Kamlepo Kalua wayankhura mosaopa ndipo iye Wati wamvaso kuti they’re planning to kill his son

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 7. 09. 2024

Komentáře • 165

  • @AlbertEngelbercht
    @AlbertEngelbercht Před měsícem +28

    Mwachitamakola kuwaphalila unenesyo, chiuta wamusungeni dada kamulepo,we are In democracy time!!!!.

    • @user-dp9uy6qt7x
      @user-dp9uy6qt7x Před měsícem +1

      Makolawaka 😊kwalinamwe manda
      6 jjjjjoo9ooj .0pll0
      V

  • @petermanMitambo
    @petermanMitambo Před měsícem +11

    Very powerful speech.long live Mr KALUA. may God protect you from these heartless swines

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Před měsícem +10

    Good massage Mr u are the strongest man

  • @georgemsowoya6525
    @georgemsowoya6525 Před měsícem +4

    Mcp pamoz ndi achakwera achepa there days are numbered....live long dad kaluwa and much love to fredo kiss ,,, I speak divinely protection in that family ,God be with you

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Před měsícem +3

    Mr kamlepo kaluwa one of the greatest politician in Malawi u fought for democracy MCP is getting us backwards to dictatorship arresting and killing innocent people this is not what the voters wanted.

  • @PrinceernestBorniface-x1m
    @PrinceernestBorniface-x1m Před měsícem +6

    Apolisiwo ndi chakwela onse machende awo fotsek...

  • @MosesKalenge
    @MosesKalenge Před měsícem +2

    Powerful massage bwana Mr KALUA ❤🎉🎉🎉

  • @normantondole2669
    @normantondole2669 Před měsícem +4

    Why not taking them (police) to court Mr Kalua?

  • @JailosGazahBoica
    @JailosGazahBoica Před měsícem +4

    My Land 😢😢😢our warm heart of Africa 😢😢😢😢our peace,joy and harmony county has turned into Sodom and Gomorrah 😢😢😢😢

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Před měsícem +8

    I support kamlepo munthu wa mkulu kwambiri mumakwanila.

  • @MadalitsoMalamba
    @MadalitsoMalamba Před měsícem +6

    MCP makolo amkatiuza kuti ndi chipani chakupha ndiye tikutha kuonadi and I don't think wachinyamata ozindikira bwino mkumakaponyera vote MCP....

  • @CliftonMaseya
    @CliftonMaseya Před měsícem +9

    Mvamvekatu ma words umu 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @brightsonsaidi
    @brightsonsaidi Před měsícem +2

    Pls bring out the CCTV footage here, ASAP. It will have a heavy impact on people's minds

  • @MikeMerecah
    @MikeMerecah Před měsícem +2

    Konwani kamponje ndiwe opusa kwabasi ukuona ngati kamlepo kalua ndi size yako, Bwana my God protect your family,,,,,,,,

  • @StevenTembo-mb7rm
    @StevenTembo-mb7rm Před měsícem +2

    Well said I hope pala ni wanthu wa umunthu wawo wapulika and if they may attempt to kill Fredo this country will go beyond what happened in Kenya. We are ready

  • @unitelectronicmedia4581
    @unitelectronicmedia4581 Před měsícem +3

    This man is loaded!
    Wati ndigenda waponda MWALA

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj Před měsícem +2

    🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏🙏
    Father kamulepo kaluwa tili pambuyo panu

  • @FrancisMbewe-xn2pl
    @FrancisMbewe-xn2pl Před měsícem

    Powerful Papa ❤ palibe wamuyaya tonse tizafa bas

  • @alicegama8138
    @alicegama8138 Před měsícem +2

    Apo ndipo wamanya kuti watumbuka wokhumba yay kuwaseweleska

  • @user-wf8xm3km3s
    @user-wf8xm3km3s Před měsícem +2

    What a powerful message

  • @shaffiejumah6385
    @shaffiejumah6385 Před měsícem

    We respect you mr kalua we leant alot and we still learning much love...

