How can Usi talk he had more time to talk in the past. But while he is in this sanking boat we saw him being silent for sure. A silent baby on journey dies with hungry but the crying baby always finish the journey with full belly. Shame for him.
Imfa iyi nde yawawađđđ, koma ndadandaula ndi aMalawi anzathu amene atayaso miyoyo usikuwuđđđ, mizimu yawo iwuse mu mtendere wa AMBUYEđ
Malawi wachita chiwewe. Amene akuchita zinthu Ali phee kumene Ali kufuna kuyipitsa mbili ya anthu ena. We belong to the Lord Almighty and one day we shall retain. Usiyeni nzimu wa Saulosi uwuse mu mtendere.
Ifa ndi thawi Muthu wina aliyese azalawa ifa and paliponse pomwe angakhale ifa ikupezani olo mutakhala malinga otani. Muthu wina aliyense alinayo thawi yofera ndipo thawiyo ikakwana sangayichedwere kapena kuyifulumikisitsa ai ndipo dzikoo lapansi ili ndi chabe ndinchitsangalalo chonyenga basi
Mama a kaliyati ambuye azikutsogolelani pa tchito yayikulu imene mukuyigwila.koma dziwani ichi amayi chipani cha utm panopa chidzakhala ndi mphavu komanso sapoti yayikulu kuposa kale.inu ndinu atsogoleli chabe koma chipani chili ndife anthu wokwiya chifukwa ndi amene timavota.
Ussi is a betrayer,Mai kaliat congratulations,MHSRIP,Mr chilima đđđđđđđđđđđđđđđđ,chakwera why why why you killed chilima
Congratulations ntchewu fans,stone chakwera with his team.mugendeni chakwera palibenso chabwino apa amada,amada arise,atiphera athu athu akumwera ameneyu.chipolowechi osawone ngati ntchitha .Rest in peace all.
We should thank for the Woman Patricia Kaliati to stand strongly. I think God uses her for he is not scares God he connectes to even the one whose heart is flaming up.
Guys lm not politician but why president Lazarus chakwera said in his speech that, i know your anger is beyond limit but don't fight back the wrong, now which wrong? Silent of manganya bring many questions all the part of world.
I heard that chakwera promise him to be VP but he is stupid if he will accept it he saporsed to say something in this matter see kaliati she is very strong woman
Not kuti azitukwana ai palibe member wa UTM amene akutukwana koma him as a vice president of the party anayenera iyenso kutenga mbali yokhazikisa Bata kumamvesa zimene zikukambidwa osamayankha zoti anthu akukayikireni as if munayamba mwapengapo
I'm not a politician but this death has affected the whole nation since our VP was so humble in all areas
Tiwalila mpaka kale kale, MHSRIP
Mai Patricia Kaliati ndimakulondani inu ndinudi mai wathu ndiodziwa ndale ndiutsogoleri, mulungu akudalitseni RIP SKC đą
How can Usi talk he had more time to talk in the past. But while he is in this sanking boat we saw him being silent for sure. A silent baby on journey dies with hungry but the crying baby always finish the journey with full belly. Shame for him.
I totally agree with you. She is indeed a Super Woman. Infact, I admire her courage đȘ.....
AKWENI SHOULD RISE UP AND BE BRAVE ENOUGH TO FILL SKC POSITION.
Manganha bwanji?
Mcp has lost it, no matter whether they did it or not but God had chosen this way to bring them down . Paja Mulungu anaumisa mtima wa pharaoh mwadala
Kaliati is wise and crever enough keep it up
Mpungwe sinjira yokodzera zinthu inde Komano ngati chilungamo chikusowa zimakhala zomvuta,aboma akanakhala kuti kafukufuku wapangidwa nkuziwapo chilungamo sibwenzi zili choncho,komanso akadawamvetsa zoti anyamula okha osapanga nkhanza padipiti bwenzi ili nkhani ina,anyani amvumbwawo mukadawaudza kuti asabwere kumeneko anthu akanadekha koma mukumanyanya kumachita kuwapatsa pepani zopusa
Kafukufuka si 1+1.Sizingatheke tsiku limodzi
Zonsez zikuchitila chifukwa chakusowa chilungamo kwa boma kwasalaku ndi by fire by force
RIP SKC ,as a Ngoni from Ntcheu ndalira kupita kwanu a Chilima, mpaka ndakhetsa msozi.
