AFORD AKUPEPHA UTM KUTI APANGE ALLIANCE- ZOMWE ZAYANKHULIDWA KU NSOKHANO

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 12. 07. 2024

Komentáře • 66

  • @RachelDongolosi
    @RachelDongolosi Před měsícem +7

    Amen 🙏 mawu amphavu Mulungu akutetezeleni azitsogoleli amene mukuimila a Malawi osaopa Mulungu alinafe

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Před měsícem +3

    MTAMBO kakhaleni kunyumba...tinatopa nanu.AFORD SIYINGAWINE MWANA WAWUPANDU IWE..UMVE ZIMENEZI KOMWE ULIKO

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Před měsícem +1

    Vyakuyoghoya vya mtambo ni boza lekha😢😢

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb Před 18 dny

    Utm udf my vote

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před měsícem

    That's good l dea God be with you we love you pangani gwilidzano Ife tili pa mbuyo Pano

  • @WatipaCawinga
    @WatipaCawinga Před 28 dny

    Magufuli wathu kupoto

  • @marthaphiri3600
    @marthaphiri3600 Před měsícem +1

    Join hands with all the opposition parties, gawani mipando molingana campaign wisely win 2025.

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

    Alliance tapanga kale ndi UDF musavutike ❤❤❤❤

  • @LuwisKaigwaze-gr6cg
    @LuwisKaigwaze-gr6cg Před měsícem

    Musayembekeze kuti mudzalamulira dziko lino aford

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před měsícem

    Bomo ylo ❤

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Před měsícem +1

    Amen 🙏

  • @IshmailDukuturu
    @IshmailDukuturu Před měsícem

    Mbuzi iyi Timothy

  • @johnussenu2848
    @johnussenu2848 Před 28 dny

    Utm and udf boma

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune Před 28 dny

    Join

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 Před měsícem

    Chihana is my vote

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Před měsícem

    🫡🫡🫡🫡🫡🫡

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před měsícem

    Munthu oyipisitsa mtima Timothy sitingakumvere

  • @PeterPhiri-u7h
    @PeterPhiri-u7h Před měsícem

    MuKufuna alliance mukuopa chani

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Před měsícem

    Yambani zomwe mukunenazo musanalowe muboma ,kenako Anthu adzakhulupilila Kuti mukufuna kutukula dziko. Anthu Andale inu mumangotizunza,Anthu wovota kumabvutika inu Ana anu akuphunzila kunja

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff Před měsícem

    Mulungu wamakamu kanthani onse omwe adzunza nzimu wa skc lest in peace ndipo chauta langani ndithu

  • @yusufsadic2930
    @yusufsadic2930 Před měsícem

    Wabodz uyu
    Mumater mukamafun mavot
    Mumakhal ngat anthabwino
    Chilimanso amater
    Chakweranso amater

  • @jamessoko9480
    @jamessoko9480 Před měsícem

    Aaaaaaa....,ndimo mukuyowoyela mwa wandyale. Pa mupando khale waka,kujikuzga kwake uko,mwaluwa ivyo mukapangana.

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

    Utm & UDF Boma 2025 ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @Dickies-mk8cd
    @Dickies-mk8cd Před měsícem

    Tiyeni tikavote mwanzeru mcp must go.

  • @PrinceKachimanga
    @PrinceKachimanga Před měsícem

    Mtambo NDI MBUZI...mavuto alipo panowa,anyani akulamulira panowa..mesa anawathandizila kukhala pampando ndi iyeyo😂😂

  • @ntombiunice8637
    @ntombiunice8637 Před měsícem

    Mtambo ndikhuluku...u minister unamurephera

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Před měsícem

    Zimenezo2 zithera konko mwene

  • @user-rg9zc6eo2q
    @user-rg9zc6eo2q Před měsícem

    My vote afod

  • @alickkachepa3801
    @alickkachepa3801 Před měsícem

    Move

  • @BwanaGD
    @BwanaGD Před měsícem

    Komatu mtambo munthawi ino ukanankhala chete kaye munalumbwa kwabili nthawi inja ife kukopeka nanu lero munagopita kukamuphetsako chilima inu kumabwerako ndiye muliena nthawi inoyo mukanadenkha kuyamba kulingalira pazomwe munachita aaa

  • @Syakinongwa
    @Syakinongwa Před měsícem

    Team up and cartel leadership positions within your team. Otherwise forget individual-party leadership as there is no way you can beat MACOPA.

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh Před 28 dny

    Iwe Mtambo leka bodza unatiputsitsa padzana kulankhula ngt zamzeru kma sitingakhulupilire munthu ngt iwe

  • @user-bv8wo2fn4e
    @user-bv8wo2fn4e Před měsícem +1

    I hope if all mupoto must vote for AFORD

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 Před měsícem

      Mtamboyu akunena zoona nthawi Chihana Senior UDF imamunyengerera chifukwa Chihana anali ndi MP ambiri anali ndi mphamvu koma chifukwa chakugawanikana alibenso mphamvu

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Před měsícem

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @user-jn9tz3li3v
    @user-jn9tz3li3v Před měsícem

    Mtambo mpaka kumuziwa Mulungu kkkkkkkkk ndale ndizovuta

  • @user-wk7ut7ld1x
    @user-wk7ut7ld1x Před měsícem

    Mtambo you are Malawian julias malema and your party aford you get 9% of the votes that is my prediction

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Před měsícem

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Před měsícem

    Chipani cha UTM chija ayamba kuchikanganirana. Chizungu chake SCRAMBLE FOR UTM. Ena apita kwa Aford, DPP ndipo ena atsala ku MCP. Thats my opinion. You got yours take it or leave it.

