kodi athu amenewa akuyakhulawa ndi akuti,,, koma pano ali kutiko pano anthu amenewa?????????????????????? may almighty true living GOD FORGIVE THEM JUST BECAUSE OF THEIR SPEECH
Kupatula zot zomwe mwakambazo but nthawi ya UDF aaa guys ndalama imapedzeka...mboni ndi mavenda.. Chilima for the first time ndinkamufila but nnangowona kut nayenso zinali nkhobwe zen zen nnamutuluka
Anthu awa ndiye ndi abodza enieni komanso abodza Eni Eni.Abakili munkawanyoza aja ndi amene anatimvetsa kukoma kukoma dziko lathu la Malawi.inu agalu mukupanga chani chiyambireni cha boma lanu
Atupele Ali ndi experience than them u can see they're destroying our country instead of kuli kwedza dzikoli. Atupele anali Nduna Koma sanabe what if atakhala president obvious sangabe
Malonjozo aanthu andale paradise yanu ndi padziko lino lapnsi basi kwa Mulungu jahena fire waiting for u .Quran said dziko lapnsi lakwanila kukhala jana kwa anthu osaopa Mulungu mmodzi mwa iwo ndi atonse alliance aboma la Malawi ndaona lero after Malonjozo awo
Iwe galu kwabasi chilima wamva bakili tsungafane naye unambitsa kuba kwakoko umaona kwadzako galu iwe...lero iwe bell yako tsukuyenda mtumba galu iwe chilima ndemvu zoyerazi galu
which alliance is coming from God....if I may ask you as MCP -UTM did you give people a cheaper fertilizer and food,,,, All politicians are just the same.
Galu wamuthu the whole world ndi chilima kuyankhula ngati waduka muthu lero nayoso akuyakhamilandu yakatangale komaso maboza iyeyo one million jobs yilikuti?? Kudya katatu kulikuti so waboza ndani apo??
INU A ALLIES NU NDIYE MWACHITA KUPOSA MBAVA ZONSE ZOMWE ZAKHALA ZIKULAMULIRA MALAWI.😢INE KUKUDABWANI KUSIYA KUTUMIKIRA MULUNGU, NKUKALOWA SATANIC...! God forbid. Koma ku ubusako zimandako bwino bwino? Kapena ndi aja okhalira Kuba cha khumi aja...! Charlatans😢
Mwa chilima ndinkaona material ngati Julius malema koma mmmm mikozo yeni yeni. Malawi wanga ine
😂😂😂😂😂😂 Koma ndaseka
Chakwera failed us, but Chilima can not be a solution 🚮🚮
kodi athu amenewa akuyakhulawa ndi akuti,,, koma pano ali kutiko pano anthu amenewa?????????????????????? may almighty true living GOD FORGIVE THEM JUST BECAUSE OF THEIR SPEECH
Lero Nanu muli ndi milandutu mumkanena anzanu kumadziona ngati ndinu ochenjera
Nawenso mbava yachabechabe
Bolanitso bakili zinthu zimayenda bwino
Osamatchula yesu pa zopepela zanuzo
Chilima boza limenero
mtambo ndi m'bulundi...😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂akagwele
Mbava za Tonse Alliance ndiye bolanso mmbuyomu,
Kodi achilima siwaja adapanda akazi awo aja ?
Happy and good speech today but remember tomorrow your not a leader someone will Judge you
🕊📖.........✍
Mwaziona amutambo chakwera ankafuna mmuchose mmatope lero ndi izi aliyese amene adamuolosa akufuna atamupha
Kupatula zot zomwe mwakambazo but nthawi ya UDF aaa guys ndalama imapedzeka...mboni ndi mavenda..
Chilima for the first time ndinkamufila but nnangowona kut nayenso zinali nkhobwe zen zen nnamutuluka
Bakili ndimunthu wabwino ❤ mukamati ndiwakuba osaona manyazi iii akudyeselani ?
Atupele ndi mbuzi ngati bambo ake😂😂
Anyamata ndie akugwira ntchito momasuka,😂😂😂😂ntchito sizikusowa chilima ndi chakwera eishhhh😮😮😮😮😮
Adale nose wakumoto basi palibeso zokambilana iyayi fire 🔥
Were still waiting jobs 1million
Kkkkkkkkkk mamuna mzako mpachuludi nanga mesa ndi awaa zawakanikawa
Fetlizer lero 90 pin fuel 2pin
Anthu awa ndiye ndi abodza enieni komanso abodza Eni Eni.Abakili munkawanyoza aja ndi amene anatimvetsa kukoma kukoma dziko lathu la Malawi.inu agalu mukupanga chani chiyambireni cha boma lanu
guyz chilima nda azizake omwewo mavuzi awo ndithu anyapapi setezawo
chakwera NFUNDO ALIBE😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Atupele Ali ndi experience than them u can see they're destroying our country instead of kuli kwedza dzikoli. Atupele anali Nduna Koma sanabe what if atakhala president obvious sangabe
Bwanji Kodi tizimulemekeza bakili muluz coz anasiya ndale
Chilima ndamuda sangandinyozere atupele
Aliyense Ndimbava, inunso mukumvera izi ndinu akubanso, Don't judge anyone.
