Za wulurika zoti Chakwera Ndi Gulu lake ada mverana Ndi ma Israel agwetse ndenge muda kwera Chilima Ndipo ada Chita kuwa ombera nkuwa maliza mowatema nchi kwanje, Chakwera Yehova wolenga zonse amudalitse Ndipo wamvetsa manyazi mulengi wolenga Zonse koma Yesu adati wakupha ndilu panga nayenso azafa ndilu panga masiku achepe achuluke Chakwera azafa monga m'mene ada phera Wanthu amene adafa kuchi kangawa
Amen Abusa mwalankhula ndi moyo wanga. Funso langa Likupita kwa Chakwera ndi Monica…Kodi kuti mukhale pamene mulipo tsiku lalero chifukwa cha ndani? Kodi kupanda Chilima bwenzi Uli president? Kodi achina zikhale Ngoma kuti azikhala a position yomwe alinchifukwa cha ndani? Kodi ukanakhala kuti sunawine bwenzi aliposition yomwe Ali? Chikondi ulibwanji zikhale ngoma ndi a nzake at abwera ndi nfundo yokhupha chilimaukanawalesaa pokumbukukira zimene chilima anakuchitira. Munthu oipa okupha koma u call urself aman of God Monica ndiiwe Jezebel amupha munthu Kamba ka malo ake omwe. Muli ndi Tsoka
Achimwene zaziko lapansi nzosata,zisiyeni mulandile yesu pakuti palibe ngakale omozdi oziwa siku lake,satana asakuumiseni mtima,mwa yesu muli mtendele,amen pastor
Achitireni chifundo pakuti sakudziwa chomwe akuchita...mau onsewa mukumupasa Chakwera wa olo asazawinenso koma tsiku uzawafuna koma osawapeza samala bale ikudza thawi ndipo sikale ndipo palibe dziko lapasi kusitha kulikonse komwe tidzakuwone popanda kuchirimika pa wekha...chisoni chikumandipeza Maka kwa ana Ang'ono amene mutenga gawo lovala matemberero pa mau a Mulungu...koma ngati inuyo muli oyera kwa thuthu ndimawona ngati ndinu amene mungaliyike dziko li pabwino chifukwa Mulungu siwamasewera...ndipo sapanga nawo za tchezerazo... komanso amene akukutumaniwo ana awo anachita bwino kale ena Ali Kumaiko akunja koma Inu ndi ine mmmmmm busy kumangoyakhulapo..tayeserani kupanga zanu muone zimene Mulungu akuchitireni Ambuye akuthandizeni
Za wulurika zoti Chakwera Ndi Gulu lake ada mverana Ndi ma Israel agwetse ndenge muda kwera Chilima Ndipo ada Chita kuwa ombera nkuwa maliza mowatema nchi kwanje, Chakwera Yehova wolenga zonse amudalitse Ndipo wamvetsa manyazi mulengi wolenga Zonse koma Yesu adati wakupha ndilu panga nayenso azafa ndilu panga masiku achepe achuluke Chakwera azafa monga m'mene ada phera Wanthu amene adafa kuchi kangawa
😭😭😭😭
Koma Malawi😮
Chakwera wakupha,ndipo mulungu amukanthamula, power message 🙏🙏🙏🙏 May bless this word
Ndine msilamu Koma ulaliki iwuwu mmmm muli utenga wabwino moti inetso wandikuza kwambili. Ndipo ndaphuzira zambiri.ndipo ngati Chekwera anali m'busa wachoonadi ulaliki uwu awugwilize ntchito 😢😢
Mbusa oipa palibe wamvapo
Ndiye chakwela akupha anthu omwe sanamulakwire mulungu amulange ndithu
Wakhutu wamva
Powerful msg
Straight from God
Powerful
Ndipo zoona
Ulaliki uwu ngat Ali ndi nzelu munthu umasintha machitudwe akee ndikuona kut zikolino anthu akut chaniii
Ameeen abusa uthengawu ogunda mtima kwabasi .... koma tipemphe chimodzi nyimbo ikuimba pansi pansiyoo ikulakwitsa ojambulanu plz muzadzaikenso tikamavera ulaliki
Ulaliki wabwino km nyimbo imenei ndadana naye opangayo
@@DuncanDestiny Ndimaona ngati ndilindekha amene ndadana ndikanyimbo kaoko bola kakadakhala ka uzimu.... coz moti tinvetsele ulaliki tikunvetsela kanyimboko kaye kuti kakuti chani Mwaona? Pena ngati kaja amaika mma filimu osakhala bwino ... hope sadziikaso kanyimboko tikuwafunila zabwino zonse potipatsa ma program
❤❤❤ ulaliki uyu mwayankhula ndi moyo Dr chikangawa akwiya osaseka olo kuyankha mpaka azikanda posayamba ....Amen abusa chakwera koma.wamva bwino bwino ulalikiwu ndi wako kufuna zako osabwerako ...😭😭 rest in peace chilima...pano chakwera alimbe mwedzi ❤❤❤ abuse ambuye andalise uthengawu Amen
Amen apo chakwera akumva Koma akuonangati dziko likuyenda
🤣🤣🤣🤣🤣akuti eti
Truth n worthy preaching, Amen
Amen Abusa mwalankhula ndi moyo wanga.