  • @emmanuelsambo1158
    @emmanuelsambo1158 Před měsícem

    It was only SKC

  • @chrisboyce2
    @chrisboyce2 Před měsícem +1

    UTM ikuyenera ibwerele ku DPP ndipo Ife angoni a ku Ntcheu tili ready kudzawavotera DPP Pamodzi ndi UTM ngati alliance

    • @KikaImran
      @KikaImran Před měsícem

      You re very right. Sindinavoteko and if DPP coraborate with UTM i ll vote for them though am 100% sure that andale ndi oipa onse, they re there for their empty bellies

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Před měsícem

    Koma chaka chino ziliko ndithu.

  • @MosesNyalugwe-ll8hh
    @MosesNyalugwe-ll8hh Před měsícem

    Maloto achumba

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Před měsícem

    Kkkkk mtambo sungatunamize adah ndife a utm we are together with DPP

    • @spargomw
      @spargomw Před měsícem

      I agree with you 100%❤❤

  • @chrispinechirwa2655
    @chrispinechirwa2655 Před měsícem

    Ili ni lirombo yayi 😂😂😂😂

  • @josephgabriel1016
    @josephgabriel1016 Před měsícem +3

    Timothy sangatinamize for the second time.....

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Před měsícem

    Koma a Enock muchenjere ndi mtambo,mugawana zida 2025 isanafike chifukwa aliyense akuyankhula ngati ndi president payekha.Nanga mmene akuyankhulira mtambomo akuyankhula ngati vice president wa chipani ngati?Akudziwa kuti kupatula Ku hrdc sangayambitsenso gulu lina lotchuka paokha,nchifukwa chake asankha AFORD.Akuti safuna mpando chonsecho amayankhula ndi zodiak kuti afuna Udindo ngati platform yoti adzikhala influential

  • @chrisgremu740
    @chrisgremu740 Před měsícem

    Ndiye Chakwera akawinaso 2025 Mutani?

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Před měsícem

    Regionalism inamkanika chihana ,you can't win the national presidency without people from other regions.Nthawi zina musanayankhula mudzikhala Kaye pansi nkuuzana kuti kodi izi ndizoyenera kudziyankhula pagulu?Mukuti unduna simukuufuna chonsecho mukudziwa kale kuti simungadzawine u president wa 2025.Ngqkhale iwe mtambo pa ticket ya AFORD sungawine kuchitipa u mp ,nthawi imene munali nduna palibe chomwe munawathandidza anthu aku chitipa

  • @BrightNyoni-yd4ip
    @BrightNyoni-yd4ip Před měsícem

    Mumakwana a hot 265 watching you from lusaka Zambia twatotela sana

  • @BestonChagala
    @BestonChagala Před měsícem

    Vuto ndiloti ena pa imfa ya chilima afuna kutchukirapo.Aford yakhala zaka 30 but no progress koma pano they are claiming to be friends of chilima just to capitalise on the direction less supporters of utm.Ku AFORD kuli ndani odziwa ndale kuposa kaliati?And in terms of popularity utm ili pa mwamba kwambiri kuyerekeza ndi AFORD

  • @Donnex-gn2sf
    @Donnex-gn2sf Před měsícem +2

    Aford akuwona kuti ku UTM kulibe utsogoleri komabe sizingatheke chifukwa a Aford akufuna mpando and UTM nayo yikufina mpando 🤣🤣🤣🤣

    • @user-qp8kh2hj9o
      @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

      Ife tapanga kale ndi UDF musavutike 😂😂😂😂😂

  • @TiyesNayuma
    @TiyesNayuma Před měsícem

    Chitsilu iweyo you failed as a minister

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Před měsícem +1

    I don't trust NTAMBO ,NTambo vuto nngosamudalila Komanso nkovuta kumukhulupilila uyu . Ife aMalawi mukanakhala Ngati Bingu ,mmali ndi munthu wosavuta ,kungomupangila njira ya chakudya basi ,President ameneyo adzakhala WA muyaya. Ngati dziko Lili ndi chakudya ,ma business amayenda BWINO .Koma aaaaa uyuyu ayi mwina

    • @actuarialscience2283
      @actuarialscience2283 Před měsícem

      Ngakhale banja limayenda bwino ngati chakudya chikupezeka. Zovala ndi zina zimaphweka kugula.

  • @user-eh1gn1nj9d
    @user-eh1gn1nj9d Před měsícem

    Kodi imfa ya Chilima mukupangira campaign Mulungu akukanthani ndithu

  • @HappyAntenna-sf9qx
    @HappyAntenna-sf9qx Před měsícem

    iweyo ukumenyela ufulu wako ndalama zakuthela

  • @MercyNkhoma-b6h
    @MercyNkhoma-b6h Před měsícem

    Koma a Mtambo akunena zoona kuti samafuna mpando? kkk