We were watching this program while taking our dinner but upon following it, the whole appetite vanished comrades there are some people who are evil than Pharaoh of Moses' time😭😭😭😭
A court nawonso akugona pa ntchito yao, munthu kufika pomatukwana ma officer kumangomusiya? Mesa mumakamutenga by force kuti akakhe madzi kae ku prison?
In this case, my opinion is to arrest both the husband and his sister. They are all wrong, Anti-Corruption bureau has to take a stand together with the social welfare with people of disability. The court has to help in judging righteously, that child needs a great and total support especially from his dad. The love from your parents brings joy to yourself. That bail has to be null and void, apolisi nawo azitha kumvetsetsa what is going on before coming up with judgements, malo mokonza zinthu they'll end up spoiling. Don't take sides, do what is right.
Apolice opondeleza onse mulungu achitenanu mai uyu akumusogolela nchimwene wake wakuphayu mawa nayeso azapeza vuto kuposa limeneli ndipo ndikupempha mulungu achite back to sender
Very bad, one who so called wachitetezo akuthandizila kupha mwana kamba ka ndalama. Mulungu azakulangani. Kangawude program nkhaniyi musasiyile pomwepa follow it till end. Inunso amabungwe ntchito koma iyi athandizeni mayi moyo ndi banja lawo. Apolice Maka apa lucheza very soon mulungu akulangani choyipa chisata mwini pitani mukabweze ndalama mwadyayo. Iwenso munthu wanambo ufiti uwu ziwa kuti uzafa uchonsenso ziwanda wayika mwa mwanayo. Mulungu akulanga kunjaku kuli mulungu.
Wow😮 this is very sad and it is a criminal offence arresting a child that committed no crime, this should be followed up and if possible these girls can sue the officers who did such
Ndiye kut opanda ndalama ku police kulibe nthandizo lake et, muthokoze kut anthuwa angokhala ndi umunthu mkadakhala ine mbambadi mkadafufuza komwe wapolice adalandira ndalamayu amakhala mkadakamuonetsa kut ena atengerepo phuxilo, apo bii mkadasaka petrol mkukabusa office ya police coz palibe phindu kwa anthu osauka, ndamva ululu kwabasi
Mudzina la Yesu matsoka komaso matembelo apite kwa aliyese amene watengapo gawo lozuza komaso kusautsa banja limeneli akumane ndi zilango mulungu awonetsa ukulu wake in Jesus name
Mwana osalakwa ambuye muchite nayo mwana mu phavu yamuzimu wanu ambuye muyendelen mwana munamupasa mphatso ndinu tikumupelekaso kwa yinu oipa azachite manyazi amen
Mulungu wazatheka bwanji ndinu nokha amene muli ndi thandizo kwamwana ameneyi muchite zodabwisa
Eish
police yaku ku malawi mmmm mbola chinyengo ...i wish ndingathandizepo ..
ambuye akhuze ndikuthangatilapo
Ambuye mkhuzen mwanayo ndi dzanja lanu la machiliso.mwana akuvutika uyu chitan chodzidzwisa pamoyo wake.
Mai a mwana musatope kusamalira mwanayo.
Azibambo kwenikweni ndi chani zoona kuzunzisa mwana chifukwa cha ndalama? Mulungu akupasen mtima wa umunthu komanso zomwe akuona mwanayo taganizirani muli inuyo.
Apolice aku Malawi simukudziwa ntchto yanu maka maka inuyo amene mwatenga gawo lalikulu kudya ndalama kuti Norman oipayo asamangidwe Mulungu akuyenderen ndithu.
Mabungwe pls loweleraponi mwanayo apeze thandizo loyenera.
Nanu Police Muziona Nkhani Zodyapo Ndalama aaah Kungokhala ndimtima Wautsamunda basi, Inu Nkhani yozikamba yokha iyi Mboni ndimwanayo koma Mpaka kudyapo Ufiti chani
😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢😢 please tiyen tikondane
Nkhaniyi saname yandimvesa chisoni mulungu oziwa kulanga alanhidwe chemwali wamwamunayo pamodzi ndi mwamunayo mmene amapwetekela mwana mwana wokongola oooh ambuye aoneni
Ambuye simunalephelepo ndinu wamphavu zonse tikukupemphani kuti ndimphavu zanu zonse mumuchilitse mwanayo kuti oipayo azindikile zaukulu wanu
Bwanji mwanayo osakamusiyila mfitiyo kt angomumaluzapo.Anthu ena ngoipa mtima kuposa chinyama chakuthengo.
