A JOYCE BANDA ATULUKA TONSE ALLIANCE 11 August 2024

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 09. 2024

Komentáře • 241

  • @gumambalule7675
    @gumambalule7675 Před 29 dny +4

    Your Excellenccy Madam Joyce Banda, this is a pure show of political maturity. Ankhalakale pandale ngati inu mukuyenera 4:32 kuphunzitsa atsogoleri amawa good politics like this. What you have done here ndi zodabwitsa komanso zapamwamba. Honestly sindimayembekezera kumva inu mukulankhula chonchi. May God bless you with more wisdom as displayed here

  • @JarvisJames-e9o
    @JarvisJames-e9o Před měsícem +18

    Maganizo abwino Mai we support you from Lusaka zambia

  • @lacksonsiyadi943
    @lacksonsiyadi943 Před měsícem +10

    Akuti koma utm ndi mcp sizingatheke kugwirizananso anaiwala maiwa ??????

  • @SteveniBanda
    @SteveniBanda Před 27 dny +2

    Akufunachani ameneyu nthawi yoseyi analikuti amatani asatipusiseso anthu ayiwalakale

  • @GaryMakhumula-mu3du
    @GaryMakhumula-mu3du Před měsícem +15

    bolako mmayiyu pan'gono Than chakwera, APM my vote 😎

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi Před 29 dny +2

    Joice Banda please mukhale pamndanda woima pa president because ulamuliro wanu unali bolani than utsogoleri ulipowu

  • @MphatsoGoodson
    @MphatsoGoodson Před měsícem +7

    Yes Mai khani ndiimeneyo mwachita bwino mwachako😊

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem +12

    Ndakayika ngati Mcp ingadzawine chisankho chifukwa mizimu inaphedwa kuchikangawa ija idzakhala ili ku chisankho komweko 2025

    • @user-ww4ei5fb7d
      @user-ww4ei5fb7d Před měsícem

      Kkkkkkkk

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Před 29 dny

      @@user-do2cs8nf4b ndipo ndipephelo lal
      Nga daily kuti mulungu atichotsele zikhanilazi zimenezi

    • @SolokingChimzy-yt7dj
      @SolokingChimzy-yt7dj Před 28 dny +1

      😂😂😂😂😂.nanga ngat anthu aja ali kugahena inu muli ndi mphavu yochosa mizimi Yao frm the hello kubwela kuzisankho?

    • @user-ww9rj2wx8d
      @user-ww9rj2wx8d Před 28 dny

      Ndipotu eeeeeeee chakwela mulungu amuone

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před měsícem +9

    😂😂😂😂Akuti anasokoneza UTM singagwirizane ndi MCP Indee mama🙌🙌🙌

  • @limbanikamanga7514
    @limbanikamanga7514 Před měsícem +1

    "Munthu kuti uzitchule mtsogoleri nde kuti anthu azikhuta" - Joyce Banda, circa 2024.
    Anthu ali "eh mfundo koma zimenezi"
    As a country, we deserve what we are going through.

  • @FefieTenisha-du7ge
    @FefieTenisha-du7ge Před 29 dny +1

    I don't understand the level of confidence and faith that harbors in the minds of politicians
    They know they can't win but they dish out money like crazy
    What do they benifit? The godly praises or what?

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Před 29 dny +1

    former president if u were still president Malawians could hv changed for better life for all.

  • @victormbewe7462
    @victormbewe7462 Před měsícem +6

    I think ku MCP kwachuluka kudzikonda komanso dyera

    • @SaidiMbawa-st6bj
      @SaidiMbawa-st6bj Před měsícem

      Sizinayambe lero kutuluka gwilizano pamakhala vuto

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Před měsícem +1

    Thank you Mama Banda,mwazindikira mtunda munakwera uja unaligned opanda madzi,mangotayako thawing,tiyamike poti mwanyamulako miphika yanu ndi madengu omwe.

