UDF ndi DPP Ndizipani Zokhazo Zoti A Malawi Angavotele - Concerned Citizen
Vložit
- čas přidán 21. 05. 2024
- On Nyasa VoiceBox, a concerned citizen says, UDF and MCP are the only parties worth their salt in 2025.
Pa Nyasa VoiceBox, nzika yokhudzidwa yati UDF ndi MCP ndi zipani zokha zomwe a Malawi angavotele mu 2025.
#malawi
Apm my vote ❤❤❤❤❤
Atupele muludzi ndi mulosi ameneuja analisela zoona kuti Chakwela sangaendese dziko tiyeni tivotele nsigoleli woonabpatali
Za zii, dziko lidalaka Bakili Muluzi. Kamuzu Banda adasiya china chili chonse chili m'malo, makampani, ndizinthu zambiri koma Bakili Muluzi adadzawononga china chili chonse. Chodabwitsa palibe wina aliyense amene amalankhura za izi kuti Elson Sixpence Bakili Muluzi adawononga dziko lino.
God bless you bro 2025 DPP woyeeee ❤❤❤ tinapanga mistake mulungu atikwiyira chifukwa.chake tiliku bagamoyo
Msonda si munthu ai, hule pa ndale uyu, kulowa uku, kulowa uku, osakhazikika munthu.
Powerful
Walankhula aise size ndithu😂😂😂😂😂
Apm my vote 2025
Thanks munthu wankulu walankhula mwamphamvu
Eeeeee ine no comment ❤❤
❤❤❤
Mwalankhula Baba Takumvani
Speaking truth❤
Mumakwana goodness
Amen
Tikukonza Malawi osati Zambia ndeno enanu lekani zomayelekeza ndi maiko ena sitikukhala ku Zambia ife ayi.
Zina umangoona utaziyamba 😂😂😂😂😂😂😂❤❤
Kuyakhula kwabwino musonda sangayakhule zabwino ndiwodwala ameneyo
Mcp ndi utm zipani zimenezi anthu ana zituluka kale
Power to that 👊
Auzeni man osawanyengelera
Awuzen zoona zake asamapuse
Auze ase achina nsonda
Mawu omveka bwino ndinthu...
Zoonadi Brother tilipambupanu
Don't take him again people like this guy Muthu opanda chipani
Akwen uzimvere mumtolo😂😂😂😂 zopanda mzeru amalawi tatopa nazo
Apm boma ilo❤
Mwalakhulatu chilungamo apa
Mwamveka ndithu
Maganizo anu amenewa
Kumalawi kuli anthu oganiza kwambili eeesh
GOD BLESS you malawi 🇲🇼 watha wafika pa Zimbabwe akaliyati uchitsilu atakutha ndalama a mcp kumabwekela ngati dziko likuyenda bwino iiiiii mulungu achite nanu kuyambila chakwela chilima ndiwotse akuyamikila boma ili ndagalu kwabasi uchisilu wanu akaliyati magayile amalawi otse mayi uchiysilu unakumelani ati
Komad ❤❤❤❤❤
Izo ndizowona mavuto achiluka malawi achoke anthu okubawo
Tikhale ndi maso auzimu ndithu
DPP+UDF=Fire Works!!!!!!!!
Kodi a msondawa ndi chani kwwni kweni
Atupele anati msogoleri asathawe udindo olo zinthu zitzuta bwanji ndiye chilima athawe ayii
Inu amene mukumuzuzula Patricia Kalitati mwakoma pati. Chonsechi mukutankhula choncho kuti namwe mudzapeze mpando muzabe bwimo misonkho ya a malawi 2025
Ngakhale inuyo mukunama mukulankhula zambwerera. UDF ndi DPP zidalephera, musanamize wanthu inu, akulonjezani mpando inu. DPP kungakhale quite? Zabodza zimenezo
Opanda nzeru
Inu
Mau abwino kwambiri zikomo
akula vumbwe otatha patsekela sonda
Otilangiza, otikonda mulipo ndithu, chonde anthu timve. 2025 is our last hope to solve all these tribulations.
Muuzeni galu ameneyi.....kamwa yake ngati wizilo
Mzeru za ansonda zinakalamba
😮😂😅😂❤😅😮😮😅❤❤❤❤❤❤😅🎉
Dpp moto
Muziwa era chisoni amsonda mutu unajama afunika kubox1 ku zomba akasungeko pang'ono mutu ubasrelamo unataya
amapha anthu mcp kale bambo ake a chakwela ndi kukuyu mbuzi za wanthu
A Nsonda simungawasiyanise ndi mbatata bolanso mbatata ili ndi nzeru!
