BON KALINDO LERO PA 17 JULY 2024 |

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 28. 08. 2024

Komentáře • 124

  • @johnmpatama1461
    @johnmpatama1461 Před měsícem +6

    Watching from Stellenbosch Capetown

  • @SahilluYusuf-sk7es
    @SahilluYusuf-sk7es Před měsícem +2

    He us totally true to convince us ,anyera many I aMCp.Even UTM was there because of Chilima

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Před měsícem +7

    Anthu safuna ku sogolera dziko ayi amafuna maudindo ndi ndalama palibe chazelu chomwe angachite

  • @DanielKatengeza
    @DanielKatengeza Před 10 dny

    Watching from Spain

  • @AlickDaud
    @AlickDaud Před měsícem

    Watching from Botswana the Dcccccc

  • @JohnfosterNkusengwa
    @JohnfosterNkusengwa Před 11 dny

    Watching from cape Town pa boma the DC

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Před měsícem

    Watching from S/A

  • @OsmanGift-f4p
    @OsmanGift-f4p Před měsícem +1

    Watching from SA cape town langa. Bon kalindo you the powerful do not just leave like that help Malawi from this creaminals

  • @KayRolly-l7n
    @KayRolly-l7n Před měsícem

    Watching frm Johannesburg. This man is wise.

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm Před 12 dny

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri chilungamo chiyende ngat madzi umakwana Iweyo

  • @aubreykatembe3081
    @aubreykatembe3081 Před měsícem +1

    Takawabanduledi DC

  • @AngolanChinga
    @AngolanChinga Před měsícem

    I'm hear cape town khayelisha but i love bon kalindo always God bless you bro

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Před měsícem

    Tell them,watching from Durban South Africa ❤❤❤❤

  • @CHRISSYBALALIKA
    @CHRISSYBALALIKA Před měsícem +1

    Kuyankhura chilungamo osaopa aliyense 🔥🔥 more fire DC

  • @HamitonFrank
    @HamitonFrank Před měsícem +1

    Watching from Johannesburg the DC

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Před měsícem +1

    50+1 is here to stay.... munangoifuna kuti muthane ndi dpp inu mukuithawa zanu musova

  • @OsimanIbnAkim
    @OsimanIbnAkim Před měsícem

    The DC munthu ooooopsa💪💪💪

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Před měsícem +2

    Chilima anatisiya ,Koma UTM ,mupangisa Kuti chipanichi muwononge ,Kalindo ndizowona akunenazi

    • @VincentMagriva
      @VincentMagriva Před měsícem

      Ndipo they need money olo zot tsiku limene Dr saulosi chilima anakumana nalo mosayembekezela nawonso azakumana nawo anaiwala pa dziko lapansi palibe wamuyaya this is your time ndalamazo ibani koma musamale pot pot baibulo limat tsoka ntunde nd nyanja pot oipayoo wasikira komweko

  • @JibuzahDrag
    @JibuzahDrag Před měsícem

    Watching from Johannesburg South Africa

  • @user-gn4mx2es3k
    @user-gn4mx2es3k Před měsícem

    Ine monga Vice DC ndikungogwedeza mutu pa zomwe bwana wangawa akulankhula

  • @EmmanuelMalata-r4j
    @EmmanuelMalata-r4j Před měsícem +1

    Mr Born kalindo more fire mumatiyiimlira❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před měsícem

    Iwedi ndichilombo the DC ndimwana woopsa

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem +1

    Akaliyati bingu anamwalira mmanja mwanu mnachitapo izi mnali anduna nthawi yimeneyo mlomwe mzanu mnachitapo izi nyifwa yikuwawa kufwa kwa kwachilima ambiri mwasangalala kuti mpeze mavoti koma ziwani kuti maw lanu simkuliziwa

  • @UlemuKwilambo-o3j
    @UlemuKwilambo-o3j Před měsícem

    Watching from SA, Bloemfontein free State

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of Před měsícem

    kukamba mosabisa phuma LA mai kaliat ndi bambo njalawa liononga chipani anthu awiri awa ndamene akuchita zinthu mwa phuma kwambili

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Před měsícem

    AniBo umakhwana,tikuverani ndithu,kuchokera kuno ku Molere,masambanjati.