  • @user-rc3ze2oi7u
    @user-rc3ze2oi7u Před 29 dny +1

    MAI BANDA NDAYAMIKA CHIFUKWA CHA SPEECH YANU YA BWINO YOSANYOZA MUNTHU THAT'S GOOD GOD BLESS YOU

  • @Kamwachale
    @Kamwachale Před měsícem +1

    This is politics at its best. PP is still with MCP, it's just a strategy of dividing votes in the south

  • @chiefmitengo
    @chiefmitengo Před 29 dny +1

    It's obvious Tonse singapitilire , ma cadets akuona ngati PP and MCP zayambana,. Ng'oooooooo😅. Musova. Chakwera and Joyce Bomaaaaaaa❤❤❤

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 Před měsícem +6

    Let's move 😂😂😂 DPP 🎉

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune Před měsícem +5

    Mayi awa anachita kuabela mavote

  • @kagisocollen
    @kagisocollen Před 28 dny

    Thanks so much

  • @chiefmitengo
    @chiefmitengo Před 29 dny +1

    Amene akupanga support DPP ndi asatana ndipo mukalangidwa kumwamba agalu inu afiiti, tchito kutukwana Azimai Basi, munabadwa kuti Kodi? Pitala wanu wamanyiyu kwawo ndikuti? Mama Joyce Banda wakumasulani.

    • @JusticeNyirenda
      @JusticeNyirenda Před 26 dny

      Zako izoooo 🥱🥱🥱 DPP 🥳 kwinaku 💙💙💙

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b Před měsícem +5

    Chakwela chikangawa from Zambia 🇿🇲

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Před 28 dny +1

    Komat muthuy sanatuluke mu mcp

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před měsícem +1

    Paja a Malawife ndi zitsilu akakupasani nsalu basi muzakavotele chifukwa cha nsalu muzizavutikanso muone maiwa anaba ndalama azadya moyo wawo onse komanso zizukulu zake inu mukugona ndi njala 😂😂😂😂

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d Před 28 dny +1

    Vuto amalawi mumaiwala simachedwa kukopeka

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r Před 21 dnem

      Ndipo nde Simukunama. Ndi anthu opepela kwambili

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Před měsícem +1

    Mayi mumachedwa kutuluka Ku mandaku mwayitha our vision is in you

  • @kagisocollen
    @kagisocollen Před 28 dny

    Thanks

  • @fosternyirenda-wo4eb
    @fosternyirenda-wo4eb Před měsícem +1

    Angapezeke ndi namba ya mai Banda ,ndigaireni plz

  • @alickmkatsonga172
    @alickmkatsonga172 Před 29 dny

    This is disadvantageous to DPP, kuno ku southern region we need one unified political block, apoo biii MCP will have a smooth walk over come 2025,
    DPP, UDF UTM PDP zonse from region imodzi

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Před měsícem +2

    Achita bwino kwambiri chipani chilichose chiyime pachokhapachoka ndiye bwino chigawo chapakati pali chipani chimodzi pomwe kumwera kuli zipani zambili kupoto kuli ziwiri

  • @emmanueljelemani4203
    @emmanueljelemani4203 Před měsícem +4

    Munasokonezadi your excellency UTM singapangedi alliance ndi MCP... 😂

  • @DinaRobert-q6w
    @DinaRobert-q6w Před 25 dny

    Am in Tanzania listerning to my former president,I wish I could visit you .but I don't HV transport .what your talking are very fuandastically

  • @CleverChikowi
    @CleverChikowi Před měsícem +1

    I now conquer with UTM's decision of withdrawing itself from the alliance, it was timely

  • @user-mg6jh7ht9i
    @user-mg6jh7ht9i Před 28 dny +1

    Mayi madeya

  • @bamusmajawa1619
    @bamusmajawa1619 Před měsícem +4

    Bwanjiso Nanga a Tonse alliance 😂

  • @HarrisonMwanga-xy4sc
    @HarrisonMwanga-xy4sc Před měsícem +4

    Mai,achita bwino,mcp yatumbwatu,ngati anakalowa okha ku meneku 😂😂😂😂😂moto buuuuu

  • @mathewskapinga5227
    @mathewskapinga5227 Před 27 dny

    Nkhalamba iyi songatsogolere dzoko

  • @Blessings-b7h
    @Blessings-b7h Před měsícem +1

    Palibe cha mzeru chimene mungapange amai ofoira inu chitsilu cha munthu dziko linayamba kusokonekera chifukwa cha inuyo.

