VICE PRESIDENT MICHAEL USI AZIZIMUTSA OGWILA NTCHITO KU CHIPATALA.17 July 2024

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 28. 08. 2024

Komentáře • 504

  • @EnossDzuwa
    @EnossDzuwa Před měsícem +44

    Zomwe wayamba kupanga Ussi ndi zofunikira kwambiri ndipo zithandiza anthu kumagwira ntchto zawo moopa lamulo kmaso kufika ku ntchto mu nthawi yake, Big up VP

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani Před měsícem +24

    Well deserve Usi, bola lisakhale sewero koma pakhale solution cfk ma doctors ndiye amatiwonjezadi

  • @noelmithi7848
    @noelmithi7848 Před měsícem +12

    That's the way to go , well done our VP Michael usi

  • @vitumbikochinguwo6227
    @vitumbikochinguwo6227 Před měsícem +3

    Kind of leadership we have been waiting God bless you

  • @LemarSmith123
    @LemarSmith123 Před měsícem +10

    Excellent ❤❤❤❤❤❤ imeneyi ndentchito imene ikufunika muno dziko la MALAWI

  • @JoyceNkhokwe
    @JoyceNkhokwe Před měsícem +3

    Keep it up bwana mudzayenderenso nthawi yogulitsa feteleza wamakoponi anthu amavutika amalipiritsidwa ndalama yapamwamba muzipangapanga l like it

  • @francislimbani-jd7ft
    @francislimbani-jd7ft Před měsícem +3

    The type of leadership I have always prayed for to my country. ❤

  • @stanleykumwembe4719
    @stanleykumwembe4719 Před měsícem +5

    Uyuyu aliza athu uyu😢, guy’s, Big up Dr Michael Usi, thawi ndi ndalama guys, maiko amzathuwa akutuyukuka njira zake ndi Izizi guys.

  • @marthachapepa2692
    @marthachapepa2692 Před měsícem +2

    If Malawian leaders of government departments will work like what Mr V P did, I hope there shall be no laziness and corrupt people in our country . I salute this team spirit.

    • @itubiz1501
      @itubiz1501 Před měsícem

      This guys knows what he is doing and others will not even like him cause of his good works, only God can protect and guide him...well done Mr Vp

  • @ngwilasephron7197
    @ngwilasephron7197 Před měsícem +1

    That'll help so much ,the same as John pombe Magufuli was doing in Tanzania, I really appreciate it

  • @user-px9gd6fc6w
    @user-px9gd6fc6w Před měsícem +2

    Wow that's a Great move bamboo asikono 🤔 our VP so much ❤️ you from Lusaka Zambia 🇿🇲 one of followers

  • @ShakilaChagwa
    @ShakilaChagwa Před měsícem

    Congratulations 🎉Mr VP, Good work

  • @umalimaganga
    @umalimaganga Před měsícem +3

    Koma kumeneko 😅😂😂 that's the spirit. Ineyo I work overseas we don't play jokes about time.

  • @user-jl9yk8jd6g
    @user-jl9yk8jd6g Před měsícem +2

    I can see other hospitals afraid that which one will be next!??🤣🤣🤣🤣🤣🤣 It's your hospital of course!!!🤣🤣🤣🤣🤣... Big up Mr VP

  • @EllenChabwera
    @EllenChabwera Před měsícem +3

    This is good Malawi akozeke izizi ndiye zofunika kwambiri thanks bwana VP matiganiziladi amalawi🎉

  • @LovenessLester
    @LovenessLester Před měsícem +2

    Keep it up mr VP, DR Manga more 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @clementgama-u5p
    @clementgama-u5p Před měsícem +4

    Well done Mr VP kwathu kwa gaga HC kuli Ambulance yopanda mafuta ofwala amagula okha mafuta ngati akufuna kugwiritsa ntchito ambulance

