BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 10. 05. 2024

Komentáře • 97

  • @osmanmalinda939
    @osmanmalinda939 Před 2 měsíci +9

    The first program kuonera ndikuseka nawo limodzi 😊 pamene enawa kumangokhala kulozana zala basi. What a great man

  • @TabiaNicks
    @TabiaNicks Před měsícem +5

    Long live our former president

  • @GhettohVibies-wn9zo
    @GhettohVibies-wn9zo Před měsícem +1

    Respect to you our X President Dr Bakili Muluzi🙏🙏🙏💕

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y Před 2 měsíci +3

    Pule amene anawafesa kukoma amalawi paka nthawi yochepa😢😢 mulungu akudaleseni mr muluz ndi wumoyo ndimakukondan❤❤❤❤❤

  • @luetec
    @luetec Před 2 měsíci +2

    what a wonderful interview, ViVa a tcheya, the best well dressed president in Malawi

  • @waxyamidu5638
    @waxyamidu5638 Před 2 měsíci +2

    Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 Před 2 měsíci +8

    Long live Dr Bakili Muluzi❤❤❤❤❤❤

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před 2 měsíci +3

    Atcheya tsopanoooo!!! timakunyadirani president wamsangala odziwa kuseka, osakhala zinazi aaaah

  • @user-he7bu2tp8z
    @user-he7bu2tp8z Před měsícem +1

    Well spoken Dr Bakili Muluzi atsogoleri azitero tikufunilani moyo wautali pamodzi ndi family yanu Mulungu azikudalisani nthawi zonse

  • @user-qe2lz7mx7u
    @user-qe2lz7mx7u Před měsícem +1

    Bakili knows how to choose but bingu was the best ayao simuziwa economy

  • @rashiddeula5715
    @rashiddeula5715 Před měsícem +1

    This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂

  • @DonaldBanda-qi7yw
    @DonaldBanda-qi7yw Před 26 dny

    That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.

  • @ImraanYaseen25
    @ImraanYaseen25 Před 2 měsíci +1

    This man his is another level just hear his voice 😊

  • @JoshusMbewe
    @JoshusMbewe Před měsícem +1

    Long live Dr. Bakili Muluzi
    Abwanawa ndi munthu wabwino

  • @magdalinemafunase2440
    @magdalinemafunase2440 Před měsícem

    We will always Love you a chair.❤❤
    Long live.

  • @AdamSteven-ne9hg
    @AdamSteven-ne9hg Před měsícem +1

    Nantahala ife muthawi yanu long life atcheya

  • @jaydee1236
    @jaydee1236 Před 2 měsíci

    The great man 🎉❤

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p Před 2 měsíci

    Kuti enafe tisakhuzidwe ndi nkhaza za chipani chimodzi for that time Achair,,,munatinvetsa kukoma mu nthawi yanu❤❤❤❤❤

  • @WellieManonga
    @WellieManonga Před 2 měsíci +1

    Achalume kuchitekete God be with you

  • @FrankFrancis-ch3xv
    @FrankFrancis-ch3xv Před 2 měsíci +1

    Watching live from SA Durban KZN

  • @SwidiqLameck
    @SwidiqLameck Před měsícem

    I like his voice

  • @user-cw6jg6xg7h
    @user-cw6jg6xg7h Před 2 měsíci

    Long live achair!we love u!

  • @mtangaJumbe
    @mtangaJumbe Před měsícem

    Munthu amene anapangitsa Malawi kukhala owawa kwambiri panopa. Chomwe ankagulitsira ma company kwa amwenye sichikudziwika

  • @atanasioestevao9707
    @atanasioestevao9707 Před 2 měsíci +1

    Long live atcheya❤

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Před 2 měsíci

    Anamva mtunda ukufotokoza, anamva zonsezo ( I remember Mkasa's song. A Chair ndi mtunda)

  • @tiongegondwe7219
    @tiongegondwe7219 Před 2 měsíci

    Great man

  • @shakajudahTV
    @shakajudahTV Před 2 měsíci

    Much respect to our granny mumakwana 🎉🎉🎉🎉

  • @EddieBakali
    @EddieBakali Před 2 měsíci +1

    Quran on shelf mashala habibi

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 Před 2 měsíci

    Big man ever

  • @user-yk7gj1sl2z
    @user-yk7gj1sl2z Před 2 měsíci

    Allah akudalitseni a chair

  • @user-sq2uz6yl3s
    @user-sq2uz6yl3s Před 2 měsíci +1

    To be honest this man is a greatest man,,,,,,,,,,,,,,,,,long live Dr Bakili Muluzi we love you very much ❤❤❤❤

  • @ibradaglass8646
    @ibradaglass8646 Před 2 měsíci

    Pa town kumachenjela ❤❤❤achalume

  • @darlingtonchimutu8390
    @darlingtonchimutu8390 Před 2 měsíci

    The most likeable PULE of Malawi kuseka continuous

  • @CumbuNgoma
    @CumbuNgoma Před 2 měsíci

    A Gama we love you,long live

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Bakili vuto linapo ndi umbuli komanso business yake o i hope anali kupikulitsa bonya. Nfi masamba

  • @cristovaoherculano8662
    @cristovaoherculano8662 Před 2 měsíci +5

    Government doesn't run a business. It should create atmosphere for people to do business.
    Ndani wamva zimenezi bwinobwino?

