I can see kuti muikila kumbuyo bakili muluzi. But still anthu andalewa they are all the same in stealing. Bakili is not a fool kulanda dictator kamuzu boma nde muganiza angamutulukile just as easy as that ataba ka ndalama ka kwacha? He knows how to play the dice well.ma pepala onsewo anawakonza akanali m'boma cos he knew this wil happen
Komanso tiyeni tiyione nkhaniyi posatengera ndale. Kodi a boma akamanena kuti bakili muluzi anaba k1.7 billion umboni wao unali kutiko? Olo atakhala kuti muluziyi anabadi koma chofunikira apa unali umboni kapena mapepala oonetsa kuti ndalamazo zinachokeradi kwa ma donors. Koma to say the truth this case was politically motivated
@@lastonekaponya7675 koma olo amagubira Ku khothi koma a boma analibe umboni. Chifukwa a DPP akanationetsa ma cheque kapena ma list a Ku Bank oonetsa kuti ndalamazo zinachokeradi kwa ma donors. Koma bingu inali mbalame ya munthu ndi chifukwa chake mlandu umenewu ukungoononga ndalama za boma. A boma akulephera kuthetsa mlandu umenewu chifukwa akuopa kuti Muluzi akhoza kukawasumira kuti amulipire ndalama zambiri chifukwa chomuyipitsira mbiri
Munthuyu poyamba ndinkamuona ngati wa udf, koma ukamumvetsera bwinobwino udzaona kuti alibe mbali. Zomwe akufotokoza zili ndi ma facts enieni. Za mlandu wa a Muluzi aliyense akudziwa kuti a boma analephera kutulutsa umboni ku court.
Nice. Big
It's only we poor people who are arrested for small things. My country Malawi mmmmmm
Malawi lizakhala Dziko lochitisa manyazi mpaka Ambuye yesu azabwere.Silixatukuka
Palibe azalowe boma nde osaba ...never ever onse ndi okuba amene analipo alipowa onse mbava
🤝
Ndiye osamangokamba zoyipa za mbali imodzi
Nice 1
Where do you get all these
Malawi sadzathekanso basi kudachuluka anthu ozindikira akuba osaukafe tizingolira ndithu ndikumamva mbiri ngati imeneyi😭😭😭😭
We follow u
Malawi sazatheka chifukwa atsogoleri ndima big crooks
Ineyo ndikufuna history yanunso ndiyinve ikhoza kukoma kwabasi.
Next chilima please
Kkkkk zandare dzizidziwa chirimayo ridari bodza aribe umboni akusowa poyambira
Pano akudyana ndi chakwera kkkkkkk
Bingu anangommanga Muluzi pa zifukwa za ndale ndi chifukwa chake anasowa umboni
😅😂😅😅😅😂
😅😅❤😅❤😅❤❤
Mumakwana bwana pongofufuza tiziva
Malawi sazatheka kuba kumayambira kumpando kumwambako mpaka pansi
Amene ankapanga zakatangare ndi bakili muluzi ndi nduna zake
Olo bingu anali so wakuba moipa kuposa Bakili Muluzi. Kuteroko munthuyu poyamba paja amanena za Kamuzu. Pano umuone wasintha ma video ake akunena kwambiri za Bakili. Tsiku Lina umvera akukamba za bingu. Ungoti pheee udzazimvera wekha mmene bingu anabera ndalama za boma
😅❤😅😂😅😂😅😂❤
Info mumaigoba kuti biggy🤣
Komanso bingu ankaganiza mwauchitsiru. Anatsegula mlandu wa k1.7 billion alibe umboni okwanira. Akanationetsa ku khothi mapepala enieni oonetsadi kuti ndalamazo zinachokera kwa ma donors.
zostsapindulitsa izi zinapita pa nthawi yake . munali kuti panthawi yomwe mumaona pamene amaba ? onse adalamulira monga mwa plan yawo
kodi nkhani Ya George Chaponda ilipati?
I can see kuti muikila kumbuyo bakili muluzi. But still anthu andalewa they are all the same in stealing. Bakili is not a fool kulanda dictator kamuzu boma nde muganiza angamutulukile just as easy as that ataba ka ndalama ka kwacha? He knows how to play the dice well.ma pepala onsewo anawakonza akanali m'boma cos he knew this wil happen
Komanso tiyeni tiyione nkhaniyi posatengera ndale. Kodi a boma akamanena kuti bakili muluzi anaba k1.7 billion umboni wao unali kutiko? Olo atakhala kuti muluziyi anabadi koma chofunikira apa unali umboni kapena mapepala oonetsa kuti ndalamazo zinachokeradi kwa ma donors. Koma to say the truth this case was politically motivated
Tsongoleri akakhala wakuba anthu akeso amakhala akuba komaso timadziwa kuti achikulirewa ndamene akugubira ku court
@@lastonekaponya7675 koma olo amagubira Ku khothi koma a boma analibe umboni. Chifukwa a DPP akanationetsa ma cheque kapena ma list a Ku Bank oonetsa kuti ndalamazo zinachokeradi kwa ma donors. Koma bingu inali mbalame ya munthu ndi chifukwa chake mlandu umenewu ukungoononga ndalama za boma. A boma akulephera kuthetsa mlandu umenewu chifukwa akuopa kuti Muluzi akhoza kukawasumira kuti amulipire ndalama zambiri chifukwa chomuyipitsira mbiri
Chair munthu wamkulu
Ndiiwe mbuzi kwambiri umachita kuonetseratu mbali yomwe uli
Munthuyu poyamba ndinkamuona ngati wa udf, koma ukamumvetsera bwinobwino udzaona kuti alibe mbali. Zomwe akufotokoza zili ndi ma facts enieni. Za mlandu wa a Muluzi aliyense akudziwa kuti a boma analephera kutulutsa umboni ku court.
Mbuzi ndiweyo bola ifeyo akutisegula m'maso
Zinachita kuvuta mwantundu wanj mpaka air malawi kugulisa 4million nyumba?...
Mu 2000 k4 million inali ndalama yambiri. 1 dollar inali 100 kwacha, pano 1 dollar ili pa 800
Biased analysis