Iweyo bvuto lako umadana ndi MCP, that's why ngakhale udzinena zoti zikumveka, wanthu a ku Malawi, they don't take you seriously. Bvuto lako, u are too obsessed with MCP
Remember, palibe chipani Cha ndale Cha ku Malawi chimene sichidaphe wanthu . Iwe mchawa nzanga , kwathu ku Malawi , amalamulira ndi aka tolika, ufune usafune, ife a Chawa, tilibe chance. Ngakhale ukuwe pa channel yakoyo, do you think Bakili Muluzi has got an impact? Ukunamatu iweyo
Akulu mukunama zikhale ngoma adzamwalire adzasiye dzikoli nanga udindo womwe ali adzamusiyira ndani zikhale ngoma ndi wamuyaya sadzafa namga ati adzikalandira ndalama kwakagame ndani zijhale ngoma nduna yamalawi yamuyaya mpaka yesu adzabwere
Koma zoti winiko amene akumumanga sichakwera koma zikhale ng'oma sizowona, zikhale ng'omayo ali pansi pa ulamuliro wa chakwera so chakwerayo ndi yemwe akumutuma ng'omayo.
Ndi chifukwa chiyani chakwera sakumuchotsa zikhale ngati ministry of homeland? Ukakwera pa msana pa njovu usamati pansi palibe mame, tsiku likubwera limene a zikhale mulungu azakulangani be warned
...on Bon Kalindo, I think he actuarrly challenges that he misses prison. We cannot defend people who call demonstrations out of political frustration and be paid by frustrated DPP. Kalindo has the bset interest on his stomach. 3 governments never gave him a position due to lack of education. But I also want to to mention that KZN is a savage. He was also involved in the 22 massacre and I would think he was an authority during Chasowa's murder. But even if it were Richard Chimwendo, or myself, I would make sure Kalindo is disciplined. The problem in Malawi cannot be fixed by burning, looting and marching by paying street kids.
I can't see your face but I can see mbali yako and you know what we are tired and sick with is so Called mcp that's why anthu sangaiware what they have done to our parents and nthawi achisiru, and they can not take us back thank you
@@user-ld1js7dt3b I am equally disappointed with MCP. BUt as poor by choice as we are, we cannot continue sitting on the streets. If Kalindo had a good plan, he would engage the industry captains to create employment than creating looters. We all know that MCP is incapable of turning the tide, we rather remove them in 2025. But we run the risk of worsening the situation by disturbing the already non-existent economy. By the way, currently in Malawi, there's no party that can govern. They are all gangsters and thieves. So creating a nation of looters will never solve any problem beyond 2025.
God is watching what MCP is doing and we are also watching, we have answers in 2025, may God continue taking care of our president, president for the poor
Big mumatiyankhulira zakhosi I hope uthengau umufika zikhale yo maonekedwe akeonso ngat wamkulu wa asing'anga
Ndizofunaka kwambiri kumaudza chilungamo tili munthawi yakuswa kuswa😂😂😂 BAMBO ZIKHALE
Powerful voice
Bring him back Bon kalindo the DC we want to see him walking freely in the Streets of Malawi
Koma abale chaaaaa kd zikhale ng,oma watan watching from mawalian
Ulemu wanu big man God bless you tikuziwa zambiri because of you
Following from Western Cape South Africa
Long live this channel 🎉
It's content that people love...keep it up Bro. We're learning more about your vids
Always you stand for us elder ❤Watching from Venezuela in Caracas 🇻🇪
Iweyo bvuto lako umadana ndi MCP, that's why ngakhale udzinena zoti zikumveka, wanthu a ku Malawi, they don't take you seriously. Bvuto lako, u are too obsessed with MCP
Remember, palibe chipani Cha ndale Cha ku Malawi chimene sichidaphe wanthu . Iwe mchawa nzanga , kwathu ku Malawi , amalamulira ndi aka tolika, ufune usafune, ife a Chawa, tilibe chance. Ngakhale ukuwe pa channel yakoyo, do you think Bakili Muluzi has got an impact? Ukunamatu iweyo
@@user-nj4ob8jw6y😢❤😢❤❤ ❤❤😮😮😮😮😮😮😮😮😮
Always you stand 4 us 💗💗💗🌏🌏
Ndpo muuzen zikhale ng'oma galu ameneyo watikwana
Keep on doing great job
Sad news about Kalindo
Akulu mukunama zikhale ngoma adzamwalire adzasiye dzikoli nanga udindo womwe ali adzamusiyira ndani zikhale ngoma ndi wamuyaya sadzafa namga ati adzikalandira ndalama kwakagame ndani zijhale ngoma nduna yamalawi yamuyaya mpaka yesu adzabwere
😢 Koma ul bhobho aise kk mutuwo sulbho hope so
How do you know history from moçambique ine nde moçambique ndipo zomwe ukunenazo zoona zokha-zokha livro De historia Vai contrar todos
Big up bro we r following you
Your the best
Uyu ndi kamuna
You are the best
We have been waiting for this boss
Big up broh, following
The best tv inded
Koma zoti winiko amene akumumanga sichakwera koma zikhale ng'oma sizowona, zikhale ng'omayo ali pansi pa ulamuliro wa chakwera so chakwerayo ndi yemwe akumutuma ng'omayo.