  • @ignasiolucianobanda8493

    Basi program ikhale kulandira nsalu aaaaaaa zaziiiiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @user-ji4ed6dl3i
    @user-ji4ed6dl3i Před 28 dny

    Great news

  • @user-xd2uz1bh3l
    @user-xd2uz1bh3l Před měsícem +2

    Apusiseni amalawi opusa wa

  • @chifundoKaluvi-ey5uw
    @chifundoKaluvi-ey5uw Před měsícem

    Mukungovutika boma nila father adadi Peter wamuthalika

  • @GospelMakonyola
    @GospelMakonyola Před 29 dny

    My vote

  • @Mrgfpatrick
    @Mrgfpatrick Před měsícem +1

    Ma civil servants onse avotera JB,chimunthu chimakweza ma salaries ichi😂😂😂

  • @FefieTenisha-du7ge
    @FefieTenisha-du7ge Před 29 dny

    The tonse alliance was an alliance on paper not a pragmatic one...
    It's very unwise and foolish to think that you were part of the alliance
    What contributions did ur party make as part of the alliance for the benefit of Malawians...
    Too late madam former President

  • @SophieBanda-el8ri
    @SophieBanda-el8ri Před 28 dny

    Koma Mesa akuti mgwirizano inali wakuti convention ikachitika ndekuti alliance yatha, nde akamayi atuluka atuluka chiani oti mgwirizanowo palibe watha.

  • @ThokoGomeza
    @ThokoGomeza Před 28 dny

    Mai ndi mai amakhala ndi chifundo mwina tione mai yu

  • @ThokoBanda-c6g
    @ThokoBanda-c6g Před 24 dny +1

    Aibo Jesus 😢

  • @gracesawa-zl6uo
    @gracesawa-zl6uo Před 28 dny

    Congratulations amai 🎉🎉

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Před měsícem +6

    Mmmm inuyo munalikuti a JB nkhani ya njala aaaaa komanso mukumvekeralabe ka chikangawa

  • @RobertCosmas-bo1uo
    @RobertCosmas-bo1uo Před 28 dny +1

    Otsatira DPP kutukwana amatha

    • @user-fh3dn8kt2j
      @user-fh3dn8kt2j Před 28 dny +1

      Eeeee ndipo alibe anzawo mmmm zochititsa mserutu zopanda Umulungu

  • @ExcitedMackerel-pr4bp
    @ExcitedMackerel-pr4bp Před 29 dny

    Kumanga khola mbuzi zitabedwapo zonse zomwe mukuchita apazi😅😅😅

  • @user-kp8zh9qg2m
    @user-kp8zh9qg2m Před 29 dny

    Akusauka kamba ka iweyo ndi amene munapanga zopoira

  • @PempheroAlufandika
    @PempheroAlufandika Před 29 dny

    Asatinamize awa ndiokomedwa Ku domasi komweko koma town sagabwere

  • @GeorgeKambwiri-xr9ri
    @GeorgeKambwiri-xr9ri Před 29 dny

    Mayiwa sungafanize ndi mbuzi ikulamula panoyi

  • @user-wq9ex2sf3b
    @user-wq9ex2sf3b Před měsícem

    Ami mulungu akudaliseni mwatuka kutose a MCP ndi asatana achikangawa from Zambia 🇿🇲 lsk.

