Vendor Ndi Munthu Ofunikila Pa Chuma Cha Dziko - Bon Kalindo
Vložit
- čas přidán 3. 07. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo talks about the importance of the government creating an enabling and business-friendly environment in Malawi to boost the country's economy and development.
Ku Nyasa VoiceBox, a Bon Kalindo akukamba za kufunika koti boma likhazikitse ndondomeko zabwino zochitila bizinesi m’Malawi kuti atukule chuma ndi chitukuko cha dziko lino.
#malawi
Mukhale ndi moyo chikhaleli Mr boni kalindo tsoka kwa iye amene amamunyoza boni kalindo ife timamulekeza chifukwa timamutenga ngati Tate wathu mulungu adzikhala nanu thawi zose ❤❤
Yehova azikusunga ndi moyo born kalindo andalewa chikondi alibe ndi a Malawi komaso nkhalamba za MCP zatizolowela kwambiri