  • @AlliSaiti
    @AlliSaiti Před měsícem +5

    We need this kind of readership

  • @AffectionateGondola-cv7qj
    @AffectionateGondola-cv7qj Před měsícem +1

    I love that and I had no doubt with this guy keep up mr VIP

  • @ChristopherKanzere
    @ChristopherKanzere Před měsícem +2

    Go ahead Mr VP don't flashing
    Anthu akumudzi akadwala amavutika amafika ku chipatala muthawoyake koma MA doctor amabwela nthawi yomwe afuna

  • @JacobBanda-s1f
    @JacobBanda-s1f Před měsícem +1

    Bwana mwabwera,this is beautiful dziko lathu liziyenda bwino

  • @YahayaUndiya
    @YahayaUndiya Před měsícem +1

    This is so interesting Mr vp❤❤

  • @ApocheC.
    @ApocheC. Před měsícem +1

    Real definition of Manganya 🔥🔥🔥

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Před měsícem +2

    Congratulations Mr VP, ukuku ndiye kutumikira ziko komwe mumafunika please continue

  • @WestonMsani
    @WestonMsani Před měsícem +1

    Keep it up Mr VP ,,,,,anthu akalowa muboma amatayilila kwambili thawi sasamala ntchito

  • @ChristyBauleni
    @ChristyBauleni Před měsícem +1

    If this coninues our country can be transformed
    Those Who will be caught not working must face the law

  • @OZIELBLESSINGS
    @OZIELBLESSINGS Před měsícem +2

    Sanje sumana, ganizo lopambana kwambili Mr vice president ❤❤❤❤

  • @user-hq2io8nk7s
    @user-hq2io8nk7s Před měsícem

    Thanks very much Mr VP, this is a good work you have started .Keep it up and it is my appeal to ask you travel hospitals because many deaths occur because of hospital staff wickedness. You have also plan to visit other government departments

  • @LoydKameza
    @LoydKameza Před měsícem +3

    Great work Mr VP ❤

  • @PiliraniDanielDaniel
    @PiliraniDanielDaniel Před měsícem

    Keep it up until my country Malawi is changed

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Před měsícem +1

    The spirit of SKC

  • @grenanakhozwe3735
    @grenanakhozwe3735 Před měsícem

    Well done Mr Vice President ❤️❤️

  • @paulbanda9638
    @paulbanda9638 Před měsícem +1

    Michael usi weldone apose kugwira ntchito a president, ali busy iwowo kuba ndalama, zikakhala cho ndizakuvotela ine

  • @humphreysidie4747
    @humphreysidie4747 Před měsícem +1

    He was supposed to fire the DHOvfrom the spot coz it can't b that the head of the entire hospital is not in the office at 8, we have so many educated ppl who can do that job so well.... Many ppl would have learnt from this

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v Před měsícem +1

    That's good work Mr vice president ma doctors ambiri amajaira kwambiri

  • @phillgwedera3755
    @phillgwedera3755 Před měsícem

    this is what we call the calling of a leadership. be blessed the VP

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Před měsícem

    Good start Mr. VP, keep it up for the betterment of Malawi, anthu m'bomamu akugona kwambiri.

  • @stuartswirase7en977
    @stuartswirase7en977 Před měsícem

    The small things matter, one step at a time it's possible to fix things big up our VP

  • @clementlukhele9551
    @clementlukhele9551 Před měsícem

    This is awesome Mr vp💪🏻💪🏻💪🏻❤❤

  • @HappyChipozi
    @HappyChipozi Před měsícem

    This is so good

  • @EliasDzoole-js8vx
    @EliasDzoole-js8vx Před měsícem

    I can see chilima in him well done bwana ussi

  • @RonaldKanyimbo
    @RonaldKanyimbo Před měsícem

    That's what's up a vp.....am loving this

  • @FynessChikadza-y8h
    @FynessChikadza-y8h Před měsícem

    This is good approach,big up Dr VP

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Před měsícem

    Bravo bravo good work Mr vice president we silute you for what you have done❤❤❤❤

  • @user-gs5mu2px7z
    @user-gs5mu2px7z Před měsícem

    Well done👏👏

  • @YamikaniLiyenda
    @YamikaniLiyenda Před měsícem

    I support this idea and this plp are so stupid

  • @IshueBaneti
    @IshueBaneti Před měsícem

    What I like most about this government is akuphunzisa mmalawi kuti osangwira ntchito asadye Malawian are lazy izizi bwana pitilizan do it whole heartedly for the people and not for votes plz sir