😢😢😢😢 chiuta akatiranga koma police officer wuzinganizire kukhala iwe uka natani ????
Sing'anga mkulu ndiye YESU, amukhuze mwanayo akhale bwino
Mwana ali pa ululu uyu 😭😭 ambuye ndinu dokotala oposa ma dokolata mumaika njila popanda njila ambuye chitani mwakufuna kwanu
Amen
Zomvetsa Chinsoni 😭😭..moyo wa Mwana Gracian ukudzuzika chifukwa chabambo ake oipa mtima kufuna kulemera...koma chikumbutima chimusowese mtendere ndithu
Koma officer in charge Mulungu akuyendere mwapaderadera, ndiwe oyipa
Maganizo anga,mwanayo mupite naye kumapemphelo chifukwa anamuika ziwanda Bambo akewo
Mpaka kulolera kuzunza mwana mzimu osadziwa kanthu cjifukwa chandalama ,m,bambo ameneyu
Mulungu muchitepo kanthu PA moyo WA mwanayu komanso langizo Kwa apolisi athu mmalawi muno mwachulusa kwambiri chinyengo mukuyenera kugwira ntchito yanu moopa mulungu
Ndipemphelo lokha limene lingamumasule mwanayuu
Tizalangidwa chifukwa chachimo lalingono pollice yamalani ndintchito yanu chifukwa mulungu azaweluza and nthawi yasala pangono mwana akuonekelamu kumalimba ntima ndikumusekela opanda chisoni
Malawi wabwino uja ali kuti? Izi ndiye ziti guys 😢😢😢
Mulungu awakhululukile apolice onse amene akupondeleza nkhani iyi komanso amukhuze Gracious ndi dzanja lamachilitso
Mulungu mumuyendele mwana uyu pamodzi ndi mayi uyu mzina ndi mphanvu Zanu poti inu simulephera
Apolice ziphuphu mpaka kuzunzisa mwana osalakwa Aboma zonsezi mukuwona komanso mukuziwa
Tieni abale tithandize Gracious..sister wathuyu akuvutika nae...mwana...
Banja la Moyo osadandaula, Mulungu salakwitsa as Iam talking God is in control ndipo kuzuza kokha komwe akuchita pa mwanayi Mulungu akuona
😢😢😢 Zomvetsa Chisoni kwambiri,
Koma agalu osakawa akuthandizira kuchotsa moyo wamwana, 😭😭😭 Ambuye akuoneni
Koma anthu tikuziwa kukwatibwa ndi afiti😢Lord have mercy iiiiiiiiiiiii ambuye amukhuze Greycious oipa wo achite manyazi
Mmm koma kunjaku kuli anthu oyipa mitima koma ndithu kufuna kupha mwana cholinga mukhwimire damu iweyo mamunawe ukumva bwanji komwe uliko ukamazunza magazi ako ? Kodi nanu apolice mukuvutika chintundu chani mpaka nkumadya ndalama kuzera nkhani zomvesa chisoni nkhati izi ? Inu chemwali eni a mwana ziyikeni mwamulungu odziwa kulanga awalange anthu amenewa inuyo limbikirani posaka chithandizo chamwana china chilichonse chomwe mwalandidwa chisiyeni. Ambuye mwainu nokha ndimomwe muli machiliso mupaseni mwanayu kuchira nsanga ndikupempha kuzera mwa mitukiki yanu yonse ameni
Mwana akudzudzika chifukwa cha apolice kamba kadyela landalama
Kulakwa mwana osalakwa kuzuzika mulungu muyendeleni😢😢 zibambo otani ameneyo mwana wake yemwe ufiti otani umenewo ndalira😢
Ambuye mukhuzen mwanayo ndi zanja la machiliso.... mwanayo ali pa ululu kwambiri chitan kufuna kwanu mbuye wanga😢😢😢😢
Ameeen
We were watching this program while taking our dinner but upon following it, the whole appetite vanished comrades there are some people who are evil than Pharaoh of Moses' time😭😭😭😭
This guy is very wicked, evil scarem
This is unfair treatment 😡😡
Panopa ineyo nnazipanga kuti munthu kundibela, kundilakwila kulibwino ndithane naye ndekha bola mtamudziwa. Ndilibe mawu zomwe a police anandipangila pankhani yoti ndikukadandaula ineyo kunditenganso ngati ineyo ndiye olakwitsa ndipo a police achizimayinso ngati awo ondipanga zoophyazo 🙌🙌 ndipo mulungu adzikukanthani ndipo muliko ndimakutembelerani ndikukupemphelerani pamodzi ndiokubayo. Mulungu wazifundo awathandizepo
Wapolici ameneyu akuyenera kuchotsedwa tchito akalime nandolo
Chilungamo chimamasula osadandaula mulungu ndi wakuntha..ndipo tsiku lina udzakhala umboni wanu..nkhulupilirani..
