Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho
UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!
And madam Patrucia Kaluati being the leader of utm presidential.candidate.cos she is has got experience of leadership.by profession she is a teacher and again she has experience of political leadership.she was in dpp .wurh Bingu wamutharika and peter mutharika
A UTM panokhs simungalamule dziko ndpo position yanu izingokhala 3 or 4... Koma chifukwa chot ndinu okulamtima mumadzimva ngat muli nkuthekera... Kachipani ka ma MP 4 koma matama thooo🤣🤣🤣
A Kalindo zindikirani ichi dziko la Malawi ndi latonse, is not about resignation of its members in government positions. Stop misleading people, eg Usi won't resign cos he is serving Malawians not MCP.
UTM back to DPP never we r on our own🔥🔥🔥🔥🔥
Koma fact ndiyakut apapa a UTM mwaphunziladi angakhale achedwa koma this is brave idea , tili ku mbuyo kwanu .
UTM should first stand on its own. Build the party
❤❤❤This guy he's genius Ndipo amati fightiler kwambiri 🔥
Asiyeni a UTM apange zomwe agwirizana
From town centre Mitchell's capetown bon ndimakudyadilan kwambili God ahead u bro
Iwe ndi machine🔥🔥🔥
Ndale zokha zokha,mwasiya masewero abwino, ndalama iwonongesa mbiri
Kalindo salimoyesa 🎉🎉🎉🎉🎉🎉👍👍👍👍💯
Uyuyu a Malawi ambr mmamupeputsa ,.koma nthw idzakwana ubwino wake muzaudziwa
Chitsime chimaoneka chokuya madzi akaphwa
Mupwetekana
Mumakwana Mr DC
Utm bwelenani ku dpp kuti udzamange amene anapha chilima
Kkkkkk Manganya adali Yudasi zoona, bwato satsilana pakati pa nyanja kkkkkk
Fakafaka mumatiimilila braz
The DC is right
Kalindo the man of the momenti %100
Nkhani ikhale UTM , AFORD ndi UDF apange alliance, president achoke ku UTM ndekuti azapeza ma vote Ku north , central pang'ono koma ochuluka ku southern nde kuti azaiphula bho bho
Mr bon kalindo thanks live on zambia Lusaka
Mission possible
UTM welcome back to DPP family
Eeeh ndine bon ...... 😂😂😂 Kuipatsatu fireee
Boooooooooon Kalindo!🔥
Mr DC hohoho🔥🔥🔥
Chikati hahahaaa Ndipo chimaseka modelela Chi Born Kalindooooo
Born kalindo ndakamuna
So good 👍
Pangolini tsopano
Ubwino wake ovota ndife, and kalikonse kochitika pansi pathambo Mulungu amachionetsa poyera
God first
Propaganda at its peak. Ife anthu osauka takana kuti ndiwe president wathu
Mmakwanila big
Pakhala mabvuto olimbilana utsogoleli APA ifee phee Ku MCP basi
Well did
L
Mawu a Bon sapita pachabe nd Yosef mwana wa maloto😅
Good
Born kalindo akamuna bambo
Uthenga ukupita kwa Michael Usi aka Manganya
Munyengo yong'alula🔥
UTM ISAPHATIKIZANE NDI DPP CHIFUKWA MKAZI WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POTHAWA MOTO KU SODOMU..PAMENE NGELO WA AMBUYE ANAWAUZA KUTI ALIYENSE ASAYANG'ANE MBUYO. KOMA MKAZI WAKE WA LOTI ANAYANG'ANA MBUYO POGANIZIRA MOWA WAKE WOMWE ANKAPHIKA KUSOMUKO NKUMAGULITSA. IYEO ANASANDUKA CHULU CHA MCHERE. SO UTM NSO MUKAPHATIKANA NDI DPP MUSANDUKA CHULU CHA MCHERE.MUKHALA STUCK AND DORMANT DEAD WOOD .!!!
Carry on pangolin
This is boooooooorn Kalindo🤣🤣🤣💯🔥
This is the truth utm plz bwererani ku dpp
Ichichi chinabwera🔥🔥🔥.
Pangolin iweyo the DC
Born!!!!!!!!!!!! Kalindo!!!!!!
Akuti anzanu wo anavota kale😂😂
Chilungamo kalindo
And madam Patrucia Kaluati being the leader of utm presidential.candidate.cos she is has got experience of leadership.by profession she is a teacher and again she has experience of political leadership.she was in dpp .wurh Bingu wamutharika and peter mutharika
Born💥💥💥
Ku dpp tikataniko? Chilima anatulukako ndipo sanabwelere mpaka kufa kwake ndiye ife tufuna mufuna mzimu wake utikanthe?
Ndeee kupusako do you think kut utm payokha ingagwetse mcp yotiiii ili m'boma inuyo dziko lanu simulikondayiiii amkolo chilima ananena yekha kut ku dpp anachokako analibe vuto lililonseee ndee inu ndare simuzidziwa Bola mungokharah chete ngt muganiza kut mungazawine panokha kuchotsa chipan cholamulachi
A UTM panokhs simungalamule dziko ndpo position yanu izingokhala 3 or 4... Koma chifukwa chot ndinu okulamtima mumadzimva ngat muli nkuthekera... Kachipani ka ma MP 4 koma matama thooo🤣🤣🤣
Kkkkkk
Mwana wakwathu DC tie nao kung'alurako
The DC 💥💥💥💥💭
Dolo kwambiri bonte kalindo😂
Kkkkkkķ tiligu mwati
Tiuze zoona ife tiri nga nga pa mbuyo pa DC
🔥
The DC Born Kalindo
Booon kalindo ❤❤❤❤
Inu kusokoneza basi
UTM 🕊️🕊️🕊️
Apa mwapala, za alliance so ayi
Thawi yong'alura 😅😅
We don't have opposition in Malawi
Tidzavote popanda ID plz
Zimene ukufuna iweyo abwelere ku Dpp ....
The fact is Kodi Njoka kudulidwa Mutu ingayende?
The DC
Munyengo yong'alula
Zikomo kwambiri azaona chomwe Chinameta nkhanga mpala mcp palibeso
Bwana kwambr😂😂
😢😢😢😢
Ichi chimaseka udyo..
Uyu ndi neneri ndithu
Boooon kalindo
Nde dpp zabwino?
Manganya 🚮🚮🚮
😂moyo moto Aye!
Boooooooooooooooooon kalindo the DC
Akakhala okha olo atapanga bwanji olo atatani sangawine ndipo akazabera dziko lizakhala mmanja mwa chinyamata
Kung'alura bas
Mau bg kkkkk😂😂
Kkk
Tisasogoze kukangana tieni tione patsogolo...
Emrove
Koma chikuseka😅😂🤣🤣
Musiyeni Manganya asangalale ndi mdalitso wake, ndi Mulungu adalola kuti akhale pa mpando umenewo. Sizoti iyayi wa UTM weniweni apange resign, kuti chani? Kulephera kwanu musade nako anzanu amwayi.
Hehehehehe kweeee ulira sunati
zoona kalindo chilungamo
kung'alura
We are not going for coalition again
UTM chipani cha pa social media🤣
Komatu ndiye kuli kung'alula🤦
Uyusotu amangolubwa
Chayankhula bwinotu
Utm
😂😂😂
Uyuyu ndi 🔥🔥🔥
Correction utm has vast followers so let utm.stand alone..and its gonna win with the majority.nos
😂😂😂😂
A Kalindo zindikirani ichi dziko la Malawi ndi latonse, is not about resignation of its members in government positions. Stop misleading people, eg Usi won't resign cos he is serving Malawians not MCP.