Zikhale ng'oma musiyeni azatha ndi anzake aku mcp omwewo ingotini phe mcp ndi mcp mnkango ukanyowa sikuti ndi kambuku ayi
Super voice
Thanks bro mumatiyimilila
Big love brother ❤❤❤
We love you too much ❤❤❤
Bulutu Chakwela Nyawuuuu Gule Wankulu masanziiiiiiiiii Enieni Bwantasaaaa,Walisaukitsa Dziko Lamalawi Mwalitenga anga Zakubanja Kwanu Agalu inu .Come 2025 Out and Jailed
Respect you big brother, keep it up. Watching you from muscat Oman.
Azikhale kumwamba kuli mulungu siku Lina mudzasowa chowilingula Bon kalindo ndi munthu osalakwa mukupangilanji? Zotele ndi moyo wake
Wishing you moyo wautali bro mumatimilila
Bon kalindo mmmmm alibe maso mphenya awo
Let's pray for Bon Kalindo
Atsogoleri ambiri a mu Africa sakalowa ufumu wakumwamba
Siku likubwela azamwalila ndithu kufuna osafuna
Zikhale ng'oma ndi wamuyaya sadzaona IfA komanso pampando pomwe alipo anayamba po ndiiyeyo sadzacoka zikhale ng'oma wasatanic nkhope ngati usiku wapha mabrund lero ukudzudza prezdent wathu chisiru kwambiri khope yoopsayo ngati mdima
Ulemu wanu mr
Ndi chifukwa chiyani chakwera sakumuchotsa zikhale ngati ministry of homeland? Ukakwera pa msana pa njovu usamati pansi palibe mame, tsiku likubwera limene a zikhale mulungu azakulangani be warned
Always respect u big
Atsogoleli a MCP onse ndimasatana afiti anthu okupha
Auzeni zoona zikhale ng'oma chi ndi munthu osaphuzira
Best history ❤
Nthawi ikwana ya zikhale mulungu akuonaso asiyeni atase nthawi yawo kuipa kwa chakwera kotenga ma big fish kukhala nduma munthu wakupha ameneyo
Amalawi vuto ndi kuiwalansanga mwaona lero zikhale mutu ngati zungu
I love you brother
Bwana
I really hate MCP zikhale ng'oma azayankha mulando tsiku lina MULUNGU simunthu.
Koma samora machelo anapha anthu ambili ngati Kamuzu kuno kwathu ndikhulupila tikunena pano ali ku gahena wosewa.
Dolo wa madolo ndwe 1 💥🔥💯
Zikhala ng'oma uziopa mulungu zimene ukupanga sizabwino
😂😂😂😂😂 azikhare ng'oma mwanva komwe muliko
Zikhale ng'oma typing and deleting😂😂
Irene Chirwa ndikukufuna
Wasala pangono kufa alibe masiku onsewo
Zikhale ng'oma akukhala akukhala Ku rwanda
Kukhala ku opposition ndikowawa😂😂😂😂😂😂
Komanso zikhale ng'oma akuyiwala kuti pompano taika chigawenga cha mcp John tembo amene amaona ngati sazafa lero alikuti ndipo wasa sisiliya kadzamila zigawenga zokhazokha zimenezi zazimuna ndizazikazi
Inuyo ndi big, ndine mozabique, inuyo mumanena zowona zenizeni pitilizani tchito yabwino big.
Amuna m'dala bambo
❤
MCP se Boma koma kupha Abale athu komaso kuba
...on Bon Kalindo, I think he actuarrly challenges that he misses prison. We cannot defend people who call demonstrations out of political frustration and be paid by frustrated DPP. Kalindo has the bset interest on his stomach. 3 governments never gave him a position due to lack of education. But I also want to to mention that KZN is a savage. He was also involved in the 22 massacre and I would think he was an authority during Chasowa's murder. But even if it were Richard Chimwendo, or myself, I would make sure Kalindo is disciplined. The problem in Malawi cannot be fixed by burning, looting and marching by paying street kids.