Imfa iyi nde yawawađđđ, koma ndadandaula ndi aMalawi anzathu amene atayaso miyoyo usikuwuđđđ, mizimu yawo iwuse mu mtendere wa AMBUYEđ
Respect the burial ceremony of the late VP Chilima no matter where you are please avoid misbehave.
Palibe munthu amene adalengedwa kuti sadzafa ndipo kuti adzafa bwanji uchitsiru chabe ukuonekawu
Chilikwanzako Chima phweka a braz. Chikakhala nyumba mwako it feels different
Chilungamo chioneka chifukwa MULUNGU alowelerapo ndipo aliyense amĂšne akuweruza anthu ena chikhalireni alibe umboni achita manyazi posachedwa
God Knows everything May your soul Rest internal peace tonse tikudikira komko
Malawi wachita chiwewe. Amene akuchita zinthu Ali phee kumene Ali kufuna kuyipitsa mbili ya anthu ena. We belong to the Lord Almighty and one day we shall retain. Usiyeni nzimu wa Saulosi uwuse mu mtendere.
Chitipa chimaziipitsa mbiri chokha ndipo mbiri yake yaipadi
Chaziipitsa mbiri chokha
Indeed good people die young and l quote mmmm the pain is hard to bearđđđđ
Malawi suzasintha tilibe moyo wausamunda omweujađđđđđ
Ussi amudyesa chibaziii ambuye akamakatha a agyptu akathira limodzi ndi usssi
Oh! Wajoina ma Lacoste mwachinsisi?
Respecting the burial ceremony of the late leader will be of more importance. Malawi is one and very small
Michael usi has chosen to be silent at this mourning time of our beloved vice president why????? Michael usi mwakhala chete bwanji
Ma Lacoste anamuseka pakamwa
Mwambo woyika SKC umafunika utazayamba nsanga Kuti udzathenso nsanga Kuti mwina anthu obwerera adzayende kukadali koyera. Enafe timabisalira pochita zoyipa chifukwa tawona mdima.
Skc !unali, uli ndipo uzakhalabe hero wanga. Rest in forever peace.
Tiyeni monga mwini wake analiri honorable Chilima pamene moyo wake unali olandila chipongwe koma sanabwezere monga anali ofasa ndi ondekha tiyeni tichite Chimodzi modzi kuti mzimu wao uunse mumtendere osatha kuti mwini wake kumene akupita apitilize kukondwerera đđ
Sizipangisa kupereka moyo kwa otisiyawa chofunika ndikulira maliro ndi mtima osweka komanso olorerana kuti munthuyu alowe mmanda mwamtendere
Warm heart of Africa ija yaonongeka đđđđđđđ
Democracy ndi nyasitu,Kamuzu anatiuza kale
Mr akuopa kulankhulapo coz iyeyo nd part of tchile ndpo moto uli behind his back đđđđ
Mulungu akudalitseni mai kaliyati chifukwa chamau achilimbikitsođđđđđđ
Great speak anakhoma
Mr usi umkakulatu mtima pamene APM inali m'boma ...lero uli chete ngati bubu onetsatu u master akowo ...
Zikumveka ndithu zimenezi koma, young generation tingoti tiyeni tiike maliro chifukwa tataya mbadwa ya ife đđđđđđ
Zikuwawa komađđđ
Action pasogolo osafooka guys zibonga zituluke zochuluka kumeneko ntcheu morefire
Maico utsi amuchose muchipani ndifiti arindi chakwera
My fellow Malawians let's bury our hero peacefully other than causing havoc
Kulira kwanga nkosatonthozeka,,
Bvuto ndiumbuli ndiumphawi kubvetsa kumakhala kobvuta koma ndikuyamika bambo njawala komaso mai kaliat ambuye akudalitseni
Mr usi tiyankhuleni koma
Titsalila kosaiwali malawi dot for geet vice president history
Zovuta kuvesa kmabe RIP DR SKC
MCP yanyika it will b difficult for them kukapanga campaign ku ntchewu.
