MAFUNSO OVUTA OMWE ATOLANKHANI ANAWAPANIKIZA NAWO A BON KALINDO LERO PAMENE AMACHITITSA CONFERENCE

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 7. 09. 2024

Komentáře • 358

  • @AiameAdamo-su1nt
    @AiameAdamo-su1nt Před měsícem +22

    Kuyankha mafunso mosanyengelela munthu the DC😂😂😂.

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Před měsícem +1

      Mafunso ake ATI amalephera kuyankha o ha ha ha ha ha

  • @stevechikaonda3145
    @stevechikaonda3145 Před měsícem +6

    Tinene kuti wopaanda nzeru nduyu walemba kuti atolankhani anapanikiza Kalindo, coz he has been consistent and confident in his responses to the posed or you just wanted to lure us and watch this

    • @edsongeorge8032
      @edsongeorge8032 Před měsícem

      nkhaniyi ndiyoona malume opanda nzeru ndamene walemba izi.

  • @macrinenduna1024
    @macrinenduna1024 Před měsícem +21

    Pamenepa mukati atolonkhani anapanikiza mafinso, ndifunso liti lajejemetse Malawi Fist?

    • @user-vt4zo7eo2s
      @user-vt4zo7eo2s Před měsícem +1

      Ineso sindikupeza olo limodzi

    • @user-hm9nc7lz6e
      @user-hm9nc7lz6e Před měsícem +1

      Palibe malawi first number one

    • @MarkJere-c2d
      @MarkJere-c2d Před měsícem +1

      Njila imodzi yofuna kut muonele kaaaa kkkk

    • @user-zy1eh3pt8v
      @user-zy1eh3pt8v Před měsícem

      I had the same question 😂😂😂😂

    • @edsongeorge8032
      @edsongeorge8032 Před měsícem

      @@user-zy1eh3pt8v inenso I wanted to ask kuti ndipati pomwe Bon kalindo ?

  • @danielmurichi5673
    @danielmurichi5673 Před měsícem +7

    Anyamata wa ali serious bwino kwambiri
    Keep it up osagonja ndipo boma limeneli lisamale osama one ngati malawi ndiiwowokhawo nafeso ndi malawi
    Pasafe olo mmodzi panewa kuteloko nkhondo idzayamboka chifukwa nthawi tiliyi ndiya democracy
    Tikufuna ufulu oyankhula osati kuopsezedwa

  • @user-sb2mw3xz4j
    @user-sb2mw3xz4j Před měsícem +9

    😂😂😂Koma KALINDO eish big respect,

  • @KingfrahMachado
    @KingfrahMachado Před měsícem +4

    Ndipo inu a bon mulungu aziwe pachilungamo chimene mukuonesa kwaife amalawi osauka❤

  • @TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT
    @TEACHTHEWORDMINISTRIESINTERNAT Před měsícem +12

    In fact chilungamo chake anayenera kuti adzigula sticker ndi amene wagwidwa atazemba pa boarder. Wokhulupirika apatsidwe sticker yaulele, wozemba akapezeka agule sticker ngati mbali imodzi ya chindapusa.

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Před měsícem +6

    The DC woyeeeeee 🎉🎉🎉🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @KingfrahMachado
    @KingfrahMachado Před měsícem +4

    Akapusa mwezi sivuto end President aziter kuyakha mopanda mantha💪💪💪🔥

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z Před měsícem +6

    We love you Mr DC

  • @CharityGondwe-bw9gs
    @CharityGondwe-bw9gs Před měsícem +12

    Mumatiimilira mr kalindo ndi azanuwo murandire ulemu❤❤❤❤❤❤❤

    • @InnocentMtafya
      @InnocentMtafya Před měsícem

      Musaiwale atamupatsa u ambassador kupita kunja, anazasanduka munthu wina nkumati a Malawi sioafela koma makobidi nde dilu, mwaiwala, eti anapepesa...🤔🤔mmmhhh!(Ndalamaa eeeh!!!!)

