Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya
This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂
That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.
Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi
The first program kuonera ndikuseka nawo limodzi 😊 pamene enawa kumangokhala kulozana zala basi. What a great man
Long live our former president
Respect to you our X President Dr Bakili Muluzi🙏🙏🙏💕
Pule amene anawafesa kukoma amalawi paka nthawi yochepa😢😢 mulungu akudaleseni mr muluz ndi wumoyo ndimakukondan❤❤❤❤❤
what a wonderful interview, ViVa a tcheya, the best well dressed president in Malawi
Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya
Long live Dr Bakili Muluzi❤❤❤❤❤❤
Atcheya tsopanoooo!!! timakunyadirani president wamsangala odziwa kuseka, osakhala zinazi aaaah
Well spoken Dr Bakili Muluzi atsogoleri azitero tikufunilani moyo wautali pamodzi ndi family yanu Mulungu azikudalisani nthawi zonse
Bakili knows how to choose but bingu was the best ayao simuziwa economy
This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂
That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.
This man his is another level just hear his voice 😊
Long live Dr. Bakili Muluzi
Abwanawa ndi munthu wabwino
We will always Love you a chair.❤❤
Long live.
Nantahala ife muthawi yanu long life atcheya
The great man 🎉❤
Kuti enafe tisakhuzidwe ndi nkhaza za chipani chimodzi for that time Achair,,,munatinvetsa kukoma mu nthawi yanu❤❤❤❤❤
Achalume kuchitekete God be with you
Watching live from SA Durban KZN
I like his voice
Long live achair!we love u!
Munthu amene anapangitsa Malawi kukhala owawa kwambiri panopa. Chomwe ankagulitsira ma company kwa amwenye sichikudziwika
Long live atcheya❤
Anamva mtunda ukufotokoza, anamva zonsezo ( I remember Mkasa's song. A Chair ndi mtunda)
Great man
Much respect to our granny mumakwana 🎉🎉🎉🎉
Quran on shelf mashala habibi
Big man ever
Allah akudalitseni a chair
To be honest this man is a greatest man,,,,,,,,,,,,,,,,,long live Dr Bakili Muluzi we love you very much ❤❤❤❤
Pa town kumachenjela ❤❤❤achalume
The most likeable PULE of Malawi kuseka continuous
A Gama we love you,long live
Bakili vuto linapo ndi umbuli komanso business yake o i hope anali kupikulitsa bonya. Nfi masamba
Government doesn't run a business. It should create atmosphere for people to do business.
Ndani wamva zimenezi bwinobwino?
Ine ndinamva, tcheya si munthu wamba baba anakonza
umenewu ndi ntondo endeed
Achair Allah bless you ❤❤❤❤❤
Ulemu wanu acheya timakunyadirani kwambiri potibweretsela ufulu Allah bless you more
Long live Muluzi
Malawi ndi dziko lokhalo lomwe mapresident opuma akumva kukoma. Ulemu wanu a Chakwera.
Taonani a Muluzi,mayi JB, Khumbo, APM, Chilupha n ena.
Simungathe kusangalatsa aliyese koma ndinu big man muthu wa bwino kwambili
Big man
Big man tsopano ❤❤❤
putin waku malawi bakili
Nice
Ku machinga Kwa chikweo ndiye kwathu 😂😂😂
Sizaiwa former President pa free education primary sizophweka
Watch live from Nyambadwe
Kholo pa ndale
Mr fake money... Kape wina amene anazesa mavuto mmalawi.kugulitsa ma company chitsiru
Long live former president a chair anthu
kuntunda 🔥
Atcheya woeeee!
Ndale ndi tchimodi cz muli kuba muli bodza
Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi
❤❤❤
Bambo anagwila ntchito yotamandika awa. Mulungu adziwapatsa dza bwino iwowa
Kuchitekete
Mumakwana acheir
Sogoreri aziseka abale .Atcheya inuyo ndati inuyo inuyo Atcheya mulungu azikudalitsani
Awa ndatcheya kuchikweza kkkkkk
Achair ine ndilipo nkubwera konko ndithu
Mwana wakwathu
Achalume koma atcheya mmm amathandiza
Achakulungwa wachiyao
Tcheya ndikaswiri
Atcheya mmakwanila
Atcheya
Kumtunda
Muthu wakulu kwambiri
President olankhula zonveka bwino,,,not zinaziyi
10:20
M,tunda wa m,ndale
Kungogulitsa ma company a boma basi ndalama kupochera achalume anali ochenjera
A Chair palibenso
Uyu ndi amene anayamba kugwirisana ndi amwennye nkhani yobera amalawi
Achisilu inu
professor
Tate wokondeka
Kungocho kela kuchalichi kuvuna udndo ngamti chakwera
Bigy...
Achalume🥸
Byson mwaona
Awa anali adindo
Tionele zimenezi
Mbava iyi ndi yomwe inaononga zuko lamalawi
Achisilu inu you know not
Umbuli
Owononga sukumuona
Munthu wamkulu ❤❤
munali munthu
Munthu wamkulu
By mentioning Late Chikufwa Chihana he was being honest, that name contributed a lot to Malawi democracy!
Mukatero ndinu mtumbuka , mumapopanatu
The worst present ever
Anakulamulirabe 10 yrs for sure