Sa utm nda amalawi osweka mtima
Glorify to almighty God for this lost of chilima life
Koma mwambo uthe nsanga chonde muyende usana osati utsiku ngati momwe umayendera dzulu
he s pro mcp
We never keep silent till chakwera atamusata chilima
Zooonadi kuti ndife okhudzika funso ndi loti boma lidatenga nthawi pokayafuna ndege ija lero mukuona ngati achinyamatafe ndife okondwa nanu?
Zochitisa manyazi kwa atsogoleri a utm ,bad example
Mwina munakapepha achakwela
A president achakwera chimene amachita amachiziwa and ndi muthu oipa wapha Mr chilima
Zoon osationongel mbir
Ifa ndi thawi Muthu wina aliyese azalawa ifa and paliponse pomwe angakhale ifa ikupezani olo mutakhala malinga otani. Muthu wina aliyense alinayo thawi yofera ndipo thawiyo ikakwana sangayichedwere kapena kuyifulumikisitsa ai ndipo dzikoo lapansi ili ndi chabe ndinchitsangalalo chonyenga basi
Usi pajatu pazokambilana zilizose za UTM akumuthamangitsa nde mutakhala inu mungatani
OSAONETSA NKWIYO ANYANI AWAWA AZOLOWELA AND AZINGOPITILIDZA KUCHOTSA MIYOYO YA ANTHU ENA.KOMA NGATI MUKUFUNA BATA .MWAUDZE A BOMA ASATENGE MBALI MAKAMAKA POLANKHULA PAMALILO .AND MWAMBO UYAMBE NTHAWI YABWINO MALILE AYIKE NTHAWI YABWINO.POKHAPO ZITHEKA .KOMA KUNGOPELEKA MPATA KWA NDUNA KULANKHULA ZINTHU ZIKAIPA
Kaliat wayankhula ngat wanzeru
I don't even think that chilima will go like that R I P
Mr.Usi has been sidelined just because he was not politicking as others have been ding
Apa nkhondo yapa chiweni ndimene umayambira mumaiko ena ngati simkuziwa
Chilungamo chikuoneka kale maganizo amalawi ndamodzi palibe kusintha kulikonse sitikusowekela maumboni ena
Ndipo iwe ndikugwirizana nawe anthu ena sizikuwawawa chifukwa abale awo ndi a mcp komaso afawo sabaleawo palibenso kufuna umboni wachani zinthu zikulankhuka zokha,zomwe zachitika achita kupha anthu awa pano simungawanamize amalawi kulibe chakwera amaonangati wabisala osadziwakuti wabisalamumbatata nsana ukuoneka nyekwe asowa nayo mtendere,
zosayenda
We so disappointed with this government
Koma ife amalawi tisayembekezere kuti boma lingabwerese chungamo poyera MMM ayi
Votolake inuyo chilingamo chikukusowan agalu inu
Malawi ana uzidwa ndi malemu kuti tisaope tisagonje tisaope komanso ma demo pa malawi anayamba kale
Zadabwisadi,olo speech yake sindinayimvepo but he could stand up and say something,let's wait n see
Ku UTM munthu amene ali mtsogoleli wawonetsa kulila kwenikweni ndi Dr Usi!!!!
Ngakhale one ndikanagenda athu achakwela athu oipa kwabasi
Mama a kaliyati ambuye azikutsogolelani pa tchito yayikulu imene mukuyigwila.koma dziwani ichi amayi chipani cha utm panopa chidzakhala ndi mphavu komanso sapoti yayikulu kuposa kale.inu ndinu atsogoleli chabe koma chipani chili ndife anthu wokwiya chifukwa ndi amene timavota.
