APM Sanaluze Zisankho Mu 2019 Ndi Mu 2020 - Innocent Mutholo
Vložit
- čas přidán 21. 05. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, says that in his opinion, when he analyses the number of votes cast for APM in 2019 and 2020, APM won the election free and fair.
Pa Nyasa VoiceBox, Innocent Mutholo, wati malinga ndi maganizo ake, pamene amasanthula mavoti a APM mu 2019 ndi 2020, APM adapambana pachisankhocho mwaufulu.
#malawi
Apapa chofunika tilape mulungu akhululukile Malawi chifukwa chakwela akadapanda kulamulila dziko la Malawi dziko la Malawi kukanakhala khondo yoopya chifukwa athu amafuna chakwela kwambili ndipo mulungu adalola kuti ateteze Malawi kusakhale khondo koma chakwela alamulile kuti athu adziwe kuti sakwela si muthu oyenela kutumikila dziko ndipo amaene amafuna chakwela aona okha kuti chakwela si muthu
Ndiye anthu akalore kut munthu mmodz yekha galunso ndiwuyo akabwerese nkhondo
@@chrisneySwanepoel-yu5vd ambuye atithandize
Zowonadi
Very true,amalawi avutika mokwaila,chifukwa cha adindo anjiru,mwaona zimene amapanga Mulungu, disorganized of Ministers chifukwa mulungu anakwiya,zonsezo Mulungu akuona,tionana 2025 sitilola zopusa zilizonse kudzikolanthu la Malawi
Uku ndiye kuyankhula kwenikweni kwas chilungamo .....
Mr game changer ayi ndithu mumaziwa kuyankhula kwambili
I by myself personally I agree with this man, game changer he is 100%right, anaba boma a tonse alliance,
Zoonad kwambiri Mr. Gama changer💪💪
Koma chakwera mulungu akuwone Malawi panopa wukuvesa chisoni Kuti wudye mavuto okhaokha
Very true
50+1 must be abolished
Im agree with you game changer
Come on Brother man game changer.
I agree with you Game changer🎉
God remember us🙌🏾
Uku ndiye kukamba Mr game changer continue fighting for Malawi, Malawi open your eyes
❤❤❤❤❤ zowona DPP Vot kujoni Kuno kwatopesa mwina tingabwere kwa2
And God remains big judge even if earthly judges rule otherwise
Ma Judge aku Malawi ndi adyera, amagwira ntchito akuyang'ana Umphawi wawo😂😂😂😂😂. Alipo oweluza wa Chilungamo ndiye Mulungu basi.Ma judge nawoso akayankha Milandu pamaso pa Mulungu.Kazilandiran ndithu ma Envelope'wo nd zomwe zikakhale Mboni zanu kumwamba
Ngwira tnchito akupasa ndalama msatiputsitsepo apa
Keep it up brother
Chulungamo ukuyenda ngati madzi okumva wamva osamva asamve ndipo tikumvutika kwambiri kuno ku malawi chifukwa cha MCP Chakwera Chakwera ndi Chilima UTM 😢😢😢 Abuye chitanawoni anthu amenewa
That judgement was not fair indeed
Manyaka aboma...mbuli zenizeni zankhanza
Tikufuna anthu ngati inu
Two blind persons can not lead each other properly for both of them are unable see what is ahead of them.
Ngakhale mayi Jane Ansah anenanso kuti APM ndi amene anawina ndipo chisankho chinayenda bwino
God bless you malawi wafika pa Zimbabwe lelo 2025 kumvota no ID ngati akufuna dzimenedzo polembetsa mamvoti popo pakakhale elembetsa ma ID chilinga aleyetse atsalephele kumvota chifukwa cha alibe ID dzikalepheka apo bolani vote ilepheleke adzilamula popanda kumvota kutsiyana kuti atibele tikuwona Maso anthu alephela chimene akufuna adzilamulilbe chiyani kuwopa mulandu bwanji
💪💪💪🔥🔥🔥
Totally true
Zowona big brother 🙏💕♥️
Osawopa Bwana tili nanu
Zoonadi zolanda
Gooooio !!!!!
Alekeni athana okhaokha a tonse alliance wo. Ayamba kale.
Fire 🔥🔥 plus 💪💪
Kunena soona malawi wata boma lamalawi rochimtisa manyasi chivukwachani kumalawi kukukanika 🇱🇾😭
Mutichitire chifundo mulungu pautsogoleri uwu
💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼💪🏼
Achule awa achoka basi tizikavota ngati amalawi zoona ndithu
Ndizoona. Anaberadi
Amen
True,
Maka maka chilima mulungu athane nawe ndipo unapanga zonyasa kwambiri ku dziko lino lamalawi
Munthuyo ndi sapota wa dpp, ndiye mukuona ngati anganene za nzelu?
