kuchoka chichitikireni changozi 2012,tikunena lero ndi 2024,atiuza chani ife?apite kuchitipa south akamangire kaye amaio aferedwa kaye ny'umba imene adalonjeza

  • @jamesmuyaya1158
    @jamesmuyaya1158 Před 28 dny

    Kodi when will the issue of politicizing maize end,??

  • @AbuZubeir-x4c
    @AbuZubeir-x4c Před 29 dny

    I support you amayi zinthu izi munaononga nokha nde bwerani mudzakonze zomwe munaononga

  • @ChristopherNamatika
    @ChristopherNamatika Před 27 dny

    Sabola wakale anzanga sawawa

  • @PaulOSBjaulen
    @PaulOSBjaulen Před 29 dny +1

    ❤❤❤❤❤

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 Před 29 dny +1

    Mayi, kaphikileni ana kunyumba ,ana akufa ndinjala

  • @user-io2uw2me9f
    @user-io2uw2me9f Před 29 dny

    Kunenatu chilungamo sck Joyce banda ndi mtambo sikut ndi anthu oipa koma chakwera nde mfiti theretu sanapange malonjezano ndi azake

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h Před 28 dny

    Mesa munatitulusa mu mboma mwa khaza,,,muwonadi nyengwe

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p Před 29 dny +1

    Ndale zama handouts siti tandiza amalawi.

  • @MrBone-zj1wq
    @MrBone-zj1wq Před 29 dny

    Mayi wanga contact yanu ndilibe koma ndikufuna nditalankhula nanu pofuna kuti ndithandizane nanu ku manga ma structures

  • @mcsydenynsinga7610
    @mcsydenynsinga7610 Před 29 dny

    Mujuaputa nokhatu anzanuwo mayi!! Kkkkk akakubwezelani basi muzinena kuti ndioipa akutukwana amayi kkkkkk inutu ndi a phokosodi ndithu😂😂😂😂

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh Před 28 dny

    Aaaaa inu munasokoneza amalawi musazivutepo apa

  • @SheriffNseula
    @SheriffNseula Před 29 dny

    Kodi fundo zonsezi mwayenda nazo ku tonse alliance osadzichita bwanji kumenekuja?zauhule basi
    Kodi kupanga alliance kuja mesa kuti nonse muyendetse dziko?ndiye lelo mudzinama zamfundozinso???mwaipa basi

  • @Edson-sj8vn
    @Edson-sj8vn Před 29 dny

    Alephera kubamo pano MCP ndiyoipa kkkk andalewa anakonzaa

  • @ThomasMwandila-tn7cf
    @ThomasMwandila-tn7cf Před 28 dny

    Amama mukutani nthawi yanu chakudya chinariposepose

  • @FatimaSande-lb1hd
    @FatimaSande-lb1hd Před 26 dny

    Koma amai ali pompano? 🤭 Nzibambo kudikila kkkkkkk.....

  • @vitujames53
    @vitujames53 Před 29 dny +1

    Nkhani ndi imeneyo...okumva wamva

  • @HappyAutumnTrees-cd9ye

    Anthu lero akuvutika ndinjara ndie muzit tatuluka mukutanthauza chani muwasiya anthuwa akuvutika Chonchi mulungu akuyendeleni anthu inuyo ndithu😭😭😭😭

  • @TiyanjaneMkwate-we8gu
    @TiyanjaneMkwate-we8gu Před 29 dny

    Amayi anthu asakupusiseni, panokha simungawine, even itakhala kuti si 50+1.

  • @PaulDaka-dc3re
    @PaulDaka-dc3re Před 29 dny +1

    Mayiwa achedwa nazo it's too late

  • @MrBone-zj1wq
    @MrBone-zj1wq Před 29 dny

    Mayi Banda tili nanu limodzi ndipo titipulira limodzi ngati mutafuna kutero

  • @simonmakamba9539
    @simonmakamba9539 Před 29 dny

    Mayi wanga uyu ndilibe naye vuto konse

  • @thomasmcbanda9794
    @thomasmcbanda9794 Před 29 dny

    Kuzavotera pp wavotera MCP samalani

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před 29 dny

    Mai woipa iwe kachipani Kako kam'manjako

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 Před 29 dny

    Tangopitani denfen jbk inu Mai, za ndalezi ai siyani😂😂

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Před 29 dny

    ATUMIDWA NDI MCP KUTI AGAWE MA VOTE A DPP KUMMWERA

  • @HajjAmadu-e1u
    @HajjAmadu-e1u Před 29 dny

    Maiwa ndiopa inde tikamva imfa ya chilima ati akukhuzidwa koma Pena tiziyamikira ku zomba amangra nyumba anthu akulu akulu apa ai anayesetsa mai