That's why jesus anati amene sanachimwepo atenge mwala amugende
Ndekuti iwe ndimbava ndiwe wakuba
Ndichifukwa chake mukufuna kumalimbana ndi atupele ndichani anakulakwilani Inu ili ndi chimo la bambo and not him
NDIPOSO MWINI WAKE WA TV IYI NGWAWUSILU ..AMAKONDA KUNYOZA BAKILI MULUZI KOMA NDIMAZIFUSA WHY DOES HE USE HIS NAME
Lero zakudera galu bakili umalimba naye uja lero wakutembenuza wangopusa wasocheresa amalawi galu iwe
bakili akaba, ma chenje osala amagawa moti umphawi kunalibe pomwe anyani inu mukaba mungoziunjikila nokha achule inu
Amalawi timangoombera mmanja zopanda pace. Achinyamatafe tatopa kenako tizalowa mchire n'kuyamba kupulitsa mizinga
Iwe ndi mbuzi yamunthu iwe ndiwabodz iwe sukunamiza anthu apa!!
Atupele mulidzi Vs Peter muthalika 2025 Boma UTM anthu asatanic inu
Chakwla ndichilim ndagalu opanda man kobas wallah......pano achewa ndamene akusangalala mh mulingu awakathe ndithu
soni achilima mmbwa🦮
Mtambo alibe nzeru, kulakwa kwa abambo ake Atupere chikumukhunza nchayani?
sindikudziwa apumbwawa azalowanso ndi it it 🤔🤔🤔 Linda madzi aduse uziti Wadala ukanama sikuchedwa kucha
Koma agalu atonse 😂😂
Malonjozo aanthu andale paradise yanu ndi padziko lino lapnsi basi kwa Mulungu jahena fire waiting for u .Quran said dziko lapnsi lakwanila kukhala jana kwa anthu osaopa Mulungu mmodzi mwa iwo ndi atonse alliance aboma la Malawi ndaona lero after Malonjozo awo
Agalu a anthu awa. afiti awawa ndamene akuononga dziko lathuli. Kubako kukupitilila Bola khale
Nonsenu ndinu mazoba akamazi okhaokha ndipo kwanu kwatha akabawi inu
Iwe galu kwabasi chilima wamva bakili tsungafane naye unambitsa kuba kwakoko umaona kwadzako galu iwe...lero iwe bell yako tsukuyenda mtumba galu iwe chilima ndemvu zoyerazi galu
Chonde mukapeza mpata mundipelekele moni kwa chakwela ndi saulosi kuti mboli zawo
Iwe unena mzako za bello Yako pano ili mthumba chakwera chilima agalu anthu utakhala mowa ndiye wamatokoso kunama kumeneko hell is waiting for you
Agalu nose mbava inu ndiyeno panopano bwanji?? Komaso Amalawi kutengeka mwachangu
Iweyo chilima fertilizer wa k 4 .495 akupezekera kuti ? Nankha iweyo chakwera job 1 miliyoni ziri kuti ? Nankha iweyo chimutu chachikulu chimwendo katangale ukunkanayo katangale wake uti kodi za kubutchary zija katangale apose pamenepo ? Nankha iweyo okuda nkhati kumatako kwakoko ntambo ukundiudza kuti upresidernt ulipowu siwa famiry?
mbolo zosadulazo Agalu
Km chilimayu bwanji osakamnba zoyendesela ziko lino bwanji km busy kunyoza ena yoo km Malawi
Inu 2025 muzaluza ngati ana oti akufuna kuyamba kukwawa kumene
Listening
which alliance is coming from God....if I may ask you as MCP -UTM did you give people a cheaper fertilizer and food,,,, All politicians are just the same.
Bola muluzi zinthu zimayenda
Kwambili sukunama
Chamba sichabwino, Mtambo & Chilima, Munasutilanji taonani sono mwayamba kuonekera.
Koma anagamula mulandu tawakhululukila unatha ali mfulu tsopano tiwone enawa kuti ma belo mthumba azatuluka liti
Achilima zakusi zanu ...ngati muli ndi umboni okwanira bwanji boma likusowa umboni wa mlandu wa Atcheya inu mulinawo....lero udziwe ichi.Zenje lomwe umakumbira zako umagweramo wekha ..lero ndiwe uli pa bail
Devil kuchita quote Bible kkkkkkkkk
Muzafa ngati gwanda chakwamba opanda kanthu nonse
Galu wamuthu the whole world ndi chilima kuyankhula ngati waduka muthu lero nayoso akuyakhamilandu yakatangale komaso maboza iyeyo one million jobs yilikuti?? Kudya katatu kulikuti so waboza ndani apo??