  • @pauljosephmakaula6835
    @pauljosephmakaula6835 Před měsícem

    Mupweteketsa mwana wanu ku Quatar....hopefully munakawadandaulila bwana president ku Mzuzu...nanga si ndale izi mukapangila ufulu wa ana ndi azibale...

  • @PeterMalunga-t6m
    @PeterMalunga-t6m Před 29 dny

    Kuthekeni kwake kuti munapanga mseu wake aaaaa amayi apo ndiye mwanamatu kkkkkkkkk ine ndiwakoko aa

  • @MercyHassan-p4e
    @MercyHassan-p4e Před 29 dny

    Mayi wafuko mayi Joyce Banda munatimangira nyumba zamarata pakwanthu ku Balaka ndimakunyadirani mama i ❤ you so much

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Před 29 dny

    Maturity Joice,UTM singagwirizane ndi MCP zoona inapha chilima.olo inu ndimadziwa zimakukhudzani koma simungalankhule

  • @chifundoKaluvi-ey5uw
    @chifundoKaluvi-ey5uw Před měsícem

    Kodi Peter ulikut nakusowa I adadi osati njuchi

  • @LackzenSumbudzu
    @LackzenSumbudzu Před 29 dny

    Mau amphavu amayi

  • @IgnancioKachimanga
    @IgnancioKachimanga Před 29 dny

    Kubwezatu mau amai akuti anasokoneza UTM siingagwilizaneso ndi MCP 😂😂😂😂

  • @KikaImran
    @KikaImran Před měsícem

    Ndipo JB salary increament amaidziwa

  • @LastonAlli
    @LastonAlli Před 29 dny

    More 🔥

  • @MadisonMagesi-t8f
    @MadisonMagesi-t8f Před 29 dny

    Kofunika athuwa kuwarodza basi mbuzi zawathu

  • @FrankHaruni
    @FrankHaruni Před 29 dny

    Alowe akamalidzise khani ya lakemalawi

  • @asahelmachila3026
    @asahelmachila3026 Před 28 dny +1

    Inde Joyce uli hule zoona. Richard Banda had a wife before you, and you
    had your own husband. You alleged mistreatment from your husband in order to be hule laRichard Banda. You grabbed Richard Banda from someone else and distroyed marriages, both yours and Richard's. So iwe uli hule zedi.

    • @user-fh3dn8kt2j
      @user-fh3dn8kt2j Před 28 dny

      Mmmm koma nkhani zake zomwe za ndale zi?????? Uhuu kupempha tsokatu uku za ziii sizikugwilizana achimwene mwaonjeza

  • @user-gj4li2gc8o
    @user-gj4li2gc8o Před měsícem

    This is a gud move to divide southern region votes ,dpp cannot win with these division ,nankhumwa ,atupere,Joyce Banda all from southern region

  • @user-ln3zx6wo4w
    @user-ln3zx6wo4w Před 29 dny

    Mcp tipweteka tonseija yatembenuka yiliku dpp

  • @amoschisisi2070
    @amoschisisi2070 Před měsícem +1

    Ndege ilikuti

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Před měsícem

    J b ndi mbambande amuna ena sangamake

  • @nokosemakolija-xe9do
    @nokosemakolija-xe9do Před měsícem +1

    Ndale za malawi ndi apaseni nsalu ndi t-shirt basi😭

  • @AbdullahaziziAmoswalala

    😂😂😂 ma jokes achuluka ku malawi

  • @KondwaniMunthali-vf1ws
    @KondwaniMunthali-vf1ws Před měsícem

    A iti Ntila,, Khaaaaa!! ❤

  • @AlexManuelMisomali-sv1vn
    @AlexManuelMisomali-sv1vn Před měsícem +1

    No more tonse alliance 😂😂😂😂 so Chakwere, what are you going to do ? And if you think MCP can win 2025 that means you must steal votes something Malawians can't agree and if you think that you can fool Malawians never this can not be happen

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Před měsícem +2

    mcp yàtha bàsi

  • @SellinahMkandawire
    @SellinahMkandawire Před 29 dny

    Koma mkhani ndiimeyo kaya

  • @gracesawa-zl6uo
    @gracesawa-zl6uo Před 28 dny

    Amai ndili kumbuyo kwanu🎉🎉

  • @LysanJames
    @LysanJames Před měsícem

    Allah be with you mama JB

  • @kangungufoundation2020

    Mayi waboza uyu osamukhulupilira zinamukanika uyu

  • @patrickkadzeya3020
    @patrickkadzeya3020 Před měsícem

    Akuzotembelera okha amene akukutukwani.Mulungu akudalitseni
    Mayi.