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 2 měsíci

    Achair Allah bless you ❤❤❤❤❤

    • @user-ub1vt2kq4s
      @user-ub1vt2kq4s Před 2 měsíci

      Ulemu wanu acheya timakunyadirani kwambiri potibweretsela ufulu Allah bless you more

  • @victorzakeyuzimba7742
    @victorzakeyuzimba7742 Před měsícem

    Long live Muluzi

  • @stewart.mwamughunda
    @stewart.mwamughunda Před měsícem

    Malawi ndi dziko lokhalo lomwe mapresident opuma akumva kukoma. Ulemu wanu a Chakwera.
    Taonani a Muluzi,mayi JB, Khumbo, APM, Chilupha n ena.

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Před 2 měsíci

    Simungathe kusangalatsa aliyese koma ndinu big man muthu wa bwino kwambili

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Před 2 měsíci

    Big man

  • @MonicaMbwera
    @MonicaMbwera Před měsícem

    Big man tsopano ❤❤❤

  • @Oraterbadri
    @Oraterbadri Před 2 měsíci +1

    putin waku malawi bakili

  • @ChristopherKalonga-jt8iz
    @ChristopherKalonga-jt8iz Před 2 měsíci

    Nice

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 Před 2 měsíci

    Ku machinga Kwa chikweo ndiye kwathu 😂😂😂

  • @JustinPhiri-kq2bb
    @JustinPhiri-kq2bb Před 2 měsíci

    Sizaiwa former President pa free education primary sizophweka

  • @user-hx8rr1mq7u
    @user-hx8rr1mq7u Před 2 měsíci

    Watch live from Nyambadwe

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Před 2 měsíci

    Kholo pa ndale

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Mr fake money... Kape wina amene anazesa mavuto mmalawi.kugulitsa ma company chitsiru

  • @zondiwesinging8001
    @zondiwesinging8001 Před měsícem

    Long live former president a chair anthu

  • @aureliojose763
    @aureliojose763 Před měsícem

    kuntunda 🔥

  • @osmanwanja3733
    @osmanwanja3733 Před 2 měsíci

    Atcheya woeeee!

  • @Gra898
    @Gra898 Před měsícem

    Ndale ndi tchimodi cz muli kuba muli bodza

  • @NoelKhwimba-bh3ts
    @NoelKhwimba-bh3ts Před 2 měsíci

    Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi

  • @respectednation
    @respectednation Před 2 měsíci

    ❤❤❤

  • @AlidiMusa
    @AlidiMusa Před 2 měsíci

    Bambo anagwila ntchito yotamandika awa. Mulungu adziwapatsa dza bwino iwowa

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f Před 2 měsíci +1

    Kuchitekete

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h Před měsícem

    Mumakwana acheir

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Před 2 měsíci

    Sogoreri aziseka abale .Atcheya inuyo ndati inuyo inuyo Atcheya mulungu azikudalitsani

  • @respectednation
    @respectednation Před 2 měsíci

    Awa ndatcheya kuchikweza kkkkkk

  • @user-cb9us2gn9v
    @user-cb9us2gn9v Před 2 měsíci

    Achair ine ndilipo nkubwera konko ndithu

  • @innocentmabedi3850
    @innocentmabedi3850 Před měsícem

    Mwana wakwathu

  • @christophermukaka7403
    @christophermukaka7403 Před měsícem

    Achalume koma atcheya mmm amathandiza

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Před 2 měsíci

    Achakulungwa wachiyao

  • @SullyBartsony
    @SullyBartsony Před 2 měsíci

    Tcheya ndikaswiri

  • @LangretBanda
    @LangretBanda Před 2 měsíci

    Atcheya mmakwanila

  • @rexphiri7242
    @rexphiri7242 Před 2 měsíci

    Atcheya

  • @chawezichipeta5326
    @chawezichipeta5326 Před 2 měsíci

    Kumtunda

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 Před 2 měsíci

    Muthu wakulu kwambiri

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p Před 2 měsíci

    President olankhula zonveka bwino,,,not zinaziyi

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah Před 2 měsíci

    10:20

  • @BashielSalade
    @BashielSalade Před 2 měsíci

    M,tunda wa m,ndale

  • @harrispheleni2205
    @harrispheleni2205 Před 2 měsíci

    Kungogulitsa ma company a boma basi ndalama kupochera achalume anali ochenjera

  • @rtqwtetohedron
    @rtqwtetohedron Před 2 měsíci

    A Chair palibenso

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q Před 2 měsíci

    Uyu ndi amene anayamba kugwirisana ndi amwennye nkhani yobera amalawi

  • @chinielstailoring-ro9lu
    @chinielstailoring-ro9lu Před 2 měsíci

    professor

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg Před 2 měsíci

    Tate wokondeka

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před 2 měsíci

    Kungocho kela kuchalichi kuvuna udndo ngamti chakwera

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah Před 2 měsíci

    Bigy...

  • @user-xe3xo5mu9k
    @user-xe3xo5mu9k Před 2 měsíci

    Achalume🥸

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Před 2 měsíci

    Byson mwaona

  • @user-fh5yn8xk2k
    @user-fh5yn8xk2k Před 2 měsíci

    Awa anali adindo

  • @user-nd8zg6ni7l
    @user-nd8zg6ni7l Před 2 měsíci

    Tionele zimenezi

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q Před 2 měsíci

    Mbava iyi ndi yomwe inaononga zuko lamalawi

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 Před 2 měsíci

    Munthu wamkulu ❤❤

  • @OscarChizula-qr4bi
    @OscarChizula-qr4bi Před 2 měsíci

    munali munthu

  • @AllieKaisi-je6rm
    @AllieKaisi-je6rm Před 2 měsíci

    Munthu wamkulu

  • @patrickyakobe9685
    @patrickyakobe9685 Před měsícem

    By mentioning Late Chikufwa Chihana he was being honest, that name contributed a lot to Malawi democracy!

  • @kondwanimbewe1317
    @kondwanimbewe1317 Před 2 měsíci +1

    The worst present ever