Dr. Usi, in Democracy the rule is simple, majority rules, UTM yatuluka ku alliance inuyo mwatsala nokha simuzikwanitsa, chokani ku Tonse, yendani pamudzi ndi anzanu.
Upange zomwe chilima amafuna kupanga ukudziwa kale kuti he was about to declare the separation for tonse alliance ndiye osatipusisa apa nthira kuwiri iweyo.
If I were Usi I would chosen one lose the vice president post or lead UTM . USI can has no power to lead UTM as a party unless he resigns as vice president and not work with MCP government. If Usi was intelligent politically he wouldn't have accepted the vice president post that MCP new would weaken him politicallly .
Usi believes money buys favour in politics but he doesn't know what the voters who are true UTM wants and the pain they are have gone through in this bloody alliance . Undiwolose ndi kakutafune)
Usi is best leader of Malawi, chilima anasankha usi wanawonapo China chake Cha nzeru... I love you usi with my all heart God bless you
Alibilethu nzeru,,zidya chabe ndalama,,monse muja umatani kupanga zimenezo
Palibe chazelu apa palibe
Kabambe wapangitsa wina kuvala makaka a utm
Awa wanthu si a UTM. Ndi a Wadya Zake alibe Mlandu. Usi angowaveka makaka a UTM. UTM ndi imodzi ya Akaliyati basi.
Mwanena zoonadi
Ma sapota osewa ndi a MCP akowapatsa malaya awo🎉
Ndale zotukwanizana zinatha nkhani ndiyoti mukambirane Ku UTM Kuti zinthu ziyende bwino
Powerful speech
Dr Usi you are a democratic leader
Dr. Usi, in Democracy the rule is simple, majority rules, UTM yatuluka ku alliance inuyo mwatsala nokha simuzikwanitsa, chokani ku Tonse, yendani pamudzi ndi anzanu.
Kodi inu chikuvuta ndichiyani kunena kuti ndi mcp or utmost palibe amene angakuvutitseni,athu akufuna kungodzowa bwana.
Kkk kodi magalasiwo amakhala akuyabwa
Kodi a usi mukuvalabwinotu kodi ndi malaya achilima
and those people are not UTM atengedwa kundilande bangwe and other areas. apasidwa ma 200 hands every one of them
Ali yekha kumenekoko ..
Upange zomwe chilima amafuna kupanga ukudziwa kale kuti he was about to declare the separation for tonse alliance ndiye osatipusisa apa nthira kuwiri iweyo.
Mumafuna umboni? Zodana pa ndale ndizomwe zikuononga Malawi wanthu
Political hatrage will not take us nowhere usi is the unifying factor
If I were Usi I would chosen one lose the vice president post or lead UTM .
USI can has no power to lead UTM as a party unless he resigns as vice president and not work with MCP government. If Usi was intelligent politically he wouldn't have accepted the vice president post that MCP new would weaken him politicallly .
Iwe dyera bambo sikono chifukwa chani iwe ukulabadira za imfa ya chilima
Ulibe nthawi yobwezela pamenepo ukutani
Ndalama zoopsa kwambiri
Very good very good Boss
Kkk usi ase ❤
Usi believes money buys favour in politics but he doesn't know what the voters who are true UTM wants and the pain they are have gone through in this bloody alliance . Undiwolose ndi kakutafune)
Nthawi yoseyija simunkalamvala jeaz ya Utm mukamvala chilima atamwalira aaaaa zochititsa manyazi
Ndipo inu akufuna kunamiza ndani?
zoti UTM ili magulu angapo kod ndi zoonadi eti? 😂
Ndipo musakaike😂😂
@@user-zw8ns7bk7s kkkkkk zovuta kwabas
KOMA AMALAWI NDINUDI OVUTIKA KOBASI KUMASEKELELA ZIMENEZI ZOONA
inu gulu lachina kaliyati akuononga chipani muona division
Kd uli mbali iti usi?
Anthu opusa owombera m'manja
Inuyo ndiwa kulu
Koma kunena Zona umu muli mzeru kungot anthu timafuna kunyonzana koma ussi muli usogoleli
Awapasa zingati
Ndipo apa mr chikangawa ndinu azodiyaki ngat ndabale and achakwera ndikoko chaka chamawa uku akuchoka
That's great
Thawi zina chete ndibwino
Kumanani ndi team yanu muvane
Wabodza sitikufuna ife tili ndi Kabambe,,osatiphstikiza ndi MCP
Lero Limenero, Mwayamba kuvala makaka a UTM. Zopusa
Km inu zelu mulibe
Tipaseni ngongole zo timwele mowa kape iwe
But the late Chilima spoke himself of leaving tonse alliance audibly
ever since he has never been in that a tire, why now ?
Tabweretsan tonse wadula apa,mukuponya za Usi yekha bwanji
Abale ako asati athu
Mr utsi chisogolo chikhala chotani chifukwa utm iyima payokha ndipo ichitisa convention mukapikisana nawo,
Amanganya nanunso lero mpakana mwavala UTM 😂😂😂😂😂
A usi mudzichita manyazi mukafuna kulankhula,ifetu zoti inu sa UTM ife timadziwa komaso inuyo nokha pansi pa mtima wanuwo mumadziwa kt sinu a UTM,,dziwani kt mwabisara mm'batata nsana ukuonekera,,,, silent big killer
Iwe ndiwe wacp
We are following with a laughing gesture factless
Yes
UTM yachina Kaliati ndi one
Convention ya utm ndi imene ikathetse kugawanikana kpmwe kulipo muchipani cha utm
Kausiru aka ....kangonama ngongole ngongole koma sizikuoneka....wa MCP uyu
😂😂😂😂😂😂
Mukamalizile kuchitipa
Kodi abwanawa magalasiwa amakulira amawangwira ngwiratu
Ka utm kabodza😂😂😂
Manganya ndi ponyelela pa munthu munthu woyipa kwambili.,...amalawi ndi anthu apusa opanda zeru
Ndipo inu osamufunsa kuti chichitikireni ngozi ija anapangapo chani monga iye wokhala wa chiwiri wake? Anali duuuuuuuu nthawi yonse ya maliro ija.
Mboli yako iweee
Wabisala mbatata msana wawonekela mwazikakamiza lero kuvala makaka a utm? Chinyengo cheni cheni ndipo sindinamvele mkomwe speech yanuyu a manyanya ndangobwela kuzaponya comment yangayi 😂😂😂😂😂😂😂
Akucheza amanganyawa
Koma amalawi dyera kumaombera mmanja zimenezi
Azimai adyela awa iiiiiiii
Uyu ndi Satana uyu unamusogoza iwe Galu
koma akulu mulibe manyazi bwanji
Nthawi yamarilo, munali zii, no Word, Why now talking after Chilima's death??
Mzeru palibepo apa manganya uku4ira hvy
Mumkaoneka azeru ku tikufelanji kunjatu
China ndi china... Panali madolo ambili koma malemu adasakha awa. Pali chifukwa, dolo amaziwa dolo
Ngongole zake mukupereka oziwana nokhanokhazi?
idyani ndalamazo
Gona nkuphe iweso
VP muli zeru
Osapusisa anthu mambala iwe
Kachisilu aka
udzamva nkhwangwa ili mmutu