You're the voice of the voiceless Brother! May God of hope feel you with more life and blessings because you're fighting for us! On another way,we as Malawians we're not united as the way how other countries do. So mine is a request to all my fellow Malawians that let's unite and make one Malawi and fight for Malawi so that we can ease ourselves and our descendants from this burden! Let's develop a new type of life of fighting for our country not just stay and see corruption being done in our Country! The main reason is that TIMAKHALA NDI MANTHA POKUFUNA KUCHITA ZINTHU CHIFUKWA TIMANGOTI WE CAN'T PROTEST AGAINST THE GOVT KOMANSO TILINDI MOYO OSIYILANA ZINTHU! Ngati spirit iyi ipitilire Malawi sazatukuka!
Chakwera must be arrested for killing Malawians through lies. And very surprising that the opposition parties are still sleeping. Shame on you opposition sides who know how to make impossible and useless promises in rallies but do not know how to do your job. STRONG MESSAGES TO YOU OPPOSITION PARTIES: Silence does not solve problems but it sells out. Please try to serve your people not only your families because it is people who put you into that positions you are proud of.
Man osaopa continue giving the truth, Pompano tikhala tikukakavota nthawi yake yatha remember next year ndi kampeni don't worry Man well are following you
Our brother we play for you may Allah protect you komanso ndizowona big enawo sakwiya koma tambala wakuda sadzasinthanso basi mcp ndichipani chakupha basi anthu akufa m'midzimu ndinjala chifukwa cha kuyipa ntima kwa chakwela
Ku Malawi pakali pano kulibe Ufulu, tabweleranso mu one party system of government, timakunyadilani Brother you are true freedom fighter Almighty bless you.
So touching, this bakili muluzi channel is the best amd truth, tell them the truth, .. chiuta wamudangilileni akulu , ivo mukuyooya nivakusekeska yayi kwe nivachitima according ivo wakuchita wa mcp . 😢 wathu wakukavuka dele dele kumalawi uko , njala , ifa daily. Shameful..
Koma l think do not say that .some gyz a m 'boma mu akukuuzan zambir za ma gyz WA ...coz zitha kuwapanga impower , and anthu omwe akukuuzaniwo anthu kunkhala ndi Mantha ndiye aziwopa kukuuzan zambir
I wish you should've teach me and if they arresting you as they looking for you this channel should continue to tipitirire kuwayalusa mbava za anthu Ulemu wanu boss
If the government arrest this guy, the Whole Malawi will undertake and action. Who agree with me?
Where iwe Uli Phee Ku south Africa
Tikuyenera kupanga chinachake chokozekera ifeyo tili kumalawi konkuno tikuona mavuto akulu akulu
Tikuyenera kukhazikitsa chitsogolo chabwino izizi zatopetsa
Very true
I pray for you big asazakupezen
Simugwidwa olo ataphenga IN SHA ALLAH mulungu akutetezerani ndithu
Big love brother May almighty Allah bless ❤
Boma ili likudana nd chlungamo, pazonse zomwe akupanga , akuyiwala kt kunjakuno kili mulungu amene amawona, brother pitilizan kuyima pachlungamo ndpo mulungu azikutetezelan palipose pamene mungayende mulungu alinanu limodz🙏❤
You're the voice of the voiceless Brother!
May God of hope feel you with more life and blessings because you're fighting for us!
On another way,we as Malawians we're not united as the way how other countries do.
So mine is a request to all my fellow Malawians that let's unite and make one Malawi and fight for Malawi so that we can ease ourselves and our descendants from this burden!
Let's develop a new type of life of fighting for our country not just stay and see corruption being done in our Country!
The main reason is that TIMAKHALA NDI MANTHA POKUFUNA KUCHITA ZINTHU CHIFUKWA TIMANGOTI WE CAN'T PROTEST AGAINST THE GOVT KOMANSO TILINDI MOYO OSIYILANA ZINTHU!
Ngati spirit iyi ipitilire Malawi sazatukuka!
Inu ndi big. Started following you the very first day you created this channel. Always eager for the next talk
Kkkkk good job Bro
😂😂😂😂😂 lelotu mwalusa kwambiri
You're always wonderful and great man
Thanks bro, God bless you
A malawi tiyeni tipangeko kathu tisasiyire muthu modzi ichi ndichilungamo tiyen i tirole chiyende ngati madzi ukatero mulungu adzakumenyera khondo
Tell them Dr kakuba ameneyo setezake
Keep up the good work sir,we are proud of you
Lero mwakwiyatu bosss😂😂
Kkkk yaa lero more fire
Chakwera must be arrested for killing Malawians through lies. And very surprising that the opposition parties are still sleeping. Shame on you opposition sides who know how to make impossible and useless promises in rallies but do not know how to do your job. STRONG MESSAGES TO YOU OPPOSITION PARTIES: Silence does not solve problems but it sells out. Please try to serve your people not only your families because it is people who put you into that positions you are proud of.
Love you bakili muluzi Chanel umatiziwitsa zobisika menemomo❤zambili timaziwa ndi inuyo abambo great job bro.