  • @user-kn9jz4qp9h
    @user-kn9jz4qp9h Před měsícem

    This is beautiful Bwana VP

  • @DaynaKalimanjira-kj2gw
    @DaynaKalimanjira-kj2gw Před měsícem

    Nice Mr usi

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Před měsícem

    This is very good Mr. VP

  • @JamesChiphwanya-tb3tq
    @JamesChiphwanya-tb3tq Před měsícem

    For the first time VIP president to do this thanks so much.anthu ongwila ntchito zipatala za boma amaonjeza kwambili amangwila ntchito 2 ours

    • @NovassTambala
      @NovassTambala Před měsícem

      This is first time kumalawi Vic president kuyedela zipatala guys big up

  • @user-fs5gr8iv5s
    @user-fs5gr8iv5s Před měsícem

    Zikomo kwambiri Ambuye akutezeni anthu akuvutika bweraniso kuno ku ofesi ya DC kuno kukasungu DC CHIDAKWA

  • @FumbwaLyson-3710
    @FumbwaLyson-3710 Před měsícem

    Big up ndinzomwe tikufuna usii uyuu ndi katundu he come to deliver❤❤❤❤❤

  • @nowachiumia3716
    @nowachiumia3716 Před měsícem

    Good work Dr usi Kip it going forward

  • @DalisoulMwale-wu1bf
    @DalisoulMwale-wu1bf Před měsícem

    Big up Malawians

  • @MercyChimaliro-fi6mv
    @MercyChimaliro-fi6mv Před měsícem

    Keep it up our Vp.in so doing you will carry majolity

  • @EugeniaNgoyi
    @EugeniaNgoyi Před měsícem

    That's lovely Mr Vp

  • @pettersen2717
    @pettersen2717 Před měsícem

    That's what I expected of manganya... 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Před měsícem +2

    So you have to go also to migration, ma passport sitikuwaona

  • @GloryShaba
    @GloryShaba Před měsícem

    This is the way to go❤❤❤

  • @isaacgmc
    @isaacgmc Před měsícem

    Zosezo mwayamba ausi mwachedwa mwayamba ndawi yosaenela . Komaso atu sangagwile chito opanda malipilo abwino

  • @user-re7fo3be2z
    @user-re7fo3be2z Před měsícem

    Respect Vp

  • @UlayaInan
    @UlayaInan Před měsícem

    Mwaiyamba bwino avice president ntchito

  • @liffawazili2840
    @liffawazili2840 Před měsícem

    It's necessary, people in government office to be working as if they are in private sector. When it's 7:00 it's exactly 7:00 coming late you have to write a report or else advise your immediate supervisor that your won't report in time.. Let's embrace it , Malawi can completely change. IN ADDITION, we should have the spirit of serving our people. Tisaiwale Tinkaisaka nthcito imeneyo, mulungu anatipatsa, tiyen nafeso titumikire whole heartedly. God bless Malawi

  • @peterbyson6269
    @peterbyson6269 Před měsícem

    This is the way we should lead❤

  • @jelsonmlowoka8611
    @jelsonmlowoka8611 Před měsícem

    Servant leadership proud of you Mr vice president

  • @user-iq5xk6ju7y
    @user-iq5xk6ju7y Před měsícem

    Excellent move Bwana VP ❤❤❤

  • @GiftJulius-gx2kb
    @GiftJulius-gx2kb Před měsícem

    Well done vp.kip it up

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni Před měsícem +1

    Ndye mpakana TV ayesa tikufelanji et?

