Vuto si a police ayi, vuto ndi malamulo a dziko lathu. Zikanakhala kuti kuli malamulo kwathu kuno, kuyambira galu akumuti bwanayo ndi a police onse anapanga zimenezo bwezi pano atamangidwa onse.
Let lawyer's fight for this man's justice, the foreigner and police men need to answer to the LAW. This is not acceptable, #Chakwera do something urgently. Owners of the land are suffering at the cruelty of foreigner's
Muthune ndikumalota ndili ku school pafupifupi tsiku lilonse Koma school ndinasiya 2019 nditalemba mayeso a4 anthu amati za school ndimadziganizira kwambiri komano sidziri choncho ndani Muthu angandimasulire maloto amenewa.
It's bad that these kind of things are too much in Malawi since it's not new issue. Ambli akulavulazidwa kwambli nd apolis I think many they are not knowing their role
This is a very bad situation and their Asian bossis using the abuse of his power and it's a felony charges against this poor innocent man May the Lord heal him and have mercy on his soul.
a mabungwe please lowelelanipo po thandiza felix kut mwenye ameneyu amuliupile ndithu ndipo ndalamazisakhale zochepa chifukwa uku ndye ndikuphana komaso a police wo alanbdiole zilango
Mwenye ameneyo azkpita kwawo ndiwankhaza..kukanakha kuno ku South Africa akadapanga zonthekela kuti amuyimbe mlandu..koma Malawi mmmmm sadzantheka..amasamgalala ndikuti Malawi nzawo adzivutka....zomvetsa chisoni😢😢
Vuto ndi apolice sanagwire ntchito yawo mwadongosolo ngati anthu oti anaphunzila ntchito yawo bwino bwino.
Vuto si a police ayi, vuto ndi malamulo a dziko lathu. Zikanakhala kuti kuli malamulo kwathu kuno, kuyambira galu akumuti bwanayo ndi a police onse anapanga zimenezo bwezi pano atamangidwa onse.
@@ChilpaKamcholotimbuzi zap0lice kupha mbalewanga chifukwa cha mwenye that's bullshert
Ndipo apolice akuno amadana ndi anthu oyela khunguwa sangapange zimenezi kwa munthu wakuno nzawo
Amangidwe ameneyo
Let lawyer's fight for this man's justice, the foreigner and police men need to answer to the LAW. This is not acceptable, #Chakwera do something urgently. Owners of the land are suffering at the cruelty of foreigner's
Akulankhula momvetsa chisoni kmso chilungamo chokhachokha ambuye a lowelerepo mmmmm😢😢😢
Mayi walankhula chilungamo. Komanso banja iri Ambuye alikhudze mwapaderadera 😢🙏
Exodus 14 vs 14 igwira ntchito pa moyo wanu mulungu akumenyelani khondo
Malawians please let's help our fellow brother
Police ikupanga chinyengo yasiya kuona chilungamo chankhan ikufuna ndalama mbili yonyasa imeneyo
Ntolankhan ari bho kwambiri amafusa ma professional 😊
Tikuthokoza maloya ozipeleka woo mulungu asogolele zonse ❤❤
Ulamuliro wa MCP muli nkhanza
Amalawi please kaocheni company imeneyo basi thats too much 😢😢
Ku Malawi kuno kulibe apolisi
A Malawi okhaokha kumazunzana chinchi
Lord have Mercy on us
Apolice njala ngaphe munthu wakwanu chifukwa cha mwenye kupusa police ziwani kuti mwenye simubale wanu ndichifukwa chake mumafa udyo muzi ntchito mulozedwa Apolice
Anthu wosauka ku malawi alibe ufulu mmmm
izo nde zoona
Mulungu ndiwoo khulupilika pemphelani machilitso ndikumbwezeletsa kwathupi olo mulungu apange upalechoni wakumwamba chachikulu tikupemphela moyo ambuye akukhuzeñi ambuye alimbaliyanu
May God almighty bless Abel Zulanga. Mafunso akuya komanso kulondoloza nkhani mwachidwi.
Pepeni kwambiri Mr Felix ,Ambuye akukhuzeni ndi dzanja la machilitso....
Amabungwe Ntchito yanu imeneyo
I wish Bushiri could come in and assist this family for daily nsima so that the wife should not run away from this man
That's my prayer
That's my prayer
Iphani apolice onse apanga izi zimene zikuchitikazi sizabwino abwanaonso panga nawon zinthu
Ambuye alowerere ..why police nkhaza izi mukuzitenga Kuti dziko lathu la ufulu ..Koma mudzayankha
Good work Abero❤❤❤❤
Chonde if someone can help get justice for this man, wenela police imatchuka ndi nkhani za nkhaza....
plesident akutipo chani azipita amwenye wa kwawo
Muthune ndikumalota ndili ku school pafupifupi tsiku lilonse Koma school ndinasiya 2019 nditalemba mayeso a4 anthu amati za school ndimadziganizira kwambiri komano sidziri choncho ndani Muthu angandimasulire maloto amenewa.