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Před měsícem

      Kkkkk go ko nko sambe madzi achitedze basi 😂😂😂 😂😂😂 kalindo umakwana

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Před měsícem

      Osadanda tililimozi ati u ze 💪💪💪🔨🪓🗡️ bwino zatikwana

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Před měsícem +2

    Bon .you are very intelligent gentlemen. Iam behind you❤❤❤❤❤

  • @BenedictFriday-c2w
    @BenedictFriday-c2w Před 24 dny

    The DC keep it up the good work

  • @DollarChagamba
    @DollarChagamba Před měsícem +7

    Palibe fuso lomwe lawakanika kuyankha

  • @user-bi5lg8mg9y
    @user-bi5lg8mg9y Před měsícem +24

    Mr Bon kalindo z very strong weapon speech

    • @StanleyDama
      @StanleyDama Před měsícem

      Do y know the meaning of weapon ?

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Před měsícem

      ❤❤❤ 1277 kkkkkk

    • @SteveniBanda
      @SteveniBanda Před měsícem

      Gwira chito kalindo 😂😂😂😂 kuswa kuswa kung'alura kung'alura😂😂 tiyenawo osawasiya😂😂

    • @ChipanganoPhiri
      @ChipanganoPhiri Před 24 dny

      Big boss

  • @user-rb7mp3rv7g
    @user-rb7mp3rv7g Před měsícem +5

    Pamenepa mafunso ovuta alipati please ma topic anuwa tamaonani Kaye aaaa😂😂

    • @martinndawala8125
      @martinndawala8125 Před měsícem +1

      Amangofuna anthu akhale ndi chidwi chowonera 😂😂

  • @HanishKenneth
    @HanishKenneth Před měsícem +7

    Kutchaya kugwetsa we are united

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju Před měsícem +3

    The DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥MRA sikuganizira ife ochita malonga...in add off kubweretsa sticker ndi njira imodxi yofuna kusokoneza ife a business kuti tisamapindule ...Boma lionepo bwino apa....

  • @PetroGondwe
    @PetroGondwe Před měsícem +1

    Kalindo is a true light to Malawian paths.youths wake up please,osamangovina amapiano fight for your nation and your future.

  • @daviebanda5098
    @daviebanda5098 Před měsícem +4

    Kkk akut amathamanga ndimasuti😂😂😂😂 booom the DC🔥🔥🔥

  • @AronZayaweh
    @AronZayaweh Před měsícem +8

    Masiku atha kale awaa chakwela abwelele kudambw

    • @UssenNjirinah
      @UssenNjirinah Před měsícem

      Kkkkkk mpaka pele ajawuleje kudambwe Kwene chinyago changatama ku state house chijaule kwawo kwawo kudambwe

    • @user-dl4ud7mp4n
      @user-dl4ud7mp4n Před měsícem

      😂😂😂😂😂

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Před měsícem +5

    Mr Chikangawa akutitola kwambiri

  • @PatYøna
    @PatYøna Před měsícem +2

    Yesterday I saw achinyamata akulemba anthu a kwa tongole in area24, ndinafusa modzi wa Iwo anati atumidwa kuti alembe anthu osati obwera but amagazi ... Kuti adzilandira ntukula pakhomo every month and fertilizer. But onse ogula malo ayi asamulembe. Is this fair abale inuuuu 😢😢😢

  • @PastinaHope
    @PastinaHope Před měsícem

    Tikuthoza kwambir a bon karindu pa zime mpatipangira ife osauka mulungu akhare ND Inu nose ❤❤🎉

  • @FrancisMbwana-z5l
    @FrancisMbwana-z5l Před 29 dny

    Very powerful from kalindo

  • @DysonChiumia
    @DysonChiumia Před měsícem +3

    The DC🔥

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 Před měsícem +3

    The DC🔥🔥🔥🔥

  • @EffordKapichi
    @EffordKapichi Před měsícem +1

    You are our weapon chief

  • @user-ee1ci2ku6o
    @user-ee1ci2ku6o Před měsícem +6

    We are frant of you mr kalindo DC 💪💪💪💪

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Před měsícem

    Kalindo ndinkamuna ogona kukhomo kosachinjika abro 🔥🔥🔥🔥 Yehova apilile kumusunga ndimoyo wautali