Funso langa Likupita kwa Chakwera ndi Monica…Kodi kuti mukhale pamene mulipo tsiku lalero chifukwa cha ndani?
Kodi kupanda Chilima bwenzi Uli president?
Kodi achina zikhale Ngoma kuti azikhala a position yomwe alinchifukwa cha ndani?
Kodi ukanakhala kuti sunawine bwenzi aliposition yomwe Ali?
Chikondi ulibwanji zikhale ngoma ndi a nzake at abwera ndi nfundo yokhupha chilimaukanawalesaa pokumbukukira zimene chilima anakuchitira.
Munthu oipa okupha koma u call urself aman of God
Monica ndiiwe Jezebel amupha munthu Kamba ka malo ake omwe.
Muli ndi Tsoka
❤ eti osatsutsana eeee
Muoneni maso ake ngati chikangawa chakwera yu
Apule mudakapuma Kaye kumatchilitchi enawa, kodi yanu ija mudatseka, chifukwatu kwinaku akukudzudzulani mulaliki, ndiyesa mukudzimvera 😮
😂😂😂😂
@@MisheckAselo Zonse ndi Nthawi dzidikira nyengo, Mulungu amaona zonse, Amen
@@fradrickMuvula Ndipo sagona satopa sapumula ndiye mulungu ameneo 🙏
Kodi president akukangalika kumapita ma church akuona ngati a zibusa sakuona momwe a Malawi akudusila munyengo zowawa ndi MCP....😅😅😅😅
Wabalalika komanso akufuna kuziphimba ngt ndi khritu ndipo sanakonze nawo chiwembu....ati tiiwale tiziti ndiwabwino iyeyu
❤ exactly my question,akuzivutisiranji pilizi,ndendiiyo maulaliki akungopherezera iyetu zovesa chisoni Zochititsa shame.
Chikangawa anali dendekere ngati akumva
Abusa mwafutsa bwino kuti chikangawayo anamulakwira chani chilima?
BRAVO my uncle kuima pa chilungamo osaopa. Uncle amwana makwana🎉🎉
Achimwene zaziko lapansi nzosata,zisiyeni mulandile yesu pakuti palibe ngakale omozdi oziwa siku lake,satana asakuumiseni mtima,mwa yesu muli mtendele,amen pastor
Tamuuze chakwera akuchita manyadzi akuopa kunthawa yemweyo galuiwe
Power messeg...God bless u pastor
Wise advice to Mr President. Thank you man of God. I am sure Mr President was strengthened in fight for the National unity
Amen abusa umeneu umatchedwa udani opasirana imwe akazi anga amalalika dairly kuti udan opasirana Ido very very dangerious ndipo ilo maubale amavuta kwambiri thank you pastor
Kuseli pa unai wawo akupangana kuti akupangire chiwembu.
Some one told me that when the gospel is coming take it as God is speaking to your own life not to some one
❤❤ Ambuye Mulungu akudalitseni pofukula malemba ngati awa, ndipo ndaona bwino kuti a Chakwela ndiozindikila pa zinazake iwo anachita polimbana ndi akapolo a Mulungu. Mulungu sanyozeka kapena coloration, Tsoka limafika tsiku la Mulungu lowawa!!!
