Video není dostupné.
Omlouváme se.

BLACK BOX YA NDEGE IJA AKUTI ILI KU STATE HOUSE TAMVANI ZOMWE AKUNENA

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 13. 07. 2024

Komentáře • 93

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll Před měsícem +10

    😅 Lucifer chakwera , 2025 uzikalamulira ku Maula prison

  • @Mamahashim-xw2bg
    @Mamahashim-xw2bg Před měsícem +7

    Ambuye mulungu wowona zapaziko lapasi ndi kumwamba anthu amenewo awonekere poyera ndithu ayaluke wallah😭😭😭💔

    • @BrownMulipaa
      @BrownMulipaa Před měsícem

      Kkkkkkkk( mbuzi zawanthu amaona ngat abisala

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před měsícem +4

    Fufuzani zonse zibwele poyela, , sakugona Chakwera ndi mizimu , nchifukwa chake wayamba kupemhela lero, wanya.

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před měsícem +1

    Chakwela you mast go ❤

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 Před měsícem +2

    May the souls rest in peace,tisasiye imfa yawo ulele,Malawi tuyeni timenyele nkhondo ufulu wathu,ngati anzathu AK kenya

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz Před měsícem +6

    chikangawa party kumwamba kuli mulungu ndithu prison woyeeeeeee😂

  • @AnthonyMhango-e9q
    @AnthonyMhango-e9q Před měsícem +1

    Thanks for let us known watching in Cape town Athlon

  • @FloraRonard
    @FloraRonard Před měsícem +2

    Ayi zikomo.Mizimu yawo iwuse ndi mtendere

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 Před měsícem +1

    Mulungu malungu mulungu wanga chonde chonde chonde titandidzeni ife

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Před měsícem

    God keep on blessing chakwera

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu Před měsícem +1

    Chakwera he is very wicked man under the sun

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Před měsícem +3

    Kumwamba kuli Yehova palibe chobitsika pansi pathambo

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i Před měsícem +1

    Ambuye mwatisiyila mikango

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja Před měsícem +3

    Zobisika zonse zizabwela poyera

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Před 29 dny

    Zilibwino kuti ili ku state house Ndi kumalo otetezeka kwambili musade nkhawa 😅😅😅😅😂😂

  • @user-px9jd9co3v
    @user-px9jd9co3v Před 23 dny

    By and by, the truth is being uncovered

  • @DevisonHala
    @DevisonHala Před 25 dny

    Manyazi bwaaaa

  • @CharityMkandawire-t8u
    @CharityMkandawire-t8u Před měsícem +1

    Pa dziko lapansi palibe chinsinsi, nd tikulira ndi amalawi ambiri mulungu akumva ma dandaulo athu

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje Před měsícem +2

    Ambuye ndiwabwino tiyenazoni

  • @KattieKamangirah
    @KattieKamangirah Před měsícem +1

    Ndipo chilungamo chiyende ngati madzi onse amene anatenga gawo pa imfa za anthu amenenewa ambuye awakathe pansi pompano.

  • @user-fd2su4ig1f
    @user-fd2su4ig1f Před měsícem +2

    Saima nawo

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg Před měsícem

    Oh my God
    Ambuye achite nanu inu nonse mudampha anthu awaaaa palibe chinsinsi padziko la pansi

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv Před měsícem +3

    Mitima itsika pokhapoka chakeraxo afe basi

  • @DavidJoel-l5q
    @DavidJoel-l5q Před měsícem +2

    Mulungu wabwino masiku omaliza za chinsinsi zizaululika

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před měsícem +2

    Chakwera akafera kundende 2025 aafune asafune simeneso sitekanditu musawonaso zicomo

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he Před měsícem +2

    Ayaluka bas

  • @HoseKatsekera
    @HoseKatsekera Před měsícem

    mulungu ndiwachifundo, ziwululika

  • @elias.m.chunga
    @elias.m.chunga Před měsícem +1

    Koma mbuli zinazi... GPS? Imatanthauza chani mwati?? 😅😂😅😂

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před měsícem

    Mulungu yekha ndi amene akudziwa koma chilungamo chidziwika

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Před měsícem +1

    Obviously boma la chakwera ndilomwe linapha chilima

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Před měsícem

    Uyuyu chakwerayu murandu ukadziwika bwinobwino akuyenera kukhara Ku perisson

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz Před měsícem

    Wanya basi galu ameneyi chakwela

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Před měsícem

    MCP boma tikayivotelabe

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před měsícem +1

    Chakwera sapuma ndi maliro amenewa, adzazimangilila ameneyu.

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Před měsícem +1

    Alibe manyazi ayima

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Před měsícem

    Kkkkkk sayimanso ndithu

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Před měsícem +4

    Mundege munali zigawenga Ambuye tiyankhulen

    • @eunicesaiti
      @eunicesaiti Před měsícem +1

      😢😢😢😢😢😢😢

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 Před měsícem

      Iyeyu adakwera nawo ndegeyo ndi zigawengazo?

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 Před měsícem +1

      Inenso ndikuti, Uyu agwidwa posachedwa, pakuti Mulungu adzaulula chilichonse kuphatikiza uyu akudzitcha mboni yu.

