UDF ndi DPP Ndizipani Zokhazo Zoti A Malawi Angavotele - Concerned Citizen

Sdílet
Vložit
  • čas přidán 21. 05. 2024
  • On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen says, UDF and MCP are the only parties worth their salt in 2025.
    Pa Nyasa VoiceBox, nzika yokhudzidwa yati UDF ndi MCP ndi zipani zokha zomwe a Malawi angavotele mu 2025.
    #malawi

Komentáře • 83

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 24 dny +4

    Apm my vote ❤❤❤❤❤

  • @user-oc9vl9xz8e
    @user-oc9vl9xz8e Před 23 dny +3

    Atupele muludzi ndi mulosi ameneuja analisela zoona kuti Chakwela sangaendese dziko tiyeni tivotele nsigoleli woonabpatali

    • @user-nj4ob8jw6y
      @user-nj4ob8jw6y Před 22 dny

      Za zii, dziko lidalaka Bakili Muluzi. Kamuzu Banda adasiya china chili chonse chili m'malo, makampani, ndizinthu zambiri koma Bakili Muluzi adadzawononga china chili chonse. Chodabwitsa palibe wina aliyense amene amalankhura za izi kuti Elson Sixpence Bakili Muluzi adawononga dziko lino.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 Před 23 dny +1

    God bless you bro 2025 DPP woyeeee ❤❤❤ tinapanga mistake mulungu atikwiyira chifukwa.chake tiliku bagamoyo

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Před 24 dny +2

    Msonda si munthu ai, hule pa ndale uyu, kulowa uku, kulowa uku, osakhazikika munthu.

  • @AbrahamLLoyd-xb2xc
    @AbrahamLLoyd-xb2xc Před 20 dny

    Powerful

  • @phindiswatshibo7101
    @phindiswatshibo7101 Před 24 dny +2

    Walankhula aise size ndithu😂😂😂😂😂

  • @user-zg6mn8qr4m
    @user-zg6mn8qr4m Před 21 dnem

    Apm my vote 2025

  • @user-lb5gt4uv3s
    @user-lb5gt4uv3s Před 23 dny

    Thanks munthu wankulu walankhula mwamphamvu

  • @PaulChaposa
    @PaulChaposa Před 23 dny

    Eeeeee ine no comment ❤❤

  • @HassanZubeli
    @HassanZubeli Před 17 dny

    ❤❤❤

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf Před 23 dny

    Mwalankhula Baba Takumvani

  • @andrewmtendere3167
    @andrewmtendere3167 Před 22 dny

    Speaking truth❤

  • @amiduclement2142
    @amiduclement2142 Před 18 dny

    Mumakwana goodness

  • @user-oq7hi3hd4p
    @user-oq7hi3hd4p Před 23 dny

    Amen

  • @user-qz5gj3tf2t
    @user-qz5gj3tf2t Před 16 dny

    Tikukonza Malawi osati Zambia ndeno enanu lekani zomayelekeza ndi maiko ena sitikukhala ku Zambia ife ayi.

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Před 23 dny

    Zina umangoona utaziyamba 😂😂😂😂😂😂😂❤❤

  • @PeterPhiri-nd6op
    @PeterPhiri-nd6op Před 23 dny

    Kuyakhula kwabwino musonda sangayakhule zabwino ndiwodwala ameneyo

  • @joaquegerman2250
    @joaquegerman2250 Před 24 dny +1

    Mcp ndi utm zipani zimenezi anthu ana zituluka kale

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm Před 23 dny

    Power to that 👊

  • @user-pt5wn7nu1d
    @user-pt5wn7nu1d Před 24 dny +1

    Auzeni man osawanyengelera

  • @PheladiMafologela-ii3vd
    @PheladiMafologela-ii3vd Před 23 dny +1

    Awuzen zoona zake asamapuse

  • @MalawiMuslim-TV
    @MalawiMuslim-TV Před 24 dny +1

    Auze ase achina nsonda

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 Před 24 dny +1

    Mawu omveka bwino ndinthu...