Asondwa ndi amisala wosamayanga edzi ikuwasunguza mutu
asonda ingodekhani
Chisilu ndi ambuyako osati msonda galu iwe sankho basi
Kodi boma amayendetsa motani kkkkkķ koma Malawi ufulu
Munthu wankulu mumadzwa kuyankhula zoona ndithu Komanso chilima wakumananazo ndi ochenjera nzake chakwera amamutola Peter Mutharika samayankhula chifukwa ndi munthu ophunzira kwambili ndi chifukwa samayankha zopusa ndipo Peter Mutharika ndi munthu opamulungu ndi chifukwa anthu amamukonda kwambili
Adadi ndi atupele amalosela koma amalawi satana anati sekama kumaso pano taonani njala ilili kumalawi
M'manja mwanu akulu, mau amphamvu.
Utim is only party to change Malawi,, DPP under Peter, shit up
Auzeni agalu amenewa a chilima zangakhalenso pusident mu dziko la malawi wolo atatani wagwa nayo 😂😂😂😂😂😂
Iweyo ukuyala zakaliyatiwe ndikaliyati yemwoyo nonse ndinu zitsilu osatiuza chipani choti tisankhe ayi
Wokamba moyipa msondayu, osati wokalamba bwino ayi, simukumuona makutu oyima ngati nkhumbawo kkkkkkkkkkk
Ulemu wanu mabwana,, kulankhula moona mosaopa makape amenewa.. agwa nayo amenewa, Olo atayesera kubera aonabe nyekhwe yoopsa.
Odi ndiwelenga ma comments ine chonena ndilibe
Regionalism koma adah
Asonda ndachisilu nkalamba yopanda zeru
Akulu palibe angasithe dziko lapansi penapaliponse zithu zandula pa Zambia soya pieces mk700
Soya pices wake uti ife tikugula 150 bodza silabwino
Zoonadi Asoonda ingokalapee mwalandila kale chibanzi
Chokani adpp mufuna muwa pusitseso a UDF ngati momwe munawa pusitsila muja
Palibe kanthu
Bola zipani zopusazi
Zichoke.
Choka iwe mchawa wasankho muwafuna anthu aku mpoto pompano galu iwe fotsek.
Iwe nawe munyane wa ku mpoto ulije zeru wasankho pakati pa mchawa ndi mchewa wasankho ndikuti? Namwe wakwithu mahala ngakichepa mcp munayamba mwakhala nayo imwe ? Pala ku Malawi kuno kuli mtundu wasankho ndiye mchewa nambala 1 panopo maudindo m'boma almost 90 percent chigawo Cha pakati mchewa Kodi mwabadwa muma 1990s eti?ndipo kuno ku mpoto tisayerekeze kivotere mcp si chipani chimenechi chankhanza chatikomera wanthu wanandi kuno kupoto foseki
Ku malawi aliyense amafuna kukhala wandale, political analyst, judge etc.
Nanga zopusa zikukambidwa apazi ndi chani?
CZcams yaphweka.
Chilungamo chaku sinanitu akulu
@@mafukenimasangwi5487
Chilungamo chake chiti pamenepa?
Dpp, utm mcp udf
Pp etc being party nothing is wrong but who is leader. Serious kuvotera Peter muthalika albinos killer stupid mbava ndi chisale nepotism galu racist president galu galu zitsilu zomwe vikavotere Peter muthalika galu
😂 udziwe lero boma lililonse limakhetsa mwadzi popanda kukhetsa mwaz boma silingayende ulamulilo wa u president suzozedwa kuchokera kwamulungu Koma satana
And satana ndiamene amawalumbilitsa ena amapha mosaonetsera kuzera munjira zosiyanasiyana nde ngongole zomwe amatenga maiko akunja aja
Kupatsidwa ma billion awulele so dzungu sapeleka chithu chaulele komaso satana sapeleka zithu zaulele kungovomeredza palibe wabwino sir
You are being a tribalist
Munthuyu muli kulankhula mwa usogoleli
Maganizo anu amenewa
NO PAIN NO GAIN IWEI SLM BOY GO BACK 2 SCHOOL GALU