A Chakwera Ndi A Mutharika Onse Ndi Olephela - Samuel Lwara
Vložit
- čas přidán 9. 07. 2024
- On Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara says neither His Excellency Dr Lazarus McCarthy Chakwera nor former president Prof Peter Mutharika are fit to rule this country. They are both failures.
Pa Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara wati Olemekezeka Dr Lazarus McCarthy Chakwera kapena pulezidenti wakale Prof Peter Mutharika sayenera kulamulira dziko lino. Onsewo ndi olephera.
#Malawi
Samuel you are right ✅ 👌....Chakwera ndi Muntharika...tiwaona zintchito zawo....Onsewa olephwera we.Need New Blood....Mkulu uyu akalankhula chilangamo....zoona zokhazokha......More Fire 🔥 Samuel...👍👍👍👏👏👏👏👏👏
Vuto munthuu akalakhula ngamo mumamuda kma chilungamo chimawawa keep it up nr Rwala
Ukhale president iweyo
Zoona ndithu zimene a kunena Rwara
Ofcz munthalika failed somehow but these one eeeh aonjezaa
I'm really agree with you Samuel , keep it up and don't fear. True true big.
Chilungamo chosatenga mbalin keep up the good job, zitseguleni mitu mbuli zimene zimavotera atsogoleri olephera, 80% ya anthu ovota ndi mabulutu, akufuna Chakwera olephera kubweretsa Mutharika olepheranso.
Ndizoonadi. APM, CHAKWELA, awa ndi anthu olephela, bwanji tiyeseko afford nawoso tione kulephela kwao
Chipani cha dpp bingu anapanga chitukuko kwambiri and ndimachikonda koma president amayenera kukhala wina ku dpp ko , sankhani president wachinyamata ife tikamuvotela , dpp bola singafanane ndichakwera koma ma president tiyese atsopano
Mwayankhula bwino kwambiri, anthu amadana ndi chilungamo
I prefer, Muthalika ataimanso ndi Atupele,
Zikhiza kukhala bwino, akazatopa, mwana azapitirize,
Koma zomatenga anthu isaziwika bwinozi,
5yrs it's not a joke guys
Mr lwara you are number one! Apm and chakwera same what's up group both are fools. Malawi is a cursed country leader ship is worse.
Unaonako dpp ikugula fertilizer ku butchery,kwatsala iweyo akumange mpamene utadziweno kuti pakati pa awiriwa Pali kusiyana.
Apa mwalankhulapo za nzelu lero.peter is not a solution to our problems tinamuyesa kale
Ndizoona onse ndi olephela koma devaluation mmmmmmmm ndiyopweteka kwa achinyamata ogwila maganyu ife APM my vote
Pena pake nanuso Mr Lwara mumaganiza moperewera kwambiri,inuyo mungafanizire Peter ndi chakwera? Like seriously?
Kkkk mwina akufuna aime iyeyo kukhala president kkk
Pa Peter pokhapo ndie wapenga Peter sungamufanizilire ndi chakwera APM akufunika than any one
That's very true , only a patriotic Malawian cannot vote for failed leaders Chakwela and muthalika.
Ndinu achitsilu alwara sungafanizile MCP ndi DPP aaaaa anyamata alipo muboma akupanga chani
Inu ndiye mu kuwona owina ndi ndani, plz musapange zoti wina mungomuioitsa mbiri koma mudzilankhula kuti zinthu zisinthe. Pano tikufuna kuti tisinthe dziko ndiye osinthayo ndi APM zisiyeni zikhale chonho
Akulu ngat Mfundo zakutheran ndibwino kukhala osayankhula kalikonse, inuyo pangan Alliance nd Lyton Mangochi muyambitse chipani chanu coz apapa mwaonetsaso uchitsiru ofanana nd Lyton Mangochi.
