ANG'ALULA MOSAIPA LERO PA 10 July 2024

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 9. 07. 2024

Komentáře • 31

  • @TisopeChagala
    @TisopeChagala Před 17 dny +7

    Chawezi asazabwerenso

  • @lysonmhone5425
    @lysonmhone5425 Před 17 dny +5

    Kuswa kuswa
    Kufotokoza mmene ziliri pa ground
    Mavuto anayala mphasa dzikoli
    90% ndi anthu osauka

  • @kennedybanda
    @kennedybanda Před 17 dny +2

    Mosatayitsana nthawi vision 2063 ndibodza lamkunkhuniza ndithu.
    Malawi wachulukitsa usatana.

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 Před 17 dny +1

    Yes chawezi asazabweleso apangisa kuti ine ndisamavele program iyi

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI Před 18 dny +4

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 Před 17 dny +1

    Atsongoleri anthu onse ationongera Mother Malawi......Very sad Nation😢😢😢

  • @HamzaShaff-vo3ci
    @HamzaShaff-vo3ci Před 17 dny +1

    Ngat mukufuna kt tizikupangan for4 mumuchose chawez

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před 17 dny +1

    Program imenei lelo ikumveka bwino kwambiri.
    Tikupempha chonde Chawezi uja asamapezeke kumibawako ameneuja ndiwa Mcp

  • @ChembeWaimba
    @ChembeWaimba Před 17 dny

    Kuyankhura it's simple kungonena mavuto sungatchule mavuto amene tadusamo, wabodza iwe kagwere uko, ine ndiye sunganinamize chilungamo ndikuchidziwa, cadet program muziwonera nokha.

  • @user-lp2sd7lt8b
    @user-lp2sd7lt8b Před 17 dny

    Kabambe anali m'boma kale bwanji sanapange zimene akunenazi

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před 17 dny

    Akalindo aja kungomangidwa ma million akumalowa ku ACC kwawo, ife kutimanga basitu tikafela konko

  • @hopembendela
    @hopembendela Před 17 dny +1

    Malawi we have weak politics if the politicians stop stealing the money malawi will be a better country again

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Před 17 dny +1

    😭😭😭 Malawi wanga

  • @user-cy9zp4fb2m
    @user-cy9zp4fb2m Před 17 dny

    Yes vutodi ndy atsogoleli😢

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki Před 17 dny

    Malawi is not a country it's a farm for politicians!

  • @user-qz3ol8mj2c
    @user-qz3ol8mj2c Před 17 dny

    Very good analysis the question is , what have you done at your level to help the situation apart from making this good analysis?

  • @fredgabrielnyangulu
    @fredgabrielnyangulu Před 17 dny

    Vuto lathu ife a Malawi vision yeni yeni tilibe chomwe timakhala nacho ndi kusintha zipani basi ndipo akabwera zomwe amadziwa ndi kuba . Chomwe chimandinvetsa chisoni munthu walembedwa ntchito ndi amphawi Ndalama zomwe akulandira ndi misonkho ya a Malawi more over amalandira ndalama zambiri ndie ndimadabwa kuti akamapita ku misonkhano ati akufuna allowance za chani ndalama zomwe timawalipira ndi zomwe amayenera kuti azigwiritsa ntchito ndipo ma Civol servant ndi omwe amawononga misonkho yathu chifukwa munthu akulandira ma million koma akuti misonkhano chili chonse cha ndalama za amphawi

  • @ChisomoMandawala
    @ChisomoMandawala Před 18 dny

    Tiyenawoni ma comrade

  • @user-xx4jb9se3z
    @user-xx4jb9se3z Před 17 dny

    Ai dzana 60 .chomwe tapanga bro kuba kupha ndi maulendo opita ku junja pa passport kulibe kkkkk

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před 17 dny

    A Victor mumalongosola bwino, vuto lakula kwambiri zaka 4 zapitazi chifukwa cha Utsogoleri wa Chakwera, sakudziwa chilichonse.

  • @goodwilljeza8419
    @goodwilljeza8419 Před 18 dny +1

    Man subwoofer

  • @rexnyalugwe4910
    @rexnyalugwe4910 Před 17 dny

    Queen Elizabeth hospital mwati unamangidwa liti?

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i Před 17 dny +2

    Zakhala bwino kuti munthu oipa uja chawezi Banda palibepo

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před 17 dny

    Chakwela wapha Chilima

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica Před 17 dny

    60 partys shaaah?

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 Před 17 dny +1

    Kadziko kamalawika mwati kadziko or kamunda?kadziko komvesa chisoni kwambili ndiye kanakakhala kadziko kakakulu akanapanga nako bwanji ngat tikukalephera kukatukula pano?muli nsanje kwambili mujadziko kamalawi,chikondi mulibe.kadziko komvesa chisoni kakang'ono koma zochitika Eeeeh 👹👹👹.tianthu takenso timaoneka ngat tozindikila koma ziro ku 10.mumakhala ngat muli anthu anzeru koma heeee!!zero ku 10.tanzania and zambia ndikaiona kuisilira ngat ndikakhaleko ndisamuke kumalawi.nzimai akuchita kuitukula Tanzania kuona ma bridge amakono.sitima zapantunda koma kumalawi vuto kumangoyang'anana basi kuipidwa ndikuphana popanda kanthu.andale athu malo mopitisa chitukuko amalimbana ndimunthu.malo momanga misewu or ti mabridge tamitsinje tomwetu kulephera ngat boma kukonza ma bridge a standard.malawi mulibe mitsinje yaikulu ikulu yoti mutha kukhala ma bridge akulu akulu.maiko anzathu akupanga zimabilidge zazitali 20 to 50 kilometer koma ife ka bridge ka 1 kilimeter matatalazi kut kamangidwe.azitsogoleli athu ndalama amakhalangati ndizawo akuchosa thumba mwawo osati zathu.look pano misewu yambili ingoikidwa pa central region tinganene zoti zitukuko zambili zangodzadzana pakati komanso ti madevelopment akuphangilato tosekesa kwambili.ndikumanyadila tikupanga chitukuko zopusa basi.tamayendani maiko ena.bvutonso losankha azitsogoleri okut sanayendewa ndizimenezi timakangowa votera azikapeza mabusiness awo.akamadzasiya zitalemera ife kutisiya manja lende iwo ndibanja lawo atalemera.

  • @retirementtoafrica
    @retirementtoafrica Před 17 dny

    Tsopano malamulo amati musanachotse logo yaeni ake anapanga video yi khaya ndi times, zodiak olo mibawa kuti musadzabvutane nawo.

  • @DawoodIssah-mp1yi
    @DawoodIssah-mp1yi Před 17 dny

    Ufulu wotilamulira
    Osati
    Wozilamulira,
    Akulamula dziko la Malawi ndi ndani?
    Akulamula ndi America ndi Britain
    Osamanena kuti ufulu wozilamulira
    Almost more than 90% ya boma or dziko la Malawi zikuchokera
    Or kuuzidwa ndi ma west.

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před 17 dny

    😂😂😂 60 years for nothing shame malawi

  • @wakisawinga2744
    @wakisawinga2744 Před 17 dny +1

    Very sad nation 😭😔

  • @user-ux3ed3ni1p
    @user-ux3ed3ni1p Před 17 dny +1

    Where are SKC reforms? Why is Malawi being held back?