Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 07. 2024

Komentáře • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b Před 19 dny +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @EversDman
    @EversDman Před 18 dny

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya Před 18 dny

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Před 19 dny +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane Před 12 dny

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri Před 18 dny

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k Před 19 dny +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g Před 18 dny

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp Před 18 dny

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 Před 19 dny

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t Před 19 dny

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael Před 19 dny

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Před 19 dny

    Big up bro

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před 19 dny

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy Před 18 dny

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu Před 19 dny

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @AffickChaona
    @AffickChaona Před 16 dny

    ❤❤❤❤❤

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Před 19 dny

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Před 19 dny +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před 19 dny

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d Před 19 dny

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x Před 18 dny

    Zoona amwene

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před 19 dny

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před 19 dny

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 Před 19 dny

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq Před 19 dny

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg

    The DC 🔥

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula Před 18 dny

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 Před 19 dny

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg Před 19 dny +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js Před 19 dny

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l Před 19 dny

    Awa ndie mawu

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m Před 19 dny

    Ai zikomo 🥱

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa

    Ambuye akudalitsen

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 Před 19 dny +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 Před 19 dny

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi Před 19 dny

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @SmartMoles
    @SmartMoles Před 18 dny

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x Před 19 dny +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 Před 19 dny

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v Před 19 dny

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi Před 19 dny

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Před 18 dny

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Před 18 dny

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q Před 19 dny

    Dc

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 19 dny

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa Před 19 dny

    Dzelu zachepa kkkk

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l Před 18 dny

    Mumatiyimilila

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu Před 19 dny

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 Před 19 dny

    Kalindo samaopa😂😂

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr Před 19 dny

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga Před 18 dny

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd Před 19 dny

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns Před 19 dny

    Ati kutitola kapena chani

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j Před 19 dny

    Awuzeni

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward Před 18 dny

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k Před 19 dny

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera Před 18 dny

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro Před 18 dny

    😂🤣😂🤣

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 Před 19 dny

    😂😂 kung'alulatu

  • @pempheroraynnoxmpesi8713

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @GiftKulture
    @GiftKulture Před 19 dny

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @AaronLitete
    @AaronLitete Před 19 dny

    Kkkkk boma lopusa

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do Před 19 dny

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f Před 18 dny

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 Před 19 dny

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f Před 19 dny

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k Před 19 dny

    😂😂😂😂

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b Před 19 dny

    😅😅😅😅

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 Před 19 dny

    Bigiliman naweni

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i Před 19 dny

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o Před 19 dny

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j Před 19 dny +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri Před 19 dny

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Před 19 dny

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Před 19 dny

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n Před 19 dny +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 Před 19 dny

    😂😂😂😂😂