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Před měsícem +1

    Ayiwala zoti achoka pampando, shame on you. May God be with you Kamlepo

  • @samchibenene4458
    @samchibenene4458 Před měsícem +1

    God is great be safe and your family Mr kamulepo

  • @WillamChihana
    @WillamChihana Před měsícem +2

    Mwayowoya bwana ndipo nakondwa nazo fundo zino zose chiuta wakuona vose

  • @JuliusChamwanje
    @JuliusChamwanje Před měsícem +3

    History we learn alot

  • @tamandaninampinga
    @tamandaninampinga Před měsícem +1

    Thanks dada for the message

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw Před měsícem +2

    Good massage kalua

  • @PrinceThom-pe6ie
    @PrinceThom-pe6ie Před měsícem +2

    Don't worry dad 2025 mcp police tizayikhaulisa

  • @PrinceernestBorniface-x1m
    @PrinceernestBorniface-x1m Před měsícem +2

    This is very stupid insane 😠... Chakwela should resign galu wachabechabe

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Před měsícem +9

    WE LOVE U KAMLEPO...MCP YIKUTULUKA M'BOMA CHAKA CHA MAWA...

  • @johnmponda9070
    @johnmponda9070 Před měsícem +1

    Oh my God Malawi police and Malawi defence force are just used they don't even know what they responsibility is really shame on them

  • @user-vf2fo1mb2c
    @user-vf2fo1mb2c Před měsícem

    Yebo mwawanthu, don't touch Tumbuka people, we believe in Jesus

  • @user-ex7jn2fh1g
    @user-ex7jn2fh1g Před měsícem +1

    I love the the guy

  • @SolokingChimzy-yt7dj
    @SolokingChimzy-yt7dj Před měsícem +3

    Ndikukaika ngt anthu afike nthaw yovota bwinobwino ..zikundionekela ngat mavote azizizi akhoza kuchitika mu Mziko muno...

  • @augustMag
    @augustMag Před měsícem +1

    Mmmmm koma abale mpaka kukuonongerani zinthu mnyumba abweze katundu ameneyo

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem +2

    Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa ❤ Chakwela you mast go watikwana

  • @user-so7wg6ii5m
    @user-so7wg6ii5m Před měsícem +4

    Message ya mphamvu ❤

  • @HendrixGrem
    @HendrixGrem Před měsícem

    Wise speech Honourable

  • @user-ro1pl7rv7z
    @user-ro1pl7rv7z Před měsícem +1

    *Amtumile mwenye* kwabasi nambo ngadandaula Mcp chipani changalumbana Ata panondi.

  • @FrancisMbewe-xn2pl
    @FrancisMbewe-xn2pl Před měsícem

    We fear God not person 💪🔥

  • @lumbaninyirenda8223
    @lumbaninyirenda8223 Před měsícem +2

    kumpoto MCP kulibe vote

  • @ElemiahKavute
    @ElemiahKavute Před měsícem +1

    Mupheni kkkkkkk andale amwene 🤣🤣🤣🙌 atitu enawo anyumwe kkkk muphenitu akamlepo akusendeno muone

  • @AbdulSelemen-q5j
    @AbdulSelemen-q5j Před měsícem

    Osaopa osaopa palibe wambewu padziko pano, ndipo kalikonso kazalawa imfa.

  • @wonganikaunda
    @wonganikaunda Před měsícem +2

    Mukapha uyu nde muyalukatu poyerayera

  • @zayedmitawa8345
    @zayedmitawa8345 Před měsícem

    Andale amafuna kukhala pa mpando forever yet amapanga zoononga mu nthawi yochepa
    I don't understand then at all.
    Being good will not make you lose anything at all but being bad eeeh ndi izi za cheucheuzi

