Koma steve konda banda uli ndi ulemu ndi amalawi osati galu chawezi kodi mwamuyitanilanji kùmibawa akufuna anthu azida ndi mibawa tv yabwino chawezi usamale usamapite pa pa tv utaledzela panya pako
Mmm koma konda Banda ndiwa mcp kuyambila kale kale nthawi imeneyo mukukhala kuchiwembe. Nde zomwe mumayakhula zopepelazi pena ife sitimadabwa nanu😂😂😂😂😂😂😂
Achawezi mukuti akunyasidwa asamaonere uko nde kuononga bznes yaeni, Zina kulibwino osayankha simufa be professional my brother. Izi zomati siyani kuonerazi mmmm doesn't sound professional
Bola inuyo osati garu chawezi mbuzi yamunthu sapota wa mcp otukwana amalawi
Komanso APM BOMA 2025
Palibe WINA
APM my vote
Koma steve konda banda uli ndi ulemu ndi amalawi osati galu chawezi kodi mwamuyitanilanji kùmibawa akufuna anthu azida ndi mibawa tv yabwino chawezi usamale usamapite pa pa tv utaledzela panya pako
Chawezi awononga tv yanu galu ameneyu
Inu ndiye mumaima pa chilungam km si galu uja Chawez ndi nyani wachabebr
Chawezi ❤❤❤❤umatha kulankhura mwachifundo mwachisoni mwa bwino momveka bwino
Follow how professional times tv is with it's kwagwanji and hot current osati zoyankhula ngati program mumapanga kuti muzionera nokha
Yah but forget about mcp 2025
Akuluakulu chilungamo chiyende ngati madzi kaya wagwilidwa ndi amuna kaya akazi lamulo ligwile ntchito basi mavenda enieni amadziwa poyala katundu wawo
Apm boma
Good message guys ❤
I like you guys ♥️♥️♥️♥️
Kondwa Banda ndi wabodza mukunyadila ndalama zangongole muzabweze ndinu pamodzindi ana wanu amenewo akazachokapo 2025
Ali zunguli zunguli ntchalitchi atavala jejete Yolanda 😂😂
Aaaa Shame guys penapake tadzilankhulani pozindikira kuti kuliso mawa. Ngati anthu ambiri akudandaula munthu mmodzi zoona inu osadzifusa kuti why munthuyu? Chawezi mukapanda kumuchotsa zionetseratu kuti inuyoso mwagulidwa ndi mcp paja mcp iripa plan yogula anthu media
Zoona amadziwa akakavota 👍
Ndichifukwa chake dziko la Malawi silimatukuka chifukwa Cha m, sanje ndi khaza
Apm boma ine kuno ku south Africa ndi magulisa agalu koma anangondiuza malamulo amagulisidwe akhe sanandilande
Mmm koma konda Banda ndiwa mcp kuyambila kale kale nthawi imeneyo mukukhala kuchiwembe. Nde zomwe mumayakhula zopepelazi pena ife sitimadabwa nanu😂😂😂😂😂😂😂
Zowonadi
Timava kukoma
Ndi mibawa t/v
Mumakwana ndi Gwedegwede
Ndende ya ku south Africa akayidi amalowa mbulanda Koma anthu amalowesabe mafoni kudende
Ine ndi mkona sindimavera program yanu
Banda banba ndakuthokodza kwambiri ife maveda
Koma chawezi muchose
Kambani zoona tifuna chilungamo
Ndimadabwa ma grass a Maso alikuti
Iwe umakamba chilungamo
Mbambande inuyo
Dpp vote
DPP My vote
Achawezi mukuti akunyasidwa asamaonere uko nde kuononga bznes yaeni, Zina kulibwino osayankha simufa be professional my brother. Izi zomati siyani kuonerazi mmmm doesn't sound professional
Mcp 2025 boma kale
You mad
Ukulota Dzuka uliko😂😂😂
Kweni iwe
Zakutulo ase
DPP my vote 💙💙💙💪