  • @PetroKachingwe-jf7dh
    @PetroKachingwe-jf7dh Před měsícem

    That's good work VP Continue

  • @yahayaomar7077
    @yahayaomar7077 Před měsícem

    First time kuyamba kuona Vice president akupanga zimene Dr Michael usi apanga anthu ogwila ntchito m'boma amapanga ulesi kwambiri chifukwa choti palibe owayang'anila and they respect time thank you Mr Usi tikufuna atsogoleri ngati inuyo, vote for Michael Usi

  • @FarooqPias1625
    @FarooqPias1625 Před měsícem

    Even it looks like show off but I love it, i hope vp his doing this with good intention, not only to show off. we need our government with real solution.

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb Před měsícem +1

    zabwino kumayamika
    Great job bwana usi

  • @MachitidweYobu
    @MachitidweYobu Před měsícem

    Mostly all the government hospital they do not know time management they take this for granted lero aziona

  • @PraiseMitton
    @PraiseMitton Před měsícem

    Amalawi musapusisike ndizomwe akupanga a VP awawa ali kale mbali ya chakwera asakuphimbeni mmaso ndizabwino zonse zimene azipanga panopa Amalawi kupusa aaaaaa pilizi 😭😭

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Před měsícem

    Thank you very much bwana Vice President

  • @mrsmkjb2411
    @mrsmkjb2411 Před měsícem

    Let’s hope this will continue and is just not a “starter show”!

  • @elizabethmapira2773
    @elizabethmapira2773 Před měsícem +1

    Ndipo muwauze a Vice president kuti chipatala Cha Chikwawa amalipilitsa anthu kuti anthandizidwe,MOTi anthu ena amabwerera asapatsidwa chinthandizo chifukwa chosowa ndalama yopereka Kwa manesi ndi madolotala

  • @giftmwale8475
    @giftmwale8475 Před měsícem

    Our able vp keep it up

  • @ChikondiLikapa
    @ChikondiLikapa Před měsícem

    ❤❤❤❤i love you mr vp tapitilizani izi musaleke ayi yendelani kuma office onse aboma 🎉🎉

    • @user-bi6pb5gc8t
      @user-bi6pb5gc8t Před měsícem

      Uyende mwambiri ngakhaleni mumakampani muone nyansi zimene zikuchitika ndimene anthu ogwila ntchito akuvutikila komanso utifufuzileko Kuti amene anakagula fetilaiza kubushala ndindani chidukwansotu mavuto enawa mukuwabwelesa ndiinu anthu amaudindo mukuba kwambiri misonkho yathu

  • @justinmadeya
    @justinmadeya Před měsícem

    Pitilizani ndithu a VP chifukwa athu amaluza miyoyo chifukwa cha kuchedwa kwa thandizo . Well done ❤

  • @Rometcma
    @Rometcma Před měsícem +1

    Anduna alikuti a azaumoyo amalawi umbuli unakula this is not his duty inu munaonapo vp from other countries kumapanga zimenezi 😂😂😂😂😂😂😂

    • @LukaThawe
      @LukaThawe Před měsícem

      Kodi iye wayenda Ngati nduna ya zaumoyo Kodi president sanayendepo kuchipatala mwaganiza bwanji man cadet

  • @AshimayeGama
    @AshimayeGama Před měsícem +1

    Zaziiiiii nanga makwhala alikuti mbiliyako

  • @user-rc3ze2oi7u
    @user-rc3ze2oi7u Před měsícem

    BWANA V.P MWAYAMBA BWINO KWAMBIRI ZIMENEZO NDIZIMENE TIMAFUNA KUWAPANGA ANTHU KUTI AZIGWIRA NTCHITO 🎉🎉🎉
    MUSALEKERE POMWEPO MUZIFUNSASO MAKHWALA ALIPO?