M'busa uyu amalalikira hvy Shalom pastor
Chakwera Nzeru ulibe ndithu ntima wako oopanda chifundo unapherani chilima? Unaputa nkwiyo wa Mulungu unapangiranji zimenezi? Mulungu yekha akudziwa za mkati mwako continue Rest well Chilima 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
God bless you man of God
AMEN....DZIKO LIMANYENGA! TIYENI TAZILAMBIRA MULUNGU MOWOONA. AMBUYE AZITIDALITSA.
❤ powerful gospel
Ambuye yekha azudalitsani chifukwa cha mau awa,Amen
Uthenga wamphamvu uwu chakwera ngati uli nawo Mzimu wa Mulungu udziwe chimene Nzimu Woyera akulakhura ndi iwe Abusa Ambuye akudalitseni koposa uthenga wamphamvu uwu 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌😳
Azibusa oyima pa chilungamo osati kumangodya ndalama ayi lalikilani dziko limve
Ifetu chilima sitikaziwa kuti amapita Ku church. Tinaziwa atapitati or tsiku lofela kuti amapita Ku church asembe ananenatu, lelo zikutani nanga
@@AliceChipeta-pc3nbmutichani kodi inu
Mposoo
It's my testimony God bless you pastor 🙏
Kkkkkkkk mkudzachita chomudzidzimukila Amen"yo😂😂
😂😂😂😂😂 Afuna athawe
A great representation of a man of God........May God Bless you
Powerful preaching Man of God 🙏
Ameeeeern limbani mtima achakwela adani a.ene muli nawo inuyo simnapunep amen
Chakwera anapha Chilima palibe kupuma ameneu kumatako kwake kukutetha moto
A limbe mtima ndani
chakwera wake utiiiiiiiiiiiiiiiiii haha mfitiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii
😂😂😂😂😂😂
Kupempha kupasa usiru umangoombela m'manja zilizose
Powerful message
Go deeper man of God
Akulu akulu ng.oma yokweza mawu sichedwa kusweka perekani miyezi iwili wina wake abwela poyera kunena zaifa ya skc mnzimu wa skc ulipo
Inetu nduvomerezana Nanu.
Miyezi iwiri wina apenga misala
Kamveleni limpopo uku zilikotu ziliko
Amen power message Ali ND khutu anve God bless u pastor
Powerful prayer 🙏🙏🙏🙏
Amen unthengs wamphamvu
Amen powerful massage from above
Ulaliki wochokera ka Mulungu.... Nzeru
Ican even see Chakwera showing his sympathetic nerve by looking at the pastor
Powerful message my pastor
Amen amen ndipo chakwela ngt alindi nzeru watengapo phunziro
Powerful lecture!!!!!!
Uthenga wamphamvu mulungu akudalitsen Abusa
Amen abusa Chirwa uthenga wanu wandilimbikisa kwambiri👏👏👏
My Advice to the President ,bwelelani mmanja mwa Mulungu ,zadziko ndidzosala ,ndinu mtumiki kapitilizéni utumiki
Powerful massage ❤
Abusa.Ngakhale mwameta mbali komabe lalikilani ndithu za nyengo
😂😂😂
Kkkkkk
Abusa awa akulirikira bwino. Sakularikira monyoza a president. Ukundiyekusamvetsetsa ulaliki.