  • @JailosGazahBoica
    @JailosGazahBoica Před měsícem

    May God protect you and your family

  • @natashamathala8715
    @natashamathala8715 Před měsícem +6

    Koma nde mwangoti 3stars apa pali nkhani apa tiuzeni zambili bwanaaa

  • @VincentTembenu-ip5ii
    @VincentTembenu-ip5ii Před měsícem +1

    Mmm mpaka I know akumidima omwe mumadalila 2025 Kuli ntchito

  • @KateRose-sh8zl
    @KateRose-sh8zl Před měsícem +1

    Pathu sipadziko zoona but the voters are suffering bwana

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo Před měsícem

    Kuyankhula kwabwino uku, nawo apolice alibe nzeru angowagwiritsa ntchito malipiro ochepa km kumangozunza anthu

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před měsícem

    Mmmm nde afika posausano... Kupha bas!!!!! Eeee why Malawi now

  • @user-cx5hh8yf5h
    @user-cx5hh8yf5h Před měsícem +1

    😂 koma kwachema osapanga mantha aonese

  • @glynbulambo
    @glynbulambo Před měsícem +1

    Mwana wamupoka wayoghoya wa chewa mfela za Eni 😅

  • @kidneyblessingschilinguloj7292

    Rise up Kamlepo we want peace

  • @FiskaniTonymahone-vl3og
    @FiskaniTonymahone-vl3og Před měsícem

    Chakwera, don't know,do good, be good, live good, he's no good..

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem +1

    Tavuka na mcp onse wa mcp mavi yao (komaso inu akamulepo mukufoila kwambili mr kalua u sleep too much

  • @zaitwazaitwa941
    @zaitwazaitwa941 Před měsícem +1

    Koma ndiye Kwachema

  • @Amunandife3212
    @Amunandife3212 Před měsícem

    Ing'aluleni bwana Kaluwa,,,,,,,,,,,,

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim Před měsícem +6

    Chitukuko chA razalo ndikupha basi

    • @user-tk6qh9zs7h
      @user-tk6qh9zs7h Před měsícem

      Ngati muja Chinalilinso Chitukuko Cha Peter Mutharika pakupha Issah Twaib Njaujyu, Buleya, Masambuka, Tambala Family kutchulapo chabe ochepa

    • @isaacpelani
      @isaacpelani Před měsícem

      ​@@user-tk6qh9zs7hmuli m'bomatu. Tengerani umboniwu kukhoti tidziwe zoona zenizeni. Mwina munkapha ndinu kuti muipise mbiri yaamnzanu

    • @LukaThawe
      @LukaThawe Před měsícem

      Yah ndimakape

  • @BenjaminMoffat
    @BenjaminMoffat Před měsícem

    big boy ting set

  • @Amunandife3212
    @Amunandife3212 Před měsícem

    Leader

  • @RABSONChisambi
    @RABSONChisambi Před měsícem

    30:24 my God protect you kamulepo and your family ilike what you saying

  • @HawaiijeminieHawaii
    @HawaiijeminieHawaii Před měsícem

    Fact

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj Před měsícem

    We love you Kamulepo Kaluwa

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Před měsícem

    Achilundi samalani, msaone ngati mwafika. Lindani madzi achilundi apite nde mziti mwadala, nzosiilanatu izi osasimbwa.

  • @MagretMvula
    @MagretMvula Před měsícem +1

    Dadi apa mwafikapo muuzeni zoonaasiye chibwanamooto uyake asazolowele

  • @IsaacTsinde
    @IsaacTsinde Před měsícem

    Mwayankhula abwana

  • @MuhammadBAKILI-kl2mj
    @MuhammadBAKILI-kl2mj Před měsícem

    Kamulepo kaluwa mumatiyomilira munatsala nokha (RIP chakufwa chihana)

  • @emanuelnziza1193
    @emanuelnziza1193 Před měsícem

    Awawa ngat ali mau awodi. Aah the Man must be suspected sure

  • @chifundochimenya6368
    @chifundochimenya6368 Před měsícem

    😢 indeed this world it's not our home am crying Malawi

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb Před měsícem +1

    Afa okha

  • @user-bm1sf4sk1p
    @user-bm1sf4sk1p Před měsícem

    Powerful

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg Před měsícem

    With heavy heart

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Před měsícem

    Akapha mwana inunso tiyeni tikaphe awo.
    Ofunika kuyamba kubwenzera. Zatopetsa.
    Athuwa akufuta chifukwa amalawi sabwenzera.