Asowa choyankhula awa
Iwe mutharika ungafanize mbudzi ngati chakwela? Iwenso ndi kape kwambiri
Yes Mr Lwarwa thus fact APM thus not a solution
Lwala Mutu wako sakugwila waoneka kale omwe amasankha ndi anthu iweyo sungafanizile Mutharika ndi chakwera , Mutharika anthu amasangalala kwambili kuposa pano ndi chifukwa anakuthamangitsa mnyumba ya Malawi housing, iweyo ziyankukula zako zopusazo amalawi Peter Mutharika wooyee
Naweso larwa izi ife ai. chifukwa a Peter mutharika sungafanizire chakwera never. Pali zambiri zomwe simungafananitse
Kodi bambo Lwara, amene afuna nzake pakati pa Peter ndi Saulosi ndani? Khalani ndi cipani canuco. Kuposa kunena zopusa ngati cidakwa. Kodi wanzeru? Nanga ulikuti ndipo ukutani?
Koma.lero ndee mwayankhula zopepelatu
Peter angafanane ndi chakwera
Inu ndi munthu amene amanena zinthu zimene sadzidziwa. Munapha zipani 9 kukhala ndi kusunga MCP. Lero mulalata?
Ndipo kwambii timufuna atupele mulunzi😊
Yes ur right koma mukananena oyenera muzipanimo
Lawala is looking for chihana but AFORD alone can't win how old was mandera both are candidates let them exercise their freedom
Mnthalika inde analephela Koma anayesesa, kusiyana ndiwomwe alipowa
ndimakupanga follow koma lero wangomunyoza muthalika panya pako ndipo ndakutuluka
Atumidwa awa, akuona ngat titha kusankha iwowa
Bola APM kusiyana ndi chakwera, nthawi ya APM zinthu zinaliko bwino kusiyana ndi chakwera.
2020 mumanenaso Chocho kut alowe anyamata lelo bwanji
Apm ndimunthu wankulu kwambili kuliphika dziko lino
Muthalika satukwana muthu olomodzi ndiwante ndele zd
Iweyo suzakalamba omwe anakubala nd sikana wina nyamata sibwino kwanu kulibe agogo
Mbuli iwe Mtumbuka opanda mfundo atakulanda nyumba ndiye wowowoooo. Ndale zako zilibe tsogolo "mark my word"
As itikut peter alibwino koma tikut apm alikobwino kusiyana ndi chakwera basi
Iwe uzilimbana ndi chakwela otsati Peter ngati wapasidwa ndalama ukazibwedze uyaluka komanso uchita manyanzi 2025
Apm amalize term yake munamulandila nsanje upresident l support Dpp 100%
Alwala mwayamwa tikutulukani mwayambaz,inu nthawi ya DPP mungayerekezere ndinthawi inu.
Inu nthawi ya DPP anthu amamangidwa chonchi or kukwera kwazinthu zinafika apa?
Njara,kusowa kwamankhwala mzipatala,kukwera kwa zinthu mungayelekeze ndinthawi ya DPP
Mulilanaye APM chomwe timadziwa APM sanaluzepo ndewu akamamenyana 1 to 1 kukanikana ndiye mubweletse 1 to 5 ndiye 5 a wine muziti m'modziyo walephela? Anthu adyela Inu tandiyankheni alwara komanso kamenyedye ka m'modzi uyo sikanasithe 40 pelesenti ndiyomweyo anapezanso pa 1 to 1 mulila ndi APM 2025 APM boma
Lwara ndi wa ganyu sasamala za amalawi akungifuna kuti amupatse ndalama koma APM sangamupatse ndalama n'gooooo ozavotela APM ndife amalawi akumudzi amene tikudziwa ubwino wa APM tikufuna feteleza ontchipa ife
Galu nzimayiiwe athu anzeru avotera dppp pitamuthalika amayesetsa kuti athu tizidya chakwera anabwera kudzaba njara yavuta km muthalika zakudya zimatsika ntengo
Kodi osalephela ndi ndani ngati ukutiso peter ndiwolephela iweyo wachitapo chiyani ?
Kuyambila pano usazanyozeso muthalika ndimunthu watendele
Kodi a lwara muli mbali iti
President wanu pano ndi mdani
....jnutu mwasowa kolowera ..
.mmene chakwera waonongela zikoli mungayerekeze ndi apm....inuyo mukukhala ngati mbuli bwanji
Mmene peter amasiya upresident katundu anali pati.....iweyo lwara wangosowa kolowera .....osachita support Enock chihana bwanji monga wakwanu.....usiletu kuyankhula za peter......amalawi chiyembekezo chimene tasala nawo ndi peter
Nkhani yodya mabanzi ndiyovuta, chilungamo chimasowa ndikumagoyankhula mozungulira opanda solution.