  • @YamikanipilatoPilato
    @YamikanipilatoPilato Před měsícem +2

    Number one chi dc

  • @BlessingsNyirenda-ru7ss
    @BlessingsNyirenda-ru7ss Před měsícem +2

    More fire born kalindo

  • @williammasiano1194
    @williammasiano1194 Před měsícem +2

    Viva Malawi 1st ...eish anthu amafika potopa

  • @emmanuelmuyilaa
    @emmanuelmuyilaa Před měsícem +4

    Koma kumeneko❤

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem +5

    Kumpoto kumwera tikuoneka ngati sindife amalawi. Koma achigawo chapakati ndi a Malawian. Kumupoto kulibe chilichose i love you Mr DC and your members mademo alhalepo tikufuna chilungamo si nkhondo koma kukoza ziko lathu

  • @JonathanHeadson
    @JonathanHeadson Před měsícem +3

    Mafunso akeso ati ovutawo nanu

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 Před měsícem +6

    Kuchokera 2020 mupaka pano chimene tapidula ndibomali kukumangidwa boza kulankhula mozikona kulekerera muchitidwe wa katangale kulembana pamutundu ntchito kuononga immigration kuononga ACB kuononga admac kuononga apolice kuononga nkhalango ya chikangawo po gwesako ndege kuononga nrb kuononga chipani cha utm kusunga nduna zachiwewe muchipani zopanda phindu. Ndizina zambiri zaonongeka kumalawi ndichitukuko chimene talandila kumalawi for 4years mmmm

  • @isaacthawani5442
    @isaacthawani5442 Před měsícem +2

    Ndie awa akut mafuso ovuta mene akuyakhiramo sukuona kt dola ndi kalindoyo mbuzi iwe

  • @FloridaMakwinja-eq2ek
    @FloridaMakwinja-eq2ek Před měsícem +4

    The DC moto wokhawokha

  • @DonPhiri-u2j
    @DonPhiri-u2j Před měsícem

    Ife tikungodikira mulungu atithandize coz ulosi wa malemu grace chinga unanena kale kuli kuti kukubwera chipani cholimbana ndi mwazi komaso thukuta kma mukamaliza zonsezi muziwe kuti mulungu achitapo mbali yake ife tikuyembekeza pamulungu osati munthu amen

  • @PeturosiNyirenda
    @PeturosiNyirenda Před měsícem +1

    😂 bon kalinda nd 1🎉

  • @PropeeLucious
    @PropeeLucious Před měsícem +2

    Ndati ndikuuze I kuti bon kalindo akupusisani eye ndi ganyu imeneyi please please achinyamata musamangotenga ndizina zili zonse mtambo anakunamizan pano ndi bon kalindo please changamuka achinyamata mmalo mosaka ndalama kuti moyo wanu usithe muli busy kuchemelera munthu wina mmmmmmm

    • @SalaJawali
      @SalaJawali Před měsícem

      Utiuza zopusa zo ife tilibe Maso owonela kuti dziko muno zinthu sizilibwino

    • @robenallie6985
      @robenallie6985 Před měsícem

      Iwe ndi wa mcp

    • @SharonNdadza
      @SharonNdadza Před měsícem

      Nawe akupasa a mcp ndrama? Chonsechonso azimbuyanu akuvutika mma midzi uko

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Před měsícem

      @@SharonNdadza ndye zoyankhula za kalindo zipangisa kuti ambuye asavutike mmmmmmm mbuli za kalindo muzafa chifukwa chosatilq zinthu zopusa ngt zimenezo

    • @PropeeLucious
      @PropeeLucious Před měsícem

      @@SalaJawali iwe ndye kalindo ndi amene angasithe zinthu musanamizidwe kuti kape ngt amene uja palibe chimene angaphule

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Před měsícem +1

    Kalindo ndi wa DDP chonde a Malawi musapuse naye akudya ndalama za peter anapatsidwa target