osapitako kumene akuitaniko apolice apo biii tipange ma demo
Koma apolice amenewo kunali kuwamangisa ndithu
😭😭😭zokhuza kwambir
Nkhani yomvetsa chisoni 😢😢😢😢😢😢
Apólice opusa osapola panchombo komaso amina mmutu mwao akuononga mbili zabwinoza za azao
ndipaseni map a aunt akewo ndikawasiyile chipolopolo chimodzi chakumutu ndi mbuzi
Mulungu wayakobo mulungu wa davite mulungu wa eliya ndikupempha kut muonesele ukulu wanu pa mwana uyu ndikumulandisa manja mwa mikango iyi amen
Eeeee ayi izi zaonjeza ambuye 😢😢😢chitanipon kathu ambuye
Mudzina layesu achilitsidwa
😢😢😢msaname ndalira
A police sakuchita bwino olo pang, ono
Dziko la Malawi Mulungu atikhululukire chifukwa amphawi tili pamavuto akulu kwambiri Koma Mulungu kumwamba kulibe Sankho apolice mukamakonda ndalama kusiya chilungamo dziwani Kuti kumwamba kulibe mphawi kulibe ndalama chepesani zimenezo
Kulakwa abale mwana akuzimzika😢😢
A court nawonso akugona pa ntchito yao, munthu kufika pomatukwana ma officer kumangomusiya? Mesa mumakamutenga by force kuti akakhe madzi kae ku prison?
Mwana wamwezi angasuke mmimba.mmmmmm anthu ndioipa Mulungu ateteze mwanayu
Adzakukantha mulungu ulibe masiku galu wabambo iwe
A police amenewo Mulungu awayendere ndithu
Kulakwa mmmmm ndalamazo zakoma bwanji kuyerekeza ndi moyo wamwana mmmmmm
Mulungu alowelele pazosezi mwana akunzunzika uyu ngati bambo ake alibe eish koma azibambo enawa ndiyafiti kwambili
Tangognizani Ali chemwli wanu mungave bwanji khzatu idzi
Malawi nkhalani wachifundo komatso achisoni ku malawiko ineyo ndikanakhala ndili ndi ndalama ndikanapanga zinthu zina
Komatso please amabungwe tenganipo gawo
Agalu onse awo apolice muwamange
Zandikhudza kwambiri😭😭
Mulungu awakanthe mumunayo ndi apolice onse apangawo zonsez
😢😢😢 alibe
Mmmmmm kma abale inu mwana adalakwa chiyani kut akalandile ululu umenewo mmmmmm Ambuye mukhudzen mwanayi Ambuye
Zandikhudza abare anthuwa athandizidwe
In this case, my opinion is to arrest both the husband and his sister. They are all wrong, Anti-Corruption bureau has to take a stand together with the social welfare with people of disability.
The court has to help in judging righteously, that child needs a great and total support especially from his dad. The love from your parents brings joy to yourself.
That bail has to be null and void, apolisi nawo azitha kumvetsetsa what is going on before coming up with judgements, malo mokonza zinthu they'll end up spoiling. Don't take sides, do what is right.
Ndisaname zandiwawa kuchokera poyambilira mpakana kumapeto nkhani iyi yandivesa chisoni yanditulutsa misonzi koma chifukwa chani mwamuna uyu aliolimba mtima chonchi ........apolice akumalawi vuto siinuyo vuto ndi boma la malawi momwe zikuyendera koma china ndi china chilungamo pa nkhani iyi tingopempha mulungu alowelelepo .........chisomo walankhula mwachikulu😢😢 ....chisomo mulungu akuthandizani pepani kwambiri .......agogo ake amwana ndizoonadi simungakhale ndi mtendere pa zomwe zililimo pepani kwambiri mayi anga mulingu alimbali yanu mabungwe oona za ufulu chonde chonde lowelelanipo hapa komaso apolice omwe muli ndi khalidwe ngati mwachita apa mulungu akulangeni ......
Apolice opondeleza onse mulungu achitenanu mai uyu akumusogolela nchimwene wake wakuphayu mawa nayeso azapeza vuto kuposa limeneli ndipo ndikupempha mulungu achite back to sender
Mmmh 😢
Koma apolec wankulu wazengeleza khani Malo mwa cilungamo
So sad
Very bad, one who so called wachitetezo akuthandizila kupha mwana kamba ka ndalama.
