Ku MCP Kuli Nkhanza - Samuel Lwara
Vložit
- čas přidán 10. 07. 2024
- Samuel Lwara, today discusses Intra- Party Politics in the Malawi Congress Party and his experiences dealing with State House.
Samuel Lwara, lero akukambirana za ndale zamkati pa chipani mu Malawi Congress Party ndi zomwe adakumana nazo ndi State House.
#malawi
You are a legend Mr Lwara. I love your wisdom, I wish these leaders had this kind of wisdom. They are so consumed with greed and they can't even see the bigger picture
Munayakhula bwino koma misiye kulimbana ndi APM alibenanu. Zifukwamumuwuzeso chakwela ndinduna zakezose azipanga zawo amusiye APM
Good Messnge Mr Rwala
May Tonse Alliance leaders accost the H E and redress the current national teasers.Learn to canvass amicably to bring solidarity where there is schism.
Zaziii
Greedy and dictatorship is worsening in Malawi is the poorest country in the world.
Ine ndimadabwa Kodi athu akusaka inu amenewo ana awo alibe kuti muwapheleso ana awo kuti AVE pain Mene imawawila?
Inu ndimakusatani koma pamene mwamunyoza peter takutulukani iweyo munthu wako sukugwira ndi wachabe
Inuu mafuna aziku sangalasani inuu nwauponda
Ati kuchipatala ndinakumanakp ndi atumbuka anzanga anandithandiza.....kkkkk okheeee😂
Ndmakulava sumaopaso same as DC
Nkaka akulembanso MSCE 😅😅
Ndiopanda nzeru mfiti yopanga ndale usiku
Akulembera kuti
@@user-xt2ic5gg1g Akulembera ku nyumba kwake. Paja MCPigs ndi ya katangale.
😂😂😂Nde ngati ankhonze zikhala ndalama zomwe wa bazo alibe busy kuhonga kuti amuuzire mixeeeee
Mwayankhula bwino Mr Larwa
MCPigs ndi ufiti
Zovuta kwabasi
Chakwela ndi wakuba ndi chifukwa nduna zake zakuba sazichosa chifukwa iyeso ndi mbava ku Kenya president wachosa mbava zonse koma Galu ayi chifukwa naye mbava
Give people direction not just talk
Zikhale ng'oma ndi kapee
Mcp timayidziwa tikadwabwakuti mukati yasitha komatikadziwakutisinasithe mwanawasatna oroatasaduka gero sarrepherakuchitazakwao
High five