Chilima Simtsogoleri Wabwino - Bon Kalindo

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 31. 05. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo says, Vice President Saulos Chilima is not presidential Material. If he was he would have show solidarity with the poor Malawians who are suffering under Tonse Alliance.
    Ku Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo akuti, Vice President Saulos Chilima is not Presidential Material. Akadakhala akadawonetsa mgwirizano ndi Amalawi osauka omwe akuvutika pansi pa Tonse Alliance.

Komentáře • 82

  • @Luxemaven8686
    @Luxemaven8686 Před 22 dny

    Bon Kalindo you have gained a supporter!!!!

  • @user-qq1uj7ct6n
    @user-qq1uj7ct6n Před měsícem +2

    booooon kalindo Mo fayaa. keep on to give us truly updates. inu mumalankhula chilungamo chokha chokha

  • @user-tb6yh1kx3o
    @user-tb6yh1kx3o Před měsícem +2

    Honest speaking Mr DC Big up

  • @LoyidKarebe
    @LoyidKarebe Před měsícem +1

    Go ahead Mr kalindo we are following you

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 Před měsícem +2

    Mukunena zoona big, koma mmalawi opusa akuona ngati chilima ndiwabwino

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y Před měsícem +10

    Komatu a Kalindo munthu osamuipitsa choncho. Inu musamunene Chilima kuti oipa lero. Mwagwira naye ntchito limodzi. Kuipa kwa munthu amadziwa ndi Chauta basi. Inunso muli ndi zonyansa zanu.

  • @EagerChicken-qj6xu
    @EagerChicken-qj6xu Před měsícem +3

    Kodi inu mumkamuuza chilima ngati ndani? Osachita naye msanje. Pangani zanu akulu

  • @AlastairGutt
    @AlastairGutt Před měsícem +2

    Kalindo is matured now

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Před měsícem

    Chakwera ndi Chilima wooooyeeee,muwaphe A Malawi onse mukatha mutenge mitemboyo muitafune Mukhute,popeza ndalama mwawa bera Kale,koma muziwe masiku amatha ndikugona adaku voterani wokha samaziwa zoti Chibwenzi chankhwangwa chokoma pokwera, Amalawi mukaza voteranso awa izo ndi zanu wanthuwa ndi aka Nyimbi Anunkhisa Malawi.

  • @macksonkalasa9668
    @macksonkalasa9668 Před měsícem +2

    Koma kumanidwa udindo kulira mpakana 4 years

  • @ellahmwams831
    @ellahmwams831 Před měsícem +1

    Mr kalindo moto 🔥 🔥🔥

  • @beakab2378
    @beakab2378 Před měsícem +1

    Zooona zokhazokha, Chilima wakhala duuuuu a Malawi tikulira, olo one day osalankhulapoyi mmene m"boma mukubedwera ndalamamu, nde atifune pano? Ine ndamitsikatu, he won't get my vote

  • @ishmaeldama8906
    @ishmaeldama8906 Před měsícem +5

    Bon he is talking the truth, but u can see other people they talking sheet, be very careful my fellow Malawian, we must wake up guys, zinazi sizotengela kupita ku school, khalani pansi moganiza bwino, malangizo awuleletu awa,all the way from johannesburg

  • @user-zm9sf2mj7u
    @user-zm9sf2mj7u Před měsícem

    Mbambande mr presdent bon kalindo kwathu kwa chulu zinthu sizilibwino tikukhalangati tili mkamwa mwa mikango

  • @RodwellLupiya
    @RodwellLupiya Před měsícem

    Bwana Born Kalindo pqjatu ndinu amene munamukakamiza Chilima kuti avomere kukhala vice president lero mukumunyozaso . Komaso inuyo mumatiuza kuti sindinu wandale koma chosecho mukuwauzaso anthu kuti akqvotere aford , udf kqpenda dpp.

  • @devimatope9980
    @devimatope9980 Před měsícem

    man of integrate😂😂😂 Bonnnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri from Njeza village ..T/A mabuka, mulanje😊😊😊😊😊

  • @esternguluwe
    @esternguluwe Před měsícem

    Bwanji adzangotiimra bon kalindo yomweyo pa u president,akuoneka ali ndi nzeru kwabasi

  • @EagerChicken-qj6xu
    @EagerChicken-qj6xu Před měsícem +1

    Musamuipitsile mbiri a chilima inunso simulibwino.

  • @user-yh3ys3qn6p
    @user-yh3ys3qn6p Před 22 dny

    Chisilu mbuzi 😢😢😢

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Před měsícem +1

    Apadi akunena zoona zaka zonse takhalayi chilima ali.duuuh nde angabwele kwa ife kutiwuza chani ??