  • @user-ky8eq5ek1p
    @user-ky8eq5ek1p Před 24 dny +1

    Zoonadi Brother tilipambupanu

    • @user-et3il7pi7t
      @user-et3il7pi7t Před 23 dny

      Don't take him again people like this guy Muthu opanda chipani

  • @vincentmatemba1659
    @vincentmatemba1659 Před 23 dny

    Akwen uzimvere mumtolo😂😂😂😂 zopanda mzeru amalawi tatopa nazo

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y Před 23 dny

    Apm boma ilo❤

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Před 23 dny

    Mwalakhulatu chilungamo apa
    Mwamveka ndithu

  • @lawrencemwafulirwa
    @lawrencemwafulirwa Před 24 dny +1

    Maganizo anu amenewa

  • @jeffreypesulo3917
    @jeffreypesulo3917 Před 20 dny

    Kumalawi kuli anthu oganiza kwambili eeesh

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 Před 23 dny

    GOD BLESS you malawi 🇲🇼 watha wafika pa Zimbabwe akaliyati uchitsilu atakutha ndalama a mcp kumabwekela ngati dziko likuyenda bwino iiiiii mulungu achite nanu kuyambila chakwela chilima ndiwotse akuyamikila boma ili ndagalu kwabasi uchisilu wanu akaliyati magayile amalawi otse mayi uchiysilu unakumelani ati

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Před 23 dny

    Komad ❤❤❤❤❤

  • @YinomiyaEko
    @YinomiyaEko Před 12 dny

    Izo ndizowona mavuto achiluka malawi achoke anthu okubawo

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Před 11 dny

    Tikhale ndi maso auzimu ndithu

  • @ivychithyoka1551
    @ivychithyoka1551 Před 24 dny

    DPP+UDF=Fire Works!!!!!!!!

  • @user-is5dl7np9g
    @user-is5dl7np9g Před 23 dny

    Kodi a msondawa ndi chani kwwni kweni

  • @EnockMunthali
    @EnockMunthali Před 23 dny

    Atupele anati msogoleri asathawe udindo olo zinthu zitzuta bwanji ndiye chilima athawe ayii

  • @AugustineTheu-of6nv
    @AugustineTheu-of6nv Před 22 dny

    Inu amene mukumuzuzula Patricia Kalitati mwakoma pati. Chonsechi mukutankhula choncho kuti namwe mudzapeze mpando muzabe bwimo misonkho ya a malawi 2025

  • @user-nj4ob8jw6y
    @user-nj4ob8jw6y Před 24 dny +1

    Ngakhale inuyo mukunama mukulankhula zambwerera. UDF ndi DPP zidalephera, musanamize wanthu inu, akulonjezani mpando inu. DPP kungakhale quite? Zabodza zimenezo

  • @user-st6bt5vv9c
    @user-st6bt5vv9c Před 23 dny

    Mau abwino kwambiri zikomo

  • @TadalaPaul-dk6xi
    @TadalaPaul-dk6xi Před 23 dny

    akula vumbwe otatha patsekela sonda

  • @omarajibu860
    @omarajibu860 Před 23 dny

    Otilangiza, otikonda mulipo ndithu, chonde anthu timve. 2025 is our last hope to solve all these tribulations.

  • @isaaczuze
    @isaaczuze Před 11 dny

    Muuzeni galu ameneyi.....kamwa yake ngati wizilo

  • @joaquegerman2250
    @joaquegerman2250 Před 24 dny +1

    Mzeru za ansonda zinakalamba

    • @ThomasShuga
      @ThomasShuga Před 22 dny

      😮😂😅😂❤😅😮😮😅❤❤❤❤❤❤😅🎉

  • @LackzenSumbudzu
    @LackzenSumbudzu Před 9 dny

    Dpp moto

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx Před 24 dny

    Muziwa era chisoni amsonda mutu unajama afunika kubox1 ku zomba akasungeko pang'ono mutu ubasrelamo unataya

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x Před 23 dny

    amapha anthu mcp kale bambo ake a chakwela ndi kukuyu mbuzi za wanthu

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 Před 23 dny

    A Nsonda simungawasiyanise ndi mbatata bolanso mbatata ili ndi nzeru!

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y Před 23 dny

    Asondwa ndi amisala wosamayanga edzi ikuwasunguza mutu

  • @HalordDzampana-cq4qx
    @HalordDzampana-cq4qx Před 24 dny

    asonda ingodekhani

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Před 24 dny

    Chisilu ndi ambuyako osati msonda galu iwe sankho basi

  • @user-rf4br1fv2z
    @user-rf4br1fv2z Před 24 dny

    Kodi boma amayendetsa motani kkkkkķ koma Malawi ufulu

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o Před 22 dny

    Munthu wankulu mumadzwa kuyankhula zoona ndithu Komanso chilima wakumananazo ndi ochenjera nzake chakwera amamutola Peter Mutharika samayankhula chifukwa ndi munthu ophunzira kwambili ndi chifukwa samayankha zopusa ndipo Peter Mutharika ndi munthu opamulungu ndi chifukwa anthu amamukonda kwambili

