MICHAEL USI WAYANKHA ZOMWE ANANENA A FELIX NJAWALA KU MZUZU.

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 13. 09. 2024
  • MICHAEL USI WAYANKHA ZOMWE ANANENA A FELIX NJAWALA KU MZUZU.

Komentáře • 83

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před měsícem

    Usi is best leader of Malawi, chilima anasankha usi wanawonapo China chake Cha nzeru... I love you usi with my all heart God bless you

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem +1

    Alibilethu nzeru,,zidya chabe ndalama,,monse muja umatani kupanga zimenezo

  • @LiyayaNyamula-j3b
    @LiyayaNyamula-j3b Před měsícem +6

    Palibe chazelu apa palibe

  • @ThokoFiliyamu
    @ThokoFiliyamu Před měsícem +5

    Kabambe wapangitsa wina kuvala makaka a utm

  • @stevezulu2108
    @stevezulu2108 Před měsícem +3

    Awa wanthu si a UTM. Ndi a Wadya Zake alibe Mlandu. Usi angowaveka makaka a UTM. UTM ndi imodzi ya Akaliyati basi.

  • @user-es4jt6ds8m
    @user-es4jt6ds8m Před měsícem +1

    Ma sapota osewa ndi a MCP akowapatsa malaya awo🎉

  • @MiracleMalichi
    @MiracleMalichi Před měsícem +1

    Ndale zotukwanizana zinatha nkhani ndiyoti mukambirane Ku UTM Kuti zinthu ziyende bwino

  • @CyrusBanda-l5y
    @CyrusBanda-l5y Před měsícem +1

    Powerful speech

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 Před měsícem

    Dr Usi you are a democratic leader

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před měsícem

    Dr. Usi, in Democracy the rule is simple, majority rules, UTM yatuluka ku alliance inuyo mwatsala nokha simuzikwanitsa, chokani ku Tonse, yendani pamudzi ndi anzanu.

  • @ConfusedAstronaut-qv6wq
    @ConfusedAstronaut-qv6wq Před měsícem

    Kodi inu chikuvuta ndichiyani kunena kuti ndi mcp or utmost palibe amene angakuvutitseni,athu akufuna kungodzowa bwana.

  • @GiftKumbambe
    @GiftKumbambe Před měsícem

    Kkk kodi magalasiwo amakhala akuyabwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Před měsícem

    Kodi a usi mukuvalabwinotu kodi ndi malaya achilima

  • @wisdomsadyalunda2001
    @wisdomsadyalunda2001 Před měsícem +1

    and those people are not UTM atengedwa kundilande bangwe and other areas. apasidwa ma 200 hands every one of them

  • @billymhoni9527
    @billymhoni9527 Před měsícem +3

    Ali yekha kumenekoko ..

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 Před měsícem

    Upange zomwe chilima amafuna kupanga ukudziwa kale kuti he was about to declare the separation for tonse alliance ndiye osatipusisa apa nthira kuwiri iweyo.

  • @user-sh6gi5uq3l
    @user-sh6gi5uq3l Před měsícem

    Mumafuna umboni? Zodana pa ndale ndizomwe zikuononga Malawi wanthu
    Political hatrage will not take us nowhere usi is the unifying factor

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Před měsícem

    If I were Usi I would chosen one lose the vice president post or lead UTM .
    USI can has no power to lead UTM as a party unless he resigns as vice president and not work with MCP government. If Usi was intelligent politically he wouldn't have accepted the vice president post that MCP new would weaken him politicallly .