Kkkkkkk 😂😂😂🤣🤣🤣koma chilima
Mpaka lit
Kodi adadi apanga lit nsonkhano si sizizi ai
Yiwe machende ako
Pano 2023, azimayi 1million analandira capital kodi, nanga achinyamata
Kape iwe choka ukuti nyadza pita ukachape kamwa
Panyapako lwe galu wa muthu
Nde lero mbuzi ndindan 🤣🤣🤣 atambo kuda kulibiiiih ndi mtima omwe
Apa Malawi wadzadza ndi atsogoleri onama akuba abodza mbuzi za anthu zitsilu agalu
Ndipo mbuzi zake osangoti mbuzi Koma mbuzi zamano kunsi
Osalira munka vota nokha lero ndiizi tinkakuuzani kuti mcp ndiyakupha yankhanza pano kusintha kumene amanenaku ndikuphanaku ndiye pano mukulira kufananso adadi mumawanyoza aja bwa mumawombera mmanja zigawenga inu muluzi anakutsegulani mmasoyo kuti mudzikhala ndi ufulu olankhura munamunyoza ngakhale amakuuzani kuti osazavotera mcp kuyipa kwake amakudziwa anthu osanva inu lero ndiizi ndipo uku ndikuyamba chabe ankakugulitsani fertilizer ndi pakamwa mk4500 koma pano mukugula mk100 + zauzand thumba limodzi ,atupele ndi bambo ake mumawanyoza aja ndiawo sanakwiye nanu anamuperekeza chilimawa ndipo adad wo akuchita bwno kusalankhura msanga pazimene anthu mukukumana nazozo chifukwa ndiinu anthu osanva muphunzire kuti nthawi zina ndibwino kumanva makolo akamakulangizani look now this is just the beginning for mcp izi ndinjoka izi
Anthu Inu Mulungu azakuotchani sure
Mmmm indedi mbudzi ikakodwa amalonda ali pafupi ndithu.eeeeish anthuwa mngodzuwa kunama ndithu.
Burundi ngat iwe, ungotiombanitsa mitu bas
Kupepela amalawi tawonani pano mwaja mwala waukulu olepela kuuswa ndi amala ya yikulu
galu iwe osantchula yesu pazopusa zakozo
Chokani apa ana njoka Inu anthu akuba tionana 2025 ino muona nyoooomphamba za kuba
Panyapanu agalu inu pano mukupanga cani? Iwenso chilima macende ako
Awa ndi achitsiru chilima
Mamvuto okha okha dziko lathu lamalawi palibe wabwino zed pandale angokhala ngati ayao bodza lokha lokha basi
Uzipusisa achewa ndi atumbuka zot inu mukuba saakudziwa
Chakwera ndi satana mpaka kusiya ubusa ndikuyamba usatanic eeee koma satana akugwiradi ntchito yake
Let's we forget
Koma Dziko la Malawi kaya ndi umbili ndiye Kuti ndichifukwa Chake tizikhumbila anzathu akutukuka
INU A ALLIES NU NDIYE MWACHITA KUPOSA MBAVA ZONSE ZOMWE ZAKHALA ZIKULAMULIRA MALAWI.😢INE KUKUDABWANI KUSIYA KUTUMIKIRA MULUNGU, NKUKALOWA SATANIC...! God forbid. Koma ku ubusako zimandako bwino bwino? Kapena ndi aja okhalira Kuba cha khumi aja...! Charlatans😢
Siku lotenga minyama 😢😢😢😢
Muzayankha kwamulingu time is coming
Mwana opanda ulemu iwe, iwe si wakuba?
Mbuzi iyi
kd afolenawa akuti chani ?kutereko ukuwona ngati ungati lamulire kuno kumalawi kuno aiiiii
Lakulemphelani Boma , lamutondani Boma ,Anyamata inu
Chilima uzipusisa achawa omwewo
Iwe ofoira waononga chilima
Mukhalila yomweyo anzanu akuchita bwino
Masendako wedoda sunanyoko
Kodi campaign yanu inali against muluzi kapena Atupere kkkkk
THEY GOVERN OUR GRANDFATHER'S GRANDMOTHERS FATHERS AND MOTHERS WE WILL TAKE OUR DESTINY OURSELVES AM GOING TO GOVERN THEIR CHILDREN SO HELP ME GOD
Tikumalizani a tonse alliance
Izizi nde zausilu a malawi nafeso ndiopepela kwambili lelo ndi zimenezo agalu achabe chabe
Galu wamunthu chakwera ndi chilima mbava za anthu mulungu adzakulangan
Zitsilu izi mmene mukubera agalu inu
Mtambo garu kwabas
Mundichimwisa chonde
Onsewa NDl mbava amalawiwa kaya ndiu mphawi kaya umbuli amaombela mmanja nzopusA zomwe
Nanga iwe milanduyo ulibe
Chilima kutha mawu kwambili mmmmm lero si izi hiyaaa