  • @MadalitsoChipangula-i3z
    @MadalitsoChipangula-i3z Před měsícem

    Mwana uvuta kwambiri the Dc zimenezi ndizo zofunika kwambiri kunokwanthu kumalawi

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 Před měsícem

    More fire bon

  • @jamessingini-fh1bz
    @jamessingini-fh1bz Před měsícem

    I cant wait pa 8 August ,bravo team Dc❤

  • @JohnBanda-ux9fy
    @JohnBanda-ux9fy Před měsícem +2

    The DC ❤❤

  • @ChikondiMaguza
    @ChikondiMaguza Před měsícem

    Am coming to join u guyz❤

  • @TachikoMwanamanga
    @TachikoMwanamanga Před měsícem +1

    The DC 🔥🔥❤️

  • @OMEXTWAIBU
    @OMEXTWAIBU Před měsícem +1

    Chakwela my vote ❤

  • @HiAlvin
    @HiAlvin Před měsícem +2

    DC awavula Ngati anadya ndalama akabweze alephera kufusa

  • @RasLuntha
    @RasLuntha Před 28 dny

    We must fight for our rebarty and freedom

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb Před měsícem +2

    Mafunso onse ayankhidwa, what else do u want?

  • @TanazioUziyele
    @TanazioUziyele Před měsícem +2

    Aaa akalindo ndale

  • @Atheeeefire
    @Atheeeefire Před měsícem

    Respect the DC keep the fire burning

  • @user-eo2hl9ug1h
    @user-eo2hl9ug1h Před měsícem +1

    Muyende..bwino...Isha. Allah

  • @COSMASSDAVITY
    @COSMASSDAVITY Před měsícem

    D.C MWANA OVUTA NDIWE NYO😂❤

  • @MercyJohnsonkanchure
    @MercyJohnsonkanchure Před měsícem +2

    Mr DC ulemu wanu kuti yimilira Amalawi

  • @evalisterphiri8435
    @evalisterphiri8435 Před měsícem

    This is true, ma profit ndiochepa kale koma BOMA ili palipose utulutse ndalama and now this mmm.... Mademo akufunikadi

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Před měsícem

    Komano bon kalindo wawayankha bwino.Lopanda nzeru ndiboma ndiutsogoleri omwe ulipoli.Pa 8 go konko

  • @user-sm4vo2uo7g
    @user-sm4vo2uo7g Před měsícem +3

    The dc mwana wachabe

  • @DanJohn-ws5gl
    @DanJohn-ws5gl Před měsícem +2

    Mbambande the DC

  • @user-oe3dz7dy4j
    @user-oe3dz7dy4j Před měsícem

    Zoona amacharger ndarama popereka chidindo,,, your true fighter kalindo

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c Před měsícem

    Born kalindo respect big up

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem

    Ife tikudikila pa 8 pano ✊💪✊

  • @serakillo8668
    @serakillo8668 Před měsícem

    Born ❤❤❤ ndi one guys timakufirani abro❤❤❤

  • @MagunjeNewa
    @MagunjeNewa Před měsícem

    Mr Born kalindo hoyeee

  • @user-ri8em6my2e
    @user-ri8em6my2e Před měsícem +1

    Bon tiwomboleni asatana amenewa asatibere chonde 😭😭

  • @user-pe2tu1ip3v
    @user-pe2tu1ip3v Před měsícem

    Good news ❤good work

  • @WillmotChiuimia-vr6ou
    @WillmotChiuimia-vr6ou Před měsícem

    Yes , kuyankha kwabwino ndinthu mmm ndikanapanga nawo mademo amenewo yes yes

  • @user-dk6yc8pl2m
    @user-dk6yc8pl2m Před měsícem

    The DC ❤❤❤❤❤

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před měsícem +1

    Mulungu akusungeni ndi moyo gays wina aliyese ukumba zenje pa inuyo agwelemo yekha mudzina la yesu

  • @RobertChisenga-ci2mq
    @RobertChisenga-ci2mq Před měsícem

    I wish bon kalindo azakhere minister of the land
    Kaya zikhare ng,oma mai yolam kukuyu
    Azakhara mwaufumu muno kaya.