Mulungu azakulangani.
Kangawude program nkhaniyi musasiyile pomwepa follow it till end.
Inunso amabungwe ntchito koma iyi athandizeni mayi moyo ndi banja lawo.
Apolice Maka apa lucheza very soon mulungu akulangani choyipa chisata mwini pitani mukabweze ndalama mwadyayo.
Iwenso munthu wanambo ufiti uwu ziwa kuti uzafa uchonsenso ziwanda wayika mwa mwanayo. Mulungu akulanga kunjaku kuli mulungu.
A police akuyenera afufuzudwe mwana samalowesedwa mu cell...
😢😢😢
Guys mwana akuchita kumvesa chisoni shame this world is so cruel
Why kuzunza mzimu osalakwa like that God have mercy upon the child 😅
😢😢so sad
Lord have mercy
3:35 pm Malamulo aku Malawi amakomera anthu andalama, apolice athu chilungamo alibe
😢😢😢😢😢😢😢
Ngakhale Police yathu itagwira bwino ntchito chotani, a police ngati awqva Luchenzacndi Thyolo akuonetseratu kuti analowa upolice kutu adzibera anthu mu njira ya ziphuphu
Sister munakwati ndi mfiti munayenela kuzisiya mmanja mwa chauta ndamene akudziwa mawa la muthu
Chifukwa chiyani apolice amazuza anthu osauka palibe chabwino chomwe munthu osauka amalandila thandizo kwa police koma malawi
Lord have mercy 🙏
Nkhani iyi ili pati tilowelelepo pls link us
A police Aku thyolo chilungamo chimawamvuta
Let the plan of devil fail in Jesus name
Zosakhala bwino ai ikani ma number anu .
Mwana wabwino ngati uyu ..so bad ...
Zovetsa chisoni eeeee
Boma lilowelelepo there has been Child abuse apa..
Wow😮 this is very sad and it is a criminal offence arresting a child that committed no crime, this should be followed up and if possible these girls can sue the officers who did such
What a beautiful baby. God will punish the father of that baby, and he will never see peace in his life. Mr. Zulanga continue with the good works.
Ndiye kut opanda ndalama ku police kulibe nthandizo lake et, muthokoze kut anthuwa angokhala ndi umunthu mkadakhala ine mbambadi mkadafufuza komwe wapolice adalandira ndalamayu amakhala mkadakamuonetsa kut ena atengerepo phuxilo, apo bii mkadasaka petrol mkukabusa office ya police coz palibe phindu kwa anthu osauka, ndamva ululu kwabasi
Koma a Police .aku Malawi hmmmm you are very wicked
Yehova. Munkhwaskani mwana uyu na zanja linu lakuchizga
Zoopsatu
Inetu ndalila kwambili ndipo zandikhuza koma mulungu khuzeni mwana ndikono wamadalitso amen
Mudzina la Yesu matsoka komaso matembelo apite kwa aliyese amene watengapo gawo lozuza komaso kusautsa banja limeneli akumane ndi zilango mulungu awonetsa ukulu wake in Jesus name
Iiiiiii koma abaleeee?😢😢😢😢
pray for me Malawi,when i get rich all the corrupted police will be fired
fokoffffff
nkhani ya straight ngati iyi akulu achitetezo ndikupanga chinyengo mpaka kudzudzitsa moyo wa Gracious 😢😢😢😢😢
So bad 😢😢😢
ndadaula kwambiri koma and zandipangisa kulira
Very bad
So bad😢
Bad
Ambuye mkhuzen mwanayo ndi dzanja lanu la machiliso.mwana akuvutika uyu chitan chodzidzwisa pamoyo wake.
Mai a mwana musatope kusamalira mwanayo.
Azibambo kwenikweni ndi chani zoona kuzunzisa mwana chifukwa cha ndalama? Mulungu akupasen mtima wa umunthu komanso zomwe akuona mwanayo taganizirani muli inuyo.
Apolice aku Malawi simukudziwa ntchto yanu maka maka inuyo amene mwatenga gawo lalikulu kudya ndalama kuti Norman oipayo asamangidwe Mulungu akuyenderen ndithu.
Mabungwe pls loweleraponi mwanayo apeze thandizo loyenera.
Ndalila kwambili ambuye amukhudze grecious NDI mkono wamadalitso kut oipayo achite Manyaz zibambo oipa ofuna kupha mwana wake 😢😢