Man osaopa continue giving the truth, Pompano tikhala tikukakavota nthawi yake yatha remember next year ndi kampeni don't worry Man well are following you
on repeat, boss man is here, only VOICE OF A KING IN MALAWI
❤
My Allah protecte you and bless you
You are my voice keep it up chilungamo kuwawa 🎉
DO NOT FEAR SPEAK THE TRUTH THE TRUTH WILL SENT YOU FREE
Big up bro. Never give up
Let's hope you must be safe my Journalists
inu ndakatundu timakudyalani kwambili ❤❤
Anthu oipa amenewa ..big up boss Man .I was not happy when someone told mi about u kut mwamangidwa
Me too 😢
Palibe zoopsezana ndikumangidwa apa,, chilungamo chiyende ngat madzi,,,ngati akufuna kumanga akamange Chakwera chifukwa walephela kupanga zomwe analonjeza
Brother osachita mantha💪💪💪nenani chilichonse mosawopa munthu
Chakwera ndimbuzi kwambili
You are number one!
Kkkkkkk Koma apolisi matama😂😂😂😂😂😂😂
More fire,ayerekeze kukumangani atiputa Ife amalawi tonse.a fisi amenewa atikwana kwambiri tikuzunzika
Chakwera ndi satana Mulungu amulange
Our brother we play for you may Allah protect you komanso ndizowona big enawo sakwiya koma tambala wakuda sadzasinthanso basi mcp ndichipani chakupha basi anthu akufa m'midzimu ndinjala chifukwa cha kuyipa ntima kwa chakwela
Ku Malawi pakali pano kulibe Ufulu, tabweleranso mu one party system of government, timakunyadilani Brother you are true freedom fighter Almighty bless you.
Kkkkkk koma nde watopatu dolo wapsa mtima umakwana
Proud of you Boss Man, may God bless and protect you always
May Allah protect you brother
Zoona brother chakwera watikwana chilungamo chioneka paifa yawitika
Salute brother
Am proud of u bro keep it up
Hope Mr. Chakwera is listening to this golden voice. Munthuyu tu ndiwamisala amene anawona nkhondo
mavuto ku Malawi koma atsogoleri don't want to change
True fighter love you bro
More fire bro Apolice matama.
Bwana osanyumwa tili pambuyo pano ❤
big up boss mn tilipambuyopo
Mmmm zomvesa chisoni boma lankhanza
Thanks again big man
Always reality brother
Keep it up more videos
You really stand for us
❤Ndikhale oyamba ine kupeleka comment boss tinakusowani kkkk inuo tikukupephelelan Inshaallah mutetezedwa
Nanga simukunena kuphedwa kwa a stambuli u don't talk for that matafari Ana akupoly simukunena bwanji
Long live Bakili Muluzi TV.
Your true story my brother go ahead lonjezo linadulitsa mutu wayohane pazimene analonjoza chakwera zilibe thandauzo kwammalawi.
May Almighty Allah bless you abundantly
Mumatha boss man. we are with u
❤❤❤ number one boss
Ulemu wanu bigger ❤🎉
O yes wafika bro wanga
Tili kumbuyo kwanu big boss and we will not allow the government to arrest you tiyeni amalawi tipitirize kumufunira ntchito yabwino munthu ameneyu
So touching, this bakili muluzi channel is the best amd truth, tell them the truth, .. chiuta wamudangilileni akulu , ivo mukuyooya nivakusekeska yayi kwe nivachitima according ivo wakuchita wa mcp . 😢 wathu wakukavuka dele dele kumalawi uko , njala , ifa daily. Shameful..
Ulemu wanu big man timakunyadilani kwambiri
Wel done tell them one is one
Big inshAllah inuyo Allah akutetezeni basi timakukondani
Mulungu apitilize kukudalisani big man
Umandisangalatsa ase may God protect you
It's my prayer kuti peter azawine mu 2025 adzakupatsen something for this job
Koma l think do not say that .some gyz a m 'boma mu akukuuzan zambir za ma gyz WA ...coz zitha kuwapanga impower , and anthu omwe akukuuzaniwo anthu kunkhala ndi Mantha ndiye aziwopa kukuuzan zambir
Osaopa bro
Watching from rsa ❤
Big man ndinu 1
My Allah bless you
Abwana chilima pamenepajatu anapepera akanaziwa sakadamuthandiza gwape ameneyu
😂😂😂 I love this guy
Nthawi yomwe Chilima akanaima ndi ino
This guy doesn't deserve arrest
We have been waiting for this video
Koma mwana iwe umatha kuyankhula chokhacho bas timakukondela kupanda kumva zaiwe timadwala ndithu 😆😆😆🤣🤣🤣
Waitha and i have strong massage for you *please don't fear nobody* stand on justice and Almighty God 🙏 always with you
Big man wathu tsopano.
You are the voice of the voiceless malawians. Ndipo chakwela mliska pooo! Aaaa that's why I don't trust these so-called pastor 😒
Never give up bro
Love u brother man
Timakunyadlan bwana ana achepa
Great voice and well said
Ee koma wakwiya muthuyi kopsa koma umakwana bro 🔥 🔥 🔥 🔥
My Malawi shaaaaa !!! Pali nkhani apa
Zoonad mumanena chilungamo osaopa 🇲🇼🇲🇼
You are doing great job man
🔥🔥🔥Respect you boss..
I wish you should've teach me and if they arresting you as they looking for you this channel should continue to tipitirire kuwayalusa mbava za anthu
Ulemu wanu boss
need to support you bro know that tili pambuyo pako
Watching from Chipata Eastern province republic of Zambia
Your the pearls of Malawi
Matama bwno mn😂😂😂😂😂
Voice of my boss
Go deep brother
I love bakiri muluzi tv
Guys let's protect this man
Ife tinakhulupilira zoti mwamangidwa
So emotional. We’re with you bro
Apa ndiye bigy mwabwera ... mulipo respecct
Thanks brother