I can't see your face but I can see mbali yako and you know what we are tired and sick with is so Called mcp that's why anthu sangaiware what they have done to our parents and nthawi achisiru, and they can not take us back thank you
Iweyo chisulu kwambiri
@@user-ld1js7dt3b I am equally disappointed with MCP. BUt as poor by choice as we are, we cannot continue sitting on the streets. If Kalindo had a good plan, he would engage the industry captains to create employment than creating looters. We all know that MCP is incapable of turning the tide, we rather remove them in 2025. But we run the risk of worsening the situation by disturbing the already non-existent economy. By the way, currently in Malawi, there's no party that can govern. They are all gangsters and thieves. So creating a nation of looters will never solve any problem beyond 2025.
Amve ndithu amenewa
Amalawi zofuna izii okamba odalipo kut namapwala uyu otchedwa chilimayi ndi mzake mfiti chakwera wa Amonika sangapange kanthu koma amalawi kusanva
God is watching what MCP is doing and we are also watching, we have answers in 2025, may God continue taking care of our president, president for the poor
Exactly brother
❤❤❤❤
Ndiponso azalirira ching'ang'dza a MCP onse Iwo aku wona Ngati azawinanso panopa Dziko lapansi lonse ladziwa zoti chakwera ndi Tonse alliance ndi mbava zakuba dzitsiru za Wanthu
Best hx
vuto A malawife timangolilira mmimba .zoti tipange action ayi ...Anthu akummwera ife ndife zitsiru.tikungoyang,anira zathu akungomangidwa pasiku katatu . Lero nawo mafumu kumangochi ayamba kurankhura mwamanyi after kurandira Bazi. akuti kumangochi kuno mademo ayi how
akuonekadi oophya nkhope
Anthu akadzavotera LAZARUS CHAWERA palibe chabwino. Dzina lamavuto okha. Lazaro wa mubaibulo anali mphawi. Zinthu zizidzakwera daily.
👆Dzina la matemberero ili. Chonde tiganize bwino a Malawi.
Eeee
Oyipa zikhale
Akakhala paudindo kumaona azao ngati makape
Tafika
bg tilipambuyo panu muuzeni chilungamo galuu ameneyii kuti sikaleso ayi udindo umenewo ukutha so tell him truth
Zikhale ng'oma is wish he think police prison is the place to play with
Ndiye kuti mmene wasowa chonchi, Zikhale Ng'oma akusewera yapansi koma ngati kuli Satana ku MCP Mmodzi mwa iwo ndi Zikhale Ng'oma osayiwala Chakwera
Ka 40 lizakwana palibe wamuyaya iwe zikhale ng'oma ndi chakwela wakoyo
Following
First to comment
Zoon big man
Akulu zimene zimakuyamikirani ndi mbuli zizanu bwanji osamafotokozako za kuphedwa kwa Isa njainju anthu azidziwa chilungamo inuyo mcp mumadananayo Ife timangokuvetserani cadet
Iweyo mbuzuwe osalongosola zimenezo bwanji...mphaka
Zoonadi a ng'oma axaona zowawa
Wati ziiii Zikhale pano kaya ali kuti
Akamuna mumatiimilira koma letter BOM sindikuziwa kuti amapanga bwanji nanga BOM ingakwane mu invulopu?
Zikhale ngo'ma paujeni pako wamva??? Ukuzuza kalindo tizaonesana ubwino wake mukutuluka mboma
😂😂
😂😂😂 zinkhale Ngoma ndi kappe weni weni wa munthu
Wachibwana zikgare yo
Munthu wapachifila Kona kuvuta too much
Wina chinsalu chankachisi chidzamung'ambikira pakati
Zoonadi tikumanatu ameneyo oky
RIP zikhale ng'oma and chakwera
Not RIP BT sndikuziwa chizungu chake km asaksuse mumtendele km wakumoto bas
asikale ng'oma ndgalu wamunthu
Power of MCP Boma la MCP khalidwe lawo lakhaza bass but god is watching this
The best tv inded
Koma mfana iweyo!!!!
Munthu wapachifila Kona kuvuta too much
Eeee
Ngati kuli zitsiru za wanthu ndinu wanthu mumacomenter nonsense alomwe