  • @BrightKuyaka
    @BrightKuyaka Před měsícem +2

    Zoyankhula za bon kalindo zatitopetsa tsopano, katakwe ndi bakili muluzi tv

  • @user-ic7fq5yn6r
    @user-ic7fq5yn6r Před měsícem +1

    Yes DC akunena zovona

  • @KondwaniMunthali-lx5jc
    @KondwaniMunthali-lx5jc Před měsícem

    Ndiye tivotele ndani utiuze kalindo manyi ako

  • @MercyPhiri-nh9jy
    @MercyPhiri-nh9jy Před měsícem +1

    Zoona amasankha tsogoleri ndi mulungu. Inu musaweluze

  • @JonathanKamwetsa
    @JonathanKamwetsa Před měsícem

    Ipondeni Fadala........ You're a real son of Malawi........

  • @SibwenzaLevisoni-gm6rv
    @SibwenzaLevisoni-gm6rv Před měsícem

    Ndipo nkhaniyi ndioona big up DC

  • @daveskachiphaphi
    @daveskachiphaphi Před měsícem

    Tabalirankon aku mwera usabwere ndi mademo Ako pano pakati chita kwanuko

  • @DesmondKanguwe
    @DesmondKanguwe Před měsícem

    Kalindo ndiwamisala uyu

  • @GiftAsirKhwanya-ok2gu
    @GiftAsirKhwanya-ok2gu Před měsícem +1

    Akunena zoona kalindo

  • @PeterkinsJanuary-fv9wd
    @PeterkinsJanuary-fv9wd Před měsícem

    Bon kalindo ulemu wanu

  • @georgebalala3048
    @georgebalala3048 Před 24 dny

    Shaaaa this was days ago

  • @user-cf9yz3ei5o
    @user-cf9yz3ei5o Před měsícem

    Yes you are really talking

  • @user-ep7cg9bb4m
    @user-ep7cg9bb4m Před 29 dny

    Nkhanira yakwachulu yokha mwapala. Miyambe mwazimvetsa zinthu mmene zikuchitikora. Bwerani ndi ma demo anuwo tione ngati simuyaluka

  • @HakeemJossam
    @HakeemJossam Před měsícem

    anatipwetekesa asabweleso

  • @SanudiJaymofred
    @SanudiJaymofred Před měsícem

    Kalindo to the people

  • @PeterPadambo-kk5oh
    @PeterPadambo-kk5oh Před měsícem +2

    Chilima sanalakwise kanthu, cholinga akawukira muzimunena kuti amangowukira kulikonse? Apa pokha nde ayi, boma ili tinalivotera chifukwa cha Chilima, nde atulukeko chifukwa? Mesa kuli mavoti ake, musiyeni Chilima akhale, nthawi ikakwana ayankhula

  • @WilliamBanda-un5eg
    @WilliamBanda-un5eg Před měsícem

    Dzapangeni nawo compete bwanji because it seems mukudziwa zambiritu

  • @josephchika173
    @josephchika173 Před 15 dny

    Amakomadi akamwalira munthu sure

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před měsícem

    Akutitenga ife uchitsilu pomwe achitsilu ndiyiwowo amalawi asukutsula ngati tinachotsa mbuyawo kamudzi chifukwa chankhadza chakwela nde ndanitso galu kwabasi

  • @Nomsa77
    @Nomsa77 Před 25 dny

    Vchifukwa choti azakhala pa u president ndichifukwa achakwera amuphera.....
    Chifukwa chani mdziko mumalowa anthu osaziwika bwino

  • @CheloyaaChikwatuu-ob2mt
    @CheloyaaChikwatuu-ob2mt Před měsícem

    DC ❤❤❤

  • @ShukuSh-vi1hk
    @ShukuSh-vi1hk Před měsícem

    Ndizoona zimene akuankhula karindo chifukwa nthawi yakampeni ndiiyeyo amene amanyamula thumba la 50 kg sichakwera iyayi

  • @vitumbikokamanga5869
    @vitumbikokamanga5869 Před měsícem

    Chilima usogoleli mlibe ose ndi adyera same like chakwera 😅

  • @ShabanMajor
    @ShabanMajor Před 29 dny

    iwe ndikumenya bwanji mulimbana ndi DC wanga

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx Před měsícem

    Chilima waonetsa kudekha ndipo sadaukire koma kalindo ndale zidakulani

    • @grandwellkatumbi4763
      @grandwellkatumbi4763 Před měsícem

      Dziko likamaonongeka mtsogoleri wabwino sadekha ....chilima akudekha zichani pamene zinthu zikufoila mdziko muno

  • @user-zs9hn3kv3e
    @user-zs9hn3kv3e Před měsícem

    Impossible ngati munthu akugwira ntchito mmboma sangayankhulepo zotsutsa boma man limenelo nde bodxa

  • @BrianBanda-nn1gt
    @BrianBanda-nn1gt Před měsícem

    Ndizoona ndikugwilizana nazo

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w Před měsícem

    Zitsiru ndizomwe zingakhulupilire chilima opusa omwewa ndizomwe zikunamizika chilima zaupresdent alibe nazo ntchito koma iye azingodyelera mimba yakeyo