  • @SahilluYusuf-sk7es
    @SahilluYusuf-sk7es Před měsícem +1

    Watching from SA pretoria

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 Před měsícem

    Watching from midland south Africa

  • @KaisiAbdullah
    @KaisiAbdullah Před měsícem

    Watching from Durban the DCEEEEEEEEE my precedent wathu

  • @CharityKangulero
    @CharityKangulero Před měsícem

    Watching from Belleville copetown

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Před měsícem

    Watching from cape town

  • @PaulMwachande
    @PaulMwachande Před měsícem +1

    Mwiniwake oziwa ku ng'alula umakwana THE DC

  • @MariamChipoka
    @MariamChipoka Před měsícem

    Your a hero❤❤

  • @JunaKananji
    @JunaKananji Před 11 dny

    Karido Dc❤🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @JeanChirwa
    @JeanChirwa Před měsícem

    Zoona D C Walankhula Zoona.
    Keep it Up.
    God Be With You Always.

  • @joanaKachiwaya
    @joanaKachiwaya Před měsícem +1

    Ubwino wake wovota ndifeyo tikufuna Mary chilima atuluke aphulitse bomba

  • @YusufChipojola
    @YusufChipojola Před měsícem

    From tete Mozambique

  • @james-zd2nz
    @james-zd2nz Před měsícem +1

    Watching from jhb

  • @AliKaukutu-bo7cx
    @AliKaukutu-bo7cx Před měsícem

    Watching from cape town Mitchell's plan all the from malawi balak

  • @violetpotani
    @violetpotani Před měsícem

    Anthuwa ngamadyera chabe palibe chanzeru chomwe akuchita iwo bola ndalama

  • @AgnessMzengo
    @AgnessMzengo Před měsícem

    😢😢koma zoona a UTM😢koma mzimu wake utikanthe.... A malawi ndife anthu osachedwa kuiwala..... Evance Meleka anaimba kale # Adzakuiwala, uzasanduka nyasi😢chikondi cha pa dziko lapansi

  • @AmosMkandawire-re9pw
    @AmosMkandawire-re9pw Před měsícem +1

    The DC mwana wowopyaaaaaaa kwambiri tell them the truth. From South Africa

  • @LindaChikwawa
    @LindaChikwawa Před měsícem

    Mumakwana mr DC uremu wanu

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před měsícem

    Dc we love you ❤

  • @JascoUluma
    @JascoUluma Před měsícem

    Koma umanena chilungamo chokhachokha umakwana l proud of you

  • @InnocentnMbale-zq8pk
    @InnocentnMbale-zq8pk Před měsícem +1

    Ndalila ine chomwe akuchita sakuchiziwa zoona chilima azimupanga chonchi chifukwa chandalama

  • @VincentMagriva
    @VincentMagriva Před měsícem

    Ndipo they need money olo zot tsiku limene Dr saulosi chilima anakumana nalo mosayembekezela nawonso azakumana nawo anaiwala pa dziko lapansi palibe wamuyaya this is your time ndalamazo ibani koma musamale pot pot baibulo limat tsoka ntunde nd nyanja pot oipayoo wasikira komweko

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw

    I'm hearing live from khayelitcha Barracks ( Capetown)

  • @BettyByson-t4z
    @BettyByson-t4z Před 12 dny

    Flom phalombe mbambande bon,

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Před měsícem

    We will stand as UTM forever

  • @masterkachingwe7448
    @masterkachingwe7448 Před měsícem +1

    Mai Kaliyati atsongolere UTM kukhala bata and morale

  • @JonathanChimwaza
    @JonathanChimwaza Před měsícem

    Live from south Africa cape Town

  • @UlemuNewton
    @UlemuNewton Před měsícem

    Zeeeeeeeeee Dccccccccccccccc ❤❤❤❤❤❤❤❤❤kuti khazuuuuuu

  • @MarcRero
    @MarcRero Před měsícem +1

    ❤❤❤❤❤

  • @STEPHENBJNKUMBIRA
    @STEPHENBJNKUMBIRA Před měsícem

    Koma munthu uyu zimagovuta amalangiza vuto ndi ife anthu 50+1 iwewo akuti akufuna kuyichosa analowa boma ndi chani ngati zili zimenezo ndiye kuti anthu aja sakuyenera kukhala pamene paja