  • @GibsonLackson
    @GibsonLackson Před měsícem

    Ayelekeze 😳😳😳😳

  • @MussahWilliam-py1ff
    @MussahWilliam-py1ff Před měsícem

    Koma ndalama mani mmmmmh ay ndinthu mmmh anthuwa guyz samagona muja tigonera enafe

  • @ednakaluwa5414
    @ednakaluwa5414 Před měsícem

    Hon kaluwa🔥🔥🔥🔥

  • @OwenMajoni-qv3eg
    @OwenMajoni-qv3eg Před měsícem

    Osapita ku khothi bwanji a Kalua? Komanso ndalama zanga simunabwenze kuchoka 2019 paka lero mumaganiza bwanji bwana Kalua? Koma umunthu mulinawo?

  • @SydneyChiphaka
    @SydneyChiphaka Před měsícem

    Why Mr Kamulepo want to kill his own son? Sad

  • @KhumboZimba-x1z
    @KhumboZimba-x1z Před měsícem

    Mawu amphamvu kwambiri chakwerayo ngati kulikumva wamva dziko ndilizungulira

  • @JoyMpinga
    @JoyMpinga Před měsícem

    Ntchana asamuyese ghetto azaimva

  • @MirajLaja
    @MirajLaja Před měsícem

    Za phone iwalani asiyileni ikhale yawoo...

  • @kelvinedson685
    @kelvinedson685 Před měsícem

    That's fact's indeed

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Před měsícem +1

    Ndipo ndizoonadi zamawa siziziwika

  • @JaxyKumwenda
    @JaxyKumwenda Před měsícem

    Munthu wamkulu wayankhura❤

  • @MacdonaldMisomali-lt4wu
    @MacdonaldMisomali-lt4wu Před měsícem

    Aphe fredo awone

  • @ShakiraOsman-e8g
    @ShakiraOsman-e8g Před měsícem

    Komanso katundu anaonongayo abweze

  • @DavidMtambo-zm8ne
    @DavidMtambo-zm8ne Před měsícem

    Nabo bafwenge bachakwera kulije wamuyaya

  • @AustinBornface
    @AustinBornface Před měsícem +3

    Tili mukati mweni mweni

  • @prettytambala5687
    @prettytambala5687 Před měsícem

    Muzazisumire zimbava izi zidzakulipireni hiyaaaaa

  • @user-vj6jt2df3e
    @user-vj6jt2df3e Před měsícem

    Mwamuyambapo kaluwa amayabwatu chwe mwana chwe

  • @giftwisdom-km7yh
    @giftwisdom-km7yh Před měsícem

    Mwachita makola mwawa phalila unenesho.
    Chiuta wakudangirileni.

  • @ellenchipula9809
    @ellenchipula9809 Před měsícem

    Chakwera pa m’tongo pa mako

  • @user-un4pm4yt5i
    @user-un4pm4yt5i Před měsícem

    Koma ndiye ndinthawiso yakamuzutu aaa

  • @TadalaMaumbo
    @TadalaMaumbo Před měsícem

    I support you

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem +1

    Mukapusa amupha

  • @MassaukoKintu-k7s
    @MassaukoKintu-k7s Před měsícem

    Following

  • @FRANKCHIFUNIRO-c6h
    @FRANKCHIFUNIRO-c6h Před měsícem +1

    28:52

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 Před měsícem

    Koma z..ikoli ...Amwene

  • @HestingsJamu
    @HestingsJamu Před měsícem

    Our MDF and All police officers chomwe mukidziwa kumvela/kulamulidwa basi? So many things are happening in our country but why are you just watching? That's why every president chooses his own leaders in all angles right? As a real soldiers, show us kuti munasankhidwadi mwanzelu. Kapena chomwe mumadziwa kumangolandila ma order okasaka mbewa not so? Taphani wina tione ngati kadziko kathuko sikakhetsedwa mwadzi. Za ziiiiiiiiiiii