Wayambatu ku khota tidana nawetu uziyankhula za chakwela nt APM wamva machende ako galu
😂😂😂😂 yomweyo galu iweee
Koma pa ma President onse mu Malawi yemwe aliko bwino kuposa onse ndi Mutalika.
Palibe zabola apa change position peter and chakwela out 2025
Ndipo a samuel lwara mumandiwaza nsaname kkk everytime ndikamamvera ma audio anu ndimamva sugar 😂 ndimafuna ndikumvelani daily cz mumabudula mpunga wanyama, kamba simugawa. Izizi akunena apazi akutsutsa amadya thewera lamwana 😅😅😅
Zoona ine munthu uyu ndimafuna kumamumvera daily fact ndiyomwe akunenayi😂😂😂😂
Reality yowawa...odana ndzomwe ukunenazi sadziwa zomwe akufuna
Alekeni anthu akasakhe okha
Ndiyambe chochi,Neleson mandela uja sanalamulire dziko ali otha msinkhu??
chikhala kuti peter anthu akumuda bwezi kumaliro kuja anthu akumulira kut ayimile??
so iwe ukamat peter ayi what do you mean so tayimilatu iweo tione ndi mkamwa modambanamo aaarrriii.
iwe do you compare chakwela nd peter,chambaaa chani,ngat sukufuna khala usavote uzidya soya peices bass kumpotoko ndi atumbuka azakowo bwanji? pita ukooooo
Akunena zoona, koma mbuli ngati inuyo simungaone.
Ayi osanena Kuti stumbuka pliz zichepezo tseka Chikamwa icho
Wanamaiwe sudziwa ndale
Apm my vote 2025
Lwara zopela zomwe walankhula za APM chifukwa munthu wanzeru sangayerekeze mavuto tilinawowa ndi APM
Lwara tikutulukatu ali ndi chibwana
Peter anayendesapo analephera chakwera walephera you are true pezani wina
Nyamata wa chilima wasowa kolowera kkkkk
a rwara zikambani zanzeru musiye kuyankhula zopusa zanuzo
Machende ako iwe abambo akowo
Ndichifukwa achichotsa ntchito ndiwamisala wakutumayo akupusitsa koopsa 😂😂😂
Peter ndiwabwino
Lwala wayamba kukhumudwitsa wanthu chakwera ungafanizire ndi Apm?
Mr samuel.pachimanga choola timasankhako.kt ichi ngankhale chili choola km.ndinkhonza kukazinga nde anthu tikuona kt bola peter
❤❤ zowona
Ulibe mfundo nzimayi pachinyero chako dppp ikulowabe m,boma panyero pako
Mwangolongolora 18 min osanenapo oyenera anthu tigwire ziti ndiye
Mr. Lwara is a chaotic person, he wants people to applaud whatever he says, Mr. Lwara learn to be quiet sometimes, you are missing the point
opepela uyu mbuzi ya munthu
Woooozaaaaaaa sir Lwara
Apm ❤❤❤❤
Udani wako ndi a Peter usasokonedze nao anthu omukonda Peter Ife Peter ndi chiyembekezo chathu usiye kuyankhula manyi
Mwayambatu uchitsiru madala. Muthalika ndi Chakwera you cant put then together. Ya Chilima ija timakupangani support koma mwayamazi ayi
Peter mutalika ndi simungayerekeze ndi Chakwera. Vuto amalawi timaziwa kuyankhula koma mopanda zeru. Mcp udf ppp dpp mukhale pasi muone kuti kodi ndichipani chiti chimwe chapangapo zabwino muona kuti dpp inayesesa. Chinthu chimozi poti mutalika wakalamba koma still ali ndi zeru . Chilima sanawinise dpp. Dpp nditimene anayitana chilima. Chilima anawinisa mcp ndiyime isamanyade .
Iwenso mmutu mwako nzeru mulibe nzeru chakwera ungamufanizile ndi mutharika? kape iwe wosowa chonena.