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 Před 14 dny

    Munthu amakondedwa anamwalira Pamalawi

  • @NtabaKali
    @NtabaKali Před měsícem

    Yaaa

  • @YohaneFoster-vq7wp
    @YohaneFoster-vq7wp Před 27 dny

    Kalindo akufuna atibalalise Ali ndi reason behind

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx Před měsícem

    Uyu ndi wamisala chilima ndi otumidwa so sakadaima mkuyankhula mudakati ndi oukira

  • @SangwaniNkosi
    @SangwaniNkosi Před měsícem

    Chilungamo chimawawa,Koma DPP ayi ziko linaliko bwino mnthawi yimeneyo

  • @SAIKINGFRIDAY
    @SAIKINGFRIDAY Před měsícem

    Eh komatu akulu awa chilima anakulakwilani chani muja munayambila kumunenamuja mpakapano or kukuyankhani osangomusiya bwanji ndiwankulutu ameneuja amadziwa chimene akupanga nde zinazi ife mumatinyasanazo zomalimbana ndimunthu oti samakuyankhani

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před měsícem

    Aaaa chilima angoputsisa MCP tsingapase utsogole chifukwa chakwela akumva kukoma ndibanja lawo lotse nso dzoti chilima akudziwa chilungamo koma manyadzi uchitsilu mutayeni tiwone 2025 dzizatha bwa

  • @BazaarShaibu
    @BazaarShaibu Před měsícem

    Aka ndi kachilungamo

  • @francischikaya3146
    @francischikaya3146 Před měsícem

    Iwe sukuimirira a Malawi koma chipani china chomwe aliyense akuchidziwa. Ukulimbana ndi Chilima nthawi zonse bwanji? Kodi kwinako kulibe zofooka zawo. Usawaike a DPP ngati ndi Angelo lero. Sitinaiwale zomwe amachita padzana paja. Tikudziwa kuti mtunda wa kwanu ndi omweo. Usatinamize ife takana.

  • @giftmingo9293
    @giftmingo9293 Před měsícem

    Boma la Chakwera silizakhala labwino kwaiwe only if utakhala Minister. Unduna sapatsa zitsiru ngati iwe. Anthu a kwa Chulu akakuthibula bwera uzazione. Kulira 4 years kufuna udindo kkk😂😂😂😂

  • @giftmingo9293
    @giftmingo9293 Před měsícem

    Uzitiuzanso za DPP ifeyo lero? Moti ukakhala umati aMalawi angamvere ndithu iweyo kkkk

  • @LovelyGalaxy-rb7yl
    @LovelyGalaxy-rb7yl Před měsícem

    Zinthu zake

  • @user-dy4gc2hr5e
    @user-dy4gc2hr5e Před 25 dny

    Zoonadi zianthu zoipa kwambiri 😂😂😂😂😂😂😂

  • @MalakamMillie
    @MalakamMillie Před měsícem

    Chilima ndi witch craft mbuzi mwana wajoka amati tizidya katatu madzi awulere magetsi awulere fetelizer wochipa. chilima ndifiti kwambili

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o Před měsícem

    Kalindo ngati ndi chamba uzavula galu iwe ukukhale wachilungamo ndiwe mulungu?? Ndiwe galu kwambiri usatibowe uziyankhulira amako ndi anthu akwanuko

  • @henrykapinga1433
    @henrykapinga1433 Před měsícem

    Kkkkkk

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d Před měsícem

    The DDCccccccccccc

  • @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
    @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy Před měsícem +6

    The problem with Kalindo is that he wants to be the master minder of Chilima. But he has to understand that Chilima has brains. My instincts also tells me that he is indirectly campaigning for DPP.

    • @user-se4cf9qp8b
      @user-se4cf9qp8b Před měsícem

      This is true. Kalindo is 4 dpp

    • @EvanceSungani-cv9jk
      @EvanceSungani-cv9jk Před měsícem +1

      In your minds but he talks vry true posatengera za ndale,,,,,and all of this akuya khula ndizoona,,,, nokha mukuziwa mene adalankhulila chilima mu campaign ya 2019 analankhula zambili mbili zokomera Ife achinyamata koma ndzt wakwanilitsapo,,,,,inuso musamangosutsa zilizonse you supposed to see the true

    • @Littlefair7
      @Littlefair7 Před měsícem

      I fully agree with you, Kalindo is taking advantage of illiterate masses.

    • @GRACIOUSKENAN
      @GRACIOUSKENAN Před měsícem

      Which brains dear, you talking about??? No he is bad man also,can he preform good speak today how??

  • @EmilyBakali
    @EmilyBakali Před měsícem

    Kkkkkkkkk

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 Před měsícem

    Izi ndi nkhani za amalawi ngakhale a president anayankha nkhani ya America mu chichewa, translate in English nonsense

  • @angelj3771
    @angelj3771 Před 25 dny

    It a better to dellete this video. You have cursed him