  • @johnlodzani958
    @johnlodzani958 Před 28 dny

    Mwakhutakhuta 4years mwaganizano zobwela kkkk

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo Před měsícem

    Mayi oputsa inu muluzi anakhala akunena kuti mcp musazaivoterenso koma mai inu ndi Chilima mwafera kusata

    • @spargomw
      @spargomw Před 29 dny +1

      Kusamva, onse nd Chilima. Lero Chilima kulibe

    • @RuthBandula
      @RuthBandula Před 29 dny +1

      Mawu akulu akoma akaonekela.taziona Muluzi amanenadi,koma kusamva kwathu😢😢😢

  • @user-nj4pn8gx7y
    @user-nj4pn8gx7y Před měsícem

    Mwachita bwino kuchoka ku CHIKANGAWA kuja❤

  • @BenardChitera
    @BenardChitera Před měsícem

    I support you more 😊

  • @ChikondiChakwiya
    @ChikondiChakwiya Před 29 dny

    Chaka chake ndi chino muphwetekana

  • @user-nj4pn8gx7y
    @user-nj4pn8gx7y Před měsícem

    Tili pambuyo panu Mai ❤❤❤❤❤❤❤

  • @JoshuaNyirongo
    @JoshuaNyirongo Před měsícem +1

    Hoping against hope

  • @MADALITSOKALUSA
    @MADALITSOKALUSA Před 27 dny

    💪💪

  • @jestonkalipu
    @jestonkalipu Před 29 dny

    Akubwela bho

  • @kearabetswemashego3084
    @kearabetswemashego3084 Před měsícem

    Tukamulane bas mayi

  • @alfrededwinmadziataika5869
    @alfrededwinmadziataika5869 Před měsícem

    What about *Michael Usi*...when we say he's a MCP member are we wrong?.

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 Před měsícem

    Mesa munathawa Inu mwabwera 2019 cholinga anthu azakuvotereni akuba Inu mai

  • @chesterphiri7523
    @chesterphiri7523 Před měsícem

    And this has now put Manganya in a very difficult situation 😂😂😂😂

    • @JonesChingaya-yf4gg
      @JonesChingaya-yf4gg Před měsícem +1

      Manganya dyera ndimene yamukulira, koma m'mene zinakhalira muja munthu wa nzeru komanso weniweni wa Utm sakanalora u VP.

    • @chesterphiri7523
      @chesterphiri7523 Před měsícem

      @@JonesChingaya-yf4gg my thoughts exactly, I think that he knew something that we don’t know before Chilima’s death.
      And he doesn’t have political capital so MCP can not keep him come next year.
      The best he can do is to eat and get the benefits of a Veep unless if something unforseeable happens to the incumbent president otherwise no political future

  • @user-uf7xt6gp7v
    @user-uf7xt6gp7v Před 29 dny

    Ndi movie imeneyi.ali limodzi ndi mcp

  • @SimeonAbraham-u2j
    @SimeonAbraham-u2j Před měsícem

    Chakwera ndi mayiwa chakwera akuchepa

  • @ChifundoKaunda-m7k
    @ChifundoKaunda-m7k Před 29 dny

    Tsogolo lathu

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf Před měsícem +1

    mayi inu ndi achitsiru satananso chigawenga iwe

  • @kelvinmphande3754
    @kelvinmphande3754 Před měsícem

    My beloved president