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480 Před měsícem +2

    Iwe dyera bambo sikono chifukwa chani iwe ukulabadira za imfa ya chilima

  • @KinziWindasoni-h4b
    @KinziWindasoni-h4b Před 10 dny

    Ulibe nthawi yobwezela pamenepo ukutani

  • @fulabanda2115
    @fulabanda2115 Před měsícem +3

    Ndalama zoopsa kwambiri

  • @user-yk9ow5vv9j
    @user-yk9ow5vv9j Před měsícem

    Very good very good Boss

  • @kumbukanikafwafwa
    @kumbukanikafwafwa Před měsícem

    Kkk usi ase ❤

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Před měsícem

    Usi believes money buys favour in politics but he doesn't know what the voters who are true UTM wants and the pain they are have gone through in this bloody alliance . Undiwolose ndi kakutafune)

  • @NoelKambwese-fj9io
    @NoelKambwese-fj9io Před měsícem +1

    Nthawi yoseyija simunkalamvala jeaz ya Utm mukamvala chilima atamwalira aaaaa zochititsa manyazi

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 Před měsícem +2

    zoti UTM ili magulu angapo kod ndi zoonadi eti? 😂

  • @HaliJana
    @HaliJana Před měsícem +1

    KOMA AMALAWI NDINUDI OVUTIKA KOBASI KUMASEKELELA ZIMENEZI ZOONA

  • @lazaruschitsamba8394
    @lazaruschitsamba8394 Před měsícem

    inu gulu lachina kaliyati akuononga chipani muona division

  • @ModesterMbendera
    @ModesterMbendera Před měsícem +1

    Kd uli mbali iti usi?

  • @michealchaomba9761
    @michealchaomba9761 Před měsícem

    Anthu opusa owombera m'manja

  • @JustinWBanda
    @JustinWBanda Před měsícem

    Inuyo ndiwa kulu

  • @ChikondiAmosi-ue3jk
    @ChikondiAmosi-ue3jk Před měsícem +1

    Koma kunena Zona umu muli mzeru kungot anthu timafuna kunyonzana koma ussi muli usogoleli

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Awapasa zingati

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 Před měsícem

    Ndipo apa mr chikangawa ndinu azodiyaki ngat ndabale and achakwera ndikoko chaka chamawa uku akuchoka

  • @LysonChimutu
    @LysonChimutu Před měsícem

    That's great

  • @pearsonjnrsoko
    @pearsonjnrsoko Před měsícem

    Thawi zina chete ndibwino
    Kumanani ndi team yanu muvane

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Před měsícem

    Wabodza sitikufuna ife tili ndi Kabambe,,osatiphstikiza ndi MCP

  • @lucksongondwe8266
    @lucksongondwe8266 Před měsícem

    Lero Limenero, Mwayamba kuvala makaka a UTM. Zopusa

  • @YamikanChirwa
    @YamikanChirwa Před měsícem

    Km inu zelu mulibe

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba Před měsícem

    Tipaseni ngongole zo timwele mowa kape iwe

  • @davidlinerevelation3427
    @davidlinerevelation3427 Před měsícem

    But the late Chilima spoke himself of leaving tonse alliance audibly

  • @wisdomsadyalunda2001
    @wisdomsadyalunda2001 Před měsícem

    ever since he has never been in that a tire, why now ?

  • @lingstonenagoli7729
    @lingstonenagoli7729 Před měsícem

    Tabweretsan tonse wadula apa,mukuponya za Usi yekha bwanji

  • @BlessingsMaheya
    @BlessingsMaheya Před měsícem

    Abale ako asati athu

  • @JohnFrank-cg1yh
    @JohnFrank-cg1yh Před měsícem

    Mr utsi chisogolo chikhala chotani chifukwa utm iyima payokha ndipo ichitisa convention mukapikisana nawo,

  • @QochiweNkhoma
    @QochiweNkhoma Před měsícem

    Amanganya nanunso lero mpakana mwavala UTM 😂😂😂😂😂

  • @FredKanjere
    @FredKanjere Před měsícem

    A usi mudzichita manyazi mukafuna kulankhula,ifetu zoti inu sa UTM ife timadziwa komaso inuyo nokha pansi pa mtima wanuwo mumadziwa kt sinu a UTM,,dziwani kt mwabisara mm'batata nsana ukuonekera,,,, silent big killer