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 Před měsícem +2

    Ndie bola ukanapanga zimenezi ku immigration tu osati ku hospital tufuna ma passport

    • @ChikondiLikapa
      @ChikondiLikapa Před měsícem +1

      Man odwala akufa ndiye ayambe ku immigration inu ndiaja ongosusa aja eti

    • @mavmsusa1310
      @mavmsusa1310 Před měsícem

      Ku hospital nde kofunikilako. Bwana kkkk

    • @PriscahChikaonda
      @PriscahChikaonda Před měsícem

      Anthu Ena amangozindikira alankhula.

  • @emilymwale2596
    @emilymwale2596 Před měsícem

    Good development

  • @user-nz9ty3ih1v
    @user-nz9ty3ih1v Před měsícem

    akoma saname mavayisiwa ntchito anayidziwa uja wapita ujaso samafuna zachibwana uyuso sakufuna zachibwana akanati president so azigwira mene amagwirira ma vasiwa bwezi zikuyenda bho

  • @StevenMjMbama
    @StevenMjMbama Před měsícem

    Apitilize ndinthu Mr vp great job ndipo zizimutsani ma office aboma ambiri plz

  • @MfipaKapwera
    @MfipaKapwera Před měsícem

    Mwapanga bwino A v p mulayendeleso a NRB palibe chomene akupanga kumupoto kuno ambiri sanalembese.

  • @rabisonpias5131
    @rabisonpias5131 Před měsícem

    Bwana MANGA , Osawaiwalatu a Bro.. bwezi akumadzakulondolerani njiraa mumaona popondapo.

  • @frankfrankb8461
    @frankfrankb8461 Před měsícem

    Malawians you are easy to be deceived don't you know that this One is campaign for chakwera

  • @MichaelKachiboo
    @MichaelKachiboo Před měsícem

    Thats good koma mankhwala nzipatalamu ndie mulibe

  • @RaymondPhambala
    @RaymondPhambala Před měsícem

    People of Malawi, Kodi chifukwa chani sitichedwa kupusitsidwa...uyu wakhala minister Kwa dzaka 4, wapanga chani ku dziko lino ?
    Zonsezi ndi zabodza kufuna kupusitsani and izizi a MCP anadana ndi Chilima chifukwa ndiye amene amachita izi but behind the camera, so izi ndi set up, work up Malawi, you know the truth !!!!

  • @user-nn9ow8rn8w
    @user-nn9ow8rn8w Před měsícem +4

    Ku Malawi izizi zimaonjeza mupedza madokotala onse alipa Lunch...... Ma patient ma petient angokhala Komanso nthawi ya lunch yo imapitilira
    Bwanji osagawana ena atenge lunch 12- ena 1 o'clock
    Komanso pachipatala 1 hour is too much 30 minutes is enough.... South Africa that is the system ngakhale pa lunch anthu amathandizidwa and ndi 30 minutes lunch

  • @jonnahobammah6967
    @jonnahobammah6967 Před měsícem

    Well done Mr Vice president 💚💚💐💐

  • @GeorgeKambwiri-xr9ri
    @GeorgeKambwiri-xr9ri Před měsícem +1

    Zomwe tikufuna ife ngat amalawi ndizimenezi

  • @user-kr8th5oh7b
    @user-kr8th5oh7b Před měsícem

    Good start a VP , bingu mutharika ankapangaso choncho

  • @EmmanuelNkosi-ts8bn
    @EmmanuelNkosi-ts8bn Před měsícem

    This way to go Mr VP

  • @user-ww4ei5fb7d
    @user-ww4ei5fb7d Před měsícem

    Well done, civil servants need improvement

  • @AlbertEngelbercht
    @AlbertEngelbercht Před měsícem

    Wayamba bwino usi,onse asogoreli azitero bwezi Malawi alipatali,osangokhala Ku sanjika