  • @ChicoBanda-kq7py
    @ChicoBanda-kq7py Před 22 dny

    Adadi ndi atupele amalosela koma amalawi satana anati sekama kumaso pano taonani njala ilili kumalawi

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 Před 24 dny

    M'manja mwanu akulu, mau amphamvu.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před 21 dnem

    Utim is only party to change Malawi,, DPP under Peter, shit up

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Před 24 dny

    Auzeni agalu amenewa a chilima zangakhalenso pusident mu dziko la malawi wolo atatani wagwa nayo 😂😂😂😂😂😂

  • @homeremedys3748
    @homeremedys3748 Před 24 dny

    Iweyo ukuyala zakaliyatiwe ndikaliyati yemwoyo nonse ndinu zitsilu osatiuza chipani choti tisankhe ayi

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Před 24 dny

    Wokamba moyipa msondayu, osati wokalamba bwino ayi, simukumuona makutu oyima ngati nkhumbawo kkkkkkkkkkk

  • @mikesangano6624
    @mikesangano6624 Před 24 dny

    Ulemu wanu mabwana,, kulankhula moona mosaopa makape amenewa.. agwa nayo amenewa, Olo atayesera kubera aonabe nyekhwe yoopsa.

  • @WhiteRichard-cw2fo
    @WhiteRichard-cw2fo Před 23 dny

    Odi ndiwelenga ma comments ine chonena ndilibe

  • @YNOTGEORGE8
    @YNOTGEORGE8 Před 24 dny

    Regionalism koma adah

  • @user-xd1cm7tm7t
    @user-xd1cm7tm7t Před 24 dny

    Asonda ndachisilu nkalamba yopanda zeru

  • @mwale1154
    @mwale1154 Před 23 dny

    Akulu palibe angasithe dziko lapansi penapaliponse zithu zandula pa Zambia soya pieces mk700

  • @SaideeAhmed
    @SaideeAhmed Před 24 dny

    Zoonadi Asoonda ingokalapee mwalandila kale chibanzi

  • @MasegoModukanele-xg2hj

    Chokani adpp mufuna muwa pusitseso a UDF ngati momwe munawa pusitsila muja

  • @BrightPhiri-bt6ev
    @BrightPhiri-bt6ev Před 24 dny

    Choka iwe mchawa wasankho muwafuna anthu aku mpoto pompano galu iwe fotsek.

    • @user-hd7wq2yc6m
      @user-hd7wq2yc6m Před 23 dny

      Iwe nawe munyane wa ku mpoto ulije zeru wasankho pakati pa mchawa ndi mchewa wasankho ndikuti? Namwe wakwithu mahala ngakichepa mcp munayamba mwakhala nayo imwe ? Pala ku Malawi kuno kuli mtundu wasankho ndiye mchewa nambala 1 panopo maudindo m'boma almost 90 percent chigawo Cha pakati mchewa Kodi mwabadwa muma 1990s eti?ndipo kuno ku mpoto tisayerekeze kivotere mcp si chipani chimenechi chankhanza chatikomera wanthu wanandi kuno kupoto foseki

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 Před 24 dny

    Ku malawi aliyense amafuna kukhala wandale, political analyst, judge etc.
    Nanga zopusa zikukambidwa apazi ndi chani?
    CZcams yaphweka.

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Před 24 dny

    Dpp, utm mcp udf
    Pp etc being party nothing is wrong but who is leader. Serious kuvotera Peter muthalika albinos killer stupid mbava ndi chisale nepotism galu racist president galu galu zitsilu zomwe vikavotere Peter muthalika galu

    • @LamieTiger
      @LamieTiger Před 23 dny

      😂 udziwe lero boma lililonse limakhetsa mwadzi popanda kukhetsa mwaz boma silingayende ulamulilo wa u president suzozedwa kuchokera kwamulungu Koma satana
      And satana ndiamene amawalumbilitsa ena amapha mosaonetsera kuzera munjira zosiyanasiyana nde ngongole zomwe amatenga maiko akunja aja
      Kupatsidwa ma billion awulele so dzungu sapeleka chithu chaulele komaso satana sapeleka zithu zaulele kungovomeredza palibe wabwino sir

  • @user-dw9zi6bo3o
    @user-dw9zi6bo3o Před 24 dny

    You are being a tribalist

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Před 23 dny

    Munthuyu muli kulankhula mwa usogoleli

  • @lawrencemwafulirwa
    @lawrencemwafulirwa Před 24 dny

    Maganizo anu amenewa

    • @user-gx5ht9gm3z
      @user-gx5ht9gm3z Před 24 dny

      NO PAIN NO GAIN IWEI SLM BOY GO BACK 2 SCHOOL GALU