  • @heartilygarven2624
    @heartilygarven2624 Před měsícem

    Ulemu wanu Mr DC kuyankha mopanda nkhawa

  • @estherkachingwe3605
    @estherkachingwe3605 Před měsícem

    God bless you Mr Bon kalindo

  • @PeterChuma-jr1vz
    @PeterChuma-jr1vz Před měsícem

    Atolankhani agonja kunooo kkkk kuyankha mosaopa

  • @AgnessKavalo
    @AgnessKavalo Před měsícem

    Kkkk komatu bon kalindo amathamanga ali mu suit 😂😂😂😂😂😂😂 koma mdaseka mokweza mau 😂😂😂

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Před měsícem

    The DC president wa anthu osawuka 💪✊ we always with you

  • @smartselemani2070
    @smartselemani2070 Před měsícem

    Sweet talk with hidden agenda.

  • @InnocentMtafya
    @InnocentMtafya Před měsícem

    Ambwiyee !!! Mafunso afunsidwa ndimayembekezela zachabe ,koma ambwiyeee!!!

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h Před měsícem

    KATUNDU BOOOOOOOOON KALIIIIIIINDOOOOOOOOO LOVE YOU MY GUY

  • @GladsonBanda-m3e
    @GladsonBanda-m3e Před měsícem +1

    Apresitent chamba chilitho nkumati tikuimira anthu kumangadi zingongo you should read as an example kalindo

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před měsícem

    Atolankhani aku malawi ndi mbola, amafunsa zopepera kwambiri.
    Utolankhani weni weni unapita ndi achina Eunice Chipangula osati izi zathovwa.

  • @Agin2pex-ms3di
    @Agin2pex-ms3di Před měsícem +1

    Buka matevu 🎉

  • @IanAllstal
    @IanAllstal Před měsícem

    Kodi kalindo umkachedwa ndi ma drama chifukwa chani? The D C 🔥🔥🔥

  • @macksonmkandawire5718
    @macksonmkandawire5718 Před 10 dny

    Bon kalindo kkkk make ndi vice president sopano

  • @user-ii6lu1wy5f
    @user-ii6lu1wy5f Před měsícem

    We are with you Mr DC

  • @GreenBadani
    @GreenBadani Před měsícem +2

    💪👍💞

  • @innocentmusuli7380
    @innocentmusuli7380 Před měsícem

    Mongo bwereza zomwe ndakhala ndikunena kuti any time, any day, any week, any month from now achinyamata azuka ndikuchosa nyasi zonse belive this

  • @MaloneBanda
    @MaloneBanda Před měsícem +4

    Good work 💥💥💥💥

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Před měsícem

    Akalindo ayaluka mademowo kumwela Koko

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z Před měsícem

    Achina kalindo ndiakamuna osati masewela.

  • @isaacharoon5652
    @isaacharoon5652 Před měsícem

    Kalindo akuchita bwino,komano kwa anthu amene amaononga zinthu za anthu,inuyo a kalindo anthuo muzawalipila,chifukwa anthu akuba amalowelela.simutisaukisaaaaaa?

  • @ziyamporoma377
    @ziyamporoma377 Před měsícem

    Chokani apa inu mulibe strategy iliyonse other than mademo.
    Don’t worry tikakufinyani konko

  • @MarthaBango
    @MarthaBango Před měsícem

    😂😂😂😂😂iiIi ati masuti kothamanga😂😂

  • @DoulassSamuel
    @DoulassSamuel Před měsícem

    Iweyo born ukungofuna udindo usatinyasepoapa

  • @LucyTatianahChikwekwe
    @LucyTatianahChikwekwe Před měsícem

    More fire 🔥🔥🔥 the DC

  • @TANMBWANA
    @TANMBWANA Před měsícem +1

    Mr chikangawa zawavuta

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před měsícem +1

    Dc 🔥🔥🔥

  • @MarthaMalopa-kw9xw
    @MarthaMalopa-kw9xw Před měsícem +1

    Pali funso lomwe lalepheredwa kuyankhidwa apa?