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Před měsícem

    Agalu a mcp maka makaka pepe kale ndi ndi Chalakwe,aluga kwasiba

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Před měsícem

    The DC kunena chilungamo

  • @TemwaKabisa
    @TemwaKabisa Před měsícem

    Ulemu wanu Mr DC ❤❤❤❤

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa Před měsícem

    Keep fire burning mr

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni Před měsícem

    Live the DC wa ine umakwana

  • @StanleyDama
    @StanleyDama Před měsícem

    Choka iwe nesa unawauza ndiwe

  • @DOMINICSOKOSO
    @DOMINICSOKOSO Před měsícem

    Ubwino wake Ife tikuyang'ana inu konko make the utm party walks accurate there u r our trust

  • @lonnexjeke6840
    @lonnexjeke6840 Před měsícem

    Ulemu wanu Mr DC❤

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před měsícem

    Number one ❤❤❤❤

  • @user-xv5pr3ji6w
    @user-xv5pr3ji6w Před měsícem

    Tiri pano kumvera ine pat wa patrick, from Pretoria SA

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Před měsícem

    Akhaula amenewo. 50+1 mmesa anayiyambisa ndiiwowo kodi, ndiye lero akuyiopatu powona kuti sangamake.
    Mulingo omwe munamuyezera nawo Peter Mutharika 2025 walunjika pa inu achakwera ndi uhule wanuwo

  • @MarvinChilombo.flourish
    @MarvinChilombo.flourish Před měsícem

    Kalindo akundisokoneza, akuti a UTM akanadekha kaye. Aaaa nthawi ndimene yatha. akufunika apange strategize za 2025 race. After all, divisions are inevitable in politics coz even Kalindo himself can not name Chilima's successor who will be liked by everyone in the party. UTM is running out of time. Rest well SKC

  • @iqrahzaheed8633
    @iqrahzaheed8633 Před měsícem

    Kubandura kubandula

  • @GeorgeWhite-f1p
    @GeorgeWhite-f1p Před měsícem

    👍💪💪💪

  • @Kareemah-y4p
    @Kareemah-y4p Před měsícem

    Koma umanena chilungamo chokha chokha bro mumatiyimilila

  • @user-mf7hf7we2u
    @user-mf7hf7we2u Před měsícem

    Iwe umafuna zimenezi

  • @mrcool531
    @mrcool531 Před měsícem

    Akhale phee ali ndi nthawi? Next year elections

  • @patrickjaenda8288
    @patrickjaenda8288 Před měsícem

    Katundu waboma

  • @lastchipwere4481
    @lastchipwere4481 Před měsícem

    Ngati pali munthu mmodzi yemwe bon kalindo sangamuzuzule ndi Michael usi,,now i beleive

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Před měsícem

    The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo kuyankhula mosaopa

  • @freedahjere2164
    @freedahjere2164 Před 12 dny

    Zamveka ndithu

  • @user-mx5cx3gl4h
    @user-mx5cx3gl4h Před měsícem

    🤣🤣🤣the DC moto

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 Před měsícem

    Kodi inu a Kalindo siinu nomwe mumalimbikitsa kuti UTM choke ku MCP ndipo abwelere ku mene anachokera ku DPP. Ndiye lero mwapeza choyankhula chifukwa zomwe mumayembekezera sizinachitike

  • @DesireLuka-nf5is
    @DesireLuka-nf5is Před měsícem

    ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @sheila5812
    @sheila5812 Před měsícem

    UTM yama kandulo 😂😂

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Před měsícem

    Born kalindo the deceeee

  • @JustinLoka-ed4bx
    @JustinLoka-ed4bx Před měsícem

    😂😂 katundu uyoo

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 Před měsícem

    The D C, mwana oopsa kwambili. Koma kalindo UTM amayikonda kwambili. I will keep saying this now and again