Spirit of demotion
Just pray and fasting to rebuke that Spirit.
Mapephero muli mphamvu khulupirani mutsutsane nawo mzimu obwerela zithu mbuyo
Nthawi imakwana yomwe Mulungu amaonetsa mphavu zake ndipo zoti ndiwe wa Police sizioneka.
Osauka alibe mawu 😢 ,ambuye odziwa kukhuza awakhuze Mr kachingwe
Anthu kumeneko gwilanani manja kukaotcha shop ya mwenyeyo
Ndipo mulandu uwu usaime pa njira ukambidwe ndithu ndiponso m'mwenye ameneyo anyongedwe ndithu
sizoona katundu wake alipo okwana ndikumateronso hmmm ayi
Amwenye ndi akhaza kwambiri
Some of our police oficers are wicked..... Very unfortunate. I wonder the school they attend
Nanga ungasume kuti mathero ndi boma 💔🙌
Mmmm abale inu wosauka alibe mau, ndlama inamuphadi yesu, apolis akumalawi kufuna kupha malawi nzanu chifukwa chosusukira ndlama? Manyazi akugwireni ndithu ntchito yanu simukuyikwanitsa ndipo Mulungu akulangeni pamodzi ndi m'mwenye wanuyo bola zikanakhala kuti zinthu zo zabedwadi panali pombveka
Mulungu akufungatireni bambo inu pamene mukumbva zowawazi muthawi imeneyi, Koma boma limene tili nalo panoli nde ayitu yohhh
Mwenye ameneyo aphedweso bas
Kangaude plz help him to get his justice
Nayeso aphedwe mwenye ameneyo ukuku ndikuphatu kudachitikaku malawi mmmm
It's bad that these kind of things are too much in Malawi since it's not new issue. Ambli akulavulazidwa kwambli nd apolis I think many they are not knowing their role
Apolisi aku Malawi kuno atha kukupha eeee🙌🙌. Ku LL kuno kuli apolisi aku area 3 eeeee🙌🙌🙌
This has moved me into tears 😭😭
Mwenye ameneyo ndiwankhaza choncho shop chamwenyecho chikuyenera kuwochedwa , Allah akale nawo koma nkaz yo ndi fiti ameneyo kwambir komaso ndi hule kumukana mwamuna wake chifukwa choti mwamunayo wafulala tipatsen njira yoti titha kuthandizila m,bale wathuyu kochepa kamene tingakwanitse bon kalindo alowe pasewo please president was amphawi mwenje ameneyo azowe
Ndipo kwerekwere mwenye ameneyo achoke kwathu kumalawi
Anthu akuyenela kuthandizidwa ma lawyer alowelelepo apapa munthuyu munamuvulaza kwambiri chipepeso chikufunika Cha nyoo
Justice should take it's course.. plz legal aid ntchito iyooo
Osauka alibe mau
Amwetu ndi athu akhaza kwambili amachoka kwaoko alibe kalikose amalemelela dziko lathu komaso ndikumatizuza Chocho mmm
Kukanakhala kuno ku south africa akapha mu mwenyeyo
zovetsa chisoni kwambiri...Police anthu sibwino kuthamangira kumumenya munthu pa ntchito yanu...aboma chilungamo chionekepo apa dyera a Police ndi ndalama tikamakupangani chipongwe midzimu mudzitiona ngati adani anu...siose apolice magwira ntchito mwachilungamo
Nkhani yomvesa chisoni kwambili mulungu awayanganile Mr kachingwe pa mvuto lawagwela komaso a police onse ankhuzidwa pa nkhani iyi ntchito yawo inthe alandileso zilango
This is a very bad situation and their Asian bossis using the abuse of his power and it's a felony charges against this poor innocent man
May the Lord heal him and have mercy on his soul.
