GWEDE GWEDE 16MAY-CHIPANI CHA AFORD CHAMUITANA CHIHANA KU DISCIPLINE KAMBA KA NSONKHANO ADAPANGA APM

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 15. 05. 2024
  • Malawi waipa
  • Zábava

Komentáře • 38

  • @LukaAron-el5qh
    @LukaAron-el5qh Před 15 dny +3

    Bola inuyo osati garu chawezi mbuzi yamunthu sapota wa mcp otukwana amalawi

  • @WarezGroup
    @WarezGroup Před 15 dny +2

    Komanso APM BOMA 2025
    Palibe WINA
    APM my vote

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u Před 15 dny +3

    Koma steve konda banda uli ndi ulemu ndi amalawi osati galu chawezi kodi mwamuyitanilanji kùmibawa akufuna anthu azida ndi mibawa tv yabwino chawezi usamale usamapite pa pa tv utaledzela panya pako

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 15 dny +2

    Chawezi awononga tv yanu galu ameneyu

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Před 15 dny +2

    Inu ndiye mumaima pa chilungam km si galu uja Chawez ndi nyani wachabebr

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 Před 14 dny

    Chawezi ❤❤❤❤umatha kulankhura mwachifundo mwachisoni mwa bwino momveka bwino

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 Před 14 dny +2

    Follow how professional times tv is with it's kwagwanji and hot current osati zoyankhula ngati program mumapanga kuti muzionera nokha

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms Před 15 dny +1

    Yah but forget about mcp 2025

  • @ZapitaSamalani
    @ZapitaSamalani Před 13 dny

    Akuluakulu chilungamo chiyende ngati madzi kaya wagwilidwa ndi amuna kaya akazi lamulo ligwile ntchito basi mavenda enieni amadziwa poyala katundu wawo

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před 15 dny +2

    Apm boma

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Před 15 dny

    Good message guys ❤

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 15 dny

    I like you guys ♥️♥️♥️♥️

  • @Moffat-oi4yx
    @Moffat-oi4yx Před 12 dny

    Kondwa Banda ndi wabodza mukunyadila ndalama zangongole muzabweze ndinu pamodzindi ana wanu amenewo akazachokapo 2025

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll Před 15 dny

    Ali zunguli zunguli ntchalitchi atavala jejete Yolanda 😂😂

  • @ShabaniKuswere
    @ShabaniKuswere Před 12 dny +1

    Aaaa Shame guys penapake tadzilankhulani pozindikira kuti kuliso mawa. Ngati anthu ambiri akudandaula munthu mmodzi zoona inu osadzifusa kuti why munthuyu? Chawezi mukapanda kumuchotsa zionetseratu kuti inuyoso mwagulidwa ndi mcp paja mcp iripa plan yogula anthu media

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 Před 15 dny

    Zoona amadziwa akakavota 👍

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d Před 15 dny

    Ndichifukwa chake dziko la Malawi silimatukuka chifukwa Cha m, sanje ndi khaza

  • @jameskachulu8141
    @jameskachulu8141 Před 15 dny

    Apm boma ine kuno ku south Africa ndi magulisa agalu koma anangondiuza malamulo amagulisidwe akhe sanandilande

  • @JosterDick
    @JosterDick Před 15 dny

    Mmm koma konda Banda ndiwa mcp kuyambila kale kale nthawi imeneyo mukukhala kuchiwembe. Nde zomwe mumayakhula zopepelazi pena ife sitimadabwa nanu😂😂😂😂😂😂😂

  • @WarezGroup
    @WarezGroup Před 15 dny

    Zowonadi
    Timava kukoma
    Ndi mibawa t/v

  • @honourablemcgregorysc97tv

    Mumakwana ndi Gwedegwede

  • @user-sj5bl7hw4o
    @user-sj5bl7hw4o Před 15 dny

    Ndende ya ku south Africa akayidi amalowa mbulanda Koma anthu amalowesabe mafoni kudende

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e Před 15 dny

    Ine ndi mkona sindimavera program yanu

  • @francis12fombe54
    @francis12fombe54 Před 15 dny

    Banda banba ndakuthokodza kwambiri ife maveda

  • @PeterFly-mv2nq
    @PeterFly-mv2nq Před 15 dny

    Koma chawezi muchose

  • @DaviebTembo
    @DaviebTembo Před 15 dny

    Kambani zoona tifuna chilungamo

  • @hassammaulana4529
    @hassammaulana4529 Před 15 dny

    Ndimadabwa ma grass a Maso alikuti

  • @user-xc6nl9yh4i
    @user-xc6nl9yh4i Před 15 dny

    Iwe umakamba chilungamo

  • @ThoccoBondo-mx7vt
    @ThoccoBondo-mx7vt Před 15 dny

    Mbambande inuyo

  • @josephgrevaxio2847
    @josephgrevaxio2847 Před 15 dny

    Dpp vote

  • @DicksonMadula-yh6ec
    @DicksonMadula-yh6ec Před 11 dny

    DPP My vote

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 Před 14 dny

    Achawezi mukuti akunyasidwa asamaonere uko nde kuononga bznes yaeni, Zina kulibwino osayankha simufa be professional my brother. Izi zomati siyani kuonerazi mmmm doesn't sound professional

  • @uchizJoelMumba
    @uchizJoelMumba Před 15 dny

    Mcp 2025 boma kale

  • @DidaMtenje-th3uo
    @DidaMtenje-th3uo Před 13 dny

    DPP my vote 💙💙💙💪