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 Před měsícem

      @@philemontitusnkhoma7740 angakwere nawo akudziwa kut ndege yo waitchera? Mtsogoleri wathu ndi chigawenga chachikuru. Koma mulungu simunthu. Mzimu wa chilima suzagona mpaka chilombochi chitalangika.. He will never know peace in this world

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před měsícem

    Apodi ndekt anthu amenewa anali mudege mommo

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Před měsícem +1

    Chakwela ndiwakupha

  • @michaelamon9691
    @michaelamon9691 Před měsícem +2

    Koma yaaa, papa muli NDI bodza

    • @petertaulo8014
      @petertaulo8014 Před měsícem +1

      Iwe ndiye kape kwambili, nkhani yoti ilipalipose.

    • @MercyChimaliro-fi6mv
      @MercyChimaliro-fi6mv Před měsícem +1

      Ngati ndi bodza ndiye iweyo tiwuze chilungamo chako.

    • @Jasper-xk9iv
      @Jasper-xk9iv Před měsícem +1

      @@michaelamon9691 iwe macende ako ife zikutiwawatu timufuna chilima

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Před měsícem +2

      Muthu uyu amakonda kuikila kumbuyo chakwela thawi zose mungutu adzakulangani kwambili chifukwa ifa zimenezija aliyese m,pakana panopa samavetsetse muyaluka mwasala pang,ono

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Před měsícem

      @@petertaulo8014pamtumbo pamako galu iwe, iweyo panga wekha GPS uikepo number ya ndege ija ikupatsa option ya black box nde ufufuze uwone Komwe kuli black box galu iwe

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s Před měsícem +2

    Pangani mulimose ife tikufuna zenizeni zibwele poyela

  • @SandreckBezai
    @SandreckBezai Před měsícem

    Iwe ndiopusa udzazindkil okay

  • @patrickscott9086
    @patrickscott9086 Před měsícem

    Km ndye kuli kuyesesa kut chilungamo chisawoneke km Only God knows

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Před měsícem

    😂😂😂 mcp ikukuvetsani kuwawa

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Před měsícem

    mbuli zazikulu ndinuyo kulongolora kwanuko mukuwapasa mapulani kuti akataye blac box mmadzi kupusa basi kamene mwva kukamwa mbwembwembwe kharani chete afufuze chomwe cili mkati mwa black box

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali Před měsícem

    Ayaluka basi chakwera

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Před měsícem

      Kkkk munayamba liti nanu apa nthawi yamalilo mumati poyika chilima chakwera nayeso agone apa kuti mukuwona ngati moyo wachakwera uli mumanja mwanu timvomeleze imfa iliko aliyese adzafa ndindani angamulese mulungu zofuna zake

  • @solomonlapson
    @solomonlapson Před měsícem

    Kodi ndindani ameneyu akulankhulayi,, and channel yake ndi yanji

    • @user-lp8wj3vq4x
      @user-lp8wj3vq4x Před měsícem

      Ukufuna mukamupheso anthu amcp inu. Manyazi bwa

  • @lillynhlema9656
    @lillynhlema9656 Před měsícem

    Ku statehouse yikutqniko

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b Před měsícem

    Chakwela you're evil evil

  • @BenedictChikaoneka
    @BenedictChikaoneka Před měsícem

    Mudzakhumudwatu report litatchula zosiyana ndimaganizo anu.Chakwera ine Ndikuona kut Ali innocent sure.

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Před měsícem

      Ndipo srs akungotekeseka nwini wake aliphee akudziwa choonadi

  • @FrankBaison
    @FrankBaison Před měsícem

    Chakwera amangidwe

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa Před měsícem

    Inu mkususanu kuti ndizonama tatiuzeni black box yilikuti mitumbo yamanu

  • @Jerry-vm6mo
    @Jerry-vm6mo Před měsícem

    Guys olo munene zotani mzanu chilima anapita inuyo muli Moyo nde bola mugosiya nkhani Yii coz palibe chomwe chingatike nde musatinyase so chilima anapita basi zikomo

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Před měsícem

      Srs ndipo or ayankhule motani kunatha uja basi lasala ndi tsiku lachiukitso ndinthawi yokoza mitima yathu osati mabozawa atichimwisa ulele ndithu anthuwa mumutu mwawo kaya muyenda chani

  • @philemontitusnkhoma7740
    @philemontitusnkhoma7740 Před měsícem

    Galu iwe usaoutsitse a Malawi. Kodi enanu mukungoti ndondondo kwa atolankhani abodza awa moti simudadzukebe kuti uyu angifuna kuononga Malawi? Iweyo umati Achakwera asiye blackbox kuthengo komweko mpaka lero? Amalawi dzukani. Sukusulani. Uyu apezeka posachedwa. Mwana wa mfiti

    • @user-qn9vc8em6z
      @user-qn9vc8em6z Před měsícem

      Kagwere uko akutma et? Tisiye ife ndipo tidakamverabe untill 2025 woooooo ku chonguuuuu

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Před měsícem

    Komano minthu akadziwa chilungamo samakhara ndimantha gyz

  • @EdnaChiumia-h4d
    @EdnaChiumia-h4d Před měsícem +2

    Trading Lie's.... Nawe kumwamba sukalowa....let the truth revealed first b4 judging any one

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Před měsícem

    Kut gyz social media simunayizolowelembe stt house yakut?

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Před měsícem

      Panyopa pako iwe ndi Chakwera wakoyo munyera muona simunati

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Před měsícem

      ​@@Musa1828-l5dkkkkk koma ndiye muli srs tuuu nganti amako alibe

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Před měsícem

    Mulungu alipo ndipo ifa ya chilima ndiathu ena 8 ziziwika kuti anafa bwanji