  • @swadikimbwana7680
    @swadikimbwana7680 Před 29 dny +2

    Mai ndithudi munapanga chithukoko kwabasi
    Apa ndikuchita
    maDua kuti Insha Allah mukakalenso pa mpando wa Pulesideti 2025

  • @MirajiYusuf-u9r
    @MirajiYusuf-u9r Před 29 dny

    Push us mom nganganga pambuyo panu

  • @user-ol1hf7ru1v
    @user-ol1hf7ru1v Před 29 dny

    Cash get back

  • @mosesdevwe4267
    @mosesdevwe4267 Před 29 dny

    After utagulitsa ndege,,, mayi awanso nde ayitu

  • @user-chimenyaMTV
    @user-chimenyaMTV Před 29 dny +1

    Koma nyimbo YOMWE mumaika pansi simagwilizana abwana sithani beat

  • @arthurmakuluni6676
    @arthurmakuluni6676 Před 29 dny

    Inde mayi

  • @BrownMainje-sh7hj
    @BrownMainje-sh7hj Před 29 dny

    Joyce Banda iwe sukufunachani iwe sukufunachani iwe Joyce

  • @TomasKalizga
    @TomasKalizga Před 28 dny

    Bro kungokupemphani kuti mkamapanga posit ma videos muleke kuyamba kulakhulapo komaso musiye kuikapo nyimbo coz overafe zikuti sokoneza

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Před 29 dny

    Mamaawa dyera

  • @FrankFrancis-ch3xv
    @FrankFrancis-ch3xv Před 29 dny

    Nzibambo kudikula kumeneko koma mayi alipompano?joyce banda funso?😅😅

  • @dianachabs
    @dianachabs Před 29 dny

    Tipatseni signal 🚦 mama tilowele kuti?

  • @user-fh3dn8kt2j
    @user-fh3dn8kt2j Před 29 dny

    Akuima chifukwa anthu akuti awauza, kuti aime aati,,koma maiwa nde mphanvu zikupita ndithu koma dyera silabwino ataa

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev Před 29 dny

    Ndale zoyipa mwapangana zoti mugawe ma vote akumwela kuno....mmmmmmm

  • @chisomokalinda6666
    @chisomokalinda6666 Před 29 dny

    Tipaseni number yawo mayiwa

  • @user-dg5pc6rz1b
    @user-dg5pc6rz1b Před 29 dny +1

    Kkkkk mcp siyingayanjaneso ndi utm anthuwa akudziwa

  • @NtchindiChirwa-l8o
    @NtchindiChirwa-l8o Před 29 dny

    Tikumenyan ana mwachepa nazo😂😂

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před 29 dny

    😂😂😂😂😂😂 atulukamo

  • @MphatsoMkanda-g1o
    @MphatsoMkanda-g1o Před 29 dny

    Anali kale uyu

  • @sanudiphimba8619
    @sanudiphimba8619 Před 29 dny

    Mai wachinyengo uyu,

  • @kennedychinguwo1640
    @kennedychinguwo1640 Před 29 dny

    Kodi PP ndi chani??

  • @dianachabs
    @dianachabs Před 29 dny

    Amayi woyeeeeeee

  • @chimwemweshadrick5972
    @chimwemweshadrick5972 Před 29 dny

    Amaiwa amabhebhetsa

  • @williammandhlopa
    @williammandhlopa Před 29 dny

    A usi akutani ngati alliance yathaa

  • @user-gm9xj1wc2m
    @user-gm9xj1wc2m Před 29 dny

    Muli mbuli mbuli

  • @tobiousmtenje139
    @tobiousmtenje139 Před 29 dny

    Inatha kale kale,anthuni mumangokakamila

  • @ADHASAPONYILENDA
    @ADHASAPONYILENDA Před 29 dny

    Kusowa chochita manyazi awo

  • @dalitson3558
    @dalitson3558 Před 29 dny

    Uchose nyimbo ikumveka pansiyo

  • @jahmanmakwinja-ef7zn
    @jahmanmakwinja-ef7zn Před 29 dny +1

    Kung'alura mai more fire

  • @duncanKingsly
    @duncanKingsly Před 29 dny +2

    Palibepo ndikunva