Akulu mwayowoya makola chomene ineso palije uyo angasanga vote yane anthuwa palibedi munthu ofunikila Peter anapangitsa kut kuyambe ma dembo tisaiwale ulamuliro wao
Lwala nde tivotere ndanino kulephera kulitu ma stage stage enawo nde ndi zero
Inuyo mukufuna ndani mwalankhula2 zopoila lelo awotu ndimaganizo anu bwana takumvani koma uthengawo kapena mwayamba kampeni2 tizavotela inu
Akulu awanso,,,,
Auzeni zoona bwana
That is true Peter ngati anachoka pampando analephela tiwoneko zna asatinamize agogo l love your point keep it up mr🙏🙏🙏
Apeter ndiye ndiokanika bola namkhumwa osati peter aaaa ngati zili chotcho basi alipowa angopitiliza
Akulu fodya tamazimisiraniko a peter simungafanizire ndi mbuzi ya mu2 ngat chakwera
Rwala ndi opusa
Chisiru iwe...chitsiru kwabasi
APM wakalamba akapume, akakhala akungozikodzela ndiye angalamule ndani? Kwake kunatha petulo tiwone zina, munthu osadziwa kulankhula kkkkkk akagwele ndi family party yakeyo, Tiyeni amalawi tiyese Atupele ❤
Ndip or achakweratu sitikuwafuna ife ai akapume achakwer kwao tikufuna tionen Ena bas
Aaa inu mbuzi ndi nkhosa mungafanizire?
kkkk mwakalipa alomwe atanena za peter mnthalika kkkk chilungamo si mkuchifuna alomwe peter walalamba amazikozera pa mpando angalamule dziko aaaa peter wakalamba
mandela msafanize ndi gogo peter ayi
Panyapako iwe ukuona ngat popanda akukhoti achinyengo aja APM akanatuluka m'boma?
Iwe aliyese akavota yekha usati nyase usamat amalawi sakufuna dpp uziti iweyo sukufuna koma ine ndikufuna zako zimenezo mesa chilima anadziwa ndale chifukwa cha apm
Auzeni koma awa. Khala ngati ntawi yaPita analikuLwanda
Iwe ndichisiru kwambiri ukunena kiti mcp asankheko munthu wina oti ayimireso 2025 ukuganiza kuti angakhale ndani pa anthu onse okuba amene ali ku mcp kuja?? Ndiwe mbuzi kwambiri
mutharika akuwinaso mufune musafune.....APM my vote ✊
Vuto siyiwe uyakhula, vuto ndi amako anakubelaka iwe
Bola mwanva, mbavazi zomwe zidalamulilapo kale ndi nthawi yopuma zikadye ndalama zomwe zinabazo
Ndipo ndizoona tinapanga mademo 2020 chifukwa cha APM analephera nde tiyeni ngati pali wina ku DPP angazawine not APM chonde tiyeni Anthu awiriwo apume km 😂😂😂😂
Lwala akufuna udindo basi Kodi kukhala maudindo osiyasiyana ndi kusonyedza Kuti munthuyo Ali ndi experience osati chakwera amagwila ntchito Ku chipiku iweyo Wayamba kuyankhula ,opusa zopanda nzeru wasowa kolowera
Ntumbuka opanda nzeru
100% light show ndi olephela.tiyetsele,utm UDF or afford.amagona,ali pa mpando.ziko,amayemdetsa,ndi chisale.ndi,amayi akunyumba kwao.just, remember akazi awo,amachita kupita ku reserve bank kumangotenga, ndalama kumeneko,atiudza za change for what corrupt our nation? that's sheet 'we can no sitting here watching this happen.amalawi,kodi,timadziwa akamati democracy?tili kutali,ndi chitukuko mu ziko lathu.
Lelo mwalakhulako mwazelu mosakhalila mbali
Amene angavotere aford ndi ndani ....chipani cha atumbuka .....muzavoterana nokhanokha anthu oti sakukukwana 5000000 ndiye mukufuna upresident
Yes, Nothern Region has got a low population BUT has a STRONG DYNAMIC POLITICAL IDELOGY. Satengera kt uyu ndi wakwathu koma PERSONALITY ya munthu.