Mulungu awalange ma Judge amenewa.
Speak Game changer!!!!!?
Kodi monse munayambila muja kuti mupita pa mseu muzapitapo liti pomwe zinthu zikupitilila kuwonongeka???
TIZALOWA AMBIRI PAMSEU
Big man bwanji simutumiza ma audio a dj munyanane pepani ngat ndalakwisa kufusa
Simukulakwitsa tiyesela tiziponya mungoti tipatsa ka mpata pang’ono
Kkkkkkk game change ❤
Koma antnhu amaziwa kutsata nkhani
Eeeeeeee Apm anaberedwa
Mumakwana Mr game changer
Zen zen
Zoona zimezo
Ndiye ngati ukulimbana ndi majaji mbale wanga ndi dpp yakowo mulipamabvuto ndithu amene akutumawo akupweteketsa mbale wanga
MCP, yawonga zambiri.
Kodi APM , mukunena galu wakupha ma albinos ndi kuba ndi chisale
Mukuganiza ngati mwanatu mesa achakwera amamufufuza sanamupedze ndi mulandu uliwose
Kodi ku mcp kuribe wina wazeru
Chakwela Ali ngat Hule wa pa saloon yemwe amazazionesa ngt munthu wabwino koma Ali ooopsa kuposa hule yemwe Ali ku Bar
Panopa MCP yayamba kuchotsela masiku, DPP yayamba kuwengela masiku
Chilungamo chimawawa,Koma mnthu wayankhula chilungamo uyu.
Chi christu nthawi zina sichiri bwino, a chakwera ndi a khristu, zikuchitikazi ndi panichimeti kwa amalawi onse, chakwera ndi tonse alliance ndiakuba anaba boma kuli ndalama kukhala bwanji
Chakwela woyeeee mcp m'paka 2063
Ndip iwey ulem wak srs chilungam chikuveka bwin kwambir
Galu iwe
MA judge pawo pawo ndthu
Chitsime chakudya chimaoneka chikaphwa
Mulungu akuwona zonsezi tsiku la 40 lidzawakwanila anthu amenewa
Mau amphanvu 👊 👊
Dzuka Malawi dzuka
A munthalika amagona kwambili that's why analandidwa dziko....nanuso mukuyankhula kwambili koma action zilo
Kupewa sikupusa anapewa nkhondo
Ndipo ndizoonadi mulungu samalakwitsa amafuna athu amuone chakwela kuti si muthu oyenela kutumikila Malawi
Umafuna Peter apange nkhondo mbuziwe
A judge amenewo tidzawamanga
Kuyankhula kwabwanj uku mumafuna ayambitse nkhondo?
Majaji ndi amene ayika amalawi pamoto
Kkkkkkk
Zoonadi munthu wamkulu
Galu wa dpp kulila mobangula ndiye sunati ukanalila mcp 2025 boma kale
Dzinazi osamatengela kut bambo anu anali a mcp kapena a dpp koma kumaona kut nziko mwathu zinthu zikuyenda? kapena ayi ngati mumamwa tea sikuti ndi azibale anu nso onse akumwa tea ayi akuvutika mukatengala ku muziti simunaati muziwe kut azibale anunso ali mugulu lomwelo lomva zowawa
Zitsilu za nyau inu wamzelu angavotele mcp panomso?
Kumalikonda dziko lako osati umoyo wako ayi anthu akumva kuwawa
Malawi panopa akuvesa chisoni machine opanga mapassport sakugwira ntchito panopa machine wopangira ma ID akuvutaso Koma chakwera wuziwe komwe wuliko Kuti wulamuliro wako ndi mulungu yemwe ndiwokwiya ndi iwe
kkkkkkkk......Nebukadinezera uyu
Ku Lilongwe kuli machine 8 opangila ma id pomwe ma district ena ndi zero
Mutholo ndi anzako achina Ben Longwe mupeze zochita, what you're doing is not activism, this is stupidity of its highest order, mwasanduka oyankhukira zipani, zopusazi tasiyani, ngati mukufuna u activist pitani ku school mukaphunzire osati kumasokosa ndi zopusa zanuzi.
Akunena chilungamo, chilungamo chimawawa. Why 50+1, why alliance yet anakana a mec fresh vote registration? Don't you see kut the same rules of 2019, could apply for the fresh 2020 election
Simungavumeleze
Mau Amphamvu ngati amenewa tamva ndithu