She'll rise this woman
Tinayenera kupanga action kuti adziwe zatinyasa coz malilowa akayika sindikuwona nkhani imeneyi ikupitilila, anthu a ndale ndiwoyipa tinayenera kuti tingowagenda kumene
Mtumbo wako kaliati, naweso ukuziwapo kanthu usatinamize,, mesa unaimbilidwa foni kukuuza kuti umuuze DR SKC kuti asapite ulendoo, chomwe unalepherera kumuuza ndi chiyani, mapiruod ako
đđđđđđ
Ussi is a betrayer,Mai kaliat congratulations,MHSRIP,Mr chilima đđđđđđđđđđđđđđđđ,chakwera why why why you killed chilima
Iweso Patricia kaliati utisamale tikufuna iweyo
Anthu angat amwalirawo?? đđđđđđ Omg
Congratulations ntchewu fans,stone chakwera with his team.mugendeni chakwera palibenso chabwino apa amada,amada arise,atiphera athu athu akumwera ameneyu.chipolowechi osawone ngati ntchitha .Rest in peace all.
Tiyen nawo osaopa chakwera asamazitenge ngat mlungu
Kkkkkkk eeeesh tiyeni tikhale abata ngati chilima
Koma tiyeni tipereke bata president wathu timuperekeze mwa ulemu
So painful end unforgettable in history of malawi at large
Ali kumeneko ndi akutundu osat achipan
Dr salous klaus Chilima is died soul rest of peace
Ussi ndi mbuzi kwambiri,
Aboma asatenge mbali pozolankhula kuti kukhale Bata ngati akufuna mtendele
Big loss to the Malawi Nation indeed
Si aUTM amene akupagisa ziwawa koma a malawi ndiwokhumudwa koma tisamulole Santana Kutenga mbali chifukwa a Chilima anali wokonda Mulungu
Chipani chakupha inu ichi..... Mcp... Kwao ndikupha anthu.... No more vote for mcp.... Period.
We should thank for the Woman Patricia Kaliati to stand strongly. I think God uses her for he is not scares God he connectes to even the one whose heart is flaming up.
Guys lm not politician but why president Lazarus chakwera said in his speech that, i know your anger is beyond limit but don't fight back the wrong, now which wrong? Silent of manganya bring many questions all the part of world.
Did he say that?
Pay attention to the speech carefully
Mulindi zaka zingati akulu
@@mtunkhambama8352 ukufuna upange nazo chani?
đL0
Anthu agenda magalimoto amalilo kulibwanji adaniwo akabwera nde kuzakhala zotani
Maka-maka Zikhale Ng'oma, Harry Nkandawire
Tonse ngati a Malawi tikulira pomuluza wachiwiri kwa mtsogoleri choncho ndizabwinodi kuti tilire mwamtendere komanso ife ma commenter tiyeni tisatukwane koma mumuikiza mmapemphero veep kuti Mulungu amukhululukire zofooka zimene anali nako popeza njira yokalandilira zabwino kwa Mulungu ndi imfa
đđđđđ
I wonder why vice president of UTM,Dr Ussi has chosen to be so silent at this crucial time..is he pro utm or pro mcp??
Man has been mcp for long
I heard that chakwera promise him to be VP but he is stupid if he will accept it he saporsed to say something in this matter see kaliati she is very strong woman
Usi has been greased by Chakwera. He is a traitor, the modern day Judas Iscariot
Mumati azitukwana ngati munthu opanda zeru
Not kuti azitukwana ai palibe member wa UTM amene akutukwana koma him as a vice president of the party anayenera iyenso kutenga mbali yokhazikisa Bata kumamvesa zimene zikukambidwa osamayankha zoti anthu akukayikireni as if munayamba mwapengapo
đđđđđđđđ
Why u fear people UTM while they kill chilima like chicken this not gud it will be end up fight
Akaliat ngakhale atayankhula any how she was the one amafuchita influence ziolowe koma God's plan with not change because chilima is dead
Zinthu zalakwakwika fukwa chainu kaliati
Straight amayiwa sanachite bwino.
Mayo kaliyati takuthokozani.Koma a VP a utm alikuti sakuoneka Komaso sakuveka Mr Michael usi alikuti?
Michael usi ndiwopepela, ma program ake a Tikuferanji am not going to follow
Dikila aikeye malilo aveno madzi achina chimwendo banda Koma apule sidzikuwakhudza Koma ndunadzaodzi