  • @HanunKelekesa
    @HanunKelekesa Před měsícem

    Umakwana

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Před měsícem

    Zosatheka kupha iweo, iweyo ndi mwana oopsa kwambiri ,

  • @pemphero-fo9en
    @pemphero-fo9en Před měsícem

    Mwalankhulako zazelutu lero akalindo

  • @NoelBurton-x1z
    @NoelBurton-x1z Před měsícem

    The DC

  • @cictechnologies1091
    @cictechnologies1091 Před měsícem

    Munthu uyu ndi wamisara ndareka kumuvera

  • @TessMjuma
    @TessMjuma Před měsícem

    I wont be a chakwela 😂

  • @mensuremegrem8330
    @mensuremegrem8330 Před měsícem

    50+1 ilipo ndipo ndilamulo sitilola nanu mulione

  • @amosbula1249
    @amosbula1249 Před měsícem

    Bon Kalindo akunena zoona

  • @ephraimnogwe6430
    @ephraimnogwe6430 Před měsícem

    50+1 idabwera kuzakhala imene inja

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem

    Amai chilimawo sakuziwa kuti anzawo ali pachingalalo kugulisa chipanicha amuna awo sakulira chilima koma kuti akusangalala kulira ife timakuziwa

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

    Mbuli iwe thokoza MCP ndi akatundu pa nkhani za chitukuko komaso ukudya bwino chifukwa cha Boma limeneli ukulinyoza koma ndlama ukulandila from opposition 😅😅😅😅 Munda wako umenewu keep it up mpakana MCP iwina the more ukunyoza the more God's grace and popular MCP will gaining more popular 😅😅😅😅😅

    • @Creslevison-vj2sl
      @Creslevison-vj2sl Před měsícem

      Kupusa ndikulankhula mopanda umunthu apa kagwere uko apa

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      @@Creslevison-vj2sl bola wamva ndithu pajatu anthu amakonda Balaba kusiya yesu wina ndinu bola zamveka mukadakhala mukumvetsera uthenga oti ukupulimutsani bola koma za ndale aaah sorry mzeru mulibemo koma opposition ilipoyi or atawona kuti ichi ndi chabwino sangayamikile because alingati satana amatsutsa chilichonse or pasimenti akuuzani kuti mukutithila fumbi nkhani ndi maudindo adziko la pansi kungowavotera mudzanenaso kuti bola yemweuja pa social media sipobweretsera nkhani za kunyumba kwanu ayi kapena kuphunzililapo kutukwana ayiso ndiye sankha wekha panopa ndi chakwera timusapote basi akabweranso wina timusapotenso kuti dziko litikuke koma Izi aaa tikhala pamodzimodzi momwemu

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Před měsícem

      Inetu sindinyengerera pochita zinthu because mbuli zophunzila zachuluka koma zosathandiza dziko koma kumasula dziko ndi kuligawanitsa

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Před měsícem

    Ndalama yimapangisa munthu kupanda nzelu akaliyati mawwona ngati alindi nzelu koma ayi awagula adpp ndi iweyo kalindo mwagulisidwa simukulira chilima ayi nkhani yake ndikugulisa utm

  • @RamadanShafisha
    @RamadanShafisha Před měsícem

    Inu pezani ntchito yoti muzigwila

  • @MoosaChirwa
    @MoosaChirwa Před měsícem

    Chilimalism😂😂😂😂😂

  • @EliasKawuwa
    @EliasKawuwa Před měsícem

    Is that activism,or politics? Osangoqasiwa bwanji,Mesa ndi chipani chawo,Mesa iwe unachokamo? Aaaaa asiyeni ndi chipani chawo, ndani safuna kudya?

    • @oskidooscar7468
      @oskidooscar7468 Před měsícem

      Kkkkkkk
      Iyeyi amamuopa manganyanso

    • @sheila5812
      @sheila5812 Před měsícem

      Paja amapangira ma drama limodzi 😂​@@oskidooscar7468

  • @user-rt6rd1em8y
    @user-rt6rd1em8y Před měsícem

    😂😂😂😂😂😂

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t Před měsícem

    Dc kuyankhula mopanda mantha 😅

    • @NovassTambala
      @NovassTambala Před měsícem

      Your the best, washing you form cape town graders