Why is Chakwera busy visiting Churches and mosques??? He must stop testing God,,,
Nanga choti mangaya alikut anakamva nawonso uthengawu😢😢
Koma abusawa akuluwika mbavayi tuuuuuuu
Zoona abusawa alarikira mu njira Ina yoti wakumva bwino aziwapo chomwe akutanthauza koma mulungu dalisani malawi ndiposo invani mapemphero athu
Sound yanuyo (background) ikumasokoneza .......ndipo mukanaichosa
2❤ZA1ZZZ
Amen , amazing message
Chakwera samva
Mizimu yonse ikumampeza ameneyo that's why akuenda ma church tsiku lina adzafuna mamasulidwe a Mulungu uyo miximu inachuluka ya anthu
Misonzi yomulilira chilima ndi nyengo chabe. Tiyeni tithamangire kwa Yehova atiuze tivote motani. Tingayambe kuvotera amaleki
Amen amen tsikulina mulungu azayankha ❤❤❤
Koma ngati mizimu yakuchikangawa ija ena sapenga misala, ndiye kuti Malawi zoti chaka cha mmawa tizavotaso zimenezo tiiwale, cz Mulungu akutiyankhula ndithu kupyolera mwa anthu ochuluka
Powerful man of God
David sanali oti ine mdzaimanso atapangana Zina ndi Jonathan anali osunga pangano that's why zake zimatheka
Abusa mukaweluka mukawelenge YEREMIA 9 vs 25_26 pali nkhani yanu
Amen 😂😂😂 akaziwerengered
Amen abusa preach on
Mai chikangawa muziwauza zanzeru amuna anuwo osamangokonda ndalama ai muli ndwiiiiii ngati akugwilani nyanga
Abusa ometa mbali😢😢😢
Zanyengo
Chakwera akanagovomereza, mawuwo akuchoka kwamulungu
Strong words
Amen pastor 🙏🏾🙏🏾🙏🏾🙏🏾 mau mau
😂😂😂😂 ulaliki uwu wandigwira mtima pastor amen
Amen amen chakwela mukuvwa bwanji kumeneko
Amen n amen
Who is this man of God
Powerful
Chakwera my vote basi
chakwera chilima anakulakwira chani 😢😢😢
Kodi mpaka mukulephela kutabwanya iPad 😂😂😂
Chikuyankhuladi chi chakwera kuti "mdani ameneyo alipo"lol 🤣iweyoka
NThawi zonse tiava mau AMULUNGU timayenela kuwava kuti MULUNGU akulankhula ndine, ukapeleka kwawina umachoka opanda kathu,ndilimbikitsa
Ulaliki uwu ukanamupeza skc chilima mwina bwezi chakwela sanakwanise kumupha ndithu
Ngat abusa akumeta mbalimbali ine ndindan kut ndisamete😂😂😂
Age ndi kumeta osagwirizana kusonyeza kuti za UBusa zinangogweramo
Abusa osadziwa kuwopa ndikutsali Mulungu
Sangalalike zachowonadi
M'busa onyenga ma. Metedwe atiuza
😂
@@user-jn9tz3li3v😂😂😂😂
Amen🙏🙏🙏🙏🙏
Amen
Koma mkaz wa Chakwera ndiy ndinkhwangwatu....ndalama alinazo akudya koma ngat wakumudzi mmmmm zinqngokumana amenewa akuoneka kut amkauluka(ufiti) amenewa
Chapapiyo wazibera yekha zufunika kulapa kt tikloe ufumu wakumwamba
Mulungu wathu ndiwowona tikulira mulungu tiomboleni
Nyengo zapa 10june,24.kumalawi stdzaiwala mpakana Mulungu atactapo ukulu wake
Ameni abusa mwayankhula moyo wanga
😭😭😭🤣🤣🤣 mmmm nzaulendo uno abusa nampaka kumeta mmbali kkkkk
Amen uthenga wamphamvu uwu
Achitireni chifundo pakuti sakudziwa chomwe akuchita...mau onsewa mukumupasa Chakwera wa olo asazawinenso koma tsiku uzawafuna koma osawapeza samala bale ikudza thawi ndipo sikale ndipo palibe dziko lapasi kusitha kulikonse komwe tidzakuwone popanda kuchirimika pa wekha...chisoni chikumandipeza Maka kwa ana Ang'ono amene mutenga gawo lovala matemberero pa mau a Mulungu...koma ngati inuyo muli oyera kwa thuthu ndimawona ngati ndinu amene mungaliyike dziko li pabwino chifukwa Mulungu siwamasewera...ndipo sapanga nawo za tchezerazo... komanso amene akukutumaniwo ana awo anachita bwino kale ena Ali Kumaiko akunja koma Inu ndi ine mmmmmm busy kumangoyakhulapo..tayeserani kupanga zanu muone zimene Mulungu akuchitireni Ambuye akuthandizeni
Good pastor
Powerful msg
Musiyeni wazierayekha ameneyo
Amen Chakwela wava
Kkkkk hallelujah yatulukauku yowasiyisa achakwera kugona
Ndipo live atuluka thukuta m'matako Chaka chino