Malawi wachakwela anthu akuvutika😢😢😢
Always is Blantyre why? We're tired of this please try other places gha
A police kukonda ndalama. Apapa Popat amutsegulire mulandu. Amwenye amazunza antchito kwambiri. This man has to be compensated. 32:38
😢Mvuto apolisi aku Malawi ku konda ndalama kupotsa moyo wa munthu!! @meyo adzipita kwawo
This is sad...chilungamo chiyende ngati madzi
Mmmmmm kma gyz eshiii zamasiku itsilidza
This is sad😢 Amwenye nd anthu opoila 😞😤
Amalawi okha okha kuphana cz chaminthu obwera ai zikomo ndithu
Mbale wanga pepa koposa,zikoli silibwino.Boma liyenera lilipire
Km abale zamasiku omaliza sizoona kumupanga munthu choncho mpaka kumuwononga munthu kumoyo zosakhara bwno ndpo inuyo apolice mulungu akukanthen inuyo musadzafe mulungu akuoneni poika kuvulaza Mala
WI nzanu inuyo muli ndi nsambi
Mayi inu musadandaule za mnyumba kuti muzitani kuchipinda dandaulani zamoyo wa amunanu lungalunga nkubadwa mayi
No sister amaiwa akuyankha funso momwe awapatsira not kut iwoo akuzifuna zakuchipindazo
@@NedsonBilly owoooo ndimaona ngatitu chabwino ndakumvani ndithu brother
lawyer apapa agwire ntchto mwachilungamo mmwenye uyuyu adzipita kwawo
Madhara wa amakhalaso ghetto yopoyira bwezi titakawontcha kampaniyo ndikapolice komweko tsiku lomwelo anthu wopusa kwambiri 😹 😂😂
please tiyeni amalawi tikondane tokha tokha munthuyu ndi osalakwa nanu a polisi mmmm ayi musamatelo please
Koma police yathu ya Malawi simukukhoza choncho sibwino tosefe ndife athu.ndikupepha mulungu wakumwamba alowerelepo mbali zose ziwili.inu a police officer munagwira tchitoyi yakumuvulaza muthuyu ambuye akudaritseni 😂
😢😢eish koma zomvesa chisoni
Anthu amenewa ndankhaza koopsa vuto amasekeleledwa ineyo ndiye nsaname ifeyo ndopusa kwambiri amwenye wo apolice wo ayankhe, justice should be saved, kukonda ndalama apolicewa
Kumuononga m'Malawi mzathu chonchi a Police ndinu zitsiru kamba ka ndalama🥸
Koma a Malawi tokhatokha tizizunzana chonchi? we are very vulnerable ku Malawi kuno mmmm Ambuye atithandize
Amabungwe loweleranipo apa sizoona izi chilungamo chiyende apa
Amabungwe athandizeni anthuwa ndithu ali mu ululu oopsa ndithu
Amalaw mmmm kukonda ndalama ngat salandila salary
Poor policing. Machende amayake mmwenyeyo ndiapolisi. Chakwera mboliyamake
Iih ndanva chisoni 😭😭😭
Futi si yoopya pofuna, chilungamo,apa pali njila ziwili,amalawi,tiime kuthetsa, nkhani iyi.apolice,akayankhe,komaso,mwenyeyo atseke company yacheyo.waputa,kudabwe.
Very bad mulungu awakanthe onse atengapo mbalipa nkhaza iyi
a mabungwe please lowelelanipo po thandiza felix kut mwenye ameneyu amuliupile ndithu ndipo ndalamazisakhale zochepa chifukwa uku ndye ndikuphana komaso a police wo alanbdiole zilango
Mbudzi za apolice akumalawi pansi pa achakwera kudzunzana okhaokha nkhani ya anthu obwera eeshhh chilungamo chiyende ndithu
😢😢😢 dziko lanthu lomwe kumazuzika
Km apolice aku malawi mukuwonjeza kukonda ndalama ,bwanji kd sizabwinitu izi akhala bwanji muthu pa ziko lapasi mutamunga khaza conci
Kumalaw kulibe mtendere tikuphana chifukwa cha ndalama
Umphawi sizinthu abale munthu walumala okula Kula abale 😢😢
😢😢😢 zachisoni kwambiri
Police yanji yokomedwa ndalama choncho 😔😔
Eshiiiii 😢😢😢
A police amaikilana kumbuyo ipangeni follow up nkhaniyi please munthu wamwamuna nkumusi ndikutha kuona ululu omwe akudutsamo bambo athuwa
People are wicked, ntha kuwalodza ine apolisi amenewo
Abuye alowelelepo
Awalakwira abambo abale ,a police akhaza amenewo
Ammmmm too bad😭😭😭😭
#timothy mtambo ...mmwenye uyu nde ofunika mademo ajA
Uyutu ayiphula
Khaza kwa osauka koma ambuye muchitepo kathu chilungamo chiyende
I even crie 😢😢😢😢
Mmmmm kulakwa
Mtendele si Nsima #Malawi🤔.
Amabugwe ntchito iyi ndiyosavuta akuyenera chithandizo
AmaBungwetu apa zikanali zandale mukanaona kumachita kupikisana kuyankhula kuti atchuke ndicholinga chakuti apeze cholowa kuchokera kwa ndalewo.Koma apa zamunthuyu kuli Ziiiii.Akuti omenyera ufulu wa anthu bwanji osanena kuti omenyera mimba zao bwanji
Malawi Police sinasinthe olo amakamba zoti inapanga reform koma sizoona .
Eishhh
Osauka alibe mau.pamene chilima amukhulukile ma billion