  • @user-xq1wd6wq5h
    @user-xq1wd6wq5h Před měsícem +1

    Iwe ndiwe wacp

  • @DysonUmali
    @DysonUmali Před měsícem

    We are following with a laughing gesture factless

  • @FredKanjere
    @FredKanjere Před měsícem

    Yes

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Před měsícem

    UTM yachina Kaliati ndi one

  • @jamesstevenzondannkhana1805

    Convention ya utm ndi imene ikathetse kugawanikana kpmwe kulipo muchipani cha utm

  • @IshmaelNesta-rb8dx
    @IshmaelNesta-rb8dx Před měsícem

    Kausiru aka ....kangonama ngongole ngongole koma sizikuoneka....wa MCP uyu

  • @FarookIbrahim-c2e
    @FarookIbrahim-c2e Před měsícem

    😂😂😂😂😂😂

  • @kunjemangandale1118
    @kunjemangandale1118 Před měsícem

    Mukamalizile kuchitipa

  • @ShariffAlli
    @ShariffAlli Před měsícem

    Kodi abwanawa magalasiwa amakulira amawangwira ngwiratu

  • @IshmaelNesta-rb8dx
    @IshmaelNesta-rb8dx Před měsícem

    Ka utm kabodza😂😂😂

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Před měsícem

    Manganya ndi ponyelela pa munthu munthu woyipa kwambili.,...amalawi ndi anthu apusa opanda zeru

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os Před měsícem

      Ndipo inu osamufunsa kuti chichitikireni ngozi ija anapangapo chani monga iye wokhala wa chiwiri wake? Anali duuuuuuuu nthawi yonse ya maliro ija.

  • @user-gp2zp2dj1w
    @user-gp2zp2dj1w Před měsícem

    Mboli yako iweee

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu Před měsícem

    Wabisala mbatata msana wawonekela mwazikakamiza lero kuvala makaka a utm? Chinyengo cheni cheni ndipo sindinamvele mkomwe speech yanuyu a manyanya ndangobwela kuzaponya comment yangayi 😂😂😂😂😂😂😂

  • @AkimAmadi
    @AkimAmadi Před měsícem

    Akucheza amanganyawa

  • @trintasngoliwa4144
    @trintasngoliwa4144 Před měsícem

    Koma amalawi dyera kumaombera mmanja zimenezi

  • @user-rb7fs5up6k
    @user-rb7fs5up6k Před měsícem

    Azimai adyela awa iiiiiiii

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x Před měsícem +1

    Uyu ndi Satana uyu unamusogoza iwe Galu

  • @CrytonMalunga
    @CrytonMalunga Před měsícem

    koma akulu mulibe manyazi bwanji

  • @madalitsomorris6566
    @madalitsomorris6566 Před měsícem

    Nthawi yamarilo, munali zii, no Word, Why now talking after Chilima's death??

  • @Dentera215Music
    @Dentera215Music Před měsícem

    Mzeru palibepo apa manganya uku4ira hvy

  • @trickermussa472
    @trickermussa472 Před měsícem

    Mumkaoneka azeru ku tikufelanji kunjatu

  • @mdyombamw7659
    @mdyombamw7659 Před měsícem

    China ndi china... Panali madolo ambili koma malemu adasakha awa. Pali chifukwa, dolo amaziwa dolo

  • @luckymalata3387
    @luckymalata3387 Před měsícem

    Ngongole zake mukupereka oziwana nokhanokhazi?

  • @fletcherkayira4089
    @fletcherkayira4089 Před měsícem

    idyani ndalamazo

  • @Peterchavula-e2o
    @Peterchavula-e2o Před měsícem

    Gona nkuphe iweso

  • @khwimamtonga954
    @khwimamtonga954 Před měsícem

    VP muli zeru

  • @SydneyMwale-u9w
    @SydneyMwale-u9w Před měsícem

    Osapusisa anthu mambala iwe

  • @MunyetaMhone
    @MunyetaMhone Před měsícem

    Kachisilu aka

  • @peeboiofisho5254
    @peeboiofisho5254 Před měsícem

    udzamva nkhwangwa ili mmutu